< Ezekieli 12 >
1 Yehova anayankhula nane kuti,
BOEIPA ol te kai taengla ha pawk tih,
2 “Iwe mwana wa munthu, ukukhala pakati pa anthu owukira, iwowo maso openyera ali nawo, koma sakuona ndipo makutu omvera ali nawo, koma sakumva chifukwa choti ndi anthu owukira.
“Boekoek imkhui lung ah kho aka sa hlang capa nang, amih te hmuh ham mik om dae a hmuh uh moenih, a yaak ham hna khaw a khueh uh dae amih te boekoek imkhui kah coeng dongah ya uh pawh.
3 “Choncho, iwe mwana wa munthu, longedza katundu wako wopita naye ku ukapolo. Unyamuke nthawi yamasana iwo akuona. Uchite ngati wanyamuka kuchoka kumene ukukhala kupita ku dziko lachilendo iwowo akuona. Mwina adzamvetsetsa, paja ndi anthu aupandu.
Te dongah hlang capa nang, vangsawn kah hnopai te namah ham rhoekbah lamtah khothaih kah amih mikhmuh ah poelyoe pah. Namah hmuen lamloh amih mikhmuh ah a tloe hmuen la poelyoe pah. Amih boekoek imkhui loh a hmuh uh khaming.
4 Utulutse katundu wako wopita naye ku ukapolo nthawi ya masana iwo akuona. Ndipo nthawi ya madzulo, iwo akuona, uchoke monga ngati ukupita ku ukapolo.
Na hnopai te khothaih kah amih mikhmuh ah vangsawn kah hno bangla sat lamtah kholaeh ah khaw amih mikhmuh ah vangsawn kah a pongthoh bangla na thoeng pah mako.
5 Iwo akuona, ubowole pa khoma ndipo utulutsirepo katundu wako.
Amih mikhmuh ah namah ham pangbueng te thuk lamtah te long te khuen.
6 Usenze katundu wako pa phewa iwo akuona, ndipo upite kunja ku mdima. Uphimbe nkhope yako kuti usaone pansi, pakuti ndakusandutsa iwe chizindikiro chochenjeza Aisraeli.”
Amih mikhmuh ah na laengpang soah kawt lamtah a hmuep due na maelhmai dah lamtah khuen. Te daengah ni Israel imkhui ham kopoekrhai la nang kang khueh te khohmuen loh a hmuh pawt eh?,” a ti.
7 Choncho ine ndinachita monga momwe anandilamulira. Nthawi yamasana ndinatulutsa zinthu zanga nditazimanga ngati ndikupita ku ukapolo. Ndipo nthawi yamadzulo ndinabowola khoma ndi manja anga. Pamene chisisira chinkayamba, ndinasenza katundu wanga pa phewa kutuluka naye iwo akuona.
Te dongah ng'uen bangla ka saii tangloeng tih kamah kah hnopai te khothaih ah vangsawn kah hnopai bangla ka khuen. Kholaeh ah pangbueng te kamah ham kut neh ka thuk. A hmuep vaengah laengpang soah ka tloeng tih amih mikhmuh la ka pawk puei.
8 Mmawa mwake Yehova anandiyankhula nati:
BOEIPA ol tah mincang ah kai taengla ha pawk tih,
9 “Iwe mwana wa munthu, kodi anthu aupandu a Israeli sanakufunse kuti ukuchita chiyani?
“Hlang capa, boekoek imkhui kah Israel imkhui loh na saii te nang taengah thui uh pawt nim?
10 “Uwawuze kuti, ‘zimene ndikunena Ine Ambuye Wamphamvuzonse ndi izi: Uthengawu ndi wonena za kalonga wa ku Yerusalemu pamodzi ndi banja lonse la Israeli amene akukhala kumeneko.’
Ka Boeipa Yahovah loh a thui he a taengah thui pah. He tah Jerusalem neh amih khui kah Israel imkhui boeih ham khoboei kah olrhuh ni.
11 Uwawuze kuti, ‘Ndiwe chizindikiro chowachenjeza.’ “Zidzakuchitikirani monga momwe zakuchitikira iwemu. Iwo adzatengedwa kupita ku ukapolo.”
' Ka saii bangla nangmih kah miknoeknah tah kai ni. Amih te vangsawn la a khueh vetih na tamna la cet uh ni.
12 “Kalonga wawo adzatenga katundu wake nʼchisisira nʼkunyamuka. Adzatulukira pa bowo limene anthu anabowola pa khoma. Adzaphimba nkhope yake kuti asaone kumene akupita.
Amih lakli kah khoboei khaw a hmuep ah a laengpang neh a koh vetih coe uh ni. Pangbueng khui long coe ham te a thuk uh ni. A maelhmai te a thing vetih a mik dongah khohmuen khaw hmu mahpawh.
13 Ndidzayala ukonde wanga pa iye ndi kumukola mu msampha wanga. Ndidzabwera naye ku Babuloni, dziko la Akaldeya, koma sadzaliona dzikolo, ndipo adzafera kumeneko.
Te vaengah ka lawk te anih ham ka tung vetih ka rhalvong dongah man bitni. Anih te Khalden khohmuen Babylon la ka thak vaengah he he a hmuh kolla pahoi duek ni.
14 Ine ndidzabalalitsa kumbali zonse zinayi onse okhala naye pafupi, ndiwo omuthandiza ake pamodzi ndi ankhondo ake. Ndidzawalondola ndi lupanga losolola.
A kaepvai boeih te khaw anih kah bomkung bomkung neh a caembong boeih khohli cungkuem taengla ka haeh vetih amih hnuk te cunghang neh ka khoh ni.
15 “Iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, ndikadzawamwaza pakati pa anthu a mitundu ina ndi kuwabalalitsira ku mayiko ena.
BOEIPA kamah he a ming uh bitni. Amih te namtom taengah ka taekyak ham neh amih te paeng taengah ka haeh coeng.
16 Koma ndidzasiyako ena pangʼono amene adzapulumuke ku lupanga, njala ndi mliri, kuti akafotokoze ntchito zawo zonse zonyansa pakati pa anthu achilendo kumene akupitako. Pamenepo adzadziwa kuti ndine Yehova.”
Tedae amih kah hlang te amah tarhing ah cunghang lamkah neh khokha lamkah khaw duektahaw lamkah ka hlun ni. Te daengah ni athoeng uh thil namtom taengah khaw amamih kah tueilaehkoi cungkuem te a tae uh pahoi vetih BOEIPA kamah te m'ming uh eh,” a ti.
17 Pambuyo pake Yehova anandiyankhulanso nati,
Te phoeiah BOEIPA ol te kai taengah ha pawk tih,
18 “Iwe mwana wa munthu, uzinjenjemera ukamadya chakudya chako, ndipo uzinthunthumira ndi mantha ukamamwa madzi ako.
“Hlang capa, na buh te hinghuennah neh ca lamtah na tui te khoponah neh, mawnnah neh o.
19 Uwawuze anthu a mʼdzikomo kuti izi ndi zimene Ambuye Wamphamvuzonse akunena za anthu okhala mu Yerusalemu ndi dziko la Israeli: Iwo adzadya chakudya chawo ndi mantha ndi kumwa madzi awo ndi nkhawa. Zonse za mʼdziko lawo zidzalandidwa chifukwa cha ziwawa za anthu onse okhala mʼmenemo.
Te phoeiah khohmuen kah pilnam taengah thui pah. Ka Boeipa Yahovah loh he ni a thui. Israel khohmuen kah Jerusalem khosa rhoek a buh te mawnnah neh ca uh saeh lamtah a tui te a maehmanah neh o uh saeh. A khohmuen te a cungkuem ah a khui khosa boeih kuthlahnah dongah rhawp ni.
20 Mizinda imene ili ndi anthu idzasakazika ndipo dziko lidzasanduka chipululu. Pamenepo inu mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”
Khosa khopuei rhoek khaw khap uh vetih khohmuen he khopong la poeh ni. Te vaengah BOEIPA kamah te nan ming uh bitni,” a ti.
21 Yehova anayankhulanso nane kuti,
BOEIPA ol tah kai taengah koep ha pawk tih,
22 “Iwe mwana wa munthu, kodi mwambi umene ukunenedwa mu Israeli ndi wotani: ‘Masiku akupita koma masomphenya onse sakukwaniritsidwa?’
“Hlang capa, nang taengkah thuidoeknah te ta? Khohmuen kah Israel he thui pah ham khaw khohnin puh tih mangthui khaw boeih paltham coeng.
23 Choncho uwawuze anthuwo kuti, ‘Ine Ambuye Yehova ndidzawuthetsa mwambi umenewu ndipo sadzawunenanso mu Israeli.’ Uwawuze kuti, ‘masiku ayandikira oti zonse zimene ndinanena mʼmasomphenya zichitikedi.
Te dongah ka Boeipa Yahovah loh a thui he amih taengah thui pah. He thuidoeknah he ka paa sak vetih he he Israel khuiah khaw koep thoel uh mahpawh. Te dongah amih taengah khohnin neh mangthui cungkuem kah ol ha thoeng te thui pah dae.
24 Pakuti masiku amenewo sikudzakhalanso masomphenya abodza kapena kuwombeza kwa chinyengo pakati pa anthu a Israeli.
A poeyoek kah mangthui boeih neh olhnal tonghma khaw Israel im khui ah koep om mahpawh.
25 Koma Ine Ambuye ndidzayankhula chimene ndikufuna, ndipo chidzachitikadi, osachedwa ayi. Pakuti mʼmasiku anu omwe ano, inu anthu opanduka, ndidzakwaniritsa chilichonse chimene ndidzanena. Ndikutero Ine Yehova.’”
Tedae BOEIPA loh ka thui te ka thui ol bangla thoeng ni. Nangmih kah khohnin ah uelh voel mahpawh. Boekoek imkhui te ol ka thui pah vetih amah la ka thoeng sak ni. Ka Boeipa Yahovah kah olphong ni,” a ti.
26 Yehova anandiyankhula nati:
BOEIPA kah ol tah kai taengah ha pawk tih,
27 “Iwe mwana wa munthu, Aisraeli akunena kuti, ‘masomphenya amene ukuona sadzachitika kwa zaka zambiri. Iwo akuti ukulosa za zinthu zimene zidzachitika ku tsogolo kwambiri.’
Hlang capa aw, Israel imkhui, “Anih kah mangthui a hmuh te khohnin la puh tih a tue khohla ham ni a tonghma,’ a ti uh te.
28 “Choncho uwawuze kuti, ‘zimene Ine Ambuye Yehova ndikunena ndi izi: Zonena zanga sizidzachedwanso; chilichonse chimene ndikunena chidzachitikadi. Ndikutero Ine Yehova.’”
Te dongah ka Boeipa Yahovah loh a thui he amih taengah thui pah. Ka ol ka thui boeih te ka ol bangla uelh voel mahpawh. Tedae ka Boeipa Yahovah olphong he thoeng ni,” a ti.