< Ezekieli 11 >

1 Pamenepo Mzimu wa Mulungu unandinyamula ndi kubwera nane ku chipata cha kummawa cha Nyumba ya Yehova. Kumeneko pa khomo la chipata panali anthu 25, ndipo ndinaona pakati pawo atsogoleri awa: Yaazaniya mwana wa Azuri ndi Pelatiya mwana wa Benaya.
Mueihla loh kai m'phoh tih khothoeng la aka mang yan BOEIPA im vongka la kai ng'khuen. Te vaengah hlang pakul panga tevongka thohka ah lawt ana om. Amih lakli ah pilnam kah mangpa Azzur capa Jaazaniah neh Benaiah capa Pelatiah ka hmuh.
2 Yehova anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, awa ndi anthu amene akukonza zoyipa ndi kupereka malangizo oyipa mu mzindamo.
Te phoeiah kai taengah, “Hlang capa, hlang rhoek long he boethae a moeh uh tih he khopuei ah a thae cilsuep ni a. uen uh.
3 Iwo amawuza anthu kuti, ‘Nthawi sinafike yoti timange Nyumba? Mzindawu uli ngati mʼphika umene uli pa moto ndipo ife tili ngati nyama mu mʼphikamo.
Im sak ham yoei hlan, mamih tah he am dongkah maeh ni, ' a ti uh.
4 Choncho iwe mwana wa munthu, unenere mowadzudzula. Nenera ndithu.’”
Te dongah amih taengah tonghma pah, hlang capa aw tonghma pah,” a ti.
5 Ndipo Mzimu wa Yehova unandigwera ndipo unandiwuza kuti, “Unene kuti zimene akunena Yehova ndi izi. Iye akuti. ‘Izi ndi zimene mukunena, Inu Aisraeli, koma Ine ndikudziwa zimene zili mu mtima mwanu.’
BOEIPA kah mueihla te kai soah ha cu tih kai te m'voek. “BOEIPA loh a thui he Israel imkhui ah thui pah. Tedae na mueihla kah tangtlaeng khaw ka ming.
6 Mwapha anthu ambiri mu mzinda muno ndipo mwadzaza misewu yake ndi mitembo.
Nangmih rhok te he khopuei ah hmoeng tih a tollong khaw rhok neh bae,” a ti.
7 “Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti, ‘Mitembo imene mwayiponya mʼmisewuyo ndiyo nyama ndipo mzinda uno ndiwo mʼphika, koma Ine ndidzakuthamangitsanimo.
Te dongah ka Boeipa Yahovah loh he ni a. thui. Na rhok te a khui ah maeh la na khueh coeng tih khopuei he am la poeh coeng. Tedae nanmih te a khui lamloh n'hoep ni.
8 Inu mumaopa lupanga, koma lupangalo ndi limene ndidzakubweretsereni, akutero Ambuye.
cunghang na rhih uh dongah nangmih taengla cunghang kang khuen ni. He tah ka Boeipa Yahovah kah olphong ni.
9 Ine ndidzakuthamangitsani mu mzinda ndipo ndidzakuperekani mʼdzanja la alendo kuti akulangeni.
Nangmih te a khui lamloh kang khuen vetih kholong kut ah kan tloeng ni. Te vaengah tholhphu te nangmih soah ka saii ni.
10 Mudzaphedwa ndi lupanga ndipo ndidzakulangani mpaka kumalire a Israeli. Pamenepo mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Israel khorhi ah cunghang neh na cungku uh tih nangmih soah lai ka tloek vaengah BOEIPA kamah te nan ming uh bitni.
11 Mzinda uno sudzakhala ngati mʼphika wokutetezani ndipo simudzakhalanso ngati nyama ya mʼmenemo. Ndidzakulangani mpaka kumalire a Israeli.
He he nangmih ham tah am la om pawt vetih nangmih te a khui ah maeh la na om uh mahpawh. Nangmih te Israel khorhi ah lai kan tloek ni.
12 Ndipo inu mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova. Inu simunatsatire malangizo anga kapena kusunga malamulo anga koma mwakhala mukutsata zochita za mitundu ina ya anthu imene yakuzungulirani.’”
Te vaengah BOEIPA kamah te nan ming uh bitni. Ka oltlueh dongah na pongpa uh pawt tih ka laitloeknah na rhoi uh moenih. Tedae na kaepvai namtom kah laitloeknah bangla na saii uh.
13 Tsono pamene ndinkanenera, Pelatiya mwana wa Benaya anafa. Pomwepo ndinadzigwetsa pansi chafufumimba ndipo ndinafuwula ndi mawu aakulu kuti “Mayo, Ambuye Yehova! Kodi mudzawatheratu Aisraeli onse otsala?”
Ka tonghma li vaengah Benaiah capa Pelatiah te duek. Te dongah ka maelhmai neh ka bakop tih ol ue la ka pang. Te vaengah, 'Ka Boeipa Yahovah aw, na khawknah hil ah Israel kah a meet te na saii aih,’ ka ti.
14 Yehova anayankhula nane kuti,
BOEIPA ol te kai taengla ha pawk.
15 “Anthu okhala ku Yerusalemu akuwanena abale ako, anthu a ku ukapolo, onse a banja la Israeli, kuti, ‘Anthu onse amene anatengedwa ukapolo ali kutali ndi Yehova. Dziko lanu Yehova anatipatsa kuti likhale lathulathu.’”
Te vaengah, “Hlang capa aw, na manuca khuikah na manuca, na hlang tlannah neh Israel imkhui pum loh a pum la amih Jerusalem khosa rhoek te, 'BOEIPA taeng lamloh a lakhla uh dongah ni khohmuen he kaimih taengah khoh la m'paek,’ a ti na uh.
16 “Nʼchifukwa chake nena kwa anzako a ku ukapolo kuti, ‘Ambuye Yehova akuti: Ine ndinawatumiza kutali pakati pa anthu a mitundu ina. Ndinawabalalitsa ku mayiko ambiri. Komabe ndakhala ndikuwasunga ku mayiko kumene anapitako!’
Te dongah ka Boeipa Yahovah loh athui he thui. Amih te namtom taengah ka lakhla sak tih diklai ah amih ka taek ka yak sitoe cakhaw a pha uh khohmuen ah amih ham rhokso la rhaih ka om pahoi coeng.
17 “Nʼchifukwa chake uwawuze zimene Ine Ambuye Yehova ndikunena kuti, Ndidzawasonkhanitsa kuchokera kwa anthu a mitundu inayo ndi kuwasonkhanitsira pamodzi kuchokera ku mayiko kumene ndinawabalalitsirako. Pambuyo pake ndidzawapatsa dziko la Israeli.
Te dongah ka Boeipa Yahovah loh a thui he thui pah. Nangmih te pilnam taeng lamloh kan coi vetih nangmih te diklai lamloh kan coi ni. Amih taengah kan taek kan yak cakhaw Israel khohmuen he nangmih taengah ni kam paek eh.
18 “Akadzalowa mʼdzikomo adzachotsa mafano awo onse oyipa ndi onyansa.
Te la ha pawk uh vaengah a sarhingkoi cungkuem neh a tueilaehkoi cungkuem te anih lamloh a khoe uh ni.
19 Ndidzawapatsa mtima watsopano ndipo ndidzayika mzimu watsopano mwa iwo. Ndidzachotsa mtima wowuma ngati mwala mwa iwo, ndipo ndidzawapatsa mtima wofewa ngati mnofu.
Amih te lungbuei pakhat la ka khueh pah vetih nangmih kotak ah mueihla thai kam paek. Te vaengah amih saa lamkah lungto lungbuei ka kuel pah vetih amih te ngansen lungbuei te ka paek ni.
20 Motero adzatsata malamulo anga ndipo adzasunga mosamala malamulo anga. Adzakhala anthu anga, ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wawo.
Te daengah ni ka khosing dongah pongpa uh vetih ka laitloeknah te a tuem uh eh. Te te a saii uh daengah ni kai taengah pilnam la om uh vetih kai khaw amih taengah Pathen la ka om eh.
21 Koma kunena za amene akupembedza mafano oyipa ndi onyansa, ndidzawalanga chifukwa cha zimene achita. Ndikutero Ine Ambuye Yehova.”
Tedae amih kah sarhingkoi lungbuei neh a lungbuei kah a tueilaehkoi longpuei ah a pongpa uh te amih lu ah ka tloeng pah ni. He tah ka Boeipa Yahovah kah olphong ni,” a ti.
22 Tsono akerubi aja anatambasula mapiko awo kuyamba kuwuluka, mikombero ili mʼmbali mwawo. Ulemerero wa Mulungu wa Israeli unali pamwamba pawo.
Te vaengah cherubim rhoek loh a phae te a voeivang kah lengkho neh a phuel tih Israel Pathen kah thangpomnah tah amih sokah a so duela om.
23 Ulemerero wa Yehova unakwera ndi kusiya mzindawo ndipo unakayima pa phiri cha kummawa kwake kwa mzindawo.
BOEIPA kah thangpomnah khaw khopuei khui lamloh cet tih khopuei khothoeng kah tlang ah duem.
24 Pambuyo pake Mzimu wa Mulungu unandinyamula ndi kukandifikitsa. Zimenezi zinkachitika mʼmasomphenya monga mmene Mzimu wa Mulungu unkandionetsera. Kenaka masomphenya amene ndinkawaonawo anayamba kuzimirira.
Mueihla loh kai ng'khuen tih Pathen mueihla kah mueimae neh Khalden ah vangsawn la kai n'thak. Te phoeiah a mueimae ka hmuh te kai taeng lamloh cet.
25 Ndipo ndinafotokozera akapolowo zonse zimene Yehova anandionetsa.
vangsawn taengah ka thui ol boeih he BOEIPA loh kai n'tueng coeng.

< Ezekieli 11 >