< Eksodo 38 >

1 Anapanga guwa lansembe zopsereza lamatabwa amtengo wa mkesha. Linali lofanana mbali zonse. Msinkhu wake masentimita 137, mulitali mwake masentimita 229, mulifupi masentimita 229.
И начини од дрвета ситима олтар за жртве паљенице у дужину од пет лаката, и у ширину од пет лаката, четвороугласт, висок три лакта.
2 Anapanga nyanga imodziimodzi pa ngodya zake zinayizo, kotero kuti nyangazo ndi guwalo zinali chinthu chimodzi, ndipo anakuta guwalo ndi mkuwa.
И начини му на четири угла његова рогове; из њега излажаху рогови, и окова га у бронзу.
3 Anapanganso ziwiya zamkuwa izi zogwirira ntchito pa guwalo: miphika, mafosholo, mabeseni owazira magazi, ngowe zokowera nyama ndi zosonkhezera moto.
И начини све посуђе за олтар, лонце и лопатице и котлиће и виљушке и клешта; све му посуђе начини од бронзе.
4 Anapanga sefa yachitsulo chamkuwa ya guwa lansembelo kuti ikhale mmunsi mwa khoma la guwa lansembelo, kuchokera pansi mpaka pakati pa khoma la guwalo.
И начини олтару решетку као мрежу од бронзе испод олтара унаоколо ода дна до средине.
5 Anapanga mphete zamkuwa zinayi ndipo anazilumikiza ku ngodya zinayi za sefa ija kuti zigwire nsichi zonyamulira.
И сали четири биочуга за четири угла решетке бронзане, да се кроз њих провуку полуге.
6 Anapanga nsichi zamtengo wa mkesha ndipo anazikuta ndi mkuwa.
А полуге начини од дрвета ситима, и окова их у бронзу.
7 Iwo analowetsa nsichizo mʼmphetemo mbali zonse ziwiri za guwalo kuti azinyamulira. Guwalo linali lamatabwa ndi logoba mʼkati mwake.
И провуче полуге кроз биочуге с обе стране олтара, да се може носити, од дасака начини га шупљег.
8 Anapanga beseni lamkuwa lokhala ndi miyendo yamkuwanso kuchokera ku magalasi oyangʼanira nkhope a amayi amene ankatumikira pa chipata cha tenti ya msonkhano.
И начини умиваоницу бронзану и подножје јој бронзано од огледала која доношаху гомилама жене долазећи на врата шатору од састанка.
9 Kenaka anapanga bwalo la chihema. Mbali yakummwera inali yotalika mamita 46 ndipo kunali nsalu yotchinga yofewa yosalala yolukidwa bwino.
И начини трем на јужној страни, и завесе трему од танког платна узведеног од сто лаката,
10 Anapanganso mizati makumi awiri, matsinde makumi awiri amkuwa ndi ngowe zasiliva ndi zingwe za mizatiyo.
И двадесет ступова за њих и двадесет стопица под њих од бронзе, а куке на ступове и преворнице од сребра.
11 Mbali yakumpoto inalinso yotalika mamita 46 ndipo inali ndi mizati makumi awiri, matsinde amkuwa makumi awiri, ngowe zasiliva ndi zingwe za mizatiyo.
Тако и на северној страни завесе од сто лаката, двадесет ступова за њих и двадесет стопица под њих од бронзе; а куке на ступове и преворнице њихове од сребра;
12 Mbali yakumadzulo inali yotalika mamita 23 ndipo inali ndi nsalu yotchinga, mizati khumi ndi matsinde khumi. Inalinso ndi ngowe zasiliva ndi zingwe za mizatiyo.
А на западној страни завесе од педесет лаката, десет ступова за њих и десет стопица њихових од бронзе, куке на ступовима и појасеве њихове од сребра;
13 Mbali yakummawa, kotulukira dzuwa, inalinso yotalika mamita 23.
А на предњој страни према истоку завесе од педесет лаката;
14 Mbali imodzi yachipata kunali nsalu yotchinga yotalika mamita asanu ndi awiri, mizati itatu ndi matsinde atatu,
С једне стране завесе од петнаест лаката, три ступа за њих и три стопице под њих;
15 polowera mʼbwalo panali nsalu yotchinga ya mamita asanu ndi awiri pamodzi ndi mizati itatu ndi matsinde atatu.
А с друге стране, до врата од трема и отуда и одовуда, завесе од петнаест лаката, три ступа за њих и три стопице под њих.
16 Katani yonse yotchinga kuzungulira chihema inali yofewa, yosalala ndi yolukidwa bwino.
Сви завеси на трему унаоколо беху од танког платна узведеног;
17 Matsinde amizati anali amkuwa. Ngowe ndi zingwe za mizati zinali zasiliva, ndipo pamwamba pa mizatiyo anakutapo siliva. Choncho mizati yonse ya bwalolo inalumikizidwa ndi zingwe zasiliva.
А стопице под ступовима од бронзе, куке на ступовима и појасеви на њима од сребра; и врхови им беху сребрни; сви ступови у трему беху опасани сребром.
18 Nsalu yotchinga ya pa chipata inali yamtundu wa mtambo, yapepo ndi yofiira, yofewa yosalala ndi yopangidwa ndi anthu aluso. Nsaluyo inali yotalika mamita asanu ndi anayi, molingana ndi nsalu zotchinga bwalo. Msinkhu wake unali masentimita 229,
А завес на вратима од трема беше од порфире и од скерлета и од црвца и од танког платна узведеног, везен, у дужину од двадесет лаката а у висину по ширини пет лаката, као и други завеси у трему.
19 pamodzi ndi mizati yake inayi ndi matsinde amkuwa anayi. Ngowe ndi zingwe zake zinali za siliva, ndipo pamwamba pake pa mzati anakutapo ndi siliva.
И четири ступа за њ, и четири стопице под њих од бронзе, чепови на њима од сребра и врхови им и појасеви од сребра.
20 Zikhomo za chihema ndi zina zonse zozungulira chihemacho zinali zamkuwa.
А све коље шатору и трему унаоколо беше од бронзе.
21 Chiwerengero cha zipangizo zimene anagwiritsa ntchito popanga chihema, chihema chaumboni, zimene Mose analamulira Alevi kuti alembe motsogozedwa ndi Itamara mwana wa Aaroni, wansembe, chinali ichi:
Те су ствари пребројане за шатор, шатор од сведочанства, које је пребројао по заповести Мојсијевој Итамар, син Арона свештеника за службу левитску.
22 Bezaleli mwana wa Uri, mwana wa Huzi wa fuko la Yuda anapanga chilichonse Yehova analamulira Mose,
А Веселеило, син Урије сина Оровог од племена Јудиног, начини све то што заповеди Господ Мојсију,
23 pamodzi ndi Oholiabu mwana wa Ahisamaki, wa fuko la Dani, wa luso la zopangapanga ndi kulemba mapulani, ndi wopanga nsalu zolukidwa bwino za mtundu wa mtambo, yapepo ndi zofiira, zofewa ndi zosalala.
И с њим Елијав, син Ахисамахов од племена Дановог, дрводеља и вешт ткати и вести по порфири, по скерлету, по црвцу и по танком платну.
24 Golide yense wochokera ku nsembe yoweyula amene anagwiritsa ntchito pa ntchito yonse yopanga malo wopatulika anali wolemera makilogalamu 1,000 potsata miyeso ya kumalo wopatulika.
А свега злата што отиде на ово дело, на све дело за светињу, које злато беше приложено, свега га беше двадесет и девет таланата, седам стотина и тридесет сикала, по светом сиклу;
25 Siliva wochokera ku gulu lonse la anthu anali wolemerera makilogalamu 3,430, potsata miyeso ya ku malo wopatulika.
А сребра што дође од збора, сто таланата, и хиљада седам стотина и седамдесет и пет сикала, по светом сиклу;
26 Munthu aliyense amapereka beka imodzi, kufanana ngati makilogalamu 6, potsata muyeso wa ku malo wopatulika. Kuchokera kwa aliyense amene anawerengedwa kuyambira zaka 20 kapena kuposerapo, amuna onse analipo 603,550.
Пола сикла од главе, по сиклу светом, од сваког који уђе у број, од двадесет година и више, од шест стотина и три хиљаде и пет стотина и педесет.
27 Anagwiritsa ntchito siliva wolemera makilogalamu 3,400 kupanga matsinde 100 a ku malo wopatulika ndi makatani, ndipo makilogalamu 34 kupanga tsinde limodzi.
Од сто таланата сребра салише се стопице за светињу и стопице за завес; сто стопица од сто таланата, таланат на стопицу.
28 Makilogalamu otsalawo anagwiritsa ntchito popanga ngowe zamzati kukutira pamwamba pa mizati ndiponso kupanga zingwe zake.
А од хиљаду и седам стотина и седамдесет и пет сикала начини куке на ступове, и окова им врхове и опаса их.
29 Mkuwa ochokera ku nsembe yoweyula unali makilogalamu 2,425.
А бронзе приложене беше седамдесет таланата, и две хиљаде и четири стотине сикала.
30 Iwo anawugwiritsa ntchito popanga matsinde a pa chipata cha tenti ya msonkhano, guwa la mkuwa pamodzi ndi sefa yake ndiponso ziwiya zonse,
И од тога начини стопице на вратима шатора од састанка, и бронзани олтар и решетку бронзану за њ, и све справе за олтар,
31 matsinde ozungulira bwalo ndiponso a pa chipata pake, ndi zikhomo zonse za tentiyo ndi matsinde a malo wozungulirapo.
И стопице у трему унаоколо, и стопице на вратима од трема, и све коље за шатор и све коље за трем унаоколо.

< Eksodo 38 >