< Eksodo 30 >

1 Upange guwa lamatabwa amtengo wa mkesha lofukizirapo lubani.
Hahoi, hmuitui sawinae khoungroe anri thing hoi na sak han.
2 Likhale lofanana mbali zonse. Mulitali masentimita 46, mulifupi masentimita 46, ndipo msinkhu masentimita 91. Nyanga zake zipangidwe kumodzi ndi guwalo.
Ayung dong touh, adangka dong touh, a rasang dong touh hoi takin pali touh lah na sak vaiteh, a ki hateh khoungroe hoi a kâkuet han.
3 Ukute guwa lonse ndi golide wabwino kwambiri, pamwamba pake, mbali zonse zinayi, pamodzi ndi nyanga zake. Ndipo upange mkombero wagolide kuzungulira guwalo.
A lathueng lae hoi a tapang hoi a ki hah sui kathoung hoi na hluk awh vaiteh, petkâkalup lah sui hoi arai na pacawp han.
4 Upange mphete ziwiri zagolide ndipo uzilumikize ku guwa mʼmunsi mwa mkombero, mphete ziwiri ku mbali zonse ziwiri zoyangʼanana. Mphetozo zizigwira nsichi zonyamulira guwalo.
Arai pacawpnae rahim vah suilaikaw kahni touh na sak han. Avangvanglah na ta vaiteh, hothateh kâkayawtnae acung hrawt nahane doeh.
5 Upange mizati yamtengo wa mkesha ndipo uyikute ndi golide.
Acung teh anri thing hoi na sak vaiteh, sui tui hoi na bu sin han.
6 Uyike guwalo patsogolo pa nsalu yotchinga Bokosi la Chipangano. Apa ndi pamene ndizidzakumana nawe.
Hothateh kai ni na pato nahane hmuen lawkpanuesaknae tanae thingkong ngue nahanelah yaphni hmalah hote khoungroe hah na hruek han.
7 “Aaroni ayenera kumafukiza lubani wonunkhira pa guwalo mmawa uliwonse. Pamene akukonza nyale zija afukizenso lubani.
Hottelah Aron ni hawvah, hmaisawi hane hmuitui hah a sawi han. Amom karawitawi hmaiim a rakueng navah a sawi han.
8 Aaroni ayenera kufukizanso lubani pamene ayatsa nyale madzulo kuti lubani akhale akuyaka nthawi zonse pamaso pa Yehova kwa mibado imene ikubwera.
Aron ni tangmin lah hmaiim paangnae tueng dawkvah, hmuitui hah hmai a sawi han. Hothateh, na ca catounnaw totouh BAWIPA hmalah hmuitui lah ao han.
9 Pa guwapo usafukize lubani wachilendo kapena kuperekapo nsembe yopsereza kapena nsembe yaufa. Usathire pa guwapo ngakhale nsembe yachakumwa.
Hawvah hmuitui alouke thoseh, hmaisawi thuengnae thoseh, rawca thuengnae thoseh na poe mahoeh. Hawvah, nei hane na poe e hai na awi mahoeh.
10 Aaroni azidzapereka nsembe yopepesera machimo pa nyanga za guwalo kamodzi pa chaka. Mwambowu uzidzachitika pogwiritsa ntchito magazi a nsembe yopepesera machimo, ndipo zizidzachitika mʼmibado yanu yonse. Choncho guwa lansembelo lidzakhala loyera ndi loperekedwa kwa Yehova.”
Aron ni kum touh dawk vai touh yonthanae sathei thi hah a la vaiteh, kinaw dawkvah yonthanae a sak han. Na ca catounnaw totouh kum touh dawk vai touh yonthanae a sak awh han, hot teh BAWIPA hanelah kathoungpounge doeh.
11 Ndipo Yehova anati kwa Mose,
BAWIPA ni Mosi koe,
12 “Pamene ukuchita kalembera wa Aisraeli, munthu aliyense ayenera kupereka kwa Yehova chowombolera moyo wake pamene akuwerengedwa. Motero mliri sudzabwera pa iwo pamene ukuwawerenga.
Isarel catoun milu na touk toteh, milu na touk e yit touh tami pueng ni hringlu ratang nahanelah BAWIPA a poe awh han. Na touk toteh ahnimouh na touk dawkvah, ahnimouh koe lacik a pha hoeh nahanelah,
13 Izi ndi zimene aliyense wolembedwa mu kawundula ayenera kupereka: theka la sekeli, kutanthauza ndalama zolemera magalamu asanu ndi limodzi malingana ndi kawerengedwe ka ndalama za ku Nyumba ya Mulungu. Paja sekeli imodzi ikulingana ndi magera makumi awiri. Theka la sekeli chidzakhala chopereka cha kwa Yehova.
hetheh a poe awh hanelah ao. Touk tangcoung e naw pueng ni, hmuen kathoung koe hno khingnae a khing tangawn hah BAWIPA hanlah a poe awh han ( Khing touh teh gerah 20 touh doeh).
14 Aliyense wolembedwa mu kawundula amene ali ndi zaka makumi awiri kapena kupitirira ayenera kupereka chopereka kwa Yehova.
Touk tangcoung e kum 20 lathueng pueng ni, BAWIPA hanelah a poe awh han.
15 Anthu olemera asapereke koposa theka la sekeli ndipo osauka asapereke kuchepera theka la sekeli pamene mukupereka nsembe kwa Yehova yowombolera miyoyo yanu.
Na hringlu ratang nahanelah, BAWIPA hanelah na poe awh pawiteh, khing tangawn hlak kapap lah tami ka tawnta ni poe mahoeh. Hahoi ka mathoe ni hai hothlak kayoun lah poe mahoeh.
16 Ulandire ndalama zopepeserazo kuchokera kwa Aisraeli ndipo zigwiritsidwe ntchito ya ku tenti ya msonkhano. Zoperekazi zidzakhala chikumbutso cha Aisraeli pamaso pa Yehova, ndiponso zowombolera miyoyo yanu.”
Isarel catounnaw yontha nahane tangka teh na la vaiteh, kamkhuengnae lukkareiim dawk thawtawknae lah na pouk han. Na hringlu yontha nahane BAWIPA hmalah Isarel catounnaw hanlah Pahnim hoeh nahanlah ao nahan, telah a dei.
17 Ndipo Yehova anati kwa Mose,
BAWIPA ni Mosi koe,
18 “Upange beseni lamkuwa lokhala ndi miyendo yamkuwanso. Uliyike pakati pa tenti ya msonkhano ndi guwa lansembe ndipo uthiremo madzi.
kâpasu nahanlah rahum kawlung hoi pâhung nahanlah amkhoung na sak han. Lukkareiim hoi khoungroe rahak na ta han.
19 Aaroni ndi ana ake azisamba mʼmanja ndi kutsuka mapazi awo ndi madzi amenewo.
Ahnimouh teh kamkhuengnae lukkareiim thung a kâen awh nakunghai thoseh,
20 Pamene akulowa mu tenti ya msonkhano, iwo asambe madziwa kuti asafe. Ndiponso pamene akupita kukatumikira ku guwa lansembe ndi kupereka nsembe yopsereza kwa Yehova,
BAWIPA koe hmaisawi thuengnae thueng hanelah, khoungroe koe a hnai nah thoseh,
21 azisamba mʼmanja mwawo ndi kutsuka mapazi kuti asadzafe. Limeneli ndi lamulo limene Aaroni, pamodzi ndi ana ndi zidzukulu zake mʼtsogolomo ayenera kumadzalitsatira mpaka muyaya.”
due hoeh nahanelah, amamae kut khok hah a pâsu awh han. Hottelah ahnimouh hoi ahnimae ca catounnaw ni tarawi hane kâlawk lah ao telah ati.
22 Ndipo Yehova anati kwa Mose,
Hothloilah BAWIPA ni Mosi koevah,
23 “Utenge zonunkhira bwino kwambiri izi: makilogalamu asanu ndi limodzi a mure wamadzi, makilogalamu atatu a zonunkhira bwino za mtundu wa sinamoni, makilogalamu atatu a nzimbe yonunkhira bwino kwambiri,
hmuituinaw thung dawk a hmui katuipounge murah sekel 500 touh hoi nakzik hmuitui khing 250,
24 makilogalamu asanu ndi limodzi a mkesha. Zonsezi zikhale malingana ndi muyeso wa ku Nyumba ya Mulungu. Pakhalenso malita anayi a mafuta a olivi.
nakzik phun louk khing 500, olive satui pong 12 touh (hin buet touh) na thokhai vaiteh,
25 Ugwiritse ntchito zinthu zimenezi kupanga mafuta opatulika odzozera, mafuta onunkhira, apangidwe ndi mʼmisiri waluso lopanga zonunkhiritsa. Awa adzakhala mafuta opatulika odzozera.
hmuitui kasakkung ni a sak e patetlah hluk e satui hah kathounge satui lah na sak han.
26 Tsono uwagwiritse ntchito podzoza tenti ya msonkhano, Bokosi la Chipangano,
Kamkhuengnae lukkareiim, lawkpanuesaknae thingkong,
27 tebulo, ndi ziwiya zake zonse, choyikapo nyale ndi zipangizo zake, guwa lofukizirapo lubani,
caboi hnopainaw, hmaiimkhok, hmuitui hmaisawinae khoungroe,
28 guwa lansembe yopsereza ndi ziwiya zake zonse, ndiponso beseni pamodzi ndi nsichi yake.
hmaisawi thuengnae khoungroe hoi hnopainaw, kawlung hoi pâhungnae amkhoung pueng hah hote hmuitui hoi koung na hluk han.
29 Zonsezi uzipatule kuti zidzakhale zopatulika, ndipo chilichonse chimene chidzakhudza zimenezi chidzakhala chopatulika.
Kathoung katang e lah ao awh nahan, na thoung sak vaiteh, hote hno ka tek e pueng teh a thoung awh han.
30 “Udzoze Aaroni ndi ana ake aamuna ndi kuwapatula kuti akhale ansembe onditumikira.
Haw hanelah, vaihma thaw tawk laihoi, ka thaw a tawk thai awh nahanelah, Aron hoi a capanaw hah satui na awi vaiteh, na thoung sak han.
31 Tsono awuze a Israeli kuti, mafuta wodzozera awa adzakhala wopatulika mpaka muyaya.
Isarel catounnaw koe, hete satui heh na ca catounnaw koe totouh kaie hluk e satui kathoung lah ao han.
32 Musadzadzozere munthu wamba mafuta amenewa, ndipo musadzapange mafuta wofanana ndi amenewa. Mafutawa ndi wopatulika ndipo akhale woyera kwa inu.
Tami tak dawk na awi mahoeh. Hete sak e hoi saknae kâvan e alouke hai na sak mahoeh. Hethateh a thoung teh, nangmouh hanlah kathounge lah ao han.
33 Wina aliyense amene adzapanga mafuta wonunkhira wofanana nawo kapena kudzozera mafutawa munthu wamba osati wansembe ayenera kuchotsedwa pakati pa anthu anzake.”
Apipatethai het hoi kâvan lah a sak hai thoseh, ayâ alouk hanlah a hno hai thoseh, hote tami teh a miphun dawk hoi na takhoe han telah na dei han telah ati.
34 Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Tenga muyeso wofanana wa zinthu zonunkhira izi: sitakate, onika, galibanumu pamodzi ndi lubani weniweni.
BAWIPA ni Mosi koe a hmui katuipounge hmuitui satacte hoi onycha hoi galbanum hah na la han. Hmuituipoung e ka pâcim e frankinsen hah suekâvan lah na khing vaiteh,
35 Uziphatikize pamodzi zonsezi ndi kupanga lubani monga amachitira mmisiri wopanga zonunkhira. Athire mchere ndipo akhale woyera ndi wopatulika.
hmuitui kasakkungnaw patetlah palawi na phuen vaiteh, ka pâcim lah kathoungcalah na sak han.
36 Upere gawo lina mosalala kwambiri ndipo utapepo pangʼono ndi kuyika patsogolo pa Bokosi la Chipangano mu tenti ya msonkhano, kumene ine ndidzakumane nawe. Lubani ameneyu kwa inu adzakhala wopatulika kwambiri.
A tangawn teh katipcalah phawm hane doeh. Kai ni na pato nahane lukkareiim thung e lawkpanuesaknae hmalah na ta han. Hothateh, nang hanelah kathounge lah ao han.
37 Musapange lubani wanu potsatira njira iyi. Lubani yense wopangidwa mwa njira iyi akhale wopatulika, woperekedwa kwa Yehova.
Hote hmuitui na sak hane na pâtu e patetlah sak e teh, namamouh hanelah na sak mahoeh. BAWIPA hanelah kathounge lah na pouk awh han.
38 Aliyense amene adzapanga wofanana naye kuti asangalale ndi fungo lake ayenera kuchotsedwa pakati pa anthu anzake.”
Tami bangpatet nihai, phunep rumram hanelah hot patet e sak pawiteh, hote tami teh a miphun thung hoi, takhoe lah ao han telah ati.

< Eksodo 30 >