< Eksodo 26 >

1 “Panga chihema pogwiritsa ntchito nsalu khumi zofewa, zosalala ndi zolukidwa bwino, zobiriwira, zapepo ndi zofiira. Ndipo anthu aluso apete pa nsaluzo Akerubi.
“Prebivalište načini od deset zavjesa: od ljubičastog, crvenog i tamnocrvenog prediva i prepredenog lana. Na njima neka budu vezeni likovi kerubina - djelo umjetnika.
2 Nsalu zonse zikhale zofanana. Mulitali mwake zikhale mamita khumi ndi atatu, mulifupi mamita awiri.
Dužina svake zavjese neka je dvadeset i osam lakata, neka joj je širina četiri lakta. Sve zavjese neka su iste mjere.
3 Ulumikize nsalu zisanu kuti ikhale nsalu imodzi. Uchite chimodzimodzi ndi nsalu zisanu zinazo.
Pet zavjesa neka su sastavljene jedna s drugom, a drugih pet zavjesa opet jedna s drugom.
4 Panga zokolowekamo za nsalu yobiriwira mʼmphepete mwa nsalu imodzi yotsiriza ya mbali ina. Uchitenso chimodzimodzi ndi nsalu yotsiriza ya mbali inayo.
Napravi petlje od ljubičaste vune pri rubu krajnje zavjese u sastavljenom komadu.
5 Upange zokolowekamo 50 pa nsalu yoyamba ndi zokolowekamo makumi asanu zinanso pa nsalu inayo. Upange motero kuti zokolowekamozo ziziyangʼanana.
Napravi pedeset petlji na rubu jednoga sastavljenog komada od zavjesa, a pedeset pri rubu drugoga. Neka su petlje načinjene jedna spram druge.
6 Kenaka upange ngowe zagolide makumi asanu zolumikizira nsalu ziwirizo kuti zipange chihema chimodzi.
Onda napravi pedeset kopča od zlata. Zavjese zatim kopčama sastavi jednu s drugom. Tako će Prebivalište biti jedna cjelina.
7 “Upange nsalu za ubweya wambuzi zophimba pamwamba pa chihemacho. Nsalu zonse pamodzi zikhale khumi ndi imodzi.
Načini zatim zavjese od kostrijeti za Šator povrh Prebivališta. Načini ih jedanaest.
8 Nsalu zonse khumi ndi imodzi zikhale zofanana. Mulitali mwake mukhale mamita khumi ndi anayi ndipo mulifupi mwake mukhale mamita awiri.
Neka duljina svake zavjese bude trideset lakata, a širina svake zavjese četiri lakta. Tih jedanaest zavjesa neka bude iste mjere.
9 Ulumikize nsalu zisanu kuti ikhale nsalu imodzi ndipo zina zisanu ndi imodzi uzilumikizenso kuti ikhale nsalu imodzinso. Nsalu yachisanu ndi chimodzi imene ili kutsogolo kwa tenti uyipinde pawiri.
Sastavi pet zavjesa napose, a onda opet drugih šest zavjesa napose. Šestu zavjesu podvostruči na pročelju Šatora.
10 Upange zokolowekamo 50 mʼmphepete mwa nsalu imodzi yotsirizira ya nsalu yoyamba yolumikiza ija. Upangenso zokolowekamo zina 50 mʼmphepete mwa nsalu yotsirizira ya nsalu inanso yolumikiza ija.
Ušij pedeset petlji na rubu jednoga sastavljenog komada od zavjesa, a pedeset na rubu drugoga.
11 Kenaka upange ngowe 50 zamkuwa ndipo uzilowetse mu zokolowekazo. Ndiye uphatikize nsalu ziwirizo kuti tentiyo ikhale imodzi.
Izradi pedeset kopča od tuča, zapni kopče za petlje da sastaviš Šator u cjelinu.
12 Theka lotsalira la nsaluyo lidzalendewera kumbuyo kwa chihemacho.
A kako će zavjese od Šatora pretjecati, neka se polovina zavjesa što preostane spušta na zadnjem dijelu Prebivališta.
13 Nsalu yotsalira ya masentimita 46 mulitali mwake mʼmbali zonse ziwiri idzalendewere kuphimba mbali ziwirizo.
Od onoga što preteče na dužini šatorskih zavjesa neka po jedan lakat visi na obje strane svetoga Šatora da ga zaklanja.
14 Upange chikopa cha nkhosa zazimuna cha utoto wofiira chophimbira tentiyo ndipo pamwamba pake upangireponso chophimbira china cha zikopa za akatumbu.
Napokon napravi Šatoru pokrov od učinjenih i u crveno obojenih ovnujskih koža, a povrh njega pokrov od finih koža.
15 “Upange maferemu amatabwa amtengo wa mkesha oyimikira chihemacho.
Trenice što će nauzgor stajati za Prebivalište napravi od bagremova drva.
16 Feremu iliyonse ikhale yotalika mamita anayi ndipo mulifupi mwake mukhale masentimita 69.
Svaka trenica neka bude deset lakata duga, a lakat i pol široka.
17 Thabwa lililonse likhale ndi zolumikizira ziwiri. Upange maferemu onse a chihemacho ndi matabwa otere.
Svaka trenica neka ima dva klina da je uspravno drže. Tako napravi na svakoj trenici za Prebivalište.
18 Upange maferemu makumi awiri a mbali yakummwera kwa chihemacho.
Trenice za Prebivalište postavi: dvadeset trenica s juga, prema podnevu;
19 Ndipo upange matsinde 40 asiliva ndipo uwayike pansi pa maferemuwo. Pansi pa feremu iliyonse pakhale matsinde awiri ogwiriziza zolumikizira ziwiri zija.
onda pod dvadeset trenica napravi četrdeset podnožja od srebra, dva podnožja pod prvu trenicu za njezina dva klina, i tako redom, dva podnožja za dva klina svake slijedeće trenice.
20 Ndipo mbali yakumpoto ya chihemacho upangenso maferemu makumi awiri.
Za drugu stranu Prebivališta, sa sjevera: dvadeset trenica
21 Upangenso matsinde 40 asiliva, awiri pansi pa feremu iliyonse.
i četrdeset srebrnih podnožja, dva podnožja za dva klina prve trenice, i tako redom, dva podnožja za svaku trenicu.
22 Upange maferemu asanu ndi imodzi a kumbuyo kwa tenti, kumbali yakumadzulo.
Na stražnjoj strani Prebivališta, sa zapada, postavi šest trenica.
23 Ndipo upangenso maferemu awiri a pa ngodya yakumbuyo kwenikweni kwa tenti.
Napravi i dvije trenice za stražnje uglove Prebivališta.
24 Pa ngodya ziwirizi pakhale maferemu awiri, kuyambira pansi mpaka pamwamba ndipo alumikizidwe pa ngowe imodzi. Maferemu onse akhale ofanana.
Neka budu rastavljene pri dnu, ali na vrhu kod prvoga koluta neka budu sastavljene. Neka tako obadvije prave dva ugla.
25 Choncho pakhale maferemu asanu ndi atatu ndiponso matsinde 16 asiliva, awiri akhale pansi pa feremu iliyonse.
Neka dakle bude osam trenica s njihovim srebrnim podnožjima: šesnaest podnožja, dva podnožja pod prvom trenicom, a dva opet podnožja pod svakom slijedećom trenicom.
26 “Upange mitanda ya matabwa amtengo wa mkesha: mitanda isanu ikhale ya maferemu a mbali imodzi ya chihema,
Nadalje napravi priječnice od bagremova drva: pet njih za trenice s jedne strane Prebivališta,
27 mitanda isanu inanso ikhale ya maferemu a mbali inayo. Pakhalenso mitanda ina isanu ya mbali yakumadzulo, kumapeto kwenikweni kwa chihema.
a pet priječnica s druge strane Prebivališta; onda pet priječnica za trenice Prebivališta straga prema zapadu.
28 Mtanda wapakati pa maferemuwo uchokere pa maferemu a mbali ina mpaka mbali inanso.
Srednja priječnica neka ide sredinom trenica s jednoga kraja na drugi.
29 Maferemuwo uwakute ndi golide ndiponso upange mphete zagolide zogwiriziza mitandayo. Ndipo mitandayonso uyikute ndi golide.
Trenice obloži zlatom, a i kolutove za njih, kroz koje će se priječnice provlačiti, načini od zlata. Priječnice onda obloži zlatom.
30 “Upange chihema mofanana ndi momwe ndinakuonetsera pa phiri paja.
Tako, dakle, podigni Prebivalište prema nacrtu koji ti je pokazan na brdu.”
31 “Upange nsalu yokhala ndi mtundu wamtambo, wapepo ndi ofiira ndipo nsaluyo ikhale yolukidwa bwino, yofewa ndi yosalala. Ndipo anthu aluso apetepo zithunzi za Akerubi.
“Napravi zavjesu od ljubičastog, crvenog i tamnocrvenog prediva i prepredenog lana. Neka su na njoj izvezeni kerubini.
32 Nsaluyo uyikoloweke pa nsanamira zinayi zamtengo wa mkesha zokutidwa ndi golide zomwe zili ndi ngowe zagolide, zomwe zayima pa matsinde asiliva anayi.
Objesi je na četiri stupa od bagremova drva, zlatom obložena, s kopčama od zlata, a na četiri podnožja od srebra.
33 Ukoloweke kataniyo ku ngowe ndipo uyike Bokosi la Chipangano mʼkatimo. Kataniyo idzalekanitse malo wopatulika ndi malo wopatulika kwambiri.
Objesi zavjesu za kvake. Onda unesi Kovčeg svjedočanstva tu za zavjesu. Neka ti tako zavjesa odjeljuje Svetište od Svetišta nad svetištima.
34 Uyike chivundikiro pa bokosi laumboni ku malo wopatulika kwambiri.
Stavi Pomirilište na Kovčeg svjedočanstva u Svetinji nad svetinjama.
35 Uyike tebulo kunja kwa katani yotchinga cha kumpoto kwa chihema ndipo uyike choyikapo nyale chija kummwera moyangʼanana ndi tebulolo.
Postavi zatim stol van pred zavjesu, a svijećnjak na južnu stranu Prebivališta, prema stolu. Stol stavi na sjevernu stranu.
36 “Pa chipata cholowera mu chihema, uyikepo nsalu yamtundu wamtambo, wapepo ndi ofiira, yomwe ndi yofewa ndi yosalala, yopetedwa bwino ndi amisiri aluso.
A na ulazu u Šator napravi zastorak od ljubičastog, crvenog i tamnocrvenog prediva i prepredenog lana - vezom izvezen.
37 Upange ngowe zagolide za nsaluyo ndi nsanamira zisanu zamtengo wa mkesha ndipo uzikute ndi golide. Upangenso matsinde asanu amkuwa a nsanamirazo.”
Za zastorak isteši pet stupčića od bagrenova drva pa ih obloži zlatom. Kopče za njih neka budu od zlata. Salij za njih pet podnožja od tuča.”

< Eksodo 26 >