< Eksodo 20 >

1 Ndipo Mulungu anayankhula mawu onse awa nati:
Hat navah, Cathut ni a dei e lawk teh,
2 “Ine ndine Yehova Mulungu wako amene ndinakutulutsa ku Igupto, mʼdziko la ukapolo.
Kai teh nangmouh santoungnae hmuen, Izip ram dawk hoi na ka tâcawtkhai e nangmae Cathut Jehovah doeh.
3 “Usakhale ndi milungu ina koma Ine ndekha.”
Kai hloilah alouke cathut na bawk awh mahoeh.
4 “Usadzipangire chofanizira chinthu chilichonse chakumwamba kapena cha pa dziko lapansi kapena cha mʼmadzi a pansi pa dziko.
Lathueng kalvan thoseh, rahim talai dawk thoseh, talai rahim tui dawk thoseh, kaawm e hno hoi mei kâvan lah, meikaphawk bawk hanlah na sak mahoeh.
5 Usazigwadire kapena kuzipembedza, pakuti Ine Yehova Mulungu wako, ndine Mulungu wansanje, wolanga ana chifukwa cha tchimo la makolo awo mpaka mʼbado wachitatu ndi wachinayi wa iwo amene amadana nane.
A hmalah tabo hoi na bawk mahoeh. Bangkongtetpawiteh, nange Cathut kai Jehovah teh nang dawk yon ao telah tang ka yuem e Cathut, kai na kahmuhmanaw e ca catoun se thum, se pali totouh a napanaw e yon hah a capanaw koe ka pathung e Cathut lah ka o.
6 Koma ndimaonetsa chikondi chosasinthika ku mibado miyandamiyanda ya anthu amene amandikonda, ndi kusunga malamulo anga.
Kai hah lungpataw ni teh ka kâpoelawknaw ka tarawi e a ca catoun, a se thongsang totouh lungmanae ka kamnuek sak e Cathut lah ka o.
7 “Usagwiritse ntchito molakwika dzina la Yehova Mulungu wako, pakuti Yehova adzamutenga kukhala wochimwa aliyense amene akugwiritsa ntchito dzina lakelo molakwika.
Nange Cathut Jehovah e min hah laithoe lah dei awh hanh. Bangkongtetpawiteh, A min laithoe lah ka dei e tami teh yon tawn hoeh telah BAWIPA ni pouk mahoeh.
8 “Uzisunga tsiku la Sabata kuti likhale lopatulika.
Sabbath hnin thoung sak hanelah, hote hnin hah pahnim awh hanh.
9 Uzigwira ntchito zako zonse masiku asanu ndi limodzi.
Hnin taruk touh thung thaw panki hoi tawk awh.
10 Koma tsiku lachisanu ndi chiwiri ndi Sabata, tsiku loperekedwa kwa Yehova Mulungu wako. Tsiku limeneli musagwire ntchito iliyonse, inuyo kapena mwana wanu wamwamuna kapena mwana wanu wamkazi, wantchito wanu wamwamuna kapena mdzakazi wanu, ziweto zanu kapena mlendo amene akukhala mʼmudzi mwanu.
Hnin sari hnin teh na BAWIPA Cathut e Sabbath hnin lah ao. Hote hnin dawk, nang hoi na canaw, na sannu sanpanaw, saring, nange longkha thung kaawm e imyinnaw hai thaw tawk awh mahoeh.
11 Pakuti Yehova anapanga kumwamba ndi dziko lapansi, nyanja ndi zonse zimene zili mʼmenemo mʼmasiku asanu ndi limodzi. Iye anapuma pa tsiku lachisanu ndi chiwiri. Kotero Yehova anadalitsa tsiku la Sabata kuti likhale loyera.
Bangkongtetpawiteh, BAWIPA ni kalvan, talai, hmuen pueng koe kaawmnaw pueng hah hnin taruk touh thung a sak teh, hnin sari hnin nah, a kâhat. Hatdawkvah, BAWIPA ni hnin sari hnin hah yawhawi a poe teh a thoungsak.
12 “Lemekeza abambo ako ndi amayi ako kuti ukhale ndi moyo wautali mʼdziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa.
Na Cathut Jehovah ni na poe e ram dawk na hringsaw nahanelah, na manu hoi na pa barih.
13 “Usaphe.
Tami thet hanh.
14 “Usachite chigololo.
Uicuk hanh.
15 “Usabe.
Ayâ e hno parawt hanh.
16 “Usapereke umboni womunamizira mnzako.
Na imri koe kalan hoeh e kapanuekkhaikung lah awm hanh.
17 “Usasirire nyumba ya mnzako. Usasirire mkazi wa mnzako kapena wantchito wake wamwamuna kapena mdzakazi wake, ngʼombe yake kapena bulu wake, kapena chilichonse cha mnzako.”
Imri e im, a yu, a sannu sanpa, maito, marang hoi hnopai buet touh haiyah lungthin radueknae tawn hanh telah atipouh.
18 Pamene anthu ankamva mabingu ndi kuona ziphaliwali ndi kumvanso lipenga ndi kuona utsi umene umafuka mʼphiri, ananjenjemera ndi mantha. Ndipo iwo anayima patali.
Taminaw ni keitat lawk, sumpapalik, mongka ueng lawk, mon hoi hmaikhu a tâco e naw hah a hmu awh toteh, a taki awh dawkvah, a kâhnawn awh teh ahlanae koe vah a kangdue awh.
19 Ndipo anati kwa Mose, “Iwe utiyankhule ndipo tidzamvera. Koma usalole kuti Mulungu atiyankhule, tingafe.”
Mosi koevah Nang ni lawk dei lah ka ngai awh han. Kaimouh koe Cathut lawk dei han naseh. Kaimouh ka due hane hah puen ao telah atipouh.
20 Koma Mose anati kwa anthuwo, “Musachite mantha. Mulungu wabwera kudzakuyesani kuti mukhale ndi mtima woopa Mulungu kuti musamuchimwire.”
Mosi ni hai na lungpuen awh hanh. Nangmouh tanouk hanelah thoseh, nangmouh teh sak payonnae dawk hoi hlout hanelah ama taki hanelah thoseh, Cathut a tho toe telah taminaw koe a dei pouh.
21 Anthu aja anayima patali koma Mose anayandikira mtambo wakuda kumene kunali Mulungu.
Taminaw ni ahlanae koe vah a kangdue awh. Mosi teh Cathut onae koe kinghmonae koe lah a hnai.
22 Ndipo Yehova anati kwa Mose, “Awuze izi Aisraeli: ‘Inu mwaona nokha kuti Ine ndakuyankhulani kuchokera kumwamba.
BAWIPA ni Isarelnaw bout a dei pouh e teh, kai ni kalvan hoi nangmouh na pato e hah na panue awh toe.
23 Choncho musadzipangire milungu yasiliva kapena yagolide kuti muziyipembedza pamodzi ndi Ine.’”
Kai bawknae dawk namamouh hno hanlah ngun cathut thoseh, sui cathut thoseh na sak awh mahoeh.
24 Mundimangire guwa ladothi ndipo muziperekapo nsembe zopsereza ndi nsembe zachiyanjano, nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe zanu. Pamalo paliponse pamene Ine ndidzakonza kuti muzinditamandirapo, ndidzabwera ndi kukudalitsani.
Kai hanelah talai khoungroe hah na sak awh han. Hote khoungroe dawk nange hmaisawi sathei, yonthanae sathei lah kaawm e nange tu, maitonaw hah na thueng awh han. Ka min na bawknae hmuen pueng dawk nang koe ka tho vaiteh yawhawinae na poe han.
25 Ngati mudzandimangira guwa lansembe lamiyala, musagwiritse ntchito miyala yosema, pakuti mudzalidetsa mukadzagwiritsa ntchito zida.
Nang ni talung khoungroe hah kai hanlah na sak pawiteh, talung dei e hoi na sak mahoeh. Sum hoi thuk e talung hoi sak e khoungroe teh khinnae ao.
26 Musamakwere pa makwerero popita pa guwa langa lansembe kuti mungaonetse maliseche anu.
Nang dawk kayanae ao hoeh nahanelah, khoungroe dawk khalai hoi na luen mahoeh telah ati.

< Eksodo 20 >