< Eksodo 18 >
1 Yetero wansembe wa ku Midiyani amenenso anali mpongozi wa Mose, anamva zonse zimene Mulungu anachitira Mose ndi anthu ake a Aisraeli ndi mmene Yehova anawatulutsira mʼdziko la Igupto.
Midyanaaşine kaahinık'le, Mısayne abatteyk'le İtronuk'le Allahee Mısayneyiy İzrailybışdemee hı'iyn karbıyiy Rəbbee manbı Misirğançe qığav'uy g'iyxhe.
2 Mose atamubweza Zipora, mkazi wake, Yetero, mpongozi wake anamulandira
Mısayne abattee İtronee Mısayna xhunaşşe Tsipporayiy q'ööle uşax yı'q'əlqa qıkkeka. Mısee ögiylycarniy cuna xhunaşşe dekkıne k'anyaqa g'axiyvu. Mısee «Zı menne cigee, merna xhinne ıxhava» uvhu, dixbışde sang'un do Gerşomniy (menne cigayna) gixhxhı.
3 mwana wake wamkaziyo pamodzi ndi ana ake aamuna awiri. Mose anamupatsa mwana wachisamba dzina loti Geresomu popeza anati, “Ndakhala mlendo mʼdziko lachilendo.”
4 Ndipo mwana wake wachiwiri anamupatsa dzina loti Eliezara, pakuti anati, “Mulungu wa makolo anga anali thandizo langa. Iye anandipulumutsa ku lupanga la Farao.”
«Dekkee ı'bəədat hı'iyne Allahee zas kumag hı'ı, fironne g'ılıncıke g'attixhan hı'ıva» uvhu, mansang'unud do Eliyezerniy (Allahee zas kumag ha'a) gixhxhı.
5 Yetero, mpongozi wa Mose pamodzi ndi ana a Mose aamuna awiri ndi mkazi wake anabwera kwa Mose ku chipululu pa phiri la Mulungu kumene Mose anamanga misasa.
Mısayna abattey İtron, dixbışikayiy xhunaşşeyka sacigee sahreeqa Mısa eyxhene Allahne suvaysqa arayle.
6 Yetero anali atatumiza uthenga kwa Mose kuti, “Ine Yetero, mpongozi wako, ndikubwera ndi mkazi wako ndi ana ake awiri.”
İtronee Mısayk'le eyhecenva insan g'ıxele: – Zı yiğna abattey İtron xhunaşşeykayiy q'öne yiğne duxayka vasqa ı'qqə vor.
7 Kotero Mose anatuluka kukakumana ndi mpongozi wake ndipo anawerama ndi kupsompsona. Atalonjerana anakalowa mu tenti
Mısa abbateysqa qığeç'u mang'une ögiyl k'yorzul, ubba ha'a. Sana-sang'uke qidghınbı ha'a manbı çadıreeqa ikkebaç'e.
8 Mose anafotokozera mpongozi wake zonse zimene Yehova anamuchita Farao ndi Aigupto chifukwa cha Israeli komanso zowawa zonse anakumana nazo mʼnjira. Mose anafotokozanso momwe Yehova anawapulumutsira.
Mısee abatteys, Rəbbee İzrailybışdemee fironulqayiy Misirbışilqa alli'iyn yiğbı, co yəqqə opxhunna əq'üba, sayib Rəbbee co nəxübiy g'attivxhan hav'uva yuşan ha'a.
9 Yetero anakondwa kwambiri atamva zabwino zonse zimene Yehova anachitira Aisraeli powapulumutsa mʼdzanja la Aigupto.
İtron Rəbbee İzrailybışis yugvalla hav'uva, manbı Misirbışde xılençe g'attivxhan hav'uva geer şadexhena.
10 Iye anati, “Alemekezeke Yehova amene wakupulumutsani mʼdzanja la Aigupto ndi Farao. Wapulumutsanso anthuwa mʼdzanja la Aigupto.
Mang'vee eyhen: – Şu fironneyiy Misirbışde xılençe g'attivxhan hav'une Rəbbis şukur vuxhena!
11 Tsopano ndikudziwa kuti Yehova ndi wopambana milungu ina yonse, pakuti anachita izi kwa amene ananyoza Israeli.”
Həşde zak'le ats'an Rəbb manisa allahaaşile nimeexheyir xərra vor. Mang'vee millet hooyç'an-g'oyç'anne Misirbışde xılençe g'attixhan hı'ı.
12 Ndipo Yetero, mpongozi wa Mose anapereka nsembe yopsereza ndi nsembe zina kwa Mulungu. Aaroni ndi akuluakulu onse a Israeli anabwera kudzadya chakudya pamodzi ndi mpongozi wa Mose pamaso pa Mulungu.
Qiyğa Mısayne abattee İtronee, Allahıs medın-medın q'urbanbı allya'a. Haruniy İzrailybışin ağsaqqalar, Mısaykayiy cune abatteyka sacigee Allahne ögee gıney oxhanas abayle.
13 Mmawa mwake, Mose anakhala pa mpando kuti aweruze milandu ya anthu. Anthu anayima momuzungulira kuyambira mmawa mpaka madzulo.
Qinne yiğıl Mısa milletne məhkamayqa ilyakka. Milletıd miç'eediyle exhalqamee Mısayne hiqiy-alla iliyk'ar ıxha.
14 Mpongozi wa Mose ataona zonse zimene iye amawachitira anthu anati, “Nʼchiyani chimene mukuwachitira anthuwa? Nʼchifukwa chiyani mulipo nokha woweruza, pamene anthu onsewa ayimirira kuyambira mmawa mpaka madzulo?”
Mısayne abatteyk'le mang'vee milletık ha'an g'acumee, eyhen: – Ğu hucoone milletık ha'a? Nya'a ğu sayrena məhkama ha'a, nya'a manimeen millet yiğne hiqiy-alla miç'eediyle exhalqamee iliyk'ar axu?
15 Mose anamuyankha kuti, “Chifukwa anthuwa anabwera kwa ine kudzafunsa zimene Mulungu akufuna.
Mısee eyhen: – Millet zasqa Allahee eyhen ats'axhxhes adayle.
16 Ngati munthu akangana ndi mʼbale wake, onse awiri amabwera kwa ine, ndipo ine ndimawaweruza. Ndimawawuzanso malamulo a Mulungu ndi malangizo ake.”
İnsanar sana-sang'uka parxaçeepxhamee, zasqa abayle. Zınad manbışde neng'uqa nena bınahiyva eyhe. Sayid zı manbışis Allahne g'ayda-q'aanunbışike yuşan ha'a.
17 Mpongozi wa Mose anayankha kuti, “Zimene mukuchitazi si zabwino.
Abattee Mısayk'le eyhen: – Ğu man qotkuda deşod ha'a.
18 Ntchitoyi ndi yayikulu kuposa mphamvu zanu. Inu simungathe kuyigwira nokha. Inu pamodzi ndi anthuwa amene amabwera kwa inu mudzatopa.
Ğunar, vasqa abaylenbıb mançike saccu oozaranbı. Sang'unemee mana geeb yı'q'na işib. Vassecab mana iş haa'as vəxəs deş.
19 Tsono tamverani ndikulangizeni, ndipo Mulungu akhale nanu. Inu muziwayimirira anthuwa pamaso pa Mulungu, ndipo mikangano yawo muzibwera nayo kwa Iye.
Ğu zal yugda k'ırı gyaqqe, zı vak'le həşde sa kar eyhes. Hasre Allahır vaka ixhecen! Allahneyiy milletne yı'q'nena ixhe, milletın nyaabiy dağamiyvalla opxhan, ğu Mang'us yuşan he'e.
20 Aphunzitseni mawu ndi malangizo a Mulungu. Aphunzitseni mmene ayenera kukhalira ndi zimene ayenera kuchita.
Manbışik'le g'ayda-q'aanun, ha'asın işbı, qopkuna yəq haagve.
21 Koma sankhani amuna odziwa ntchito yawo, anthu owopa Mulungu, anthu odalirika amene amadana ndi kupeza phindu mwachinyengo. Tsono muwayike kuti akhale oyangʼanira anthu motere: atsogoleri a anthu 1,000, ena a anthu 100, ena a anthu 50 ndi ena a anthu khumi.
Milletıke kar əxən, Allahıle qəvəyq'ənan, cuvabıl ulyoozaran, pılıka alivşes dyooxhen insanar g'əvxe. Manbı aazırıng'us, vəşing'us, xhots'aling'us, yıts'ıng'us ç'ak'ınbı xhinne gyuvxhe.
22 Tsono amenewa aziweruza anthu nthawi zonse. Mlandu uliwonse waukulu azibwera nawo kwa inu, koma mlandu waungʼono aziweruza okha. Izi zidzachititsa kuti ntchito yanu ipepuke, popeza mudzagwira ntchito mothandizana.
Manbışe məhkamabı he'ecen. Cosse ha'as əxən işbı hasre cocad he'ecen, dağamınbıd, dəxənbıd vasqa allecen. Məxüd manbışe vas kumag ha'as, valqa gyooxhana işib k'ıl quvxhes.
23 Ngati mutsatira malangizowa monga mmene Mulungu wakulamulirani ndiye kuti simudzafowoka ndipo anthu onsewa adzapita kwawo mu mtendere.”
Ğu məxüd he'eene, Allahısıd man ıkkiykıneene, vasse örxəs əxəsda. Milletıd yik' sibık qı'ı xaaqa siyk'alıy.
24 Mose anamvera mpongozi wake ndi kuchita zonse zimene iye ananena.
Mısee abattel k'ırı alixhxhı, mang'vee eyhen xhineyid ha'an.
25 Iye anasankha amuna odziwa bwino ntchito zawo ndipo anawayika kuti akhale atsogoleri, oyangʼanira anthu motere: atsogoleri a anthu 1,000, ena a anthu 500, ena a anthu makumi asanu ndi ena a anthu khumi.
Mısee İzrailybışde əreençe kar əxənbı g'əvxü, milletıs ç'ak'ınbı xhinne giviyxhe. Manbışike aazırıng'us, vəşing'us, xhots'aling'us, yıts'ıng'us ç'ak'ınbı vooxhe.
26 Iwowa ankaweruza anthu nthawi zonse. Milandu yovuta ankabwera nayo kwa Mose, koma yosavuta ankayiweruza okha.
Mane yiğile otçu manbışe milletıs məhkamabıd ha'a ıxha. Manbışe cosse əxən işbı cocad ha'a ıxha, dağamınbı, dəxənbı Mısaysqa adayle ıxha.
27 Kenaka Mose analola kuti mpongozi wake, Yetero anyamuke kubwerera ku dziko la kwawo.
Qiyğa Mısee cuna abattey yəqqılqa araççe. Abatteyir siyk'alna cune ölkeeqa.