< Eksodo 11 >

1 Tsopano Yehova anati kwa Mose, “Ine ndidzalanga Farao pamodzi ndi Aigupto onse ndi mliri umodzi wotsiriza. Zikadzachitika izi iye adzakulolani kuti mutuluke mʼdziko lino. Ndithu pamene azidzakutulutsani adzachita ngati akukuyingitsani.
Derpå sagde HERREN til Moses: "Een Plage endnu vil jeg lade komme over Farao og Ægypterne, og efter den skal han lade eder rejse herfra; ja, når han lader eder rejse med alt, hvad I har, skal han endog drive eder herfra!
2 Awuze anthu kuti mwamuna aliyense ndi mkazi aliyense apemphe kwa mnansi wake ziwiya zasiliva ndi golide.”
Sig nu til Folket, at hver Mand skal bede sin Nabo, og hver Kvinde sin Naboerske om Sølv og Guld smykker!"
3 Tsono Yehova anachititsa Aigupto kuti akomere mtima Aisraeli. Komanso Mose anali wotchuka kwambiri mʼdziko la Igupto, pamaso pa nduna za Farao ndi anthu onse.
Og HERREN stemte Ægypterne gunstigt imod Folket, og desuden var den Mand Moses højt anset i Ægypten både hos Faraos Tjenere og hos Folket.
4 Tsono Mose anawuza Farao kuti, “Pakati pa usiku, Yehova adzayenda pakati pa anthu a ku Igupto.
Moses sagde: "Så siger HERREN: Ved Midnatstid vil jeg drage igennem Ægypten,
5 Ndipo mwana aliyense wamwamuna wachisamba adzafa, kuyambira mwana wamwamuna wa Farao amene amakhala pa mpando waufumu, mpaka mwana wamwamuna wachisamba wa mdzakazi wake amene ali naye pa mtondo, komanso ana oyamba a ziweto.
og så skal alle førstefødte i Ægypten dø, lige fra den førstefødte hos Farao, der skal arve hans Trone, til den førstefødte hos Trælkvinden, der arbejder ved Håndkværnen, og alt det førstefødte af Kvæget.
6 Kudzakhala kulira kwakukulu mʼdziko lonse la Igupto, kumene sikunachitikepo ndipo sikudzachitikanso.
Da skal der i hele Ægypten lyde et Klageskrig så stort, at dets Lige aldrig har været hørt og aldrig mere skal høres.
7 Koma pakati pa Aisraeli, ngakhale galu sadzawuwa munthu aliyense kapena chiweto!” Kotero mudzadziwa kuti Yehova ndiye wasiyanitsa pakati pa Igupto ndi Israeli.
Men end ikke en Hund skal bjæffe ad nogen af Israeliterne, hverken ad Folk eller Fæ for at du kan kende, at HERREN gør Skel mellem Ægypterne og Israel.
8 Nduna zanu zonse zidzabwera kwa ine, kugwada pamaso panga ndi kunena kuti, “Pita iwe ndi anthu ako onse amene akukutsatirawa! Zimenezi zikadzachitika ine ndidzachoka.” Ndipo Mose anachoka kwa Farao atakwiya kwambiri.
Da skal alle dine Tjenere der komme ned til mig og kaste sig til Jorden for mig og sige: Drag dog bort med alt det Folk, der følger dig! Og så vil jeg drage bort!" Og han gik ud fra Farao med fnysende Vrede.
9 Yehova ananena kwa Mose kuti, “Farao adzakana kukumvera, kuti zodabwitsa zanga zichuluke mʼdziko la Igupto.”
Men HERREN sagde til Moses: "Farao skal ikke høre på eder, for at mine Undergerninger kan blive talrige i Ægypten."
10 Mose ndi Aaroni anachita zodabwitsa zonsezi pamaso pa Farao koma Yehova anawumitsa mtima wa Farao, ndipo sanalole kuti Aisraeli atuluke mʼdziko lake.
Og Moses og Aron gjorde alle disse Undergerninger i Faraos Påsyn, men HERREN forhærdede Faraos Hjerte, så han ikke lod Israeliterne drage ud af sit Land.

< Eksodo 11 >