< Eksodo 10 >

1 Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Pita kwa Farao, pakuti Ine ndawumitsa mtima wake ndi mitima ya nduna zake kuti ndichite zizindikiro zozizwitsa pakati pawo
Amalalu, Hina Gode da Mousesema amane sia: i, “Felou ba: la masa! Na da e amola ea eagene ouligisu dunu ilia dogo ga: nasi agoane hamoi. Bai Na da ilia gilisisu ganodini musa: hame ba: su gasa bagade hou hamomusa: dawa: lala.
2 kuti inu mudzawuze ana ndi zidzukulu zanu za mmene ndinawakhawulitsira Aigupto ndi zizindikiro zozizwitsa zimene ndinachita pakati pawo ndiponso kuti inu mudziwe kuti ine ndine Yehova.”
Bai eno da dilia fa: no dilia mano amola aowa ilima Na da musa: hame ba: su hou hamobeba: le, Idibidi dunu da gagaoui dunu agoane ba: i, amo dilia da diligaga fi ilima olelemu. Dilia huluane da Na da Hinadafa amo dawa: mu.”
3 Ndipo Mose ndi Aaroni anapita kwa Farao ndi kukanena kuti, “Yehova Mulungu wa Ahebri, akuti: ‘Kodi udzakanabe kudzichepetsa pamaso panga mpaka liti? Alole anthu anga apite kuti akandipembedze.
Amaiba: le, Mousese amola Elane da Felouma asili, amane sia: i, “Hibulu dunu ilia Hina Gode da amane sia: sa, ‘Di da habogala Na sia: nabima: bela: ? Di da Na fi dunu Nama nodone sia: ne gadoma: ne amo fisidigima.
4 Ngati ukana kuwalola, ndigwetsa dzombe mʼdziko lako lino mawa.
Be di da higasea Na da aya danuba: dilima se nabasu ima: ne asunasimu.
5 Dzombeli lidzakuta nthaka yonse moti sidzaoneka konse. Lidzadya kalikonse kakangʼono kamene sikanawonongedwe ndi matalala aja, kuphatikizapo mitengo yonse imene ikumera mʼminda yanu.
Danuba: da bagohamedafa ba: mu. Ilia da osobo huluane dedebomu. Ilia da liligi huluane amo mugene da hame gugunufinisi amola ifa huluane hame wadela: lesi amo na dagomu.
6 Dzombeli lidzadzaza nyumba zako ndi za nduna zako ndiponso za Aigupto onse, chinthu chimene ngakhale makolo anu kapena makolo awo sanachionepo kuyambira tsiku limene anakhala mʼdzikoli mpaka lero.’” Ndipo Mose ndi Aaroni anatembenuka ndi kumusiya Farao.
Ilia dia diasu amola dia ouligisu dunu ilia diasu huluane nabamu. Ilia dilima se nabasu imunu da dilia musa: ba: i liligi huluane baligimu.’” Amo sia: nanu, Mousese da Felou yolesili asi.
7 Nduna za Farao zinamufunsa kuti, “Kodi munthu uyu adzativutitsa mpaka liti? Aloleni anthuwa apite, kuti akapembedze Yehova Mulungu wawo. Kodi simukuona kuti dziko la Igupto lawonongeka?”
Felou ea eagene ouligisu dunu ilia da ema amane sia: i, “Amo dunu da habowali seda ninima se nabasu ima: bela: ? Di Isala: ili dunu ilia Hina Godema nodone sia: ne gadomusa: fisidigima. Ninia Idibidi soge da gugunufinisi dagoi.”
8 Choncho Mose ndi Aaroni anayitanidwanso kwa Farao ndipo anati, “Pitani kapembedzeni Yehova Mulungu wanu. Koma ndani amene adzapite?”
Amaiba: le, ilia da Mousese amola Elane amo Felouma oule misi. Felou da elama amane sia: i, “Defea! Dilia da dilia Hina Godema sia: ne gadomusa: masunu da defea. Be nowa da masa: bala: ?”
9 Mose anayankha kuti, “Ife tidzapita tonse pamodzi; angʼonoangʼono ndi akuluakulu, ana athu aamuna ndi aakazi, ndiponso ziweto zathu ndi ngʼombe chifukwa tikakhala ndi chikondwerero cha kwa Yehova.”
Mousese da amane adole i, “Ninia huluane, dunu, uda, mano amola da: i hamoi da masunu. Ninia da ninia dunu mano, ninia uda mano, ninia sibi, goudi amola bulamagau huluane oule masunu. Bai ninia da lolo nasu gilisisu Hina Godema nodomusa: hamomu.”
10 Farao anati, “Yehova akhale ndi inu ngati ndingakuloleni kupita pamodzi ndi akazi ndi ana anu! Zikuoneka kuti mwakonzeka kuchita choyipa.
Felou da amane sia: i, “Na da Hina Gode Ea Dioba: le gasa bagade sia: sa. Dilia da dilia uda amola mano hamedafa oule masunu. Ninia ba: i dagoi. Dilia da odoga: su hou hamomusa: dawa: lala.
11 Ndakana! Amuna okha ndiwo apite ndi kukapembedza Yehova pakuti izi ndi zimene mwakhala mukupempha.” Kenaka Mose ndi Aaroni anathamangitsidwa pamaso pa Farao.
Hame mabu! Dilia amo hanai galea, dunu fawane da dilia Hina Godema nodone sia: ne gadomusa: masa!” Amo sia: beba: le, Idibidi dunu da Mousese amola Elane ela Felou fisimusa: , gadili sefasi.
12 Ndipo Yehova anati kwa Mose, “Tambalitsa dzanja lako pa dziko la Igupto kuti dzombe lidze pa dziko la Igupto ndi kuwononga chilichonse chimene chikumera mʼminda ndi chilichonse chimene chinatsala pa nthawi ya matalala.”
Amalalu, Hina Gode da Mousesema amane sia: i, “Danuba: misa: ne sia: musa: , dia lobo amo Idibidi soge da: iya amoga ligia gadoma. Ilia da misini, liligi huluane mugene amoga hame gugunufinisi, amo ilia da na dagomu.
13 Kotero Mose anakweza ndodo yake pa dziko la Igupto, ndipo Yehova anawutsa mphepo ya kummawa imene inawomba pa dziko usana ndi usiku wonse. Mmene kumacha nʼkuti mphepoyo itabweretsa dzombe.
Amaiba: le, Mousese da ea dagulu ligia gadole, Hina Gode da fo amo gusudili misi da amo eso amola gasi ganodini Idibidi sogega fofosu. Hahabe aya danuba: foga gaguli misi doaga: i dagoi ba: i.
14 Dzombelo linafika pa dziko lonse la Igupto ndi kukhala dera lililonse la dzikolo. Dzombe lambiri ngati limenelo silinakhaleponso nʼkale lonse ndipo silidzakhalapo ngakhale mʼtsogolo.
Ilia da gilisisu osea: le misi amola soge huluane dedeboi dagoi. Ilia idi bagadedafa amo da musa: hame ba: su amola amo defele bu hamedafa ba: mu.
15 Dzombelo linaphimba nthaka yonse mpaka kuoneka kuti bii. Linadya zonse zimene zinatsala nthawi ya matalala, zomera za mʼmunda ndi zipatso. Panalibe chobiriwira chilichonse chimene chinatsala pa mtengo kapena pa chomera chilichonse mʼdziko lonse la Igupto.
Ilia da osobo huluane dedeboiba: le, osobo da bunumai agoane ba: i. Ilia da liligi huluane amo mugene da hame gugunufinisi amola ifa fage dialu huluane na dagoi. Mola: ya: i liligi amo ifa o gisi da: iya Idibidi soge ganodini da hamedafa ba: i.
16 Mwamsangamsanga, Farao anayitanitsa Mose ndi Aaroni ndipo anati, “Ine ndachimwira Yehova Mulungu wanu ndiponso inu.
Amalalu, Felou da hedolowane Mousese amola Elane ema misa: ne sia: i. E da elama amane sia: i, “Na da Hina Gode amola alima wadela: le hamoi dagoi.
17 Tsopano ndikhululukirenso tchimo langa kano konkha ndipo pempherani kwa Yehova Mulungu wanu kuti andichotsere mliri wosakazawu.”
Be wali afadafa fawane na wadela: i hou gogolema: ne olofoma. Ali Hina Godema E da amo bogosu se nabasu fadegale fasima: ne sia: ma.
18 Mose anachoka kwa Farao nakapemphera kwa Yehova.
Mousese da Felou yolesili asili, Hina Godema sia: ne gadoi.
19 Ndipo Yehova anasintha mphepo ija kuti ikhale ya mphamvu yochokera ku madzulo, ndipo inanyamula dzombe lija nʼkulikankhira mʼNyanja Yofiira. Panalibe dzombe ndi limodzi lomwe limene linatsala mu Igupto.
Amalalu, Gode da gusudili mabe fo afadenene, bu guma: dini mabe fo hamoi. Amo da danuba: fi huluane lale Suese (Gulf) amo foga mini asi. Danuba: afadafa da Idibidi soge ganodini esalebe hame ba: i.
20 Koma Yehova anawumitsa mtima wa Farao, ndipo sanalole kuti Aisraeli apite.
Be Hina Gode da Felou ea hou bu ga: nasi hamone, e da Isala: ili dunu hame fisidigi.
21 Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Tambasulira dzanja lako kumwamba kuti kukhale mdima umene udzaphimba dziko lonse la Igupto, mdima wandiweyani.”
Amalalu, Hina Gode da Mousesema amane sia: i, “Dia lobo muagado ligia gadoma. Amasea, gasi dunasi bagadedafa da Idibidi soge huluane dedebomu.”
22 Choncho Mose anakweza dzanja lake kumwamba ndipo mdima wandiweyani unaphimba dziko lonse la Igupto kwa masiku atatu.
Mousese da ea lobo muagado ligia gadole, gasi dunasi bagadedafa da Idibidi soge ganodini eso udianaga dialebe ba: i.
23 Palibe amene anatha kuona mnzake kapena kuchoka pa khomo pake kwa masiku atatu. Koma kumalo kumene kumakhala Aisraeli kunali kowala.
Idibidi dunu huluane da ilia na: iyado dunu ba: mu gogolei amola amo eso udianaga ilia da diasu fisili gadili masunu hamedei ba: i. Be Isala: ili dunu ilia esalebe soge ganodini hadigi galebe ba: i.
24 Kenaka Farao anayitanitsa Mose ndi Aaroni nati, “Pitani kapembedzeni Yehova. Ngakhale akazi ndi ana anu apite pamodzi ndi inu. Koma musatenge ziweto zanu ndi ngʼombe zanu.”
Felou da Mousese ema misa: ne sia: i. E da ema amane sia: i, “Defea! Di da Hina Godema nodone sia: ne gadomusa: masunu da defea. Dilia uda amola mano masunu da defea. Be dilia sibi, goudi amola bulamagau da guiguda: esaloma: mu.”
25 Koma Mose anati, “Ndiye inu mutipatse nsembe zopsereza zoti tikapereke kwa Yehova Mulungu wathu.
Be Mousese da bu adole i, “Agoane hamomu ganiaba, di da ninima ohe fi ninia Hina Godema gobele salasu hamoma: ne ia: noba.
26 Koma ayi, ife tipita ndi ziweto zathu. Palibe chiweto chilichonse chimene chitatsale kuno, popeza tikasankha komweko ziweto zokapembedzera Yehova. Sitingadziwe zimene tikagwiritse ntchito popembedza Yehova mpaka titakafika kumeneko.”
Hame mabu! Ninia ahoasea ninia da ohe fi huluane amola oule masunu. Ninisu da Hina Godema nodomusa: , ohe fi afae afae amo ilegema. Amola ninia da Hina Godema gobele salasu sogebi amoga doaga: sea fawane, ohe fi ilegemusa: dawa: mu.”
27 Koma Yehova anawumitsa mtima wa Farao ndipo sanafune kuwalola kuti apite.
Hina Gode da Felou ea dogo bu ga: nasi hamoi amola e da Isala: ili fi fisidigimu higa: i.
28 Farao anati kwa Mose, “Choka pamaso panga! Uwonetsetse kuti usadzaonekerenso pamaso panga! Tsiku limene ndidzakuonenso udzafa.”
E da ougili Mousesema amane sia: i, “Dia odagi na siga mae ba: ma: ne, masa! Na da di bu ba: mu higa: i gala mabu! Eso enoga na da di bu ba: sea, di da bogomu!”
29 Mose anayankha kuti, “Monga momwe mwaneneramu, Ine sindidzaonekeranso pamaso panu.”
Mousese da bu adole i, “Di da dafawane sia: i dagoi! Di da na hamedafa bu ba: mu.”

< Eksodo 10 >