< Estere 6 >

1 Usiku umenewo mfumu inalephera kugona tulo; Choncho inayitanitsa buku limene amalembamo mbiri ya zamakedzana kuti amuwerengere.
Uti den samma nattene kunde Konungen intet sofva, och lät hemta Chrönicor och Historier; och de vordo läsna för Konungenom.
2 Anapeza kuti mʼbukumo munalembedwa zoti Mordekai anawulula kuti Bigitana ndi Teresi, awiri mwa adindo ofulidwa a mfumu amene ankalondera pa khomo la chipinda cha mfumu ndiwo anakonza chiwembu chofuna kupha mfumu Ahasiwero.
Då råkade man der uppå, der skrifvet var, huru Mardechai hade gjort förvaring, att de två Konungens kamererare, Bigthan och Theres, som vaktade vid dörrena, hade i sinnet slå uppå Konungen Ahasveros.
3 Mfumu inafunsa kuti, “Kodi Mordekai anamupatsa ulemu ndi ukulu wotani chifukwa cha chinthu chimene anachitachi?” Atumiki ake anamuyankha kuti, “Palibe chimene chinachitika kwa iye.”
Och Konungen sade: Hvad hafve vi gjort Mardechai till äro och lön derföre? Då sade Konungens svenner, som honom tjente; Honom är intet skedt.
4 Mfumu inati, “Kodi ndani ali mʼbwalomo?” Tsono Hamani anali atangolowa kumene mʼbwalo lakunja la nyumba yaufumu kuti akawuze mfumu zomukhomera Mordekai pa mtanda umene anamukonzera.
Och Konungen sade: Ho är der i gårdenom? Ty Haman var kommen i gården, utanför Konungshuset, att han skulle säga Konungenom om Mardechai, att han måtte hänga i galganom, som han honom tillredt hade.
5 Atumiki ake anamuyankha kuti, “Hamani ndiye wayima mu bwalo.” “Mulowetseni,” Mfumu inalamulira.
Och Konungens svenner sade till honom: Si, Haman står ute på gårdenom. Konungen sade: Låt honom komma in.
6 Hamani atalowa, mfumu inamufunsa kuti, “Kodi timuchitire ulemu otani munthu amene mfumu ikondweretsedwa naye?” Tsono Hamani anaganiza mu mtima kuti, “Kodi palinso ndani amene mfumu ingamulemekeze kuposa ine?”
Då Haman kom in, sade Konungen till honom: Hvad skall man göra dem manne, som Konungen gerna ära vill? Men Haman tänkte i sitt hjerta: Hvem skulle Konungen gerna vilja göra äro, utan mig?
7 Choncho Hamani anayankha mfumuyo kuti, “Munthu amene mfumu ifuna kumuchitira ulemu, imuchitire izi:
Och Haman sade till Konungen: Den man, som Konungen gerna vill ära,
8 Anthu abwere ndi chovala cha ufumu ndi kavalo amene mfumu imakwerapo wokhala ndi chizindikiro chaufumu pamutu pake.
Honom skall man hafva fram, och kläda uppå honom Konungslig kläder, de Konungen plägar draga, och den häst, som Konungen plägar uppå rida, och att man sätter en Konungslig krono på hans hufvud;
9 Ndipo mupereke chovala cha ufumucho ndi kavalo kwa mmodzi wa akalonga a mfumu a ulemu kwambiri. Ameneyu amuveke chovalacho munthu amene mfumu yakondweretsedwa naye. Akavekedwa chovalachi amuyendetse mʼmisewu yonse ya mzinda atakwera pa kavalo wa mfumu. Kalongayu azifuwula patsogolo pa munthuyu kuti ‘Ichi ndi chimene mfumu yachita kwa munthu amene yafuna kumuchitira ulemu!’”
Och man må få den klädningen och hästen uti en Konungens Förstas hand, att han ikläder den man, som Konungen gerna ära vill, och förer honom på hästenom öfver stadsgatorna, och låter ropa framför honom: Så skall man göra dem, som Konungen gerna ära vill.
10 Mfumu inalamulira Hamani kuti, “Pita msanga, katenge chovala cha ufumu ndi kavalo ndipo uchite monga wanenera kwa Mordekai Myuda, amene amakhala pa chipata cha mfumu. Usasiyeko china chilichonse chimene wanena.”
Konungen sade till Haman: Skynda dig, och tag klädningen och hästen, såsom du sagt hafver, och gör alltså med dem Judanom Mardechai, som för Konungens dörr sitter; och låt intet fattas af allt det du sagt hafver.
11 Choncho Hamani anatenga chovala ndi kavalo. Anamuveka Mordekai chovalacho ndipo anamuyendetsa mʼmisewu yonse ya mu mzinda atakwera pa kavalo, akufuwula kuti, “Ichi ndi chimene mfumu yachita kwa munthu amene yafuna kumuchitira ulemu!”
Så tog Haman klädningen och hästen, och klädde på Mardechai, och förde honom på stadsgatone, och ropade framför honom: Så skall man göra dem manne, som Konungen gerna ära vill.
12 Pambuyo pake Mordekai anabwerera ku chipata cha mfumu. Koma Hamani anapita msanga ku nyumba kwake, akulira, atafundira mutu wake.
Och Mardechai kom igen inför Konungens dörr; men Haman skyndade sig hem, och sörjde med skyldt hufvud;
13 Hamani anawuza Zeresi mkazi wake ndi abwenzi ake onse zonse zinamuchitikira. Anthu ake anzeru ndi mkazi wake Zeresi anamuwuza kuti, “Popeza kuti Mordekai ndi Myuda amene mwayamba kale kugonja pamaso pake, ndiye kuti palibe chimene mungachitepo. Mudzagwa ndithu pamaso pake.”
Och förtäljde sine hustru Seres, och allom sinom vännom, allt det honom händt hade. Då sade till honom hans vise, och hans hustru Seres: Är Mardechai af Juda säd, för hvilkom du hafver begynt att falla, så hafver du ingen magt med honom, utan du måste falla för honom.
14 Pamene anthuwa amayankhula nayebe, adindo a mfumu ofulidwa anabwera kudzamutenga Hamani mofulumira kupita naye ku phwando limene Estere anakonza.
Vid de ännu med honom talade, kommo Konungens kamererare dertill, och hastade på Haman, till att komma till måltidena, som Esther tillredt hade.

< Estere 6 >