< Estere 6 >

1 Usiku umenewo mfumu inalephera kugona tulo; Choncho inayitanitsa buku limene amalembamo mbiri ya zamakedzana kuti amuwerengere.
I A po, aole i hiki i ke alii ke hiamoe, a kauoha ae la ia e laweia mai ka buke mooolelo o na oihana; a heluheluia ia imua o ke alii.
2 Anapeza kuti mʼbukumo munalembedwa zoti Mordekai anawulula kuti Bigitana ndi Teresi, awiri mwa adindo ofulidwa a mfumu amene ankalondera pa khomo la chipinda cha mfumu ndiwo anakonza chiwembu chofuna kupha mfumu Ahasiwero.
A loaa iho la ka palapala o ko Moredekai hai ana no Bigetana, a me Teresa, na luna elua o ke alii i kiai ai i ka puka, a imi i wahi e hiki ai, ke kau i ka lima maluna o ke alii o Ahasuero.
3 Mfumu inafunsa kuti, “Kodi Mordekai anamupatsa ulemu ndi ukulu wotani chifukwa cha chinthu chimene anachitachi?” Atumiki ake anamuyankha kuti, “Palibe chimene chinachitika kwa iye.”
Ninau ae ke alii, Heaha ka mea maikai, a me ka mea nui i hanaia'i ia Moredekai, no keia mea? I aku la na kauwa a ke alii i ka poe i lawelawe nana, Aohe mea i hanaia nona.
4 Mfumu inati, “Kodi ndani ali mʼbwalomo?” Tsono Hamani anali atangolowa kumene mʼbwalo lakunja la nyumba yaufumu kuti akawuze mfumu zomukhomera Mordekai pa mtanda umene anamukonzera.
Ninau ae la ke alii, Owai la ma ka pahale? Ua hiki mai o Hamana ma ka pahale mawaho o ka hale o ke alii e olelo i ke alii, e liia o Moredekai ma ke olokea ana i hoomakaukau ai nona.
5 Atumiki ake anamuyankha kuti, “Hamani ndiye wayima mu bwalo.” “Mulowetseni,” Mfumu inalamulira.
I aku la na kauwa a ke alii ia ia, Aia, ke ku mai la o Hamana ma ka pahale. I mai la ke alii, E hele mai la iloko.
6 Hamani atalowa, mfumu inamufunsa kuti, “Kodi timuchitire ulemu otani munthu amene mfumu ikondweretsedwa naye?” Tsono Hamani anaganiza mu mtima kuti, “Kodi palinso ndani amene mfumu ingamulemekeze kuposa ine?”
Alaila, komo aku la o Hamana. Ninau mai la ke alii ia ia, Heaha ka mea e hanaia'i no ke kanaka a ke alii e manao nei e hoohanohano? Nalu iho la o Hamana maloko o kona naau, Owai ka mea a ke alii e makemake nei e hoohanohano, aoleanei owau?
7 Choncho Hamani anayankha mfumuyo kuti, “Munthu amene mfumu ifuna kumuchitira ulemu, imuchitire izi:
I aku la o Hamana i ka alii, No ke kanaka a ke alii e makemake nei e hoohanohano,
8 Anthu abwere ndi chovala cha ufumu ndi kavalo amene mfumu imakwerapo wokhala ndi chizindikiro chaufumu pamutu pake.
E laweia mai ka lole alii a ke alii i komo ai, a me ka lio a ke alii i holoholo ai, a me ka leialii i hooleiia'i kona poo;
9 Ndipo mupereke chovala cha ufumucho ndi kavalo kwa mmodzi wa akalonga a mfumu a ulemu kwambiri. Ameneyu amuveke chovalacho munthu amene mfumu yakondweretsedwa naye. Akavekedwa chovalachi amuyendetse mʼmisewu yonse ya mzinda atakwera pa kavalo wa mfumu. Kalongayu azifuwula patsogolo pa munthuyu kuti ‘Ichi ndi chimene mfumu yachita kwa munthu amene yafuna kumuchitira ulemu!’”
A e haawiia ua lole la, a me ka lio i ka lima o kekahi o na'lii koikoi o ke alii, i hoaahu ai lakou i ke kanaka a ke alii i makemake ai e hoohano, a e hooholo lakou ia ia maluna o ka lio ma ke alanui o ke kulanakauhale, a e kala aku mamua ona, Pela e hanaia'i ke kanaka a ke alii e makemake ai e hoolanilani.
10 Mfumu inalamulira Hamani kuti, “Pita msanga, katenge chovala cha ufumu ndi kavalo ndipo uchite monga wanenera kwa Mordekai Myuda, amene amakhala pa chipata cha mfumu. Usasiyeko china chilichonse chimene wanena.”
Alaila, olelo mai la ke alii ia Hamana, E wikiwiki oe, e lawe i ka lole, a me ka lio, me au i olelo ai, a e hana aku oe pela ia Moredekai, i ka Iudaio, ka mea e noho la ma ka pukapa o ke alii. Mai hoohaule i kekahi o na mea a pau au i olelo mai nei.
11 Choncho Hamani anatenga chovala ndi kavalo. Anamuveka Mordekai chovalacho ndipo anamuyendetsa mʼmisewu yonse ya mu mzinda atakwera pa kavalo, akufuwula kuti, “Ichi ndi chimene mfumu yachita kwa munthu amene yafuna kumuchitira ulemu!”
Alaila, lawe o Hamana i ka lole a me ka lio, a hoaahu iho la ia Moredekai, a hooholo ae la ia ia maluna o ka lio, ma ke alanui o ke kulanakauhale, a kala aku la imua ona, Pela no e hanaia mai ai i ke kanaka a ke alii e makemake ai e hoohanohano.
12 Pambuyo pake Mordekai anabwerera ku chipata cha mfumu. Koma Hamani anapita msanga ku nyumba kwake, akulira, atafundira mutu wake.
Hele hou aku la o Moredekai i ka pukapa o ke alii; aka, o Hamana, wikiwiki ae la ia i kona hale, me ke kaniuhu, a ua pulouia kona poo.
13 Hamani anawuza Zeresi mkazi wake ndi abwenzi ake onse zonse zinamuchitikira. Anthu ake anzeru ndi mkazi wake Zeresi anamuwuza kuti, “Popeza kuti Mordekai ndi Myuda amene mwayamba kale kugonja pamaso pake, ndiye kuti palibe chimene mungachitepo. Mudzagwa ndithu pamaso pake.”
Hai aku la o Hamana i kana wahine ia Zeresa, a i kona poe makamaka a pau i na mea a pau i loaa ai ia ia. Alaila, olelo mai la ia ia kona poe kanaka akamai, a me kana wahine o Zeresa, Ina no ka hanauna Iudaio o ua Moredekai la, a ua haule oe imua ona i keia wa, aole no oe e lanakihi maluna one, aka, e oiaio no, e haule no oe imua ona.
14 Pamene anthuwa amayankhula nayebe, adindo a mfumu ofulidwa anabwera kudzamutenga Hamani mofulumira kupita naye ku phwando limene Estere anakonza.
A ia lakou e kamailio pu ana me ia, hiki ae la na luna o ke alii, a wikiwiki lakou e lawe aku ia Hamana i ka ahainu a Esetera i hoomakaukau ai.

< Estere 6 >