< Mlaliki 4 >

1 Ndinayangʼananso ndi kuona chipsinjo chimene chimachitika pansi pano: ndinaona misozi ya anthu opsinjika, ndipo iwo alibe owatonthoza; mphamvu zinali ndi anthu owapsinjawo ndipo iwonso analibe owatonthoza.
Hahoi, kanî rahim vah sak e pacekpahleknae naw pueng bout ka pouk. Pacekpahleknae ka khang e taminaw ni a khuika ei nakunghai, hloutnae ka poe thai e tami awm hoeh. Ka pacekpahlek e taminaw teh bahu a tawn dawk hloutnae ka poe thai e tami awm hoeh.
2 Ndipo ndinanena kuti akufa, amene anafa kale, ndi osangalala kuposa amoyo, amene akanalibe ndi moyo.
Hateiteh, kadout tangcoung e tami teh kahring rae tami hlak hoe yawhawinae ao telah a ti.
3 Koma wopambana onsewa ndi amene sanabadwe, amene sanaone zoyipa zimene chimachitika pansi pano.
Hatdawkvah, vai touh hai kaawm hoeh e tami, kanî rahim sak e yonnae kahmawt hoeh rae tami teh hote kahni touh hlak hoe yawhawinae ao.
4 Ndipo ndinazindikira kuti ntchito zonse zolemetsa ndiponso ntchito zonse zaluso zimachitika chifukwa choti wina akuchitira nsanje mnzake. Izinso ndi zopandapake, nʼkungodzivuta chabe.
Hahoi, panki thapathonae hoi kahawicalah pâbaw e hnonaw pueng dawk hai thoseh, hot patetlah e hno dawkvah alouke tami ni hmuhmanae thoseh, kai ni ka pouk. Hote hno teh ahrawnghrang e hno kahlî man e hoi doeh a kâvan.
5 Chitsiru chimangoti manja ake lobodo ndi kudzipha chokha ndi njala.
Tami pathu ni teh a kut a kâtapam teh, amae a tak hah letlang a ca.
6 Nʼkwabwino kukhala ndi dzanja limodzi lodzaza uli pa mtendere, kuposa kukhala ndi manja awiri odzaza uli pa mavuto, ndipo uku nʼkungodzivuta chabe.
Roumnae hoi hmu e kutvang touh e hno teh, tawnta laihoi kahlî man laihoi hmu e kutkarum touh e hno hlak bet ahawihnawn.
7 Ndinaonanso chinthu china chopanda phindu pansi pano:
Hahoi, kanî rahim ahrawnghrang e hno bout ka pouk navah,
8 Panali munthu amene anali yekhayekha; analibe mwana kapena mʼbale. Ntchito yake yolemetsa sinkatha, ndipo maso ake sankakhutitsidwa ndi chuma chake. Iye anadzifunsa kuti, “Kodi ntchito yosautsayi ndikuyigwirira yani? Nanga nʼchifukwa chiyani ndikudzimana chisangalalo?” Izinso ndi zopandapake, zosasangalatsa!
tami teh a huiko, a canaw, a hmaunawnghanaw tawn hoeh, ama dueng kaawm ei nakunghai, panki thapathonae baw thai hoeh. A hno hmunae dawkvah lungkuep thai hoeh. Kai ni mahoima ka yue teh api hane maw ka panki aw telah ka pacei boihoeh. Hete haiyah ahrawnghrang tawntam nah hrum doeh.
9 Kukhala awiri nʼkwabwino kuposa kukhala wekha, chifukwa ntchito ya anthu awiri ili ndi phindu:
Tami teh madueng hlak tami kahni touh bet ahawi. Tawk pawiteh kahawie tawkphu a hmu.
10 Ngati winayo agwa, mnzakeyo adzamudzutsa. Koma tsoka kwa munthu amene agwa ndipo alibe wina woti amudzutse!
Buet touh rawm pawiteh buet touh ni a pathaw han. Buet touh dueng e tami rawm pawiteh ahawinae awm hoeh. Kapathawkung awm mahoeh.
11 Komanso ngati anthu awiri agona malo amodzi, adzafunditsana. Koma nanga mmodzi angadzifunditse yekha?
Tami teh kahni touh rei ip pawiteh a phubet han. Madueng teh bangtelamaw phubet thai han.
12 Munthu mmodzi angathe kugonjetsedwa, koma anthu awiri akhoza kudziteteza. Chingwe cha maulusi atatu sichidukirapo.
Tami buet touh ni buet touh tâ pawiteh ahni hah tami kahni touh ni a ngang thai. Rui kathum touh hoi pakhit e tangron teh kayawicalah thawk thai hoeh.
13 Wachinyamata wosauka koma wanzeru aposa mfumu yokalamba koma yopusa imene simvanso malangizo.
Tounnae ka ngai hoeh e, a kum kacue ka pathu e siangpahrang hlak, a lungkaang e mathoe camo teh aphuohnawn.
14 Wachinyamatayo angathe kuchokera ku ndende ndi kudzakhala mfumu, kapena angathe kubadwa wosauka mʼdziko la mfumuyo.
Thongim hoi siangpahrang koe ka phat e hai, a uknaeram dawk mathoe lah doeh a khe.
15 Ndipo ndinaona kuti iwo onse amene anakhala ndi moyo ndi kuyenda pansi pano anatsatira wachinyamatayo, amene anatenga malo a mfumu.
Kanî rahim kaawm e taminaw pueng e kong ka pouk navah, ahnimouh thung dawk siangpahrang hmuen ka coe hane, camo ao awh e hah ka panue.
16 Mfumu ikhoza kulamulira anthu osawerengeka, komabe itamwalira, palibe amene adzayamikire zomwe mfumuyo inachita. Izinso ndi zopandapake, nʼkungozivuta chabe.
Hote siangpahrang ni a uk e taminaw pueng parei thai kawi lah awm hoeh. A hnukkhu lah ka tho e taminaw ni hai hote siangpahrang hah a lungkuep thai awh mahoeh. Atangcalah, hote hno hai ahrawnghrang e hno, kahlî man e hoi doeh a kâvan.

< Mlaliki 4 >