< Mlaliki 4 >
1 Ndinayangʼananso ndi kuona chipsinjo chimene chimachitika pansi pano: ndinaona misozi ya anthu opsinjika, ndipo iwo alibe owatonthoza; mphamvu zinali ndi anthu owapsinjawo ndipo iwonso analibe owatonthoza.
Amalalu, na da defele hame hamobe hou osobo bagadega bu ba: i. Gasa fi dunu da asaboi dunuma nimi bagade hamobeba: le, asaboi dunu da dinanu, fidisu dunu hame ba: i. Bai gasa fi dunu, ili fawane da gasa gala.
2 Ndipo ndinanena kuti akufa, amene anafa kale, ndi osangalala kuposa amoyo, amene akanalibe ndi moyo.
Na da bogoi dunu ilima mudasa. Bai bogosu hou da esalusu hou baligisa.
3 Koma wopambana onsewa ndi amene sanabadwe, amene sanaone zoyipa zimene chimachitika pansi pano.
Be dunu amo da hame lalelegei da defele hame hamobe hou osobo bagadega gala, amo hame ba: beba: le, ilia hou da esalebe dunu ilia hou baligisa.
4 Ndipo ndinazindikira kuti ntchito zonse zolemetsa ndiponso ntchito zonse zaluso zimachitika chifukwa choti wina akuchitira nsanje mnzake. Izinso ndi zopandapake, nʼkungodzivuta chabe.
Hou eno na ba: le, dawa: lai dagoi. Abuliba: le dunu ilia da hawa: gasa bagadedafa hamosala: , amola liligi huluane noga: i enoenoia hahamosala: ? Bai agoane, ilia da ilia na: iyado dunu ilia gagui amo mudale ba: sa. Be amo hou da hamedeidafa. Amo da fo mabe se bobogebe defele gala.
5 Chitsiru chimangoti manja ake lobodo ndi kudzipha chokha ndi njala.
Dunu oda ilia da agoane sia: sa, dunu hihia: me hawa: afaewane mae hamone, hina: lobo sogoba: digili udigili esalebeba: le bogomu, agoaiwane dunu da gagaoui dunu.
6 Nʼkwabwino kukhala ndi dzanja limodzi lodzaza uli pa mtendere, kuposa kukhala ndi manja awiri odzaza uli pa mavuto, ndipo uku nʼkungodzivuta chabe.
Amo sia: da dafawanela: ? Na hame dawa: Be amo na dawa: Fonobahadi fawane gaguli amola dogo olofoiwane esalumu da defea. Be eso huluane fo lamusa: ne, lobo aduna amoga mae helefili hawa: hamonanumu da hamedei liligi agoane.
7 Ndinaonanso chinthu china chopanda phindu pansi pano:
Na da osobo bagade esalusu ganodini, eno hamedei liligi ba: i dagoi.
8 Panali munthu amene anali yekhayekha; analibe mwana kapena mʼbale. Ntchito yake yolemetsa sinkatha, ndipo maso ake sankakhutitsidwa ndi chuma chake. Iye anadzifunsa kuti, “Kodi ntchito yosautsayi ndikuyigwirira yani? Nanga nʼchifukwa chiyani ndikudzimana chisangalalo?” Izinso ndi zopandapake, zosasangalatsa!
Dunu afaedafa e da hisuwane fifi lala. E da mano hame amola ea eya ola hamedei, be amowane e da eso huluane hawa: hamonana. Be e da bagade gaguiba: le hame nodosa. E da nowama gasa bagade hawa: hamosala: ? Amola e da abuliba: le hahawane hou higasala: ? Amo hou amola da hamedei liligi. Agoaiwane esalusu da noga: i hame amola da: i dioi agoane.
9 Kukhala awiri nʼkwabwino kuposa kukhala wekha, chifukwa ntchito ya anthu awiri ili ndi phindu:
Dunu aduna da dafululi hawa: hamomu da defea. Bai dunu aduna da gilisili hawa: hamosea, ela hawa: hamoi da baligili ba: mu.
10 Ngati winayo agwa, mnzakeyo adzamudzutsa. Koma tsoka kwa munthu amene agwa ndipo alibe wina woti amudzutse!
Dunu ea sama afae amo dafasea bu ea sama eno amoea fidili lobolele wa: lesimu. Be dunu afae da e hisu dafasea, e da fidisu dunu hame ba: mu.
11 Komanso ngati anthu awiri agona malo amodzi, adzafunditsana. Koma nanga mmodzi angadzifunditse yekha?
Dunu aduna ela da anegagisia, ela gilisili sogobale gola diasea ela da dogoloi ba: mu. Be dia disu da gola diasea, di da habodane dogolole denesima: bela: ?
12 Munthu mmodzi angathe kugonjetsedwa, koma anthu awiri akhoza kudziteteza. Chingwe cha maulusi atatu sichidukirapo.
Dunu afaedafa ea hisu ha lai dunuma gegesea e da hame hasanasimu. Be ha lai dunu ilia adunama doagala: sea, ilia gasaga da ela hame baligimu. Efe gomei osodayale hamoi amoea da hedolo hame damumu.
13 Wachinyamata wosauka koma wanzeru aposa mfumu yokalamba koma yopusa imene simvanso malangizo.
14 Wachinyamatayo angathe kuchokera ku ndende ndi kudzakhala mfumu, kapena angathe kubadwa wosauka mʼdziko la mfumuyo.
Hame gagui dunu da heda: le, bu hi fifi asi gala ganodini hina bagade hou lamusa: dawa: Amola se dabe iasu diasu hamoi dunu da se dabe iasu diasu fisili, hina bagade hou lamusa: dawa: Be e da da: i hamosea, fada: i sia: ne iasu higasea, e da gagaoui agoai. Ayeligi dunu amo da hame gaguiwane be noga: i dawa: lai, e da amo dunu ea hou baligisa.
15 Ndipo ndinaona kuti iwo onse amene anakhala ndi moyo ndi kuyenda pansi pano anatsatira wachinyamatayo, amene anatenga malo a mfumu.
Na dawa: i dagoi, dunu huluane nowa osobo bagade goe ganodini esalebe, amo fi ganodini da goi ayeligi afae, e da fa: no hina bagade ea sogebi lamu.
16 Mfumu ikhoza kulamulira anthu osawerengeka, komabe itamwalira, palibe amene adzayamikire zomwe mfumuyo inachita. Izinso ndi zopandapake, nʼkungozivuta chabe.
Hina bagade da dunu idimu hamedei amo ouligimusa: dawa: Be e da bogosea, dunu da ea hamobeba: le hame nodomu. Amo hou da bai hamedei. Hamedeiba: le, amo hou da gagaoui dunu fo mabe se bobogebe agoai ba: sa.