< Deuteronomo 31 >
1 Tsono Mose anapita ndi kukayankhula mawu awa kwa Aisraeli onse:
Napan ni Moises ket insaona dagitoy a sasao kadagiti amin nga Israelita.
2 “Tsopano ndili ndi zaka 120, ndipo sindingathenso kukutsogolerani. Yehova wandiwuza kuti, ‘Iwe sudzawoloka Yorodani.’
Kinunana kadakuada, “Agtawenakon ita ti 120; Saankon a kabaelan ti rummuar ken umuneg; Kinuna ni Yahweh kaniak, 'Saankanto a mapan iti ballasiw daytoy Jordan.'
3 Mwini wake Yehova Mulungu wanu ndiye amene adzakutsogolerani powoloka. Iye adzawononga mitundu ina yonse, ndipo inu mudzatenga dziko lawo. Yoswa adzakutsogoleraninso powoloka, monga momwe ananenera Yehova.
Bumallasiwto iti sangom ni Yahweh a Diosmo; dadaelennanto amin dagitoy a nasion manipud iti sangoanam, ken pagtalawemto ida. Bumallasiwto ni Josue iti sangom, kas sinao ni Yahweh.
4 Ndipo Yehova adzawawononga iwo monga momwe anawonongera Sihoni ndi Ogi, mafumu Aamori, amene Iye anawawononga pamodzi ndi dziko lawo.
Aramidento ni Yahweh kadakuada iti kas inaramidna kenni Sihon ken Og, dagiti ar-ari dagiti Amorreo, ken iti dagada, a dinadaelna.
5 Ambuye adzawapereka kwa inu, ndipo inu mukawachitire zonse zimene ndakulamulani.
Pagballigiennakayonto ni Yahweh kadakuada inton masarakanyo ida iti paggugubatan, ken aramidenyonto kadakuada dagiti amin nga imbilinko kadakayo.
6 Khalani amphamvu ndi olimba mtima. Musachite nawo mantha kapena kunjenjemera pamaso pawo, chifukwa Yehova Mulungu wanu apita nanu. Sadzakusiyani kapena kukutayani.”
Pumigsakayo ken tumuredkayo, saankayo nga agbuteng, ken saanyo a pagbutngan ida; ta ni Yahweh a Diosyo ti kumuyog kadakayo; saannakayonto a paayen wenno baybay-an.”
7 Pamenepo Yehova anayitana Yoswa pamaso pa Aisraeli onse ndipo anamuwuza kuti, “Khala wamphamvu ndi wolimba mtima, pakuti iwe udzatsogolera anthu awa ku dziko limene Yehova analumbira kulipereka kwa makolo awo, ndipo iwe ukaligawe pakati pawo kuti likakhale cholowa chawo.
Inayaban ni Moises ni Josue ken imbagana kenkuana iti imatang dagiti amin nga Israelita, “Pumigsaka ken tumuredka, ta makikuyogka kadagitoy a tattao a mapan iti daga nga insapata ni Yahweh nga itedna kadagiti kapuonanda; tulongamto ida a mangtawid iti daytoy.
8 Yehova mwini ndiye akukutsogolerani ndipo adzakhala nanu. Sadzakusiyani kapena kukutayani. Usachite mantha ndiponso usataye mtima.”
Ni Yahweh ti mapan iti sangoanam; kumuyogto isuna kenka; saannakanto a paayen wenno baybay-an; saanka nga agbuteng, saanka a maupay.”
9 Choncho Mose analemba malamulo awa nawapereka kwa ansembe, ana Alevi, amene amanyamula Bokosi la Chipangano la Yehova, ndiponso kwa akuluakulu onse a Aisraeli.
Insurat ni Moises daytoy a linteg ken intedna daytoy kadagiti papadi, dagiti annak ni Levi, a nangaw-awit ti lakasa ti tulag ni Yahweh; nangted met isuna kadagiti kopia kadagiti amin a panglakayen ti Israel.
10 Kenaka Mose anawalamula kuti, “Pamapeto pa zaka zisanu ndi ziwiri zilizonse, chaka cha kukhululukidwa ngongole, pa nthawi ya Chikondwerero cha Misasa,
Binilin ida ni Moises ket kinunana, “Iti pagleppasan iti tunggal pito a tawen, ti nakedngan a tiempo a para ti pannakawaswas iti utang, bayat ti Piesta dagiti Abong- abong,
11 pamene Aisraeli onse abwera kudzaonekera pamaso pa Yehova Mulungu wanu pamalo pamene Iye adzasankhe, mudzawerenge malamulo onsewa iwo akumva.
inton umay agparang amin nga Israelita iti sangoanan ni Yahweh a Diosyo iti disso a pilienna para iti sanctuariona, basaenyonto daytoy a linteg iti sangoanan dagiti amin nga Israelita iti pagdengngegda.
12 Mudzasonkhanitse anthu onse pamodzi, amuna, akazi ndi ana pamodzi ndi alendo amene akukhala mʼmizinda yanu, kuti adzawamve ndi kuphunzira kuopa Yehova Mulungu wanu ndi kutsatira mosamala mawu onse a mʼmalamulowa.
Ummongenyonto dagiti tattao, dagiti lallaki, dagiti babbai ken dagiti ubbing ken ti gangganaetyo nga adda kadagiti ruangan ti siudadyo, tapno mangngeg ken maadalda, ken tapno raemenda koma ni Yahweh a Diosyo ken salimetmetanda amin dagiti sasao daytoy a linteg.
13 Ana awo amene sadziwa malamulo awa, ayenera kuwamva ndi kuphunzira kuopa Yehova Mulungu wanu nthawi zonse pamene mukukhala mʼdziko limene mukuwoloka Yorodani kukalitenga.”
Aramidenyo daytoy tapno dagiti annakda a saan a nakaammo, mangngegan ken masursuroda koma a raemen ni Yahweh a Diosyo, agingga nga agnanaedkayo iti daga a lasatenyo ti Jordan a papananyo a tagikuaen.”
14 Yehova anawuza Mose kuti, “Nthawi ya kufa kwako yafika. Itana Yoswa ndipo mubwere ku tenti ya msonkhano, kumene Ine ndidzamulangiza.” Choncho Mose ndi Yoswa anabwera ku tenti ya msonkhano.
Kinuna ni Yahweh kenni Moises, “Adtoy, umad-adanin ti aldaw a masapul a matayka; ayabam ni Josue ken iparangmo ta bagim iti tabernakulo, tapno mangitedak iti bilin kenkuana.” Napan ni Moises ken ni Josue ken imparangda dagiti bagbagida iti tabernakulo.
15 Pamenepo Yehova anaonekera ku tenti mʼchipilala cha mtambo, ndipo mtambowo unayima pamwamba pa khomo lolowera mu tenti.
Nagparang ni Yahweh iti tolda iti maysa nga adigi ti ulep; nagyan ti adigi ti ulep iti ngatoen ti pagserkan iti tolda.
16 Ndipo Yehova anawuza Mose kuti, “Iwe ukupita kukapuma kumene kuli makolo ako, ndipo ukangomwalira, anthu awa adzayamba kupembedza milungu yachilendo ya mʼdziko limene akukalowamo. Adzanditaya ndi kuphwanya pangano lomwe ndinachita nawo.
Kinuna ni Yahweh kenni Moises, “Adtoy, mataykanto ket makitiponka kadagiti kapuonan nga immuna a natayen; tumakderto dagitoy a tattao ken agtignayda a kasda la balangkantis a mapan kadagiti sabali a dios iti daga, ti daga a papananda tapno maibaet kadakuada. Baybay-andakto ken labsingendanto ti tulagko nga inaramidko kadakuada.
17 Tsiku limenelo Ine ndidzawakwiyira ndi kuwataya. Ndidzawabisira nkhope yanga, ndipo adzawonongedwa. Masautso ambiri ndi zovuta zambiri zidzawagwera, ndipo tsiku limenelo adzafunsa kuti, ‘Kodi masautso awa sanagwere ife chifukwa Yehova Mulungu wathu sali nafe?’
Ket iti dayta nga aldaw, sumgedto ti ungetko maibusor kadakuada, ket baybay-akto ida. Ilemmengkonto ti rupak manipud kadakuada, ken maalun-ondanto. Adunto a didigra ken riribuk ti mangbirok kadakuada, tapno kunaendanto iti dayta nga aldaw, 'Daddadaelendak dagitoy a didigra gapu ta saannakon a salsalakniban iti Dios.'
18 Ndipo Ine ndidzabisa ndithu nkhope yanga pa tsiku limenelo chifukwa cha zoyipa zimene anachita potembenukira kwa milungu ina.
Awan duadua nga ilemmengkonto ti rupak kadakuada iti dayta nga aldaw gapu iti amin a dakes nga inaramidda, gapu ta timmalliawda kadagiti sabali a dios.
19 “Tsopano ulembe mawu a nyimbo iyi ndipo uwaphunzitse Aisraeli, uwawuze kuti aziyimba, kuti ikhale mboni yanga yowatsutsa.
Isuratyo ngarud ita daytoy a kanta para kadagiti bagbagiyo ken isuroyo kadagiti tattao ti Israel. Ikabilyo daytoy kadagiti ngiwatda, tapno agbalinto a maysa a saksi kaniak daytoy a kanta maibusor kadagiti tattao ti Israel.
20 Pamene ndawalowetsa mʼdziko loyenda mkaka ndi uchi, dziko limene ndinalonjeza mwalumbiro kwa makolo awo, ndipo pamene adzadya ndi kukhuta ndi kumasangalala, iwo adzatembenukira kwa milungu ina ndi kumayipembedza, kundikana Ine ndi kuphwanya pangano langa.
Ta inton maipanko ida iti daga nga insapatak nga ited kadagiti kapuonanda, maysa a daga nga agay-ayus iti gatas ken diro, ken no makapanganda, mapnek ken lumukmegda, ket tumalliawdanto kadagiti sabali a dios ken agdaydayawda kadakuada; laisendakto ken burakenda ti tulagko.
21 Ndipo pamene masautso ambiri ndi zovuta zambiri zidzawagwera, nyimbo iyi idzakhala mboni yanga yowatsutsa, chifukwa zidzukulu zawo sizidzayiwala nyimboyi. Ine ndikudziwa zimene iwo akulingalira kuchita, ngakhale kuti sindinawalowetse mʼdziko limene ndinalonjeza mwa lumbiro.”
Inton mabirukan dagiti adu a dakes ken riribuk dagitoy a tattao, paneknekanto daytoy a kanta iti sangoananda a kas maysa a saksi; ta saanto a malipatan kadagiti ngiwat dagiti kaputotanda; ta ammok dagiti panggep a bukboklenda ita nga aldaw, uray idi sakbay nga impanko ida iti daga nga insapatak.”
22 Choncho Mose analemba nyimbo iyi tsiku limenelo ndi kuwaphunzitsa Aisraeli.
Isu nga insurat ni Moises daytoy a kanta iti dayta met laeng nga aldaw ken insurona daytoy kadagiti tattao ti Israel.
23 Yehova analamula Yoswa mwana wa Nuni kuti, “Khala wamphamvu ndipo limba mtima, chifukwa udzalowetsa Aisraeli mʼdziko limene ndinawalonjeza mwa lumbiro, ndipo Ine mwini ndidzakhala nawe.”
Nangted ni Yahweh kenni Josue nga anak ni Nun ti maysa a bilin ket kinunana, “Pumigsaka ken tumuredka; ta ipanmonto dagiti tattao ti Israel iti daga nga insapatak kadakuada, ken addaakto kenka.”
24 Mose atatha kulemba malamulowa mʼbuku, osasiyako kanthu,
Napasamak nga idi nalpas ni Moises nga insursurat dagiti sasao daytoy a linteg iti maysa a libro,
25 analamula Alevi amene ananyamula Bokosi la Chipangano la Yehova kuti,
a nangted isuna iti bilin kadagiti Levita a nangaw-awit iti lakasa ti pammaneknek ni Yahweh; kinunana,
26 “Tengani Buku ili la Malamulo ndi kuliyika pambali pa Bokosi la Chipangano la Yehova Mulungu wanu. Likhale kumeneko ngati mboni yokutsutsani.
“Alaenyo daytoy a libro ti linteg ken ikabilyo iti abay ti lakasa ti pammaneknek ni Yahweh a Diosyo, tapno adda koma daytoy sadiay a kas maysa a saksi maibusor kadakayo.
27 Pakuti Ine ndikudziwa kuwukira kwanu ndi kuwuma mtima kwanu. Ngati inu mwakhala mukuwukira Yehova ine ndili moyo ndiponso ndili nanu pamodzi, nanga mudzawukira motani ine ndikamwalira!
Ta ammok ti kinasukiryo ken ti kinatangken ti uloyo; adtoy, bayat a sibibiagak pay a kaduadak uray ita nga aldaw, nagsukirkayon maibusor kenni Yahweh; nakarkaronto ngatan kalpasan iti ipapatayko?
28 Mundisonkhanitsire atsogoleri onse a mafuko anu pamodzi ndi akuluakulu onse, kuti ndiyankhule mawu awa iwo akumva ndipo kumwamba ndi dziko lapansi zikhale mboni yowatsutsa.
Ummongenyo kaniak dagiti amin a panglakayen dagiti tribuyo, ken dagiti opisialesyo, tapno maisaok dagitoy a sasao kadagiti lapayagda ken awagak ti langit ken daga tapno agsaksi maibusor kadakuada.
29 Chifukwa ndikudziwa kuti ine ndikamwalira mudzayipa kwambiri ndi kutembenuka kuleka njira imene ndinakulamulani. Masiku amene akubwera, masautso adzakugwerani chifukwa mudzachita zoyipa pamaso pa Yehova ndi kuputa mkwiyo wake chifukwa cha zimene manja anu anapanga.”
Ta ammok a kalpasan ti ipapatayko ket dumakeskayonto ken summiasikayo manipud iti dalan nga imbilinko kadakayo; umayto kadakayo ti didigra kadagiti sumarsaruno nga al-aldaw. Mapasamakto daytoy gapu ta aramidenyo iti dakes iti imatang ni Yahweh, a paungetenyo isuna babaen kadagiti aramid dagiti imayo.”
30 Ndipo Mose ananena mawu a nyimbo iyi kuyiimba koyambira mpaka potsiriza gulu lonse la Aisraeli likumva:
Kinanta ni Moises dagiti sasao daytoy a kanta kadagiti lapayag dagiti amin a taripnong ti Israel aginggana a nalpasda.