< Deuteronomo 29 >

1 Awa ndiwo mawu a mʼpangano limene Yehova analamula Mose kuti achite ndi Aisraeli ku Mowabu, powonjezera pa pangano limene anapangana nawo ku Horebu.
Hina Gode da Moua: be soge ganodini Mousesema e da Isala: ili dunuma gousa: su hamoma: ne sia: i. Amo gousa: su E da musa: gousa: su Sainai Goumia hamoi amoga gilisi. Amo gousa: su ea hou da haguduga dedei diala.
2 Mose anayitanitsa Aisraeli onse nati kwa iwo: Inu munaona zonse zimene Yehova anachita kwa Farao, nduna zake ndi dziko lake lonse ku Igupto.
Mousese da Isala: ili dunu huluane gilisima: ne sia: ne, ilima amane sia: i, “Dilia da Hina Gode Ea hou amo Idibidi hina bagade amola ea ouligisu dunu amola ea soge amoma hamoi, ba: i dagoi.
3 Ndi maso anu munaona mayesero onse aja, zizindikiro zozizwitsa ndi zodabwitsa zazikulu zija.
Dilia da olo bagade, musa: hame ba: su hou amola gasa bagade hou Hina Gode Ea hamoi, amo huluane ba: i.
4 Koma mpaka lero Yehova sanakupatseni mtima wozindikira kapena maso openya kapena makutu akumva.
Be Hina Gode da dili dawa: ma: ne amola noga: le nabima: ne, dilima asigi dawa: su amola ge noga: iwane hame i.
5 Mʼzaka makumi anayi zimene ndinakutsogolerani mʼchipululu, zovala zanu ndiponso nsapato za ku mapazi anu sizinangʼambike.
Ode 40amoga Hina Gode da wadela: i hafoga: i soge ganodini dili oule ahoasu. Dilia abula amola emo salasu da hame wadela: lesi.
6 Inu simunadye buledi ndi kumwa vinyo kapena chakumwa chilichonse choledzeretsa. Ndinachita izi kuti mudziwe kuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu.
Dilia da agi moma: ne amola waini hano o eno agoai hano moma: ne hame ba: i. Be Hina Gode da dilia liligi huluane dilima iasu. Bai E da dilia Godedafa, amo dilima olelemusa: agoane hamosu.
7 Pamene munafika malo ano, Sihoni mfumu ya ku Hesiboni ndi Ogi mfumu ya ku Basani anabwera kudzamenyana nafe koma tinawagonjetsa iwo.
Ninia da wali esalebe sogega doaga: loba, Hesiabone fi hina bagade (Saihone) amola Ba: isia: ne hina bagade (Oge) da ninima gegemusa: misi. Be amo dunu ninia da hasali dagoi.
8 Tinatenga dziko lawo ndi kulipereka ngati cholowa cha fuko la Rubeni, fuko la Gadi ndi theka la fuko la Manase.
Ninia da ilia soge lale, fifili, Liubene fi, Ga: de fi amola Yousefe ea fi la: idi amo Ma: na: se, ilima i.
9 Tsatirani mosamalitsa mawu a mʼpangano ili kuti zinthu zizikuyenderani bwino pa zochitika zanu zonse.
Dilia! Dilia hahawane didili hawa: hamoma: ne, amo gousa: su sia: huluane noga: le nabawane hamoma.
10 Lero lino nonse mukuyima pamaso pa Yehova Mulungu wanu, atsogoleri a mafuko anu, akuluakulu ndi nduna zanu, ndi amuna ena onse a mu Israeli,
11 pamodzi ndi ana ndi akazi anu, kudzanso alendo amene akukhala pakati panu omwe amakuwazirani nkhuni ndi kukutungirani madzi.
Wali eso, dilia huluane, dilia hina bagade dunu, ouligisu dunu, dunu, uda, mano amola ga fi dunu (ilia da dilia fi amo ganodini esala amola lalu habesa amola hano nasu gaguli maha) dilia huluane da dilia Hina Gode midadi lela.
12 Mukuyimirira pano kuti mulowe mʼpangano ndi Yehova Mulungu wanu, pangano limene Yehova akuchita ndi inu lero ndi kulisindikiza ndi malumbiro,
Dilia da wali eso amo gousa: su dilia Hina Gode da dilima hamonana, amo hamomusa: amola fa: no bobogema: ne sia: musa: lela.
13 kukukhazikitsani lero lino ngati anthu ake, ndi kuti Iye akhale Mulungu wanu monga anakulonjezani inu ndiponso monga analumbira kwa makolo anu Abrahamu, Isake ndi Yakobo.
Bai Hina Gode, E da musa: dilia aowalali A: ibalaha: me, Aisage amola Ya: igobe ilima ilegele sia: i defele, E da wali dilia Gode esala amola dilia da wali Ea Fidafa, E da sia: sa.
14 Ndikupanga pangano ili ndi malumbiro ake osati kwa inu nokha,
Be amo gousa: su amola amoma nabasu hou da dilima fawane hame.
15 amene muli pano pamaso pa Yehova Mulungu wathu, koma ndi iwonso amene sali pano lero.
Be amo gousa: su da nini huluane wali guiguda: lela, ninima amola ninigaga fi wali hame lalelegei ilima E da hamosa.
16 Inu nomwe mukudziwa mmene tinkakhalira ku Igupto ndi mmene tinadutsira mayiko pa ulendo wobwera kuno.
Dilia dawa: ! Dilia da musa: Idibidi soge ganodini esalea amola fa: no eno dunu fi ilia soge ganodini lalea, amo esalebe fi ilia hou dawa: dagoi.
17 Ife tinaona pakati pawo mafanizo ndi mafano awo onyansa, amtengo ndi amiyala, asiliva ndi agolide.
Dilia da ilia wadela: i loboga hamoi ifa, igi, silifa amola gouli amoga hamoi ogogosu ‘gode’ ba: i dagoi.
18 Onetsetsani kuti pasapezeke mwamuna kapena mkazi, banja kapena fuko pakati panu lero amene mtima wawo udzapandukira Yehova Mulungu wanu ndi kupita kukapembedza milungu ya mitundu iyo. Onetsetsani kuti pasapezeke muzu pakati panu wotulutsa mankhwala akupha otere.
Dawa: ma! Noga: le ouligima! Dunu o uda o sosogo fi o fi guiguda: lela amo da ninia Hina Gode yolesili, eno fi ilia ogogosu ‘gode’ liligi ilima nodone sia: ne gadomu da hamedei. Amo hou da fedege sia: agoane idifi da heda: le, gamogai bogosu ifa hamosa.
19 Munthu wotere akamva mawu a lumbiro ili, asadzidalitse yekha mʼmaganizo mwake namati, “Ine ndidzapulumuka ngakhale nditapitiriza kuyenda njira yanga.” Zoterezi zidzadzetsa masautso pa nthaka ya chinyontho ndi yowuma yomwe.
Dunu afae wali eso lela da amo gousa: su sema nabasea, be hi hanai gasa fi fawane hamobeba: le hahawane ba: musa: dawa: sa, amo ba: sa: besa: le dawa: ma! Amo hou da dili huluane gugunufinisimu, noga: i hamosu dunu amola wadela: i hamosu dunu defele wadela: mu.
20 Yehova sadzamukhululukira. Mkwiyo ndi nsanje ya Yehova zidzamuyakira munthuyo. Matemberero onse wolembedwa mʼbukuli adzamugwera iye ndipo Yehova adzafafaniza dzina lake pa dziko lapansi.
Hina Gode da agoaiwane dunu hame gogolema: ne olofomu. Be e da Hina Gode Ea gia: i bagade ougi hou amo ba: mu. Amasea, se iasu hou huluane amo buga ganodini dedei da ema doaga: mu. Hina Gode da amo dunu dafawane wadela: mu.
21 Yehova adzasankha pakati pa Aisraeli anthu oyenera masautso monga mwa matemberero onse a mʼpangano olembedwa Mʼbuku la Malamulo.
Isala: ili fi huluane da beda: iwane dawa: ma: ne, Hina Gode da gagabusu huluane gousa: su ganodini Hina Gode Ea olelesu buga ganodini dedei, amo gagabusu huluane E da agoai dunuma aligima: ne imunu.
22 Ana anu a mibado yakutsogolo ndi alendo amene adzachokera kutali adzaona matsoka amene adzakugwerani mʼdziko muno ndiponso matenda amene Yehova adzabweretsa pa dzikoli.
Hobea diligaga fi amola ga fi soge sedagaga misi da se nabasu amo Hina Gode da dilia sogega iasi amo ba: mu.
23 Dziko lonse lidzasanduka nthaka ya mchere ndi ya sulufule. Simudzadzalamo kanthu, simudzakhala chomera chilichonse, ndi mbewu yomera mʼmenemo. Dziko lanu lidzakhala lowonongeka ngati Sodomu ndi Gomora, Adima ndi Zeboimu, mizinda imene Yehova anayiwononga ndi mkwiyo wake waukulu.
Dilia soge huluane da gugunufinisi dagoi, salafa amola sali amoga dedeboi dagoi ba: mu. Ha: i manu da hame bugi amola wadela: i gagalobo da heda: mu gogolemu. Dilia soge da Sodame, Gomoula, A:dama amola Seboimi, (amo moilai Gode da gia: iwane ougiba: le gugunufinisi), amo defele ba: mu.
24 Mitundu yonse ya anthu idzafunsa kuti, “Kodi chifukwa chiyani Yehova anachita zotere mʼdziko lake? Kodi chifukwa chiyani anaonetsa mkwiyo woopsa wotere?”
Amasea, fifi asi gala dunu da amane adole ba: mu, ‘Hina Gode da abuli ilia sogega agoane hamobela: ? E da abuliba: le ilima gia: iwane ougibala: ?’
25 Ndipo yankho la mafunso amenewa lidzakhala lakuti, “Chifukwa chakuti anthu awa aphwanya pangano la Yehova Mulungu wa makolo awo, pangano limene Iye anapangana nawo pamene anawatulutsa ku Igupto.
Amola bu adole iasu da agoane, ‘Bai Hina Gode Ea fi dunu da gousa: su (amo E da ilia aowalali Idibidi sogega fadegaloba, ilima hamoi) amo gugunufinisi dagoi.
26 Iwo anachoka ndi kukatumikira milungu ina ndi kuyipembedza, milungu imene sanayidziwe, milungu imene sanawapatse.
Ilia eno ogogosu ‘gode’ liligi amo ilia musa: hame dawa: i amola Hina Gode da ilima mae nodone sia: ne gadoma: ne sia: i, amo ogogosu liligi ilima hawa: hamosu.
27 Choncho Yehova anakwiyira dziko lino, kotero anabweretsa matemberero onse amene analembedwa mʼbuku lino.
Amaiba: le, Hina Gode da Ea fi dunuma ougi galu amola ilima se nabasu amo buga ganodini dedei ilima iasu.
28 Ndi mkwiyo komanso ukali wake woopsa Yehova anawazula mʼdziko lawo ndi kuwaponyera mʼdziko lina, monga mmene zilili lero lino.”
Hina Gode da gia: i bagade ougi ba: i. E da ougiba: le, ili sogega fadegale, ga fi dunu ilia sogega sefasili, ilia da wali eso amogawi esala.’
29 Zinsinsi ndi za Yehova Mulungu wathu koma zinthu zimene zaululidwa ndi zathu ndi ana athu kwamuyaya, kuti titsatire mawu onse a mʼmalamulowa.
Ninia Hina Gode da liligi mogili wamolegesa. Amo ouligibi hou da Ea: Be E da Ea Sema amola hamoma: ne sia: i mae wamolegele, ninima olelei, amola nini eso huluane ouligima: ne, ninima i. Amaiba: le ninia amola ninigaga fi da amo sema amola hamoma: ne sia: i mae yolesili nabalumu da defea.”

< Deuteronomo 29 >