< Deuteronomo 2 >

1 Kenaka tinabwerera ndi kuyamba ulendo wolowera ku chipululu motsatira njira ya ku Nyanja Yofiira, monga mmene Yehova anatilamulira. Kwa nthawi yayitali tinayendayenda cha ku dziko la mapiri la Seiri.
ninia da sinidigili, wadela: i hafoga: i soge amoga asi. Gode da nama sia: beba: le, ninia da Maga: me Hano Wayabo ahoasu amoga asili, eso bagohame Idome agolo soge sisiga: le ahoanu.
2 Ndipo Yehova anati kwa ine,
Amola Hina Gode da nama amane sia: i,
3 “Mwazungulira mokwanira dziko la mapiri, tsopano tembenukirani kumpoto.
‘Amo agolo soge sisiga: le bu udigili mae laloma. Sinidigili, gadili heda: ma.
4 Apatse anthu malamulo awa: ‘Muli pafupi kudutsa mʼchigawo cha abale anu adzukulu a Esau okhala ku Seiri. Iwowa adzachita nanu mantha koma musamale kwambiri.
Isala: ili dunuma amane sia: ma, Dilia da dilia fi dunu, Iso egaga fi Idome agolo soge amo ganodini esala, ilia soge ganodini golili sa: ili, baligimu. Ilia da dilima beda: mu.
5 Musayambane nawo popeza sindidzakupatsani gawo lina lililonse la dziko lawo ngakhale poti mungoyika phazi. Ndamupatsa Esau dziko lamapiri la Seiri kuti likhale lakelake.
Be dilia da ilima mae gegema. Na da ilia soge fonobahadi fawane dilima hamedafa imunu. Amo Idome soge huluane Na da Iso egaga fi ilima i dagoi.
6 Inu muyenera kuwalipira ndi siliva pa chakudya chimene mudye ndi madzi amene mumwe.’”
Be dilia da ha: i manu amola hano, ilima bidiga lamu da defea.’”
7 Yehova Mulungu wanu wakudalitsani mʼntchito zonse za manja anu. Iye wakuyangʼanirani pa ulendo wanu wodutsa mʼchipululu chachikulu. Yehova Mulungu wanu wakhala nanu mʼzaka makumi anayi, ndipo simunasowe kalikonse.
Mousese da eno amane sia: i, “Dilia mae gogolema! Hina Gode da dilia hou huluane hahawane fidi. Dilia da wadela: i hafoga: i soge amo ganodini ahoanoba, E da dili noga: le ouligi. Amo ode40wali gidigi amoga E da mae yolesili, dilia liligi huluane dilima i dagoi.
8 Choncho tinapitiriza ulendo modutsa abale athu, adzukulu a Esau okhala ku Seiri. Tinapatukira njira ya ku Araba imene imachokera ku Elati ndi Ezioni Geberi ndipo tinayenda njira ya ku chipululu cha Mowabu.
Ninia Gode Ea sia: nababeba: le, asili, logo amo da Ila: de moilai amola Isionegiba moilai yolesili Maga: me Hanoga doaga: sa, amo logo ninia da yolesili guma: dini ahoanu, Moua: be sogega asi.
9 Ndipo Yehova anati kwa ine, “Musawavutitse Amowabu kapena kuwaputa kuti muchite nawo nkhondo popeza sindidzakupatsani gawo lina lililonse la dziko lawo. Ndinapereka Ari kwa adzukulu a Loti ngati chuma chawo.”
Hina Gode da nama amane sia: i, ‘Dilia da Moua: be dunu (Lode egaga fi) ilima mae gegema amola ilima se mae ima. Na da Aa moilai ilima i dagoi amola ilia soge Na da dilima hame imunu,’” Mousese da amane sia: i.
10 (Aemi, anthu amphamvu ndi ochuluka komanso ataliatali ngati Aanaki amakhala kumeneko.
(Dunu fi bagadedafa da Aa moilaiga esalu. Ilia fi dio da Imimi. Ilia sedade olei da dunu bagade eno amo A: nagimi fi ilia sedade olei defele ba: i.
11 Ngati Aanaki, nawonso ankawayesa kuti anali Arefai, koma Amowabu ankawatcha iwo Aemi.
Eno dunu da Imimi amola A: nagimi gilisili da Lefa: ime [dunu sedade bagade] dio asuli. Be Moua: be dunu da ilima Imimi dio asuli.
12 Ahori amakhala ku Seiri koma adzukulu a Esau anawapirikitsa. Iwo anawononga Ahori pamaso pawo nawakhalira pamalo pawo monga Aisraeli anachitira mʼdziko limene Yehova anawapatsa ngati chuma chawo).
Musa: Holaide dunu da Idome soge ganodini esalu. Be Iso egaga fi da amo dunu sefasili, fane legei dagoi. Amalalu, ilisu da amo soge ganodini fi. Isala: ili dunu fi da fa: no Ga: ina: ne sogega [Gode da ilima i] ilima ha lai dunu sefasi, amo defele Iso egaga fi da Holaide dunu sefasi.)
13 Ndipo Yehova anati, “Tsopano nyamukani ndipo muwoloke Chigwa cha Zeredi.” Choncho tinawoloka chigwacho.
Mousese da eno amane sia: i, “Amalalu, Gode Ea sia: beba: le ninia da Silede Hano amo degei dagoi.
14 Panapita zaka 38 kuchokera pa nthawi imene tinachoka ku Kadesi Barinea mpaka pamene tinawoloka Chigwa cha Zeredi. Pa nthawi imeneyi nʼkuti mʼbado wonse wa anthu ankhondowo utawonongeka ku msasa monga Yehova anawalumbirira.
Ninia da musa: Ga: idesie Bania fisili, ode38gidigili, amo hou ba: i. Amo ode ganodini Gode Ea sia: i defele ninia musa: dadi gagui amola asigilai gegesu dunu, huluane da bogoi dagoi ba: i.
15 Dzanja la Yehova linatsutsana nawo mpaka wonse anathera ku msasa.
Gode da ilima ha laiwane esalebeba: le, E da mae yolesili ili fane legelalu, huluane da hame ba: i.
16 Tsono atafa munthu wotsiriza mwa anthu ankhondowo,
Amalalu, musa: asigilai gegesu dunu huluane ninia fi ganodini da bogoi dagoi ba: loba,
17 Yehova anati kwa ine,
Hina Gode da nama amane sia: i,
18 “Lero mudutsa malire a Mowabu ku Ari podzera ku Ari.
‘Wali eso dilia Moua: be soge golili sa: ili, Aa moilai bai bagade ahoasu amoga baligima.
19 Mukafika kwa Aamoni, musawavutitse kapena kuwaputa, popeza sindidzakupatsani gawo lililonse la dziko la Aamoni. Ine ndalipereka dzikoli ngati chuma kwa adzukulu a Loti.”
Amalalu dilia da A: mone dunu (Lode egaga fi) ilia soge gadenene ba: mu. Be ilima mae gegema amola sia: ga mae gegema. Bai Na da amo soge Lode egaga fi ilima ia dagoiba: le, Na da amo soge dilima hame imunu.
20 (Ilinso ankaliyesa dziko la Arefai amene ankakhala kumeneko. Koma Aamoni ankawatcha iwo Azamuzumi.
(Amo soge ea dio eno da Lefa: ime [dunu sedade bagade musa: amoga esalu ilia dio]. Be A: monaide dunu da amo dunuma Sa: masamimi dio asuli.
21 Iwo anali anthu amphamvu ndiponso ochuluka, ataliatali ngati Aanaki. Yehova anawawononga ndi kuwachotsa pamaso pa Aamoni, amene anawapirikitsa nawakhalira pa malo pawo.
Ilia sedade olei da A: nagimi dunu defele ba: i. Ilia da dunu bagohame amola bagade fi dialu. Be Gode da amo dunu fi fane legei dagoi. Amalalu, A:mone fi dunu da ilia soge gesowale fi galu.
22 Yehova anachitanso chimodzimodzi ndi adzukulu a Esau omwe anakhazikika ku Seiri atawononga Ahori powachotsa pamaso pawo. Iwo anawapirikitsa Ahoriwo ndi kuwakhalira pamalo pawo mpaka lero.
Hina Gode da amo hou defele Idome dunu (ilia da Iso egaga fi wali Idome agolo sogega esala) amo fidimusa: hamoi. E da Holaide dunu fane legei dagoi. Amalalu, Idome dunu da ilia soge gesowale fi galu. Ilia wali amola amogai esala.
23 Ndipo za Aavi omwe ankakhala mʼmidzi yofika mpaka ku Gaza, anagonjetsedwa ndi Akafitori wochokera ku Akafitori nakhala pamalo pawo).
Soge amo da Medidela: inia Wayabo Bagade bega: diala, amoga dunu fi musa: Galidi Oga esalu ilia da fi galu. Musa: dunu fi amogai esalu da A: ifimi. Ilia da soge huluane asili, Ga: isa moilai bai bagadega doaga: le esalu. Be Galidi dunu da ili fane legele, ilia soge huluane gesowale fi galu.)
24 “Tsopano nyamukani, muwoloke khwawa la Arinoni. Taona ndapereka mʼmanja mwako Sihoni Mwamori mfumu ya Hesiboni ndi dziko lake lonse. Yambapo kutenga chuma chake ndi kumenyana naye nkhondo.
Mousese da eno amane sia: i, “Ninia da Moua: be soge golili sa: ili, baligili, Hina Gode da ninima amane sia: i, ‘Hadiga! Anone hano degema. Na da Saihone (A: moulaide ouligisu dunu ea soge da Hesiabone), e amola ea soge dilima i dagoi. Dilia ema doagala: ma amola ea soge gesowale fima.
25 Lero lomwe lino ndidzayamba kuyika chiopsezo ndi mantha pa mitundu yonse pansi pa thambo kuti akuope. Iwowo adzamva zambiri yako ndipo adzanjenjemera ndi kuwawidwa mtima chifukwa cha iwe.”
Na (Hina Gode) Na gasaga, dunu huluane da dilia fiba: le beda: mu. Dilia dio fawane sia: sea, dunu huluane da yaguguli beda: mu.’”
26 Ine ndinatuma amithenga kuchokera ku chipululu cha Kedemoti kupita kwa Sihoni mfumu ya Hesiboni kukanena mawu ofuna mtendere ndipo ndinati,
“Amalalu, ninia da Gedimode wadela: i soge amo ganodini esalu, na da Hesiabone hina bagade Saihone ema sia: adole iasu dunu asunasi. Ilia da ema olofomusa: amane sia: i,
27 “Tiloleni tidutse mʼdziko mwanu. Ife tidzangodutsa ndi msewu waukulu, ndipo sitidzapatukira kumanja kapena kumanzere.
‘Ninia da dia soge baligili masusa: dawa: lala. Ninia da moloiwane baligimu amola logo hame yolesimu.
28 Mutigulitse chakudya kuti tidye ndi madzi kuti timwe pa mtengo wa siliva. Mungotilola kuti tidutse, tikuyenda pansi
Ninia ha: i amola hano manu lamu amo bidi imunu. Ninia da dia soge baligili masunu fawane.
29 monga mmene anatichitira adzukulu a Esau okhala ku Seiri ndi Amowabu okhala ku Ari mpaka titawoloka Yorodani kufika ku dziko limene Yehova Mulungu wathu akutipatsa.”
Amalalu, ninia da Yodane Hano degele, soge amo ninia Hina Gode da ninima iaha amo ganodini fimu. Iso egaga fi Idome soge ganodini esalu amola Moua: be dunu Aa ganodini esalu, da mae higale, ninia da ilia soge baligili masunu da defea sia: i.’
30 Koma Sihoni mfumu ya Hesiboni sanalole kuti tidutse. Popeza Yehova Mulungu wanu analimbitsa mzimu wake, nawumitsa mtima wake kuti amupereke mʼmanja mwanu monga wachitira lero lino.
Be hina bagade Saihone da ninia baligili masunu logo ga: i dagoi. Ninia da Saihone fane legele ea soge lamusa: Hina Gode da ea hou gasa fi agoane hamoi. Ninia da wali ea soge amogai fi diala.
31 Yehova anati kwa ine, “Taona ndayamba kumupereka Sihoni ndi dziko lake kwa iwe. Tsopano yamba kugonjetsa ndi kulanda dziko lake.”
Amalalu, Hina Gode da nama amane sia: i, ‘Ba: ma! Na da hina bagade Saihone amola ea fi gasa hame agoane hamoi dagoi. Dilia ea soge gesowale fima.’
32 Sihoni ndi ankhondo ake atabwera kudzakumana nafe mwankhondo pa Yahazi,
Saihone amola ea dadi gagui dunu huluane da Ya: iha: se soge gadenene ninima gegemusa: misi.
33 Yehova Mulungu anamupereka iye kwa ife ndipo tinankantha, pamodzi ndi ana ake aamuna ndi gulu lake lonse lankhondo.
Be Hina Gode da ninima gasa i. Ninia da Saihone amola egefe, ea dunu huluane medole legei dagoi.
34 Pa nthawi imeneyi tinamulanda mizinda yake yonse ndi kuyiwononga kwathunthu, amuna, akazi ndi ana. Palibe amene anapulumuka.
Amo esoga, ninia da moilai huluane lale mugului dagoi. Ninia da dunu, uda amola mano, huluane medole legei dagoi.
35 Koma ziweto ndi zinthu zonse zimene tinalanda mʼmizinda imene tinagonjetsayo, tinazitenga kukhala zathu.
Ninia ilia bulamagau huluane lai amola liligi huluane moilai ganodini amo lai dagoi.
36 Kuchokera ku Aroeri mʼmphepete mwa mtsinje wa Arinoni ndi ku mzinda wa ku mtsinjeko mpaka kukafika ku Giliyadi, panalibe ndi mzinda ndi umodzi omwe umene unatikanika kuwugonjetsa. Yehova Mulungu wathu anatipatsa onsewo.
Ninia Hina Gode da ninia logo fodoiba: le, ninia moilai huluane amo Aloua (amo da Anone fago bega: dialu) amola moilai eno Anone fago ganodini dogoa dialu amola eno moilai huluane asili, Gilia: de sogega doaga: le, huluane lai dagoi. Moilai huluane ilia sisiga: le gagoi da ninima gasa hame agoai ba: i.
37 Molingana ndi lamulo la Yehova Mulungu wathu, simunalowerere dziko lililonse la Aamoni, ngakhale dera lonse la ku mtsinje wa Yaboki kapena dera lozungulira dera la ku mizinda ya ku mapiri.
Be ninia A: monaide dunu ilia soge amola soge amo Ya: boge Hano bega: dialu amola moilai agolo soge ganodini dialu amola soge huluane Hina Gode da ninima mae masa: ne sia: i, amoga ninia da hame asi.”

< Deuteronomo 2 >