< Deuteronomo 16 >

1 Samalirani mwezi wa Abibu ndi kukondwerera Paska wa Yehova Mulungu wanu, chifukwa pa mwezi wa Abibu, usiku, Iye anakutulutsani mu Igupto.
Dilia Hina Godema nodone dawa: ma: ne, Abibi oubi amoga Baligisu Lolo Nasu hamoma. Amo oubi ganodini E da gasi afae dili Idibidi sogega esalu amodili gadili masa: ne fadegai.
2 Mumuphere Yehova Mulungu wanu nsembe ya Paska, chiweto chochokera pa nkhosa zanu kapena ngʼombe zanu kumalo kumene Yehova adzasankha kuti akhazikeko dzina lake.
Dilia Hina Godema sia: ne gadomusa: sogebi E da ilegei, amoga masa. Amogawi, dilia sibi o bulamagau afae amo Hina Godema nodomusa: Baligisu Lolo moma: ne, medole legema.
3 Musadyere pamodzi ndi buledi wopanga ndi yisiti, koma kwa masiku asanu ndi awiri muzidya buledi wopanda yisiti, buledi wa masautso, chifukwa munachoka ku Igupto mwamsangamsanga kuti pa masiku onse a moyo wanu muzikumbukira nthawi imene munanyamukira ku Igupto.
Amo lolo nasea, agi amo yisidi gilisi amo mae moma. Eso fesuale amoga dilia da yisidi hame sali agi moma. Dilia da musa: Idibidi soge hedolowane fisimusa: momagele mai, amo defele moma. Dilia da musa: Idibidi soge ganodini se bagade nabasu be eso afaega dilia gadili asi. Amo se nabasu dawa: ma: ne, amo agi (se nabasu agi) moma.
4 Yisiti asapezeke kwa masiku asanu ndi awiri pa katundu wanu mʼdziko lanu lonse. Ndipo musasunge nyama imene mwapereka nsembe madzulo a tsiku loyamba mpaka mmawa.
Eso fesuale amoga Isala: ili dunu ilia diasu ganodini, yisidi da hamedafa ba: mu. Amola eso age amoga, ohe medole legei amo ea hu da amo gasi ganodini huluanedafa manu. Golale hahabe amo ea hu da hamedafa ba: mu.
5 Musamangopereka nsembe ya Paska mu mzinda wina uliwonse umene Yehova Mulungu wanu wakupatsani,
6 koma ku malo wokhawo amene Iye adzawasankhe kukhazikitsako Dzina lake. Kumeneko ndiye muzikapereka nsembe ya Paska madzulo, pamene dzuwa likulowa, pa tsiku lokumbukira kutuluka mu Igupto.
Hina Godema sia: ne gadomusa: sogebi ilegei amoga Baligisu Lolo Nasu ohe medole legema. Soge amo dilia Hina Gode da dilima iaha, amo ganodini sogebi eno amoga mae medole legema - ilegei sogebi fawane. Eso dabe galu amoga dilia Idibidi soge fisi. Amaiba: le, eso dabe amoga Baligisu ohe medole legema.
7 Muyiwotche ndi kuyidya pa malo pamene Yehova Mulungu wanu adzasankhe. Kenaka mmawa mubwerere ku matenti anu.
Amo hu hano ganodini gobema amola ilegei sogebi amoga moma. Golale hahabe, dilia diasuga bu masa.
8 Kwa masiku asanu ndi limodzi muzidya buledi wopanda yisiti ndipo pa tsiku lachisanu ndi chiwiri muzikhala ndi msonkhano wa Yehova Mulungu wanu ndipo musamagwire ntchito iliyonse.
Eso gafeyale ganodini, yisidi hame sali agi moma. Amasea, eso fesu amoga, hawa: hamosu mae hamoma, be dilia Hina Godema nodone sia: ne gadomusa: gilisima.
9 Muziwerenga masabata asanu ndi awiri kuyambira pamene mwatenga chikwakwa ndi kuyamba kumweta tirigu wachilili.
Dilia da gagoma faisu eso doaga: sea, fa: no hi fesuale idima.
10 Pamenepo muzichita Chikondwerero cha Masabata pamaso pa Yehova Mulungu wanu popereka chopereka chaufulu mofanana ndi madalitso amene Yehova Mulungu wakupatsani
Amasea, dilia Hina Godema nodomusa: , Ha: i Manu Gamibi Lolo Nasu (Bedigosidi) hamoma. E da dilima hahawane udigili iasu, amo dawa: le Ema ima: ne, hahawane udigili iasu Ema gaguli misa.
11 Ndipo inu, ana anu aamuna, aakazi, antchito anu aamuna, adzakazi, Alevi a mʼmizinda mwanu, alendo, ana ndi akazi amasiye okhala pakati panu, mukondwere pamaso pa Yehova Mulungu wanu ku malo amene adzawasankhe kukhazikitsako dzina lake.
Dilia, dilia mano, dilia hawa: hamosu dunu, Lifai dunu, ga fi dunu, guluba: mano amola didalo dilia moilai ganodini esala, amo huluane dilia Hina Gode ba: ma: ne, Ea ilegei nodomusa: sogebi amo ganodini hahawane gilisima.
12 Kumbukirani kuti inunso munali akapolo ku Igupto, ndiye muzitsatira malangizo awa mosamalitsa.
Amo gasa bagade sia: noga: le nabima. Dilia da musa: Idibidi soge ganodini udigili hawa: hamosu dunu esalu. Amaiba: le, mae gogolema.
13 Mukatha kukolola tirigu wanu ndi kupsinya vinyo wanu, muzikhala ndi Chikondwerero cha Misasa kwa masiku asanu ndi awiri.
Dilia da gagoma huluane fai dagosea amola waini huluane hamoi dagosea, eso fesuale amoga Fasela Diasuga Lolo Nasu Gilisisu hahawane hamoma.
14 Musangalale pa chikondwerero chanu, inu, ana anu aamuna, aakazi, antchito anu aamuna, adzakazi, Alevi, alendo, ana ndi akazi amasiye amene ali mʼmizinda yanu.
Dilia, dilia mano, dilia hawa: hamosu dunu, Lifai dunu, ga fi dunu, guluba: mano amola didalo dilia moilai ganodini esala, amo huluane hahawane gilisima.
15 Kwa masiku asanu ndi awiri muzichita chikondwererochi kwa Yehova Mulungu wanu kumalo kumene Yehova adzasankhe. Pakuti Yehova Mulungu wanu adzakudalitsani inu pa zokolola zanu ndi pa ntchito za manja anu, ndipo chimwemwe chanu chidzakhala chathunthu.
Dilia Hina Godema nodomusa: , eso fesuale amoga amo Lolo Nasu gilisisu hahawane hamoma. Bai Hina Gode da dilia ha: i manu faisu amola dilia hawa: hamosu hahawane dogolegelewane fidi dagoi.
16 Amuna onse azionekera pamaso pa Yehova Mulungu katatu pa chaka ku malo amene Iye adzasankha. Pa Chikondwerero cha Buledi wopanda Yisiti, pa Chikondwerero cha Masabata ndi pa Chikondwerero cha Misasa. Munthu aliyense asadzapite pamaso pa Yehova wopanda kanthu mʼmanja mwake.
Dilia Isala: ili fi dunu huluane da ode huluane amoga udianawane Hina Godema nodone sia: ne gadomusa: Ea ilegei sogebiga gilisima: ne sia: ma. Amo Lolo Nasu udiana da: 1. Baligisu Lolo Nasu Gilisisu 2. Ha: i Manu Gamibi Lolo Nasu Gilisisu 3. Sogega Fasela Diasuga Lolo Nasu Gilisisu.
17 Aliyense wa inu adzabweretse mphatso molingana ndi momwe Yehova Mulungu wanu wakudalitsirani.
Amo gilisisu amoma dunu huluane da hahawane iasu gaguli misa: ne sia: ma. Dilia Hina Gode da dunu hisu hisu ilima hahawane dogolegelewane iabe, amo defele e da gaguli misunu da defea.
18 Musankhe oweruza ndi akuluakulu a fuko lanu lililonse mu mzinda uliwonse umene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, ndipo adzaweruza anthuwa mwachilungamo.
Moilai huluane amo dilia Hina Gode da dilima iasea, amo ganodini fofada: su dunu amola ouligisu dunu ilegema. Amo dunu da dunu huluane ilima defele fofada: mu.
19 Musamakhotetse chiweruzo kapena kukondera. Musamalandire chiphuphu pakuti chiphuphu chimadetsa mʼmaso anthu a nzeru ndi kusintha mawu awo kuti mlandu uyipire osalakwa.
Ilia da moloidafa fofada: su hou mae yolesili, dunu eno da bagade eno da hamedei agoane hamedafa ba: mu. Ilia da moloidafa fofada: su yolesima: ne, hano suligi mae lama: mu. Bai hano suligi da bagade dawa: su dunu amola moloidafa dunu amo ilia si wadela: sa, amola ilia fofada: su da moloi hame ba: mu.
20 Tsatani chilungamo chokhachokha basi kuti mukhale ndi moyo ndi kutenga dziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani.
Be dilia da dunu huluane defele ba: ma amola hou huluane moloidafa hamoma. Amasea, dilia da soge amo dilia Hina Gode da dilima iaha, amo huluane gesowale fimu amola amo ganodini eso huluane esalumu.
21 Musazike mtengo wina uliwonse wa mafano a Asera pambali pa guwa lansembe la Yehova Mulungu wanu,
Dilia da dilia Hina Godema oloda hamosea, amoga dafulili leloma: ne ifa uda ‘gode’ agoane liligi ea dio A: sela mae bugima.
22 ndipo musayimike mwala wachipembedzo pakuti Yehova Mulungu wanu amadana nazo zimenezi.
Amola loboga hamoi ogogosu ‘gode’ igi mogomogoi amoma sia: ne gadomusa: mae hamoma. Hina Gode da agoai liligi bagadewane higasa.

< Deuteronomo 16 >