< Deuteronomo 14 >
1 Inu ndinu ana a Yehova Mulungu wanu. Osamadzichekacheka kapena kudzimeta pamphumi chifukwa cha abale anu amene amwalira,
Un e nyithind Jehova Nyasaye ma Nyasachu. Kik usar dendu kata uliel yie wiu, kuywago ngʼama otho, kata lielo pat wangʼu,
2 pakuti ndinu anthu opatulika a Yehova Mulungu wanu. Pakati pa anthu onse pa dziko lonse lapansi, Yehova wasankha inu kuti chikhale chuma chake chamtengo wapatali.
nimar un oganda mowal ne Jehova Nyasaye ma Nyasachu. Kuom ogendini manie wangʼ piny, Jehova Nyasaye oseyierou mondo ubed mwandune mogeno.
3 Musamadye chinthu chilichonse chonyansa.
Kik ucham gimoro amora makwero.
4 Nyama zomwe mukhoza kudya ndi izi: ngʼombe, nkhosa, mbuzi,
Magi e kit le gi jamni munyalo chamo: rwath, rombo, diel,
5 mbawala, gwape, mphoyo, mphalapala, ngoma, nyumbu ndi mbalale.
ogunde, nyakech, ngawo, diend bungu, abur, mwanda gi rombe manie gode.
6 Nyama iliyonse imene ili ndi chipondero chogawikana pakati ndi yobzikula mukhoza kudya.
Unyalo chamo kit le moro amora gi jamni ma ombongʼ tiendegi opogore ariyo kendo manyamo kambula.
7 Komabe pakati pa nyama zimene zimabzikula kapena zogawikana zipondero, zimene simukuyenera kudya ndi ngamira, kalulu ndi mbira. Zimenezi ngakhale zimabzikula, zipondero zake sizogawikana, choncho ndi zodetsedwa, musadye.
To kuom mago manyamo kambula kata mago ma ombongʼ tiendegi opogore ahinya, ok onego ucham kaka ngamia, apwoyo, gi ogwangʼ terere kata obedo ni ginyamo kambula, ombongʼ tiendegi ok opogore, to gin gik mogak ne un.
8 Nkhumba simabzikula ndi yodetsedwanso ngakhale ili ndi zipondero zogawikana. Musamadye nyama yake kapena kukhudza imene yafa.
Anguro bende en gima ogak kata obedo ni tiendene opogore kamano, ok onyam kambula. Kik ucham ring-gi kata kik umul ringregi motho.
9 Mwa zamoyo zonse zimene zimakhala mʼmadzi, mukhoza kudya chilichonse chimene chili ndi minga ya pa msana ndi mamba.
To kuom gik moko duto modakie pi, unyalo chamo mago man kod thuokgi kod kalagakla.
10 Koma chilichonse chimene chilibe minga ya pa msana ndi mamba musadye pakuti nʼchodetsedwa.
To mago duto maonge gi thuokgi kata kalagakla ok onego ucham nimar kuomu gin gik mogak.
11 Mukhoza kudya mbalame iliyonse yoyenera kudya.
Unyalo chamo winyo moro amora ma ok ler.
12 Koma simukuyenera kudya izi: mphungu, nkhwazi, mwimba,
Winy ma ok onego ucham e magi: ongo, achuth, gi olit,
13 nankapakapa, akamtema, akhungubwi a mitundu yonse, ndi mtundu uliwonse wa miphamba,
gi otenga kod kit otenga duto, gi okun-okun,
14 mtundu uliwonse wa khwangwala,
gi kit agak duto,
15 kadzidzi wamphondo, kadzidzi wodzuma, chipudo, mtundu uliwonse wa akabawi,
kit tula moro amora, gi okok, kata kit olith duto,
16 kadzidzi wamngʼono, chiswankhono ndi mantchichi,
gi tula matin, tula maduongʼ gi tula marachar,
gi tula modak e thim gi mbusi gi achuth gi osou,
18 indwa, zimeza za mitundu yonse, nsadzu ndi mleme.
gi nyamnaha, gi ngʼangʼa, tula kod olik tiga.
19 Zowuluka zonse za miyendo inayi ndi zodetsedwa. Musamadye zimenezi.
Kute duto mafuyo e kweth kik ucham nimar gin gik makwero.
20 Koma chowuluka chilichonse choyenera kudya mukhoza kudya.
To unyalo chamo gik mafuyo gi buombgi ma ok kwero.
21 Musamadye chilichonse chimene mwachipeza chofaifa. Mukhoza kupatsa mlendo amene akukhala mu mzinda wina uliwonse wa mizinda yanu. Iyeyo akhoza kudya kapena mukhoza kugulitsa kwa wina aliyense amene sali wa mtundu wanu. Koma inu ndinu anthu opatulika a Yehova Mulungu wanu. Musamaphike mwana wambuzi mu mkaka wa mayi wake.
Kik ucham gimoro ma uyudo ka osetho kende. Unyalo miye japiny moro amora manie miechu mondo ochame kata unyalo uso ne japiny moro, nikech un oganda mowal ni Jehova Nyasaye ma Nyasachu. Kutedo nyadiel to kik uole cha min.
22 Muzionetsetsa kuti mukupatula chakhumi pa zokolola zanu chaka chilichonse.
Neni uketo tenge achiel kuom apar mag giu ma puotheu onyago.
23 Muzidyera chakhumi cha tirigu wanu, vinyo wanu watsopano ndi mafuta, ndi ana oyamba kubadwa a ngʼombe zanu pamaso pa Yehova Mulungu wanu pa malo amene adzasankhe ngati kokhalako dzina lake, kuti muphunzire kuopa Yehova Mulungu wanu.
Chokuru achiel kuom apar mar chambu, divai manyien kod mo, kaachiel gi nyithindo makayo mag kweth dhou kod kweth jambu e nyim Jehova Nyasaye ma Nyasachu kama noyier mondo oluongie Nyinge mondo omi ubed joma oluoro Jehova Nyasaye ma Nyasachu ndalo duto.
24 Koma ngati malo amenewa ali kutali kwambiri ndipo kuti inu mwadalitsidwa ndi Yehova Mulungu wanu, ndipo simungathe kunyamula chakhumi chanu (chifukwa chakuti malo amene Yehova adzasankha kukayikako dzina lake ali kutali kwambiri),
Ka dipo ni kar romono bor kodi ma ok inyal tero achiel kuom apar mari ma Jehova Nyasaye ma Nyasachi osegwedhigo (nikech kama Jehova Nyasaye oyiero ne Nyinge bor kodi),
25 ndiye musinthitse chakhumi chanucho ndi siliva, ndipo mutenge silivayo ndi kupita naye kumalo kumene Yehova Mulungu wanu adzasankhe.
to inyalo loko mwandugo pesa mondo iter kama Jehova Nyasaye ma Nyasachi biro yiero.
26 Gwiritsani ntchito silivayo kugula chilichonse chimene muchifuna monga ngʼombe, nkhosa, vinyo kapena zakumwa zina zosasitsa, kapena china chilichonse chimene muchifuna. Ndipo inu ndi anthu a pa banja panu mudzazidyera komweko pamaso pa Yehova Mulungu wanu ndi kukondwera.
Konyri gi pesano ka ingʼiewogo gimoro ma ihero; obed ring dhiangʼ kata ring rombo, divai kata math moketo thowi kata gimoro amora ma chunyi digombi. Eka in kod joodi duto nuchiem kanyo e nyim Jehova Nyasaye ma Nyasachu gi mor.
27 Alevi okhala mʼmizinda yanu musaleke kuwathandiza popeza alibe gawo lawo la chuma kapena cholowa chawochawo.
Kendo kik wiu wil kod joka Lawi modak e miechu, nimar gionge gi pok margi kata girkeni mowalnegi.
28 Kumapeto kwa zaka zitatu zilizonse muzibweretsa zakhumi zonse pa zokolola za chaka chimenecho ndi kuzisunga mʼmidzi yanu,
Bangʼ higni adek, keluru achiel kuom apar duto mosechiw e higano mondo ukan-gi e miechu,
29 kuti Alevi (amene alibe gawo lawo la chuma kapena cholowa chawochawo), alendo, ana ndi akazi amasiye, amene akukhala mʼmizinda yanu akhoza kubwera kudzadya ndi kukhuta. Ndipo kuti akutero Yehova Mulungu wanu akudalitseni pa ntchito zanu zonse.
mondo omi joka Lawi (maonge pok kata girkeni ma owalnegi), to gi jodak, nyithind kiye kod mon ma chwogi otho modak e miechu obi ochiem mayiengʼ kendo mondo Jehova Nyasaye ma Nyasachu ogwedhu e gik moko duto ma lwetu timo.