< Deuteronomo 13 >

1 Ngati mneneri kapena wina aliyense amene amanena zamʼtsogolo mwa maloto atuluka pakati panu, nalengeza za chizindikiro chozizwitsa kapena chodabwitsa,
“Nxa umphrofethi, loba umuntu oboniswa ngamaphupho, angavela phakathi kwenu abesebika imilingo loba isimanga,
2 chinthu nʼkuchitikadi, tsono iyeyo nʼkunena kuti, “Tiyeni titsatire milungu ina, tiyeni tiyipembedze,” (kunena milungu imene simunayidziwe),
kuthi leyomilingo loba lesosimanga ayabe ekhulume ngaso, kubonakale kusenzakala, abesesithi, ‘Asilandeleni abanye onkulunkulu’ (onkulunkulu elingabaziyo) ‘njalo asibakhonzeni,’
3 musamumvere mneneriyo kapena wolotayo. Yehova Mulungu wanu afuna akuyeseni kuti aone ngati mumamukonda ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse.
lingalaleli amazwi alowo mphrofethi loba umuntu wamaphupho. UThixo uNkulunkulu wenu uzabe elilinga efuna ukubona kumbe liyamthanda yini ngezinhliziyo zenu kanye langemiphefumulo yenu yonke.
4 Muyenera kutsatira Yehova Mulungu wanu, ndipo ndi Iyeyo amene muyenera kumuopa. Muzisunga malamulo ake ndi kumamumvera, muzimutumikira ndipo kumukangamira Iyeyo.
NguThixo uNkulunkulu wenu okumele limlandele, kanti nguye uqobo okumele limesabe. Gcinani imilayo yakhe njalo limlalele; mkhonzeni libambelele liqine kuye.
5 Mneneri kapena wolotayo ayenera kuphedwa, popeza analalikira zopandukira Yehova Mulungu wanu, amene anakutulutsani ku Igupto ndi kukupulumutsani ku dziko la ukapolo. Wolalikirayo anafuna kukupatutsani pa njira imene Yehova Mulungu wanu anakulamulirani kuti muyitsatire. Muzichotsa choyipa pakati panu.
Lowo mphrofethi loba lowomuntu wamaphupho akhe kumele abulawe, ngoba utshumayele wakhuthaza ukuhlamukela uThixo uNkulunkulu wenu, owalikhupha eGibhithe njalo walihlenga elizweni lobugqili; njalo ngumuntu obezama ukuliphambula endleleni uThixo uNkulunkulu wenu alilaya ngayo ukuba liyilandele. Kumele lihlambulule ububi phakathi kwenu.
6 Ngati mʼbale wanu weniweni kapena mwana wanu wamwamuna kapena wamkazi, kapena mkazi wanu wokondedwa, kapena mnzanu wapamtima akukakamizani mwachinsinsi, nʼkumati, “Tiyeni tipite tikapembedze milungu ina” (milungu imene inuyo kapena makolo anu sanayidziwe,
Nxa umfowenu uqobo, loba indodana loba indodakazi yakho, loba umfazi wakho omthandayo, loba umngane wakho osekhwapheni, angavele akuhuge ensitha, esithi, ‘Asihambe siyekhonza abanye onkulunkulu’ (onkulunkulu lina laboyihlo elingazange libazi,
7 milungu ya anthu okuzungulirani, kaya ndi apafupi kapena akutali, kuchokera kumapeto mpaka kumapeto kwina kwa dziko lapansi),
onkulunkulu babantu elakhelene labo, eduzane loba khatshana, kusukela emaphethelweni esigaba kusiyaphutsha ngale kwaso),
8 musamugonjere kapena kumumvera. Musamumvere chisoni. Musamuleke kapena kumutchinjiriza.
lingamvumeli futhi lingamlaleli. Lingamtshengiseli uzwelo. Lingamphephisi njalo lingamvikeli.
9 Mumuphe ndithu. Dzanja lanu likhale loyambirira kumupha, kenaka manja a anthu ena onse.
Kumele ngeqiniso abulawe. Isandla senu kumele sibe yiso esikhokhela ukubulawa kwakhe, kulandele zonke ezabanye abantu.
10 Mumuponye miyala mpaka kumupha, chifukwa anafuna kukupatutsani pa njira ya Yehova Mulungu amene anakutulutsani ku Igupto, dziko la ukapolo.
Mkhandeni ngamatshe limbulale, ngoba uzame ukuliphambula elisusa kuThixo uNkulunkulu wenu, owalikhupha eGibhithe, walikhupha elizweni lobugqili.
11 Tsono Aisraeli onse adzamva nachita mantha, ndipo palibe mmodzi pakati panu amene adzachitenso choyipa chotere.
Ngalokho wonke u-Israyeli uzakuzwa esabe, kakho loyedwa phakathi kwenu ozake aphinde enze into enjalo futhi.
12 Ngati mumvetsedwa kuti ku umodzi mwa mizinda imene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kuti mukhalemo,
Lingezwa kuthiwa kuledolobho elikwenzayo lokhu phakathi kwamadolobho eliwaphiwe nguThixo uNkulunkulu wenu ukuba lihlale kuwo
13 kwapezeka anthu ena oyipa pakati panu ndipo asocheretsa anthu ambiri mʼmizinda yanu, pomanena kuti, “Tiyeni tikapembedze milungu ina” (milungu imene simunayidziwe),
kulamadoda aphakathi kwenu asedukise abantu balawo madolobho, esithi, ‘Asihambeni siyokhonza abanye onkulunkulu’ (onkulunkulu elingakaze libazi),
14 mukuyenera kufunsa, kulondola ndi kufufuza bwino nkhaniyo. Ndipo ngati zitatsimikizikadi kuti ndi zoona kuti chinthu chonyansa chotere chachitikadi pakati panu,
kufanele libuzisise, lichwayisise lihlole ngokupheleleyo. Kuthi nxa kuliqiniso njalo kugcwaliseke ukuthi lesisinengiso sikhona phakathi kwenu,
15 muyenera kuwapha onse okhala mu mzinda umenewo. Muwonongeretu kwathunthu mzindawo, anthu ake ndi ziweto zake zomwe.
kumele lifake inkemba ngeqiniso kulabo bonke abahlala kulelodolobho. Lilichithe litshabalale ngeqiniso, abantu bakhona kanye lezifuyo zakhona.
16 Katundu yense wa anthu mu mzindawo mumuwunjike pamodzi pakatikati pa bwalo losonkhanako ndipo mutenthe mzindawo pamodzi ndi katundu wake yense monga nsembe yathunthu yopsereza ya kwa Yehova Mulungu wanu. Mzinda umenewo ukhale bwinja mpaka muyaya, usadzamangidwenso.
Buthelelani konke okuthunjiweyo kulelodolobho phakathi enzikini yalo enkundleni yokuhlanganela kwabantu lilithungele litshe lilobe lelodolobho kanye lempahla zalo zonke njengomnikelo wokutshiswa kuThixo uNkulunkulu wenu. Kumele lisale lilunxiwa lelodolobho kokuphela, lingakhiwa kutsha futhi.
17 Musapezeke ndi kanthu kalikonse koyenera kuwonongedwa kuti Yehova abweze mkwiyo wake wochititsa manthawu. Adzakuchitirani chifundo ndi kukumverani chisoni, ndipo adzakuchulukitsani monga analonjeza mwa lumbiro kwa makolo anu,
Akungabi lokukodwa kwalokho okusoliweyo okuzafunyanwa ezandleni zenu, ukuze uThixo adedise ulaka lwakhe oluvuthayo; alitshengisele umusa wakhe, abe lozwelo kini, andise amanani enu, njengoba wathembisa ngesifungo kubokhokho benu,
18 chifukwa mumamvera Yehova Mulungu wanu, kusunga malamulo ake onse amene ndikukupatsani lero lino ndi kuchita zoyenera pamaso pake.
ngoba lilalela uThixo uNkulunkulu wenu, ligcina imilayo yakhe le engilinika yona lamuhla njalo lisenza okulungileyo emehlweni akhe.”

< Deuteronomo 13 >