< Danieli 6 >

1 Kunamukomera Dariyo kusankha akalonga 120 kuti alamulire mu ufumu wonse,
Darius loh a doe phoeiah tah a ram ah mangpa ya pakul a pai sak tih ram tom ah om uh.
2 ndikusankha nduna zazikulu zitatu kuti ziwayangʼanire ndipo imodzi mwa ndunazo anali Danieli. Akalongawo amayangʼaniridwa ndi nduna zazikuluzo kuti zinthu za mfumu zisawonongeke.
Daniel te tah amih taemrhaikung pathum khuikah pakhat la om tih amih kah a soah om. Mangpa la aka om rhoek he a taengah saithainah a paek tih manghai khaw a vaitah om pawh.
3 Tsono Danieli anadzionetsa kuti akhoza kugwira ntchito bwino kopambana nduna zinzake chifukwa anali wanzeru kwambiri. Ndiye mfumu inaganiza zomuyika kuti akhale woyangʼanira ufumu wonse.
Te vaengah Daniel tah taemrhaikung rhoek neh mangpa rhoek lakli ah a poekhloep om. He kong ah he a khuiah mueihla lang tih manghai loh anih a ram pum soah pai sak hamla cai.
4 Chifukwa cha ichi, anzake ndi akalonga anayesa kupeza zifukwa zomutsutsira Danieli pa kayendetsedwe ka ntchito za dzikolo, koma sanapeze cholakwa chilichonse. Iwo sanapeze chinyengo mwa iye, chifukwa anali wokhulupirika ndipo sankachita chinyengo kapena kutayirira ntchito.
Tedae taemrhaikung rhoek neh mangpa la aka om rhoek loh ram soehsalnah te Daniel taengah hmuh hamla a longim a tlap uh. Te cakhaw he kong dongah he anih tah a uepom dongah longim neh a tholh pakhat khaw a hmuh thai moenih. Dalrhanah neh a hong boeih he tah a pum dongah a tueng moenih.
5 Pomaliza, anthu awa ananena kuti, “Sitidzapeza cholakwa chilichonse chomutsutsira Danieli kupatula chokhacho chimene chikhudza chipembedzo cha Mulungu wake.”
Te vaengah tah tekah hlang rhoek loh, “Daniel taengah longim boeih he m'hmuh moenih, a Pathen kah oltlueh dongah a om bueng ni a soah m'hmuh dae,” a ti uh.
6 Choncho akalonga ndi nduna pamodzi anapita kwa mfumu ndipo anati: “Inu mfumu Dariyo, mukhale ndi moyo wautali!
Te dongah taemrhaikung rhoek neh mangpa rhoek he manghai taengla khong tih amah te, “Darius manghai kumhal duela hing pai saeh,” a ti nauh.
7 Nduna zoyendetsa ufumu wanu, aphungu, akalonga ndi abwanamkubwa tonse tagwirizana kuti inu mfumu mukhazikitse lamulo ndi kulisindikiza kuti aliyense amene apemphera kwa mulungu wina kapena kwa munthu kupatula kwa inu mfumu, pa masiku makumi atatu otsatirawa, adzaponyedwa mʼdzenje la mikango.
Ram kah taemrhaikung rhoek neh ukkung, mangpa rhoek, olrhoep rhoek neh boei rhoek tah boeih olrhoep uh tih, “Hnin sawmthum khuiah manghai nang kah voel ah pathen neh hlang khat khat taengah thangthuinah neh aka thangthui boeih tah sathueng buep la voeih ham manghai kah oltloek neh olpaek a tloh la a saii sak.
8 Tsopano inu mfumu khazikitsani lamulo limeneli ndipo musindikizepo dzina lanu kuti lisasinthike monga mwa malamulo a Amedi ndi Aperezi, amene sasinthidwa.”
Te dongah, “Manghai aw, olpaek mah cak sak lamtah cadaek te daek laeh. Te te Media neh Persia oltlueh bangla thovael ham pawt tih hoilae boel saeh,” a ti uh.
9 Choncho mfumu Dariyo anasindikizapo dzina lake pa lamuloli.
He kong dongah he manghai Darius loh cadaek neh olpaek te a daek.
10 Danieli atamva kuti lamulo lasindikizidwa, anapita ku nyumba kwake nalowa mʼchipinda chapamwamba chimene mazenera ake anali otsekula kuloza ku Yerusalemu. Katatu pa tsiku iye ankagwada pansi pa mawondo ndipo amapemphera, kuyamika Mulungu wake, monga momwe ankachitira kale.
Cadaek a daek te a ming vaengah Daniel tah amah im la cet. A imhman ah Jerusalem benkah bangbuet te a ong tih hnin at ah voei thum a khuklu dongah cungkueng tih thangthui. Te kong dongah hlamat lamloh a saii pah te a om coeng dongah a Pathen te a uem.
11 Ndipo anthu awa anapita pamodzi ndi kukapeza Danieli akupemphera ndi kupempha Mulungu wake kuti amuthandize.
Te vaengah hlang rhoek tah puei uh tih Daniel loh a Pathen taengah thangthui neh a bih te a hmuh uh.
12 Kotero iwo anapita kwa mfumu ndipo anayankhula naye za lamulo lake kuti, “Kodi simunasindikize lamulo lakuti pa masiku makumi atatu otsatirawa aliyense amene apemphera kwa mulungu wina aliyense kapena kwa munthu kupatula kwa inu mfumu, adzaponyedwa mʼdzenje la mikango?” Mfumu inayankha kuti, “Lamulo lilipobe monga mwa malamulo a Amedi ndi Aperezi, amene sangathe kusinthika.”
Te dongah cet uh tih manghai kah olpaek kawng neh manghai te, “Hnin sawmthum khuiah manghai namah voel ah pathen neh hlang khat khat taengah aka thangthui hlang boeih tah sathueng khui la voei saeh tila olpaek na daek moenih a?” a ti nauh. Te dongah manghai loh a doo tih, “Media neh Persia oltlueh bangla ol cak tih te n'hoilae thai moenih,” a ti nah.
13 Kenaka iwo anati kwa mfumu, “Danieli, amene ndi mmodzi mwa akapolo ochokera ku Yuda, sakulabadira inu mfumu, kapena lamulo limene munasindikizapo dzina lanu lija. Iye akupempherabe katatu pa tsiku.”
Te vaengah a doo uh tih manghai taengah, “Judah hlangsol ca lamkah Daniel tah manghai namah taengkah saithainah neh olpaek na daek te ngai pawt tih a thangthuinah neh hnin at ah voei thum thangthui,” a ti nauh.
14 Mfumu itamva izi, inavutika kwambiri mu mtima mwake. Iyo inayesa kupeza njira yopulumutsira Danieli. Iyo inachita chotheka chilichonse kufikira kulowa kwa dzuwa kuti imupulumutse.
Manghai loh ol a yaak vaengah amah te muep hah tih Daniel te a loeih sak ham a ko om. Khomik a tlak hil anih huul ham thakthae la om.
15 Ndipo anthuwo anapita pamodzi kwa mfumu ndipo anati kwa iye, “Kumbukirani, inu mfumu kuti monga mwa lamulo la Amedi ndi Aperezi, palibe chimene mfumu inalamulira kapena kukhazikitsa chimasinthidwa.”
Te vaengah hlang rhoek te manghai taengla puei uh thae tih manghai te, “Manghai aw, Media neh Persia kah oltlueh bangla, manghai kah olpaek neh oltloek a khueh boeih tah thovael thai pawt te ming,” a ti nauh.
16 Choncho mfumu inalamula, ndipo anabwera naye Danieli ndi kukamuponya mʼdzenje la mikango. Mfumu inati kwa Danieli, “Mulungu wako amene umutumikira nthawi zonse, akupulumutse!”
Te dongah manghai kah a ti bangla Daniel te a khuen uh tih sathueng buep la a voeih uh. Te vaengah manghai loh avoek tih Daniel te, “Amah na bawk vanbangla na Pathen amah loh nang te dungyan duela n'loeih sak saeh,” a ti nah.
17 Anatenga mwala natseka pa khoma pa dzenje la mikango, ndipo mfumu inadindapo chizindikiro chake ndi cha nduna zake kuti wina asasinthepo kanthu pa za Danieli.
Te phoeiah lungto pakhat a khuen uh tih buep rhai te a tlaeng uh. Te phoeiah tah Daniel kah a hmuethma thovael pawt hamla manghai loh amah kah kutbuen nen khaw a boei rhoek kah kutbuen nen khaw a daeng thil.
18 Kenaka mfumu inabwerera ku nyumba yake ndipo inakhala usiku wonse osadya kanthu, osalola chosangalatsa chilichonse. Ndipo sinagone tulo.
Manghai te amah bawkim la mael dae buhmueh la hak tih a tumbael khaw a taengla khuen pawh. Te dongah a ih khaw anih lamloh a yong pah.
19 Mʼbandakucha, mfumu inanyamuka ndi kufulumira kupita ku dzenje la mikango lija.
Te dongah manghai te mincang khothaih vaengah ah thoo tih thintawn neh sathueng buep la cet.
20 Itayandikira pa dzenjelo, inayitana Danieli moonetsa nkhawa, “Danieli, mtumiki wa Mulungu wa moyo! Kodi Mulungu wako, amene umutumikira nthawi zonse, wakulanditsa ku mikango?”
A buep kah Daniel taengla a yoei vaengah tah lungnat ol neh rhap. Manghai loh Daniel te a voek tih, “Mulhing Pathen kah tueihyoeih Daniel, amah te na Pathen pai tih nang loh amah te dungyan la na bawk. Sathueng khui lamloh nang loeih sak ham a noeng a?” a ti nah.
21 Danieli anayankha kuti, “Inu mfumu mukhale ndi moyo wautali!
Te dongah Daniel loh manghai te, “Manghai tah kumhal la hing pai saeh.
22 Mulungu wanga anatumiza mngelo wake, ndipo anatseka pakamwa pa mikango. Iyo sinandivulaze chifukwa Mulungu anaona kuti ndine wosalakwa ndi kutinso sindinakulakwireni inu mfumu.”
Ka Pathen loh a puencawn han tueih tih sathueng ka te a buem dongah kai he m'phae moenih. He kong dongah kai he amah taengah ommongsitoe la n'tueng sak tih manghai namah taengah khaw tholh ka saii moenih?” a ti nah.
23 Mfumu inali ndi chimwemwe chopambana ndipo inalamulira kuti amutulutse Danieli mʼdzenjemo. Ndipo atamutulutsa Danieli mʼdzenjemo, sanapezeke ndi chilonda chilichonse pa thupi lake, chifukwa iye anadalira Mulungu wake.
Te daengah manghai te a taengah bahoeng a kohoe tih Daniel te buep lamloh doek hamla a thui pah. Daniel te a Pathen soah a uepom dongah a buep lamloh a doek vaengah khaw a pum dongah a hma pakhat khaw a hmuh moenih.
24 Mwa lamulo la mfumu, anthu onse amene ananeneza Danieli aja anagwidwa ndi kukaponyedwa mʼdzenje la mikango, pamodzi ndi akazi awo ndi ana awo. Ndipo asanafike pansi pa dzenjelo, mikango inawawakha ndi mphamvu ndi kuteketa mafupa awo onse.
Te phoeiah manghai kah a thui bangla Daniel tholh aka pael hlang rhoek te a khuen uh tih amih te a yuu a ca rhoek neh sathueng buep la a voeih uh. Tedae buep kah cirhong te a pha uh mueh la amih te sathueng loh a paco uh tih a songrhuh boeih a caep pauh.
25 Kenaka mfumu Dariyo inalembera anthu a mitundu yonse, ndi anthu a ziyankhulo zosiyanasiyana a mʼdziko lonse kuti, “Mtendere uchuluke pakati panu!
Te dongah Darius manghai loh namtu pilnam boeih neh olcom olcae taengah a daek pah. Diklai pum kah khosa, khosa te nangmih kah ngaimongnah pungtai saeh.
26 “Ndikukhazikitsa lamulo kuti paliponse mʼdziko langa anthu ayenera kuopa ndi kuchitira ulemu Mulungu wa Danieli.
Kai lamkah saithainah he ka ram kah khohung boeih ah ka paek coeng. Daniel kah a Pathen taengah a thuen, thuen doela om uh saeh lamtah birhih uh saeh. Amah tah mulhing Pathen la om tih kumhal duela cak. A ram khaw tim pawt tih a khohung loh khobawt duela a pha.
27 Iye amalanditsa ndipo amapulumutsa,
A loeih sak tih a huul. Vaan neh diklai ah miknoek neh khobae rhambae a tueng sak. Amah loh Daniel te sathueng kut lamloh a loeih sak.
28 Choncho Danieli anapeza ufulu pa nthawi ya ulamuliro wa Dariyo ndi ulamuliro wa Koresi wa ku Perisiya.
Te dongah Daniel he Darius kah ram neh Persian kah Persian Cyrus ram khuiah thaihtak.

< Danieli 6 >