23 “Inu mfumu munaona mthenga woyera, akuchokera kumwamba ndipo anati, ‘Gwetsani mtengo ndipo muwuwononge, koma musiye tsinde ndi mizu yake. Tsindelo mulimange ndi unyolo wa chitsulo ndi mkuwa ndipo mulisiye pakati pa udzu wa mʼmunda. Mulole kuti linyowe ndi mame akumwamba. Likhale ngati nyama zakuthengo, mpaka zaka zidutse zisanu ndi ziwiri.’
A o kau ike ana, e ke alii, i ka mea kiai, he mea hemolele e iho mai ana, mai ka lani mai, e olelo ana, E kua aku i ka laau, a e hoopau ia ia; aka, e waiho i ke kumu o kona aa ma ka lepo, me ke apo hao a me ke keleawe, mawaena o na mea uliuli o ke kula; a e hoopuluia i ka hau o ka lani, o kona kuleana aia no ia me na holoholona o ke kula, a hala aku na manawa ehiku maluna iho ona;