19 Pamenepo Danieli, amene amatchedwa Belitesezara, anavutika mu mtima kwambiri kwa kanthawi, ndipo anasautsidwa mʼmaganizo ake. Choncho mfumu inati, “Belitesezara usalole malotowa kapena tanthauzo lake likuopse.” Belitesezara anayankha kuti, “Mbuye wanga, ndikanakonda malotowa akanakhudza adani anu okha, ndi tanthauzo lake kwa iwo okusautsani!
Then Daniel, whose name was Belteshazzar, was appalled for a while, and his thoughts affrighted him. The king spoke and said: 'Belteshazzar, let not the dream, or the interpretation, affright thee.' Belteshazzar answered and said: 'My lord, the dream be to them that hate thee, and the interpretation thereof to thine adversaries.