< Danieli 1 >

1 Chaka chachitatu cha ufumu wa Yehoyakimu mfumu ya Yuda, Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni inabwera ndi kuzinga mzinda wa Yerusalemu ndi kuwuthira nkhondo.
Judah manghai Jehoiakim kah a ram, a kum thum vaengah Babylon manghai Nebukhanezar te cet tih Jerusalem te a taengah a dum.
2 Ndipo Ambuye anapereka Yehoyakimu mfumu ya ku Yuda mʼdzanja lake, pamodzi ndi zina mwa zida zotumikira mʼNyumba ya Mulungu. Iye anazitenga napita nazo ku nyumba ya mulungu wake ku Babuloni ndi kuziyika mʼnyumba yosungiramo chuma cha mulungu wake.
Te vaengah ka Boeipa loh Judah manghai Jehoiakim neh Pathen im kah hnopai ca te Nebukhanezar kut ah a paek. Te dongah te rhoek te Shinar khohmuen kah a pathen im la a khuen tih hnopai te a pathen kah thakvoh im ah a khueh.
3 Tsono mfumu inalamula Asipenazi, mkulu wa nduna zake kuti abwere nawo ena mwa Aisraeli ochokera mʼbanja laufumu ndi la olemekezeka,
Te phoeiah manghai loh amah kah imkhoem puei Ashpenaz te Israel ca lamkah neh mangpa tiingan lamkah khaw, angrhaeng rhoek lamkah khaw khuen hamla a thui pah.
4 achinyamata wopanda chilema, okongola, aluso mu nzeru zonse, okhala ndi chidziwitso, achangu pophunzira, odziwa kutumikira mʼnyumba ya mfumu. Ndipo anati awaphunzitsenso kuwerenga chiyankhulo cha Ababuloni.
Te vaengah a taengah a lolhmaih pakhat khaw aka om pawh camoe rhoek neh a mueimae aka then, cueihnah cungkuem neh aka cangbam, mingnah aka ming, cangnah aka yakming neh amih taengah thadueng aka om tah manghai bawkim ah om ham neh amih te Khalden ca neh ol tukkil hamla a khueh.
5 Ndipo mfumu imawapatsa tsiku ndi tsiku gawo la chakudya ndi vinyo wa ku nyumba yaufumu, ndi kuti awaphunzitse kwa zaka zitatu, ndipo kenaka adzayambe kutumikira mfumu.
Manghai loh amih ham tah a hnin hnin ah a hmuethma a khueh pah. Manghai buh neh a buhkoknah misurtui paek tih kum thum khuiah amih te pantai sak ham, a tloihsoi ah manghai mikhmuh ah pai sak ha a uen.
6 Pakati pa amenewa panali ena ochokera ku Yuda: Danieli, Hananiya, Misaeli ndi Azariya.
Amih lakli ah Judah koca lamkah Daniel, Hananiah, Mishael neh Azariah om.
7 Mkulu wa nduna za mfumu anawapatsa mayina atsopano: Danieli anamutcha Belitesezara; Hananiya anamutcha Sadirake; Misaeli anamutcha Mesaki; ndi Azariya anamutcha Abedenego.
Amih te imkhoem mangpa loh ming a paek tih Daniel te Belteshazzar la, Hananiah te Shadrakh la, Mishael te Meshakh la, Azariah te Abednego la a khueh pah.
8 Koma Danieli anatsimikiza mtima kuti asadzidetse ndi chakudya ndi vinyo wa mfumu, ndipo anapempha chilolezo kwa mkulu wa nduna za mfumu kuti asadzidetse mwa njira imeneyi.
Tedae Daniel long tah manghai buh neh, a buhkoknah misurtui neh a nok uh pawt ham a lungbuei ah a khueh. Te dongah a nok pawt ham imkhoem mangpa te a dawt.
9 Ndipo Mulungu anafewetsa mtima wa ndunayo kuti amukomere mtima ndi kumuchitira chifundo Danieli,
Pathen loh Daniel te imkhoem mangpa mikhmuh ah sitlohnah neh haidamnaha paek rhoe a paek.
10 koma ndunayo inamuwuza Danieli kuti, “Ine ndikuchita mantha ndi mbuye wanga mfumu, amene wapereka chakudya ndi chakumwa chanu. Kodi akuoneni inu owonda kuposa anzanu a misinkhu yanu pa chifukwa chanji? Mfumu ikhoza kundidula mutu chifukwa cha iwe.”
Tedae imkhoem mangpa loh Daniel te, “Kai khaw ka boei manghai te ka rhih ta. Anih long ni na caak na buhkoknah he hang khueh. Camoe kah na omngaihnah lakah balae tih na maelhmai te hmai aka tal la a hmuh eh? Ka lu he manghai taengah nan mop coeng,” a ti nah.
11 Ndipo Danieli anati kwa kapitawo amene anali mkulu wa nduna za mfumu amene anamuyika kuti ayangʼanire Danieli, Hananiya, Misaeli ndi Azariya,
Te vaengah Daniel loh buhtaem, Anih te Daniel, Hananiah, Mishael neh Azariah soah imkhoem mangpa la a khueh taengah,
12 “Chonde mutiyese ife akapolo anu pa masiku khumi: mutipatse masamba okha kuti tidye ndi madzi akumwa.
“Na sal rhoek he hnin rha khuiah n'noemcai mai lamtah ankak mah kaimih m'pae mai saeh. Ka caak uh khaw tui neh ka yun uh eh.
13 Ndipo mudzafananize maonekedwe athu ndi a anyamata amene akudya chakudya cha mfumu, ndi kuti mudzachite ndi anyamata anu monga momwe mudzawaonere.”
Te phoeiah kaimih kah mueimae neh manghai buh aka ca camoe rhoek kah mueimae te namah mikhmuh ah tueng saeh. Te vaengkah na hmuh bangla na sal rhoek taengah saii,” a ti nah.
14 Choncho anawavomera ndipo anawayesa pa masiku khumi.
Te dongah hekah ol bangla amih te a rhoi tih hnin rha khuiah amih te a noem.
15 Pakutha pa masiku khumi iwo anaoneka athanzi ndi odya bwino kuposa aliyense wa anyamata amene ankadya chakudya cha mfumu aja.
Hnin rha a thoknah dongah amih kah mueimae te a then la a sawt. Te vaengah manghai buh aka ca camoe boeih lakah a pumsa toitup.
16 Choncho kapitawo anawachotsera chakudya ndi vinyo za ku nyumba yaufumu zija nawapatsa ndiwo zamasamba basi.
Te dongah buhtaem loh amih kah buh neh a buhkoknah misur te a puen tih amih te ankak a paek.
17 Kwa anyamata anayiwa Mulungu anapereka chidziwitso ndi kuzindikira bwino mitundu yonse ya zolembedwa ndi za maphunziro. Ndipo Danieli ankatanthauzira masomphenya ndi maloto a mitundu yonse.
Tedae amih pali, camoe rhoek tah Pathen loh a taengah cangnah dongah cabu neh cueihnah boeih te cangbam hamla a paek. Te dongah Daniel loh mangthui neh mueimang te boeih a yakming.
18 Ndipo kumapeto kwa masiku amene mfumu inayika kuti adzaonetse anyamatawa ku nyumba yake, mkulu wa nduna za mfumu uja anawapereka iwo kwa Nebukadinezara.
Khohnin kuepnah a pha vaengah amih khuen hamla manghai loh a thui pah tih amih imkhoem mangpa loh Nebukhanezar mikhmuh ah a khuen.
19 Mfumu inayankhula nawo, ndipo panalibe wofanana ndi Danieli; Hananiya Misaeli ndi Azariya; Choncho analowa ndi kukhala otumikira mfumu.
Manghai te amih taengah a voek vaengah Daniel, Hananiah, Mishael neh Azariah bang he amih boeih khui lamloh hmu pawh. Te dongah amih tah manghai mikhmuh ah pai uh.
20 Nthawi zonse mfumu ikawafunsa zonse zofuna nzeru ndi chidziwitso, inkapeza kuti iwo anali oposa amatsenga ndi owombeza onse a mu ufumu wake wonse mopitirira muyeso.
Olka cungkuem dongah cueihnah neh yakmingnah amih lamkah te manghai loh a cae vaengah amih tah a ram pum kah khungvatuk neh hmayuep boeih lakah a kut parha la a hmuh.
21 Ndipo Danieli anali kumeneko mpaka chaka choyamba cha ufumu wa Koresi.
Daniel tah manghai Cyrus kah a kum khat nah hil om.

< Danieli 1 >