< Amosi 5 >

1 Israeli, imva mawu awa, nyimbo ya maliro imene ndikuyimba za iweyo:
Mwet Israel, porongo on in asor soko su nga onkakin keiwos:
2 “Namwali Israeli wagwa, moti sadzadzukanso, wasiyidwa mʼdziko lake lomwe, popanda woti ndi kumudzutsa.”
Israel el oana sie mutan fusr su anwuki oan infohk uh, Su ac fah tiana sifilpa tukakek! Sisilana el, oan fin fohk uh, Ac wangin mwet in sraklalak.
3 Ambuye Yehova akuti, “Mzinda umene udzapite ku nkhondo ndi anthu 1,000 amphamvu udzatsala ndi anthu 100 okha; mzinda umene udzapite ku nkhondo ndi anthu 100 amphamvu udzatsala ndi anthu khumi okha basi.”
LEUM GOD Fulat El fahk, “Sie siti in Israel supwala sie tausin mwet mweun, ac mwet siofok na painmoul foloko. Ac sie pac siti supwala mwet mweun siofok, ac mwet singoul na foloko.”
4 Zimene Yehova akunena kwa nyumba ya Israeli ndi izi: “Mundifunefune kuti mukhale ndi moyo;
LEUM GOD El fahk nu sin mwet Israel, “Fahsru nu yuruk, ac kowos fah moul.
5 musafunefune Beteli, musapite ku Giligala, musapite ku Beeriseba. Pakuti Giligala adzatengedwa ndithu kupita ku ukapolo, ndipo Beteli adzawonongekeratu.”
Nikmet som nu Beersheba in alu. Nimet srike in sukyu in acn Bethel — Bethel ac fah wanginla. Nikmet som nu Gilgal-mwet we uh ac fah som nu in sruoh.”
6 Funani Yehova kuti mukhale ndi moyo, mukapanda kutero Iye adzatentha nyumba ya Yosefe ngati moto; motowo udzawononga, ndipo sipadzakhala wina wozimitsa motowo ku Beteli.
Suk LEUM GOD, ac kowos fah moul. Kowos fin tia sokol, El fah putati oana sie e nu fin mwet Israel. E sac fah esukak mwet in Bethel, ac wangin sie fah ku in konela.
7 Inu amene mumasandutsa chiweruzo cholungama kukhala chowawa ndi kunyoza chilungamo.
We nu suwos su furokla ma pwaye, ac aklalfonye mwet in eisla ma lalos!
8 (Iye amene analenga nyenyezi za Nsangwe ndi Akamwiniatsatana, amene amasandutsa mdima kuti ukhale mmawa ndi kudetsa usana kuti ukhale usiku, amene amayitana madzi a mʼnyanja ndi kuwathira pa dziko lapansi, Yehova ndiye dzina lake.
LEUM GOD El orala itu uh, El orala Nasren ac oakiya acn sin itu saya. El ekulla lohsr lun fong nu ke kalem lun len, Ac ekulla len nu ke fong. El eis kof liki fin meoa uh Ac okoala nu fin faclu. Inel pa LEUM GOD.
9 Iyeyo amabweretsa chiwonongeko modzidzimutsa pa anthu amphamvu ndi kuwononga mizinda yotetezedwa),
El uniya mwet ku ac kunausla pot ku lalos.
10 inu mumadana ndi amene amadzudzula mʼbwalo la milandu ndi kunyoza amene amanena zoona.
Kowos srunga kutena mwet su lain orekma sesuwos ac kaskas pwaye ke pacl in nununku.
11 Mumapondereza munthu wosauka ndi kumukakamiza kuti akupatseni tirigu. Nʼchifukwa chake, ngakhale mwamanga nyumba zamiyala yosema, inuyo simudzakhalamo. Ngakhale mwalima minda yabwino ya mphesa, inu simudzamwa vinyo wake.
Kowos akkeokye mwet sukasrup ac pisrala mwe mongo nalos. Ke ma inge kowos ac fah tia muta in lohm wowo kowos musaela ke eot tufahl, ku nim wain liki ima in grape kato su kowos yukwiya.
12 Pakuti Ine ndikudziwa kuchuluka kwa zolakwa zanu ndi kukula kwa machimo anu. Inu mumapondereza anthu olungama ndi kulandira ziphuphu ndipo anthu osauka simuwaweruza mwachilungamo mʼmabwalo anu amilandu.
Nga etu upaiyen ma koluk lowos, ac pusiyen pacl kowos kunausla ma sap uh. Kowos akkeokye mwet wo, kowos eis molin eyeinse, ac ke pacl in nununku kowos ikol tuh suwohs lun mwet sukasrup in tia fwackyuk.
13 Nʼchifukwa chake pa nthawi yotere munthu wanzeru sayankhulapo kanthu, popeza ndi nthawi yoyipa.
Ke pacl koluk ouinge uh, el su oasr kalem yoro el ac mislana ac tia fahk ma el nunku.
14 Muyike mtima wanu pa zabwino osati pa zoyipa, kuti mukhale ndi moyo. Mukatero Yehova Mulungu Wamphamvuzonse adzakhala nanu, monga mmene mumanenera kuti ali nanu.
Suk in oru ma suwohs ac tia ma koluk, tuh kowos in ku in moul. Na LEUM GOD Kulana El fah wi kowos, oana ke kowos fahk.
15 Mudane ndi zoyipa, mukonde zabwino; mukhazikitse chiweruzo cholungama mʼmabwalo anu amilandu. Mwina mwake Yehova Mulungu Wamphamvuzonse adzachitira chifundo anthu otsala a mʼbanja la Yosefe.
Srunga ma koluk, ac lungse ma wo, ac akkeye tuh ma suwohs in sikyak ke pacl in nununku. Sahp LEUM GOD El ac fah pakoten nu sin mwet na pu su painmoulla in mutunfacl se inge.
16 Choncho izi ndi zimene Ambuye, Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, akunena: “Mʼmisewu monse mudzakhala kulira mofuwula, ndi kulira chifukwa cha kuwawa kwa masautso kudzakhala paliponse. Adzayitana alimi kuti adzalire, ndipo anthu odziwa maliridwe anthetemya adzalira mofuwula.
Ouinge LEUM GOD Fulat ac Kulana El fahk, “Ac fah oasr pusren tung mwemelil inkanek in siti uh. Ac fah solsolme mwet orekma in ima elos in wi mwet ma oasr moul nu se in tung, tuh elos kewa in tungi mas misa.
17 Mʼminda yonse ya mpesa mudzakhala kulira kokhakokha, pakuti Ine ndidzadutsa pakati panu,” akutero Yehova.
Ac fah oasr pac pusren tung ac mwemelil ke ima in grape nukewa. Ma inge nukewa ac fah sikyak mweyen nga ac tuku kalyei kowos.” LEUM GOD pa fahk ma inge.
18 Tsoka kwa inu amene mumalakalaka tsiku la Yehova! Chifukwa chiyani mumalakalaka tsiku la Yehova? Tsikulo kudzakhala mdima osati kuwala.
Ac mau fuka upaiya nu suwos su salka len lun LEUM GOD! Mea ac wo nu suwos ke len sac? Ac fah mau sie len na lohsr ac tia kalem.
19 Lidzakhala ngati tsiku limene munthu pothawa mkango amakumana ndi chimbalangondo, ngati pamene munthu walowa mʼnyumba, natsamira dzanja lake pa khoma ndipo njoka nʼkuluma.
Ac fah mau oana sie mwet su kaingkin soko lion twe sun bear soko! Ku oana sie mwet su utyak tari nu in lohm sel ac siungya pesinka uh, a wet pwasin soko ngalsilya!
20 Kodi tsiku la Yehova silidzakhala mdima osati kuwala, mdima wandiweyani, popanda powala pena paliponse?
Len lun LEUM GOD ac fah len na lohsr matoltol, ac wangin kutu srisrik kalem kac.
21 “Ndimadana nawo masiku anu achikondwerero ndipo ndimawanyoza; sindikondwera nayo misonkhano yanu.
LEUM GOD El fahk, “Nga srunga kufwa kowos oru ke pacl in alu lowos. Nga tia kuhnkuni!
22 Ngakhale mupereke nsembe zopsereza ndi nsembe zachakudya, Ine sindidzazilandira. Ngakhale mupereke nsembe zabwino zachiyanjano, Ine sindidzaziyangʼana nʼkomwe.
Kowos fin use mwe kisa firir ac mwe kisa wheat lowos nu sik, nga ac fah tia eis. Nga fah tia pac engan ke kosro fact ma kowos kisakin nu sik.
23 Musandisokose nazo nyimbo zanu! Sindidzamvetsera kulira kwa azeze anu.
Tulokinya on oraru lowos ingan. Nga tia lungse lohng pusren mwe on nutuwos an.
24 Koma chiweruzo cholungama chiyende ngati madzi, chilungamo ngati mtsinje wosaphwa!
A lela nununku suwohs in asrla oana sie unon in kof, ac ma suwoswos in soror oana soko infacl su tia ku in mihnla.
25 “Kodi pa zaka makumi anayi zimene munakhala mʼchipululu muja munkandibweretsera nsembe ndi zopereka, inu nyumba ya Israeli?
“Mwet Israel, ke nga tuh pwen kowos sasla yen mwesis ke lusen yac angngaul, kowos tuh tiana enenu in use mwe kisa ku mwe sang nu sik.
26 Inu mwanyamula kachisi wa mfumu yanu, ndi nyenyezi ija Kaiwani, mulungu wanu, mafano amene munadzipangira.
Tusruktu inge, ke sripen kowos alu nu ke ma sruloala pangpang Sakkuth ac Kaiwan, kowos fah enenu in us ma sruloala lowos ingan
27 Nʼchifukwa chake Ine ndidzakupititsani ku ukapolo, kutali kupitirira ku Damasiko,” akutero Yehova, amene dzina lake ndi Mulungu Wamphamvuzonse.
ke nga ac eiskowosyang nu in sruoh in sie facl alukela Damascus.” Pa inge kas lun LEUM GOD, su pangpang God Kulana.

< Amosi 5 >