< Amosi 5 >
1 Israeli, imva mawu awa, nyimbo ya maliro imene ndikuyimba za iweyo:
Denggenyo daytoy a sao nga idungdung-awko kadakayo, balay ti Israel.
2 “Namwali Israeli wagwa, moti sadzadzukanso, wasiyidwa mʼdziko lake lomwe, popanda woti ndi kumudzutsa.”
Natuangen ti birhen nga Israel; saanto isuna a bumangonen; nabaybay-an isuna iti mismo a dagana; awan iti mangbangon kenkuana.
3 Ambuye Yehova akuti, “Mzinda umene udzapite ku nkhondo ndi anthu 1,000 amphamvu udzatsala ndi anthu 100 okha; mzinda umene udzapite ku nkhondo ndi anthu 100 amphamvu udzatsala ndi anthu khumi okha basi.”
Ta kastoy ti kuna ni Yahweh nga Apo: “Ti siudad a rimmuar nga addaan iti sangaribo ket sangagasutto laeng ti mabati ken ti rimmuar nga addaan iti sangagasut ket sangapulonto laeng ti mabati iti balay ti Israel.”
4 Zimene Yehova akunena kwa nyumba ya Israeli ndi izi: “Mundifunefune kuti mukhale ndi moyo;
Gapu ta kastoy ti kuna ni Yahweh iti balay ti Israel: “Sapulendak ket agbiagkayo!
5 musafunefune Beteli, musapite ku Giligala, musapite ku Beeriseba. Pakuti Giligala adzatengedwa ndithu kupita ku ukapolo, ndipo Beteli adzawonongekeratu.”
Saanyo a sapulen ti Betel; wenno sumrek iti Gilgal; saankayo a mapan iti Beerseba. Gapu ta awan duadua a maitalawto a kas balud ti Gilgal, ket agladingitto ti Betel.
6 Funani Yehova kuti mukhale ndi moyo, mukapanda kutero Iye adzatentha nyumba ya Yosefe ngati moto; motowo udzawononga, ndipo sipadzakhala wina wozimitsa motowo ku Beteli.
Sapulenyo ni Yahweh ket agbiagkayo, Amangan no sumgiab isuna a kas apuy iti balay ni Jose. Mangibusto daytoy, ket awanto iti mangiddep iti daytoy iti Betel.
7 Inu amene mumasandutsa chiweruzo cholungama kukhala chowawa ndi kunyoza chilungamo.
Pagbalbalinen dagidiay a tattao a nasaem a banag ti hustisia ket ibelbellengda iti daga ti kinalinteg!”
8 (Iye amene analenga nyenyezi za Nsangwe ndi Akamwiniatsatana, amene amasandutsa mdima kuti ukhale mmawa ndi kudetsa usana kuti ukhale usiku, amene amayitana madzi a mʼnyanja ndi kuwathira pa dziko lapansi, Yehova ndiye dzina lake.
Inaramid ti Dios ti Pleyades ken Orion; pagbalbalinenna nga agsapa ti sipnget; pagbalbalinenna a rabii ti aldaw ken ay-ayabanna ti danum iti baybay ket ibuybuyatna iti rabaw ti daga. Yahweh ti naganna!
9 Iyeyo amabweretsa chiwonongeko modzidzimutsa pa anthu amphamvu ndi kuwononga mizinda yotetezedwa),
Iiyegna ti apagdarikmat a pannakadadael kadagiti nabileg tapno dumteng ti pannakadadael kadagiti sarikedked.
10 inu mumadana ndi amene amadzudzula mʼbwalo la milandu ndi kunyoza amene amanena zoona.
Kabusbusorda ti siasinoman a mangilinlinteg kadakuada sadiay ruangan ti siudad, ken gurguraenda ti siasinoman nga agibagbaga iti pudno.
11 Mumapondereza munthu wosauka ndi kumukakamiza kuti akupatseni tirigu. Nʼchifukwa chake, ngakhale mwamanga nyumba zamiyala yosema, inuyo simudzakhalamo. Ngakhale mwalima minda yabwino ya mphesa, inu simudzamwa vinyo wake.
Gapu ta ibaddebaddekyo dagiti marigrigat ken al-alaenyo dagiti trigoda, uray man no nagpatakderkayo kadagiti balay a naaramid iti bato, saankayonto nga agnaed sadiay. Nagpipintas ti kaubasanyo ngem saanyonto a mainum ti arak a naggapu kadagitoy.
12 Pakuti Ine ndikudziwa kuchuluka kwa zolakwa zanu ndi kukula kwa machimo anu. Inu mumapondereza anthu olungama ndi kulandira ziphuphu ndipo anthu osauka simuwaweruza mwachilungamo mʼmabwalo anu amilandu.
Gapu ta ammok ti kaadu dagiti panagsalungasingyo ken ti kadakkel dagiti basbasolyo— dakayo a mangparparigat ti nalinteg, umaw-awat iti pasuksok ken mangiwalwalin kadagiti agkasapulan sadiay ruangan ti siudad.
13 Nʼchifukwa chake pa nthawi yotere munthu wanzeru sayankhulapo kanthu, popeza ndi nthawi yoyipa.
Isu nga agulimek ti siasinoman a nanakman iti kasta a tiempo, ta dayta ket tiempo ti kinadakes.
14 Muyike mtima wanu pa zabwino osati pa zoyipa, kuti mukhale ndi moyo. Mukatero Yehova Mulungu Wamphamvuzonse adzakhala nanu, monga mmene mumanenera kuti ali nanu.
Sapulenyo ti naimbag, saan a ti dakes tapno agbiagkayo. Ket ni Yahweh, ti Dios a mannakabalin amin ket addanto kadakayo a kas kunkunayo.
15 Mudane ndi zoyipa, mukonde zabwino; mukhazikitse chiweruzo cholungama mʼmabwalo anu amilandu. Mwina mwake Yehova Mulungu Wamphamvuzonse adzachitira chifundo anthu otsala a mʼbanja la Yosefe.
Guraenyo ti dakes, ayatenyo ti naimbag, ipasdekyo ti hustisia idiay ruangan iti siudad. Nalabit a maasianto ni Yahweh, ti Dios a mannakabalin amin, kadagiti nabati a kaputotan ni Jose.
16 Choncho izi ndi zimene Ambuye, Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, akunena: “Mʼmisewu monse mudzakhala kulira mofuwula, ndi kulira chifukwa cha kuwawa kwa masautso kudzakhala paliponse. Adzayitana alimi kuti adzalire, ndipo anthu odziwa maliridwe anthetemya adzalira mofuwula.
Ngarud, kastoy ti kuna ni Yahweh nga Apo, ti Dios a mannakabalin amin: “Addanto panagdung-aw iti amin a plasa, ket ibagadanto iti amin a kalsada, 'Asi pay! Asi pay! Ayabandanto dagiti mannalon nga agdung-aw ken dagiti dumudung-aw tapno agdung-aw.
17 Mʼminda yonse ya mpesa mudzakhala kulira kokhakokha, pakuti Ine ndidzadutsa pakati panu,” akutero Yehova.
Addanto iti panagdung-aw iti amin a kaubasan ta lumabasakto iti tengngayo,” kuna ni Yahweh.
18 Tsoka kwa inu amene mumalakalaka tsiku la Yehova! Chifukwa chiyani mumalakalaka tsiku la Yehova? Tsikulo kudzakhala mdima osati kuwala.
Kakaasikayo a mangtartarigagay ti aldaw ni Yahweh! Apay a tartarigagayanyo ti aldaw ni Yahweh? Sipngetto dayta nga aldaw, saan a lawag.
19 Lidzakhala ngati tsiku limene munthu pothawa mkango amakumana ndi chimbalangondo, ngati pamene munthu walowa mʼnyumba, natsamira dzanja lake pa khoma ndipo njoka nʼkuluma.
Kas iti tao nga itartarayana ti leon ket adda ti oso a masabatna, wenno simrek iti balay, insadagna ti imana iti diding ket kinagat isuna iti uleg.
20 Kodi tsiku la Yehova silidzakhala mdima osati kuwala, mdima wandiweyani, popanda powala pena paliponse?
Saankadi a sipngetto ti aldaw ni Yahweh, saan a lawag? Nalidem ken nasipnget?
21 “Ndimadana nawo masiku anu achikondwerero ndipo ndimawanyoza; sindikondwera nayo misonkhano yanu.
“Kagurgurak ken karurodko dagiti piestayo, saanak a maragragsakan kadagiti napasnek a panaguummongyo.
22 Ngakhale mupereke nsembe zopsereza ndi nsembe zachakudya, Ine sindidzazilandira. Ngakhale mupereke nsembe zabwino zachiyanjano, Ine sindidzaziyangʼana nʼkomwe.
Uray man no idatonyo kaniak dagiti daton a maipuor ken dagiti sagut a bukbukkel, saankonto nga awaten dagitoy, wenno taliawen dagiti pinalukmegyo nga ayup nga idatagyo kas daton a pannakilangen.
23 Musandisokose nazo nyimbo zanu! Sindidzamvetsera kulira kwa azeze anu.
Isardengyo ti ariwawa dagiti kantayo; saanko a denggen ti uni dagiti arpayo.
24 Koma chiweruzo cholungama chiyende ngati madzi, chilungamo ngati mtsinje wosaphwa!
Palubosanyo ketdi nga agayus ti hustisia a kas iti danum, ken ti kinalinteg a kas iti kankanayon nga agay-ayus a karayan.
25 “Kodi pa zaka makumi anayi zimene munakhala mʼchipululu muja munkandibweretsera nsembe ndi zopereka, inu nyumba ya Israeli?
Inyegandak kadi kadagiti sakripisio ken daton iti let-ang bayat iti uppat a pulo a tawen, balay ti Israel?
26 Inu mwanyamula kachisi wa mfumu yanu, ndi nyenyezi ija Kaiwani, mulungu wanu, mafano amene munadzipangira.
Itag-ayonto ni Sakkut a kas ariyo ken ni Kaiwan a bituen a diosyo—dagiti didiosen nga inaramidyo para kadagiti bagbagiyo.
27 Nʼchifukwa chake Ine ndidzakupititsani ku ukapolo, kutali kupitirira ku Damasiko,” akutero Yehova, amene dzina lake ndi Mulungu Wamphamvuzonse.
Ngarud, italawkayonto a kas balud iti labes ti Damasco,” kuna ni Yahweh, Dios a mannakabalin amin ti naganna.