< Machitidwe a Atumwi 8 >
1 Ndipo Saulo anavomerezana nawo pa imfa ya Stefano. Tsiku lomwelo, mpingo wa mu Yerusalemu unayamba kuzunzidwa, ndipo onse, kupatulapo atumwi, anabalalikira ku madera onse a Yudeya ndi Samariya.
Sawoluwe Ist'ifanosi úd'ewor bontoen ik wotatni b́ teshi, Ist'ifanos b́ k'irts aawots Iyerusalemn fa'a Ik' k'oni moowu ats gisheyewo tuu b́wutsi, woshetswotsiyere okoon amants jamwots Yhudnat Semariy awurajo maantsan bad' bowutsi.
2 Anthu okonda Mulungu anayika maliro a Stefano ndipo anamulira kwambiri.
Ik ik shayirets ashuwots Ist'fanosi boduki, káári eenono kuhat bísh bo eepi.
3 Koma Saulo anayamba kuwononga mpingo. Amapita nyumba ndi nyumba, ndipo amagwira amuna ndi amayi ndi kukawatsekera ku ndende.
Sawolmó Ik'i moo t'afiyosh kaarefetstni b́teshi, mootsere moots kindt nungushuwotsnat mááts amantsuwotsn geetsdek' waat tipi moots b́ kindishiri.
4 Okhulupirira amene anabalalika amalalikira konse kumene amapita.
Bad'wutsts amantsuwotsuwere bo amts jamoke Ik'i aap'o bodanifo.
5 Filipo anapita ku mzinda wa ku Samariya ndipo analalikira za Khristu kumeneko.
Filp'osuwere Semariy kito maantsan amt ashuwotssh Mesihiyo jango b́ dani.
6 Gulu la anthu litamva Filipo akulalikira komanso kuona zizindikiro zozizwitsa zimene ankazichita, onse anamvetsetsa zimene iye amanena.
Ashuwotswere Filip'os keewuts keewo bo shishor b́ finiru adits keewuwotsi bo bek'tsok'on ik nibon t'iwintsdek'tni bo k'ebiri.
7 Mizimu yoyipa inatuluka mwa anthu ambiri ikufuwula kwambiri ndipo ambiri amene anali akufa ziwalo ndi olumala anachiritsidwa.
Kim Shayirotsuwere k'áári eenon kuhat ay ashuwotsitse bo keshfo, durwotsnat shoklirwotsn kasha bo kashefo.
8 Kotero munali chimwemwe chachikulu mu mzindawo.
Mansh kit manitse een gene'o b́ woti.
9 Koma mu mzindawo munali munthu dzina lake Simoni, amene amachita za matsenga ndi kudabwitsa anthu a mu Samariya. Iye amadzitamandira kuti ndi wopambana,
Kit manitse Sm'oni eteets ash iko fa'e b́ teshi, ashman kitotse b́ danon finat Semari ashuwotsi aditniye b́ teshi, «Taa een ash taane!» ettni b́ keewfo.
10 ndipo anthu onse, aakulu ndi aangʼono anamumvera ndi kunena kuti, “Munthu uyu ndi mphamvu ya Mulungu yotchedwa Mphamvu yayikulu.”
Ash jamo múk'onu eenonu «Ashaan ashi eene ett b́ s'egeyir Ik'i angone!» ett t'iwintsdk't bo k'ebfoni.
11 Anthu amamutsata chifukwa kwa nthawi yayitali amawadabwitsa ndi matsenga akewo.
T'iwintsdek't bo k'ebiruwere ay aawosh danon ashuwotsi adit b́ teshtsotsne.
12 Koma atakhulupirira Filipo akulalikira Uthenga Wabwino wa ufumu wa Mulungu ndiponso dzina la Yesu Khristu, anthuwo anabatizidwa amuna ndi amayi.
Ernmó Flip'os Ik'i mengisti jagonat Iyesus Krstos shútson b́ keewuts doo shishi keewo bo shishor nungushwotswere máátsuwotsuwere amanat bo gupeyi.
13 Nayenso Simoni anakhulupirira ndipo anabatizidwa, natsatira Filipo kulikonse, ndipo anadabwa kwambiri pamene anaona zizindikiro zazikulu ndi zozizwitsa.
Smonuworu b́ oreraniyere amanat b́ gupere Filp'osntonu ik wotb́wtsi, b́ finiru adits keewwotsnat milikituwotsn bek't bíadfera b́ teshi.
14 Atumwi a ku Yerusalemu atamva kuti anthu a ku Samariya analandira Mawu a Mulungu, anatumiza Petro ndi Yohane.
Iyerusalemitse fa'a wosheetsots Semari ashuwots Ik'i aap'o bodek'tsok'o boshishtsok'on P'et'rosnat Yohanisn Semari datso maantsan bo woshi.
15 Atafika anawapempherera kuti alandire Mzimu Woyera,
Semari ashuwots S'ayin shayiro bo daatsituwok'o P'et'rosnat Yohanisn amt boosh Ik'o bok'oni.
16 chifukwa Mzimu Woyera anali asanafike pa wina aliyense wa iwo; anali atangobatizidwa mʼdzina la Ambuye Yesu.
Semari ashuwots Doonzo Iyesus shútson bo gupeyi bako S'ayin shayiro konatsoru od'atse b́ teshi.
17 Ndipo Petro ndi Yohane anasanjika manja awo pa iwo, ndipo analandira Mzimu Woyera.
Mansh P'et'rosnat Yohansn bo kisho boats bo gedor ashuwots S'ayin shayiro bo dek'i.
18 Simoni ataona kuti Mzimu anaperekedwa kwa iwo atumwi atawasanjika manja, iye anafuna kuwapatsa ndalama ndipo anati,
Wosheetswotsu boats kisho bogedor S'ayin shayiro ashuwotssh b́ imestsok'o Simon b́ bek'tsok'on gizo dek'wat,
19 “Inenso ndipatseni mphamvu imeneyi kuti aliyense amene ndimusanjika manja anga azilandira Mzimu Woyera.”
«Taa t kisho boats tgere ashuwots S'ayin shayiro bodek'etuwok'o alan taash imere» bí eti.
20 Petro anayankha kuti, “Ndalama zako utayike nazo pamodzi, chifukwa unaganiza kuti ungathe kugula mphatso ya Mulungu ndi ndalama!
P'et'rosmó hank'o bíeti, «Ik'i imo gizon daatsosh n gawutsotse n gizo neenton t'afuwe!
21 Ulibe gawo kapena mbali pa utumikiwu, chifukwa mtima wako suli wolungama pamaso pa Mulungu.
N nibo Ik'i shinatse kááwu woto b́ k'aztsotse nee keewanitse kayo wee bano deshatsne.
22 Lapa zoyipa zakozi ndipo upemphere kwa Ambuye. Mwina adzakukhululukira maganizo a mu mtima mwako.
Eshe n gond finansh shiyanar naandre eree, daneraka n nibitsi gond finan orowa eteetwe wotiyal aab Ik'o k'onuwe.
23 Pakuti ine ndikuona kuti ndiwe wowawidwa mtima ndiponso kapolo wa tchimo.”
Neehe s'aam okooron ns'eentsok'onat morron tipek n wotok'o taa bek'iruwe.»
24 Ndipo Simoni anayankha, “Mundipempherere kwa Ambuye kuti zisandigwere izi mwanenazi.”
Sm'onuwere «It keewutsanitsere ik jago ti ats b́ borawok'o it it tookon taash Ik'o k'onuwere» bí eti.
25 Atatha kuchitira umboni ndi kulalikira mawu a Ambuye, Petro ndi Yohane anabwerera ku Yerusalemu, atalalikira Uthenga Wabwino mʼmidzi yambiri ya Asamariya.
P'et'rosnat Yohanisn bo gawiyakonat Doonzo aap'onwere bo keewiyakon Semari gal aywotsitse doo shishiyo nabfere Iyerusalem maantsan bo'ani.
26 Mngelo wa Ambuye anati kwa Filipo, “Nyamuka pita chakummwera, ku msewu wa ku chipululu wopita ku Gaza kuchokera ku Yerusalemu.”
Doonzo melakiyo Filip'ossh, «Tuur Iyerusalemiyere Gááz maants damiru weeron Muur maantsan amee» bí eti, weer manuwere woruwi weere b́ teshi.
27 Ndipo ananyamuka napita, ndipo akuyenda anakumana ndi munthu wa ku Etiopia wa udindo waukulu woyangʼanira chuma cha Kandake, mfumu yayikazi ya ku Etiopia. Munthu ameneyu anapita ku Yerusalemu kukapembedza Mulungu,
Bíwere tuut bíami, manno, Itiyop'iyi dats naash iko Ik'o k'onosh Iyerusalem maants amt b́ tesh, ashaan Hndeki eteets Itiyop'iyi Nugúsúsh b dets jamatse bish fintsonat b gizatse altsoniye b́teshi,
28 ndipo akubwerera kwawo atakwera pa galeta lake amawerenga buku la mneneri Yesaya.
Bí b́ datsomants bíaanefere seregelats bedek't nebiyiyo Isayas mas'afoni b́ nababefe b́tesh.
29 Mzimu anamuwuza Filipo kuti, “Pita pa galeta ilo ndipo ukakhale pafupi nalo.”
Manóóri sa'aton S'ayin shayiro Filip'osi «Seregel manok t'iinr bínton gonkeewe» bíet.
30 Pamenepo Filipo anathamangira ku galeta ndipo anamva munthuyo akuwerenga buku la mneneri Yesaya. Filipo anamufunsa kuti, “Kodi mukumvetsa zimene mukuwerengazi?”
Mansh Filip'os bíyok wos'fere amt Itop'iyi dats ashman nebiyiyo Isayas mas'fo b́ nababefere shisht «N nababiruwo b́ biitso neesh galiruwa?» bí et.
31 Iye anayankha kuti, “Ndingamvetse bwanji popanda wina wondimasulira?” Ndipo iye anayitana Filipo kuti abwere ndikukhala naye mʼgaleta.
Itiyop'iyi dats ashonwere «Taash biishde'er keewituwo aalo taash aawuk'oneya gaalo b́ faliti?» bíet.
32 Mawu amene ndunayo imawerenga anali awa: “Monga mwana wankhosa wopita naye kokamupha amachitira, kapena monga nkhosa imakhalira duu poyimeta, momwemonso iye sanatsekule pakamwa pake.
Bí b́ nababiru mas'aafi beyokonuwere hani b́ tesh, «Bí shukosh jokeyiru mererok'oyiye b́ teshi, Mererna'o b́s'iro k'ut'ewor s'ik bí etfok'o, Bíwere keewosh b́nono aawu'atse.
33 Iye ananyozedwa ndipo panalibe chilungamo pa mlandu wake. Ndipo ndani amene analabadirako za zidzukulu zake poona kuti iye anachotsedwa mʼdziko la anthu amoyo?”
Bíhe keteree, kááwu angshonowere bísh imeratse, B́ kashu datsatse k'aaúbazetsotse B́ s'ooti jango kone fal keewiti?»
34 Ndunayo inamufunsa Filipo kuti, “Chonde, uzeni, kodi mneneri akuyankhula za ndani, za iye mwini kapena za munthu wina?”
Naashmanuwere Filip'ossh, «Nebiyiyo han b́keewu kon jangoshe? B́ took jangoshemo wee k'oshi jange? Oona neesha aab taash keewwe» bí eti.
35 Pamenepo Filipo anayambira pa malemba omwewo kumuwuza za Uthenga Wabwino wa Yesu.
Filip'oswere S'ayin mas'afanatse tuut Iyesus jangosh dooshishiyo b́ nabi.
36 Akuyenda mu msewu anafika pamalo pamene panali madzi ndipo ndunayo inati, “Taonani madzi awa. Kodi pali chondiletsa kuti ndibatizidwe?”
Boamferowere aats beyok bobodi, naashmanuwere «Hamb, hanoke aatso fa'ee, tguperawok'o taan bazitu keewo eebi?» bí eti.
37 Filipo anati, “Ngati mukhulupirira ndi mtima wanu wonse mukhoza kubatizidwa.” Ndunayo inayankha kuti, “Ine ndikukhulupirira kuti Yesu Khristu ndi Mwana wa Mulungu.”
Filip'oswere «N nibi s'eenon ni'amaniyal gupewo falfne» bí eti. Naashmanwere «Iyesus Krstos Ik'o naayi b́ wottsok'o amaniruwe» b́ eti.
38 Ndipo analamulira galeta kuti liyime. Onse awiriwo, Filipo ndi Ndunayo anatsika ndi kulowa mʼmadzi ndipo Filipo anamubatiza.
Naashmanuwere seregelo b́ ned'iyetuwok'o bíazazi, Bogitetswere aatso maantsan oot't amt bo eree Filip'os Naasho b́ gupi.
39 Pamene iwo anatuluka mʼmadzimo, Mzimu wa Ambuye anamukwatula Filipo, ndipo Ndunayo sinamuonenso, koma inapitiriza ulendo wake ikusangalala.
Aatsotse bokeshiyakon Doonzoko S'ayin shayiro Filip'osi k'aaúbdek'i, janderbonuwere aani gitlo be'atse, b́woteferor geneúwefets b́weero sha'o dek't b́tuwi.
40 Koma Filipo anapezeka kuti ali ku Azoto ndipo anazungulira konse, kulalikira Uthenga Wabwino mʼmizinda yonse mpaka anakafika ku Kaisareya.
Filip'osmó Azat'ositsne b́ daatseyi, K'isariyi maantsowere b́ wafetsosh kit kitotse sha'at dooshishiyo b́ nabfoni b́teshi.