< Machitidwe a Atumwi 4 >

1 Pamene Petro ndi Yohane amayankhula ndi anthu, kunabwera ansembe, mkulu woyangʼanira Nyumba ya Mulungu ndiponso Asaduki.
Piter hoi Jawhan tinaw ni tami moikapap koe lawk a dei awh navah, vaihmanaw, bawkim kaukkung hoi sadusinaw teh ahnimouh koe a tho awh.
2 Iwo anakhumudwa kwambiri chifukwa atumwiwo amaphunzitsa anthu ndi kumalalikira za kuuka kwa akufa mwa Yesu.
gunceinaw ni duenae koehoi Jisuh boutthawnae kong hah tami pueng koe a dei awh dawkvah, ahnimouh teh a lungphuen awh.
3 Iwo anagwira Petro ndi Yohane, popeza kunali kutada, anawayika mʼndende mpaka mmawa mwake.
Hatdawkvah, Piter hoi Jawhan a man awh teh, khohmo toung dawkvah, thongim thung rum touh a paung awh.
4 Koma anthu ambiri amene anamva uthenga anakhulupirira, ndipo chiwerengero cha anthu chinakwana 5,000.
Hateiteh, Cathut lawkkatang ka thai ni teh ka yuem e tami tongpa dueng 5,000 touh a pha awh.
5 Mmawa mwake olamulira, akulu ndi aphunzitsi a malamulo anasonkhana mu Yerusalemu.
Atangtho vah khobawinaw, kacuenaw, cakathutkungnaw teh Jerusalem vah a kamkhueng awh.
6 Panali Anasi, Mkulu wa ansembe, Kayafa, Yohane ndi Alekisandro ndi ana a banja la mkulu wa ansembe.
Vaihma kacue Annas, Kaiaphas, Jawhan, Alexander hoi vaihma kacuenaw pueng hai a kamkhueng awh.
7 Iwo anayimiritsa Petro ndi Yohane patsogolo pawo nayamba kuwafunsa kuti, “Kodi munachita zimenezi ndi mphamvu yanji kapena mʼdzina la yani?”
Ahnimouh ni Piter hoi Jawhan teh tamimaya hmalah a kangdue sak awh teh api kâ lahoi maw, api min lahoi maw hete hno heh na sak awh vaw telah a pacei awh.
8 Petro wodzazidwa ndi Mzimu Woyera, anawawuza kuti, “Inu olamulira ndi akulu!
Hatnavah Piter teh Kathoung Muitha hoi akawi teh khobawinaw hoi kacuenaw,
9 Ngati ife tikufunsidwa lero chifukwa cha ntchito yabwino imene yachitika pa munthu wolumala miyendo ndi mmene iye anachiritsidwira,
sahnin vah kaimouh ni a tha kayoun e tami buet touh kabawp awh e hah lawk na ceng awh dawkvah,
10 tsono dziwani izi inu ndi aliyense mu Israeli: munthuyu akuyima pamaso panu, wochiritsidwa kwathunthu, ndi chifukwa cha dzina la Yesu Khristu wa ku Nazareti amene munamupachika koma Mulungu anamuukitsa kwa akufa.
nangmouh abuemlahoi Isarelnaw abuemlah panue sak hanlah ka ngai e teh, thingpalam dawk na pathout awh ei, duenae koehoi Cathut ni a thaw sak e Nazareth tami Jisuh Khrih min lahoi hete tami ni a dam teh nangmae hmalah a kangdue e doeh.
11 Iye ndi “‘Mwala umene amisiri omanga nyumba anawukana, umenewo wasanduka mwala wa pa ngodya!’
Hote Bawipa teh im kasakkungnaw ni na pahnawt awh e talung, patopatang poung e takinlung lah ao.
12 Chipulumutso sichipezeka mwa wina aliyense; pakuti palibe dzina lina pansi pa thambo limene lapatsidwa kwa anthu limene tiyenera kupulumutsidwa nalo.”
Hote Bawipa min hloilah kalvan rahim taminaw koevah ka rungngang thai e rungngangnae min alouke awmhoeh telah Piter ni a pâpho.
13 Ataona kulimba mtima kwa Petro ndi Yohane ndi kuzindikira kuti anali osaphunzira, anthu wamba, anadabwa kwambiri ndipo anazindikira kuti anthuwa anakhala pamodzi ndi Yesu.
Lawkcengkungnaw ni Piter hoi Jawhan e taran ahawi roinae hah a hmu awh navah, a kângairu awh. Hatnavah, ahnimouh roi teh Jisuh hoi reirei kaawm e tie hah a panue awh.
14 Koma popeza iwo amamuona munthu amene anachiritsidwa atayima pamodzi ndi iwo, palibe chimene akananena.
Hahoi, ahnimouh koe damnae kahmawt e tami hai ahnimouh koe a kangdue e a hmu awh navah banghai oun hane tawn hoeh.
15 Chifukwa chake anawalamula kuti atuluke mʼbwalo la milandu ndipo akulu abwalowo anayamba kukambirana.
Hatnavah, ahnimouh ni gunceinaw sanhedrin lawkcengnae imthung hoi a tâco hanelah kâ a poe awh teh bangtelamaw ti awh han telah amamouh dueng a kâpan awh.
16 Iwo anafunsana kuti, “Kodi anthuwa tichite nawo chiyani? Pakuti aliyense okhala mu Yerusalemu akudziwa kuti achita chodabwitsachi, ndipo ife sitingathe kukana.
Ahnimanaw heh bangtelamaw ti awh han. Bangkongtetpawiteh ahnimouh koehoi kângairuhno kamnuek e teh Jerusalem kho kaawm e tami pueng ni a panue awh toung dawkvah maimouh ni oun thai awh hoeh toe.
17 Koma kuti mbiriyi isapitirire kuwanda pakati pa anthu, ife tiwachenjeze anthu amenewa kuti asayankhulenso kwa wina aliyense mʼdzina la Yesu.”
Hete kamthang teh tami pueng koe a kampai hoeh nahanlah Jisuh e min kâuep laihoi hmalah apipatet koehai bout a dei hoeh nahanlah pakhi awh sei ati awh.
18 Pamenepo anawayitananso ndipo anawalamula kuti asayankhule kapena kuphunzitsa konse mʼdzina la Yesu.
Hathnukkhu gunceinaw hah a kaw awh teh, Jisuh min lahoi khoeroe pâpho awh hanh, cangkhai awh hanh telah a cakâ awh.
19 Koma Petro ndi Yohane anayankha kuti, “Weruzani nokha ngati nʼkwabwino pamaso pa Mulungu kumvera inu koposa Mulungu.
Piter hoi Jawhan ni, Cathut e lawk hlak nangmae lawk ka tarawi awh pawiteh, Cathut hmalah a kamcu hoi a kamcu hoeh e hah pouk awh haw.
20 Ife sitingaleke kuyankhula za zimene tinaziona ndi kuzimva.”
Kaimouh teh ka thai awh, ka hmu awh e hah pâpho laipalah kaawm thai awh hoeh ‘atipouh awh.
21 Atawonjeza kuwaopseza anawamasula. Sanathe kugwirizana njira yowalangira, chifukwa anthu onse amayamika Mulungu chifukwa cha zimene zinachitika.
Hote kamthang dawkvah tami pueng ni Cathut a pholen awh teh, gunceinaw hah bangtelah hoi ne runae poe han tie a lamthung a hmu awh hoeh dawkvah, ahnimouh ni gunceinaw hah bout a pakhi awh teh bout a tha awh.
22 Ndipo munthu amene anachiritsidwayo anali ndi zaka makumi anayi.
Hete kângairuhno lahoi ahmaloe e patetlah ka dam e tami teh a kum 40 hlai a pha toe.
23 Atamasulidwa Petro ndi Yohane anapita kwa anzawo ndipo anawafotokozera zonse zimene akulu a ansembe ndi akulu anawawuza.
Gunceinaw teh bout a tha awh navah amamae a huinaw koe bout a ban awh navah vaihma bawinaw hoi kacuenaw ni a dei pouh e hah a dei awh.
24 Anthu atamva zimenezi anafuwula ndi mtima umodzi napemphera kwa Mulungu. Iwo anati, “Ambuye wolamulira zonse, Inu munalenga kumwamba ndi dziko lapansi ndi nyanja ndiponso zonse zili mʼmenemo.
Ahnimouh ni be a thai awh hnukkhu, Cathut koe lungkânging lahoi a ratoum awh e teh, Bawipa nang teh kalvan hoi talai rahak e hnopueng hoi tuipui thung e hnopueng hai na sak, telah ati awh.
25 Inu munayankhula mwa Mzimu Woyera kudzera pakamwa pa Davide kholo lathu, mtumiki wanu kuti, “‘Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu, ndipo akonzekera kuchita zopandapake?
Bawipa ni Kathoung Muitha lahoi kaimae mintoe lah kaawm ni teh na patoun e Devit koehoi bangkongmaw khoramnaw kâpo awh hoeh, taminaw hai bangkongmaw ayawmyin lae hnonaw sak hanelah a kâcai awh.
26 Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo; ndipo olamulira asonkhana pamodzi kulimbana ndi Ambuye ndi wodzozedwa wakeyo.’
Talai e siangpahrangnaw pueng a kamkhueng awh teh, BAWIPA hoi Bawipa Jisuh hah tuk han telah ati awh.
27 Zoonadi, Herode ndi Pontiyo Pilato anasonkhana pamodzi ndi amitundu ndiponso Aisraeli, mu mzinda muno, kupanga zolimbana ndi mtumiki wanu woyera Yesu, amene Inu munamudzoza.
Herod hoi Pontius Pailat bawi teh Isarelnaw hoi Jentelnaw a hroecoe teh, Bawipa nang ni satui na awi tangcoung e, Capa Jisuh hah a taran awh teh hete kho dawk a kamkhueng awh toe.
28 Iwo anachita zimene munakonzeratu mwachifuniro chanu ndi mphamvu yanu kuti zichitike.
Na pouk tangcoung e lahoi ka tho hane kawinaw hah a kuep sak awh toe.
29 Tsopano, Ambuye taonani kuti atiopseza, tithandizeni ife atumiki anu, kuti tiyankhule mawu anu molimba mtima.
Bawipa atuvah ahnimouh ni pakhinae dawk hoi taran kahawicalah lawk ka pâpho thai nahanlah lungtangnae na poe awh haw.
30 Tambasulani dzanja lanu kuchiritsa anthu ndipo kuti, zizindikiro zodabwitsa zichitike mʼdzina la mtumiki wanu woyera Yesu.”
Patawnae pueng a roum nahanlah Bawipa na kut dâw haw. Kathounge na San Jisuh min lahoi kângairu mitnoutnaw sak thai nahanlah na poe haw telah a ratoum awh.
31 Iwo atatha kupemphera, malo amene anasonkhanapo anagwedezeka. Ndipo iwo onse anadzazidwa ndi Mzimu Woyera ndipo anayankhula Mawu a Mulungu molimba mtima.
Hottelah be a ratoum awh hnukkhu a kamkhuengnae hmuen a kahuet teh ahnimanaw pueng teh, Kathoung Muitha hoi akawi awh dawkvah Cathut e lawk hah lungtang laihoi a pâpho awh.
32 Okhulupirira onse anali a mtima umodzi, ndi maganizo amodzi. Palibe munthu amene amati zomwe anali nazo zinali zake zokha, koma amagawana chilichonse chimene anali nacho.
Kayuemnaw e kamkhuengnae teh lung suetalah ao dawkvah apipatet ni hai mae hnonaw heh, kama e hno doeh tet awh laipalah, kaawm e hno pueng teh cungtalah hno hanlah a hmoun awh.
33 Atumwi anapitirira kuchitira umboni mwa mphamvu zakuuka kwa Ambuye Yesu, ndipo pa iwo panali chisomo chochuluka.
Gunceinaw ni Bawipa e boutthawnae kong hah kalenpounge bahu hoi a kampangkhai awh dawkvah, kalenpounge lungmanae teh ahnimae lathueng vah a pha.
34 Panalibe anthu osowa kanthu pakati pawo. Pakuti amene anali ndi malo, kapena nyumba amagulitsa ndi kubweretsa ndalamazo
Ahnimouh thungvah ka roedeng e tami buet touh hai awm hoeh. Bangkongtetpawiteh laikawk, im a tawn awh e pueng hah a yo awh teh, a hmu awh e tangkanaw pueng a sin awh teh,
35 ndi kuzipereka kwa atumwi, ndipo zimagawidwa kwa aliyense amene anali ndi chosowa.
Gunceinaw e khok koevah a tâ awh teh lengkaleng a panki e patetlah a rei awh.
36 Yosefe, wa fuko la Levi, wochokera ku Kupro amene atumwi anamutcha Barnaba, kutanthauza kuti mwana wachilimbikitso,
Lungpahawinae capa tinae lah kaawm e, gunceinaw ni Barnabas telah a kaw awh e, Saipras tuilum tami, Levih catoun, Joseph teh,
37 anagulitsa munda wake ndipo anadzapereka ndalamazo kwa atumwi.
a tawn e laikawk a yo e phu, tangka hah a sin teh gunceinaw e khok koe a ta.

< Machitidwe a Atumwi 4 >