< Machitidwe a Atumwi 25 >
1 Patapita masiku atatu Festo atafika mʼdera lake, anachoka ku Kaisareya ndi kupita ku Yerusalemu.
Ndipo Festo ajhingili mu lijimbo elu ni baada jha magono madatu akalota kuhoma Kaisaria hadi Yerusalemu.
2 Kumeneko akulu a ansembe ndi atsogoleri a Chiyuda anabwera kwa iye ndi kumufotokozera mlandu wa Paulo.
Kuhani mbaha ni bhayahudi mashuhuri bhaletili shutuma dhidi jha Paulo kwa Festo, na bhalongili kwa nghofu kwa Festo.
3 Iwo anamupempha Festo kuti awakomere mtima potumiza Paulo ku Yerusalemu, pakuti anali atakonzekera chiwembu kuti amuphe Pauloyo pa njira.
Na bhan'sokili Festo fadhili juu jha habari sya Paulo abhwesiajhi kunkuta Yerusalemu ili bhabhwesiajhi kun'koma munjela.
4 Festo anayankha kuti, “Paulo akusungidwa ku Kaisareya, ndipo ndipita kumeneko posachedwa.
Lakini Festo ajibili kujha Paulo ajhele mfungwa mu Kaisaria, ni kwamba muene ikerebhuka okhu manyata.
5 Ena mwa atsogoleri anu apite nane kumeneko, kuti akafotokoze mlandu wa munthuyu, ngati anachita kanthu kalikonse kolakwika.”
Ajobhili “Kwa hiyo, bhala ambabho bhibhwesya kulota okhu ni tete. Kama kujhe ni khenu kibaya kwa munu ojho, mwilondeka kun'shtaki.”
6 Festo atakhala nawo masiku asanu ndi atatu kapena khumi iye anapita ku Kaisareya, ndipo mmawa mwake anayitanitsa bwalo nalamula kuti abweretse Paulo pamaso pake.
Baada jha kutama magono nane au kumi zaidi, akakerebhuka Kaisaria. Na ligono lyalafuatili atamili pa kiti kya hukumu ni kuamuru Paulo aletibhwayi kwa muene.
7 Paulo atafika, Ayuda amene anafika kuchokera ku Yerusalemu anayima momuzungulira. Iwo anamunenera zinthu zoopsa zambiri zimene sakanatha kubweretsa umboni wake.
Bho afikili, Bhayahudi kuhoma Yerusalemu bhajhemi karibu, bhakapisya mashtaka mazito ambajho bhabhwesilepi kughathibitisha.
8 Kenaka Paulo ananena mawu ake odziteteza kuti, “Ine sindinalakwirepo lamulo la Ayuda, kapena Nyumba ya Mulungu kapenanso Kaisara.”
Paulo akitetili ni kujobha, sio dhidi jha lihina lya bhayahudi, sio panani pa hekalu, na sio panani pa Kaisaria, nibhombi mabaya.'
9 Festo, pofuna kuti Ayuda amukonde anafunsa Paulo kuti, “Kodi iwe ukufuna kupita ku Yerusalemu, kuti kumeneko ukafotokoze mlandu wako pamaso panga?”
Lakini Festo alondeghe kwipendekesya kwa bhayahudi, efyo akan'jibu Paulo ni kujobha, 'Je, wilonda kulota Yerusalemu ni kuhukumulibhwa ni nene kuhusu mambo agha okhu?'
10 Paulo anayankha kuti, “Ine tsopano ndayima pamaso pa bwalo la milandu la Kaisara, ndiko kumene ayenera kundiweruza. Ine sindinalakwire Ayuda, monga inu mukudziwa bwino.
Paulo ajobhili, 'nijhemili mbele jha kiti kya hukumu kya Kaisari ambapo nilondeka kuhukumulibhwa. Nibhakosilepi bhayahudi, kama kya umanyi bhebhe.
11 Koma ngati ndili wolakwa, ngati ndachita kanthu koyenera kuphedwa, ine sindikukana kufa. Koma ngati mlandu umene abweretsa Ayudawa siwoona, palibe munthu angathe kundipereka mʼmanja mwawo. Ndikupempha kuti ndikaweruzidwe ndi Kaisara!”
Nikajhiajhi nikosili na kama nibhombi kyakilondeka kifo, nibelepi kufwa. Lakini kama shutuma sya bhene khenu lepi, ajhelepi munu jhaibhwesya kunikabidhi kwa bhene. Nikansoka Kaisari. '
12 Festo atakambirana ndi akuluakulu abwalo lake, anati, “Popeza wapempha kupita kwa Kaisara, kwa Kaisara udzapitadi!”
Baada jha Festo kulongela ni baraza akajibu, “Ukan'soka Kaisari; wibetalota kwa Kaisari.”
13 Patapita masiku ochepa mfumu Agripa pamodzi ndi Bernisi anabwera ku Kaisareya kudzalonjera Festo.
Baada jha magono kadhaa, mfalme Agripa ni Bernike bhafikili Kaisaria kubhomba ziara rasmi kwa Festo.
14 Atakhala kumeneko masiku angapo, Festo anafotokozera mfumuyo za mlandu wa Paulo. Iye anati, “Kuli munthu wina kuno amene Felike anamusiya mʼndende.
Baada jha kutamaapu kwa magono mingi, Festo awasilishi kesi jha Paulo kwa mfalme; Akajobha, 'Munu mmonga alekibhu apa ni Feliki kama mfungwa.
15 Nditapita ku Yerusalemu akulu a ansembe ndi akuluakulu a Ayuda anandifotokozera mlandu wake ndipo anandipempha kuti ndigamule kuti ndi wolakwa.
Bho nijhe Yerusalemu makuhani bhabhaha ni bhaseya bha bhayahudi bhaletili mashtaka juu jha munu ojho kwa nene na bhene bhakotili juu jha hukumu dhidi jha muene.
16 “Ine ndinawayankha kuti si mwambo wa Aroma kungomupereka munthu ayi. Munthu woyimbidwa mlanduyo amayenera kukumana nawo omunenezawo, kuti iye akhale ndi mwayi woyankhapo pa zimene akumuyimba mlanduzo.
Kwa e'le nene nabhajibili kujha desturi jha Bharoma lepi kumpisya munu upendeleo badala jhiake, mtuhumibhwa ilondeka kujha ni nafasi jha kubhakabili bhashtaki bha muene ni kwitetela dhidi jha tuhuma e'su.
17 Atabwera kuno pamodzi ndi ine, sindinachedwetse mlanduwo, koma ndinayitanitsa bwalo mmawa mwake ndi kulamula kuti amubweretse munthuyo.
Kwa hiyo, bhobhahidili pamonga apa, nabhwesilepi kulendela, lakini ligono lya lyafwatili natamili pakiti kya hukumu ni kuamuru munu ojho aletibhwayi mugati.
18 Omuyimba mlandu aja atayimirira kuti ayankhule, iwo sananene cholakwa chilichonse chimene ndimayembekezera.
Wakati bhashtaki bhajhemili ni kun'shtaki, nifikirileghe kujha ghajhelepi mashtaka mabaha ghaghaletibhu dhidi jha muene.
19 Mʼmalo mwake, anatsutsana naye pa fundo zina za chipembedzo chawo ndi za munthu wakufa, dzina lake Yesu, amene Paulo akuti ali moyo.
Badala jhiake, bhajhele ni mabishano fulani pamonga ni muene kuhusu dini jha bhene ni kuhusu Yesu ambajhe afuili, lakini Paulo idai kuwa ajhe muomi.
20 Ine ndinathedwa nzeru wosadziwa momwe ndikanafufuzira nkhaniyi; kotero ndinafunsa ngati akanafuna kupita ku Yerusalemu kuti akaweruzidwe kumeneko.
Nafumbibhu jinsi jha kuchungusya lisuala e'le, na nan'kotili kama ngaalotili Yerusalemu kuhukumibhwa kuhusu mambo agha.
21 Koma Paulo anapempha kuti akaonekere pamaso pa mfumu ya Chiroma, ndipo ndinalamula kuti asungidwe mpaka pamene ndidzamutumize kwa Kaisara.”
Lakini Paulo bho akutibhu abhekibhwayi chini jha ulinzi kwandabha jha uamuzi bhwa Mfalme, naamuiri abhekibhwayi hata panibeta kumpeleka kwa Kaisari.'
22 Ndipo Agripa anati kwa Festo, “Ine ndikufuna ndimumve ndekha munthu ameneyu.” Iye anayankha kuti, “Mudzamumva mawa.”
Agripa alongilili ni Festo, “Nilondeghe kabhele kumpelekesya munu ojho.” “Festo, akajobha, “kilabhu wibeta kumpelekesya.”
23 Mmawa mwake Agripa ndi Bernisi anabwera mwaulemu waukulu waufumu nalowa mʼbwalo la milandu pamodzi ndi akulu a asilikali ndiponso akuluakulu a mu mzindawo. Atalamula Festo kuti Paulo abwere, anabweradi.
Hivyo kilabhu jhiake, Agripa ni Bernike bhafikili ni sherehe simehele; bhafikili pa ukumbi ni maafisa bha kijeshi, ni bhanu mashuhuri bha mji. Ni Festo bho apisili amri, Paulo aletibhu kwa bhene.
24 Festo anati, “Mfumu Agripa, ndi onse amene muli nafe pano, mukumuona munthu uyu! Ayuda onse anandipempha ine za uyu ku Yerusalemu ndiponso kuno ku Kaisareya, mofuwula kuti, ameneyu sayenera kukhala ndi moyo.
Festo akajobha, “Mfalme Agripa, ni bhanu bhoha ambabho bhabhajhele apa pamonga natu, mukambona munu ojho; Jumuiya jhioha jha bhayahudi okhu Yerusalemu ni apa kabhele bhilonda nibhashauriajhi, ni bhene bhakapiga kelele kwa nene kwamba asitami.
25 Ine ndinapeza kuti iyeyu sanachite kanthu koyenera kufa, koma popeza anapempha kuti apite kwa mfumu ya Chiroma, ine ndinatsimikiza zomutumiza ku Roma.
Nibhona kujha abhombilepi lyalilondeka kufwa; Lakini kwandabha an'kutili Mfalme, naamuili nimpelekayi kwa muene.
26 Koma ndilibe kanthu kenikeni koti ndilembere Wolemekezekayo za iyeyu. Nʼchifukwa chake ndabwera naye pamaso pa nonsenu, makamaka kwa inuyo mfumu Agripa, kuti mwina mukamufunsitsa ndikhale ndi choti ndilembe.
Lakini nijhelepi ni khenu dhahiri kya kulemba kwa Mfalme. Kwandabha ejhe, nindetili kwa bhebhe, hasa kwa bhebhe, Mfalme Agripa, ili nibhwesiajhi kujha ni khenu kya kulemba kuhusu kesi.
27 Pakuti ine ndikuganiza kuti ndi chinthu chopanda nzeru kutumiza wamʼndende popanda kutchula zifukwa zenizeni za mlandu wake.”
Kwa kujha nibhona ijhelepi ni maana kumpeleka mfungwa ni bila kulasya mashtaka ghaghakan'kabili.