< Machitidwe a Atumwi 24 >
1 Patapita masiku asanu mkulu wa ansembe Hananiya, pamodzi ndi akuluakulu ena ndi katswiri woyankhulira anthu pa milandu wotchedwa Tertuliyo anapita ku Kaisareya ndipo anafotokoza mlandu wa Paulo kwa Bwanamkubwayo.
Chuin ninga jouvin gamvaipo henga Paul ahehset nauthu sei ding in thempu chungnung Ananias le Judate upa phabep chule Tertullus kiti minelkal them chu ahung lhung tauvin ahi.
2 Atamuyitana Paulo, ndipo Tertuliyo anafotokozera Felike nkhani yonse ya Paulo. Iye anati, “Wolemekezeka, ife takhala pamtendere nthawi yayitali chifukwa cha inu, ndipo utsogoleri wanu wanzeru wabweretsa kusintha mʼdziko lino.
Chuin Paul chu ahin puilut uvin ahile Tertullus chun gamvaipo henga Paul hehna thu hitin ahin seitan ahi: “Nangma vaihom them nale nangma jal'a keiho Judate hi phat sottah lungmonga um kahiuve.”
3 Wolemekezeka Felike ife timazilandira zimenezi moyamika kwambiri ponseponse ndi mwa njira iliyonse.
“O Lal chungnung, hiche ho jeh hin keiho kakipah lheh jeng uve.
4 Koma kuti tisakuchedwetseni, ndikupempha kuti mwa kuleza mtima kwanu mutimvere ife.
Ahin nangma kalungjin sah nompoi hijeh chun neilungset inlang phatchom chakhat neingai peh in tia kahung tao ahi.
5 “Ife tapeza kuti munthu uyu amayambitsa mavuto ndi kuwutsa mapokoso pakati pa Ayuda onse a dziko lonse lapansi. Iyeyu ndi mtsogoleri wa mpatuko wa Anazareti.
Hichepa hi phatseh a Judate umna jousea boina semjing kei mi ahi kamudoh un, chule thuhillhem Nazareth Yeshua chon a chon ho lamkai pipu ahi ti kamudoh uve.
6 Anayesera ngakhale kudetsa Nyumba ya Mulungu wathu. Ndiye ife tinamugwira.
Chukit jongle kamat uva chu aman houin jong suhboh ding agot ahi.
7 Koma, mkulu wa asilikali Lusiya anafika mwamphamvu namuchotsa mʼmanja mwathu.
Keihon keiho dan dungjuiya athu katan got u ahin, hinlah sepai jalamkai Lysias in thahat san'a kakhut uva kona ahung puidoh ahi.
8 Ndipo Lusiya analamula kuti amene anali naye ndi mlandu abwere kwa inu. Mukamufunsa ameneyu kwa nokha mudzadziwa choonadi cha zimene ife tikumunenera.”
Kaheh nauhi nangma tah in dong lechun adih tah chu namat doh ding ahi,” atin ahi.
9 Ayuda anavomereza nanenetsa kuti zimenezi zinali zoona.
Chuin Judah mi adangho jong chun Tertullus in asei jouse adih ahi atiuvin ahi.
10 Bwanamkubwayo atakodola Paulo ndi kulola kuti ayankhule, Pauloyo anati, “Ine ndikudziwa kuti inu mwakhala mukuweruza dziko lino zaka zambiri, kotero ndikukondwera kuti ndikudziteteza ndekha pamaso panu.
Chuin gamvaipo chun Paul jong thu asei sah in, chuin Paul in, “Pu, kum tamtah Judate chunga thutan'a hung pang nahi kahen, hijeh chun namasanga kipah tah in kakihonna thu seiying kate.
11 Inu mukhoza kupeza umboni wake. Sipanapite masiku khumi ndi awiri chipitireni changa ku Yerusalemu kukapembedza.
Jerusalema Pathen hou dinga kahung lhun jouva pat ni somleni jong lhing loulai ahi hi nahetdoh jeng ding ahi.
12 Amene akundiyimba mlanduwa sanandipeze mʼNyumba ya Mulungu ndi kutsutsana ndi wina aliyense kapena kuyambitsa chisokonezo mʼsunagoge kapena pena paliponse mu mzindamo.
Eihehse hohin houin'a mitoh kakinel na jong amu naisai lou diu ahin, kikhopna in ahiloule khopi lamlhong lah'a boina kasem jong amukhah lou dingu ahi.
13 Ndipo sangathe kupereka umboni wa mlandu umene akundiyimba inewu.
Hiche mihon eihehset nau hi khat cha aphotchet na apeh thei lou dingu ahi.”
14 Komatu ine ndikuvomera kuti ndimapembedza Mulungu wa makolo athu, monga wotsatira wa Njirayo, imene iwo akuyitchula mpatuko. Ine ndimakhulupirira chilichonse chimene chimagwirizana ndi malamulo ndiponso zimene zinalembedwa ndi Aneneri.
Ahin hou dih lou lamkai ahi atiu vang chu kanom'e, ajeh chu kapu kapa teuvin ana hou Pathen chu kahou ahin, Judate dan le themgao lekhabua kisun jouse dih tah a katahsan ahi.
15 Ine ndili nacho chiyembekezo chomwecho chimene iwo ali nacho mwa Mulungu, kuti kudzakhala kuuka kwa akufa kwa olungama ndiponso kwa ochimwa.
Amaho kinep na banga keijong Pathen in nikhat le midih le midih lou ahin kaithou kit ding ahi tia kinem kahi.
16 Kotero ine ndimayesetsa kuti ndikhale ndi chikumbumtima chosanditsutsa pamaso pa Mulungu ndi anthu onse.
Hiche jeh a hi mijouse le Pathen anga dih tah a hinkho manding kagot jing ahi.
17 “Patapita zaka zambiri, ndinabwera ku Yerusalemu kudzapereka mphatso kwa anthu osauka a mtundu wanga komanso kudzapereka nsembe.
Chuin kum tamtah jouvin kamite kithopina sum peding le Pathen koma kilhaina bolding in Jerusalema kahung kilen ahileh,
18 Pamene ndinkachita zimenezi, iwo anandipeza mʼbwalo la Nyumba ya Mulungu nditachita mwambo wodziyeretsa. Panalibe gulu la anthu kapena kuti ndimachita za chisokonezo chilichonse.
Houin sunga kauma ka kisuhtheng chu eiheh se hon amuvin, hiche pet'a chu kavela mipi jong umlou ahin boina ima jong aumpon ahi.
19 Koma pali Ayuda ena ochokera ku Asiya, amene amayenera kukhala pano pamaso panu, kundiyimba mlandu ngati ali ndi kalikonse konditsutsa ine.
Ahin Asia gamsunga kona Judaho mi phabep umu ahi, chule amaho chu kei hehset na ding hola umjing'u ahi!
20 Kapena awa amene ali panowa anene mlandu umene anapeza mwa ine, pamene ndinayima pamaso pa Bwalo lawo Lalikulu.
Judate houvaipoloi hon kachunga ipi chonsetna amu-uham hiche miho hi dongin,
21 Koma cholakwa changa chingathe kukhala chokhachi chakuti, nditayima pamaso pawo ndinafuwula kuti, ‘Mukundiweruza ine lero chifukwa ndimakhulupirira kuti akufa adzauka.’”
Thilkhat bouseh “thokit thudol katahsan jeh a tunia na-angsung uva kachung thu kikhol ahi,” tia kasap tailou adang ima namu lou dingu ahi.
22 Kenaka Felike, amene amadziwa bwino za Njirayo, anayamba wayimitsa mlanduwo, nati, “Ndidzagamula mlandu wako akabwera mkulu wa asilikali Lusiya.”
Chuche tahsanna lampi thudol hethem tah ahitoh kilhon in, Felix chun phat asuh saobe in, “Vaipipo Lysias hung lhun kah in khongaiyun, ama ahung tengle nathuu ngaito chen nange,” ati.
23 Iye analamulira woyangʼanira asilikali 100 kuti alondere Paulo, koma azimupatsako ufulu ndiponso kulola abwenzi ake kuti adzimusamalira.
Chuin sepai jalamkai pa koma chun, “Paul chu songkul'a koiyun lang ahin aloi agol hon avila angaichat ho abolpeh thei nading un phalna peuvin,” ati.
24 Patapita masiku angapo Felike anabwera pamodzi ndi mkazi wake Drusila, amene anali Myuda. Anayitana Paulo ndipo anamvetsera zimene amayankhula za chikhulupiriro mwa Khristu Yesu.
Nichomkhat jouvin Felix chu ajinu Juda numei Drusilla toh ahung kit in, chuin Paul chu aga kousah lhon in Paul in Yeshua Christa tahsan thudol asei chu angai lhon in ahi.
25 Paulo atayankhula za chilungamo, za kudziretsa ndiponso za chiweruzo chimene chikubwera, Felike anachita mantha ndipo anati, “Basi tsopano! Pita. Tidzakuyitanitsa tikadzapeza mpata.”
Chuin Paul in Chondih nale eima chang kitimhat chule khonunga hung lhung ding thutanna thu asei ajah phat chun Felix chu ahung kicha tan, “Tun chen lang, phat gomkom aum teng le kahin koukit ding nahi,” tin asol doh tan ahi.
26 Pa nthawi imeneyi amayembekeza kuti Paulo adzamupatsa ndalama, nʼchifukwa chake amamuyitanitsa kawirikawiri ndi kumayankhula naye.
Chujongle Paul chun sum eithimpeh khante tin, akou loi loi jin ahoupi jing jin ahi.
27 Patapita zaka ziwiri, Porkiyo Festo analowa mʼmalo mwa Felike, koma anamusiya Paulo mʼndende, chifukwa amafuna kuti Ayuda amukonde.
Chutia kumni ache jouvin, Porcius Festus in Felix pan mun chu alotan, chule Felix in Judate lung ahol jeh chun Paul chu songkul'a akhum in adalhatan ahi.