< Machitidwe a Atumwi 15 >

1 Anthu ena ochokera ku Yudeya anafika ku Antiokeya ndipo amaphunzitsa abale kuti, “Ngati simuchita mdulidwe potsata mwambo wa Mose, simungapulumuke.”
Tami bangpatetnaw ni Judah ram lahoi a tho awh teh, Mosi e kâlawk patetlah vuensomanae ka hmawt hoeh e ni rungngang lah na awm thai mahoeh, telah hmaunawnghanaw a cangkhai awh.
2 Zimenezi zinachititsa Paulo ndi Barnaba kuti atsutsane nawo kwambiri. Kotero Paulo ndi Barnaba anasankhidwa pamodzi ndi abale ena kuti apite ku Yerusalemu kukaonana ndi atumwi ndi akulu ampingo kukakambirana za nkhaniyi.
Hatnavah Pawl, Barnabas ti hoi ahnimanaw teh kâounnae puenghoi ao dawkvah, hmaunawnghanaw ni, Pawl, Barnabas hoi alouke a hnukkâbangnaw hoiyah hote laidei hanelah Jerusalem kaawm e gunceinaw hoi kacuenaw koe a cei awh hane lawk a dei awh.
3 Mpingo unawaperekeza, ndipo pamene amadutsa ku Foinike ndi Samariya, iwo anafotokoza momwe a mitundu ina anatembenukira mtima. Nkhani imeneyi inakondweretsa kwambiri abale onse.
Kawhmoun ni ahnimanaw yo a thak awh. Phoenicia hoi Samaria ram lahoi pou a cei awh navah, Jentelnaw koe a lungpatawnae kong ahnimouh ni a dei awh teh hmaunawnghanaw pueng a lunghawi sak awh.
4 Atafika ku Yerusalemu, iwo analandiridwa ndi mpingo, pamodzi ndi atumwi ndiponso akulu ampingo. Paulo ndi Barnaba anawafotokozera zonse zimene Mulungu anachita kudzera mwa iwo.
Jerusalem a pha awh navah, kawhmoun hoi Gunceinaw, kacuenaw ni a dawn awh. Ahnimouh ni Cathut ni ahnimouh hno lahoi hno a sak e naw a dei pouh awh.
5 Kenaka, okhulupirira ena amene kale anali a gulu la Afarisi anayimirira ndipo anati, “Anthu a mitundu ina ayenera kuchita mdulidwe ndi kusunga malamulo a Mose.”
Hatei Farasinaw koe lahoi ka yuem e tami tangawn ni a kangdue awh teh, Jentelnaw hah vuensoma sak hane hoi Mosi e kâlawk tarawi sak hanelah lawkthui hanelah ao ati awh.
6 Atumwi ndi akulu ampingo anasonkhana kuti akambirane za nkhaniyi.
Hatdawkvah gunceinaw hoi kacuenaw ni hote lawk paceinae pouk hanelah a kamkhueng awh.
7 Atakambirana kwambiri Petro anayimirira, ndipo anawayankhula nati: “Abale, mukudziwa kuti masiku oyambirira Mulungu anandisankha ine pakati panu kuti anthu a mitundu ina amve kuchokera pakamwa panga mawu a Uthenga Wabwino ndi kukhulupirira.
Tha hoi a kâoun awh hnukkhu vah Piter ni a kangdue teh hmaunawnghanaw, Jentelnaw ni kamthang kahawi a thai awh teh, a yuem awh thai nahanlah Cathut ni nangmouh thung hoi kai heh kadeikung lah na rawi e na panue awh.
8 Mulungu amene amadziwa mtima wa munthu, Iye anaonetsa kuti anawalandira powapatsa Mzimu Woyera, monga momwe anachita kwa ife.
Lungthin be ka panuek e Cathut ni Kathoung Muitha heh maimouh na poe e patetlah ahnimouh hai a poe awh teh ahnimouh koelah a kampangkhai.
9 Iye sanasiyanitse pakati pa ife ndi iwo, pakuti anayeretsa mitima yawo mwachikhulupiriro.
Cathut ni ahnimouh hoi maimouh khoeroe kapeknae awm laipalah yuemnae lahoi ahnimae lungthin a thoungsak.
10 Tsopano, chifukwa chiyani mukuyesa Mulungu poyika goli mʼkhosi la ophunzira, limene ngakhale ife kapena makolo athu sangathe kulisenza?
Hatdawkvah nangmouh ni mintoenaw hoi maimouh ni hai phu thai hoeh e hno teh ahnimae a loung dawk na patue e lahoi atuvah Cathut tanouk hanlah na ngai awh.
11 Osatero! Ife tikukhulupirira kuti tinapulumutsidwa mwachisomo cha Ambuye athu Yesu Khristu, monga iwonso anachitira.”
Maimouh hai ahnimouh patetlah Bawipa Jisuh Khrih e a lungmanae kecu dawk rungngang lah o teh yuem awh, atipouh.
12 Gulu lonse linakhala chete pamene amamvetsera Barnaba ndi Paulo akuwawuza za zizindikiro zodabwitsa zimene Mulungu anazichita pakati pa anthu a mitundu ina kudzera mwa iwo.
Hatnavah ka kamkhueng e tami pueng teh sairasuep lah ao awh teh, Barnabas hoi Pawl ti ni ahnimouh koehoi Jentelnaw koe Cathut ni a sak e mitnoutnae hoi kângairunae a dei awh e a thai awh.
13 Iwo atatha kuyankhula, Yakobo anayankhula nati: “Abale, tandimverani.
Ahnimanaw ni lawk dei e a pâbaw awh hnukkhu, Jem ni hmaunawnghanaw, kaie ka lawk thai awh haw.
14 Simoni watifotokozera mmene Mulungu poyamba paja anaonetsa kukhudzidwa kwake pomwe anatenga anthu a mitundu ina kukhala ake.
Cathut ni ama hanlah Jentelnaw thung hoi a miphun lah a coe nahan, ahnimouh koe hmaloe a thonae hah Simeon ni apasuek vah a dei toe.
15 Mawu a aneneri akuvomereza zimenezi, monga kwalembedwa kuti,
Profetnaw e a lawk dei e hai hete a lawk hoi a kâvan.
16 “‘Zitatha izi Ine ndidzabwerera ndipo ndidzamanganso nyumba ya Davide imene inagwa. Ndidzakonzanso malo amene anagumuka, ndi kuyimanganso,
Cakathoung ni, hetnaw e hnuklah kai ni bout ka tho vaiteh ka rawm tangcoung e Devit e lukkareiim hah bout ka sak han. Raphoe tangcoung e hote rim hah bout sak lah ao vaiteh ka caksak han.
17 kuti anthu otsalawo afunefune Ambuye, ndi anthu onse a mitundu ina amene atchedwa ndi dzina langa, akutero Ambuye, amene amachita zinthu zimenezi
Ka min lahoi ka kaw e Jentelnaw hai a yungyoe ka hring e Cathut a tawng awh nahane doeh telah,
18 zinaululidwa kuyambira kalekale.’ (aiōn g165)
ayan hoi hete lawk ka panueksakkung Bawipa ni a dei atipouh. (aiōn g165)
19 “Chifukwa chake, ine ndikuweruza kuti tisamavute anthu a mitundu ina amene atembenuka mtima kutsata Mulungu.
Hatdawkvah Jentelnaw koehoi Cathut koe lah a lungkâthung e naw koe runae poe hanlah awmhoeh.
20 Koma tiwalembere iwo, kuwawuza kuti asadye chakudya choperekedwa kwa mafano, apewenso dama, asadyenso nyama zochita kupotola kapena kudya magazi.
Meikaphawk dawk thounghoehnae, kamsoumhoehe napui tongpa yonnae, lahuen kara e moi hoi a thinaw hah roun hanelah ahnimouh koe ca lahoi thaisak hanlah ka pouk.
21 Pakuti malamulo a Mose akhala akulalikidwa mu mzinda uliwonse, kuyambira kalekale ndipo amawerengedwa mʼMasunagoge tsiku la Sabata.”
Bangkongtetpawiteh ayan hoi kho tangkuem vah Mosi e phung lawk ka dei e ao teh, hote lawk hah sabbath hnintangkuem sinakoknaw dawk ouk touk awh atipouh.
22 Pamenepo atumwi ndi akulu ampingo, pamodzi ndi mpingo onse, anagwirizana zosankha anthu ena pakati pawo kuti awatume ku Antiokeya pamodzi ndi Paulo ndi Bamaba. Iwo anasankha Yudasi, wotchedwa Barsaba ndi Sila, anthu awiri amene anali atsogoleri pakati pa abale,
Hatnavah Gunceinaw, kacuenaw hoi Kawhmoun abuemlah ni amamouh thung dawk e tami a rawi awh teh, Pawl, Barnabas hoi hmaunawnghanaw thung dawk e kahrawikung lah kaawm awh e Barsabbas telah a kaw awh e Judah hoi Silas a rawi awh.
23 kuti akapereke kalata yonena kuti, Kuchokera kwa atumwi ndi akulu ampingo, abale anu, Kwa anthu a mitundu ina okhulupirira a ku Antiokeya, Siriya ndi Kilikiya: Tikupereka moni.
Ahnimouh koe a sin sak awh e ca dawkvah, gunceinaw kacuenaw hoi hmaunawnghanaw ni Antiok kho Siria ram hoi Cilicia ram kaawm e Jentel hmaunawnghanaw kut na man awh.
24 Ife tamva kuti anthu ena ochokera pakati pathu, amene sitinawatume anakusokonezani maganizo ndi kukuvutitsani ndi zimene amakuwuzani.
Kaimouh koe e tami bangpatet ni kaimouh ni patoun laipalah a cei awh teh lawk aphunphun lah a dei awh teh, nangmouh na lungpuen awh teh, a rucatnae na poe awh tie ka thai awh. Vuensom na a awh vaiteh, kâlawk hai na tarawi awh roeroe han a ti awh. Hotpatetlae lawk dei hanelah ahnimouh koe kâpoelawk banghai ka poe awh hoeh.
25 Tsono ife tagwirizana kuti, tisankhe anthu ena ndi kuwatumiza kwa inu pamodzi ndi abale athu okondedwa Paulo ndi Barnaba,
Hatdawkvah kaimouh ni ka kâhmo awh teh, maimouh ni pahren e Pawl hoi Barnabas hoi cungtalah nangmouh koe tami patoun hanelah ka lung a kuep awh. Hatdawkvah maimouh ni Bawipa Jisuh Khrih min kecu dawkvah amamae hringnae kâphumnaw lah kaawm e,
26 anthu amene anapereka moyo wawo chifukwa cha dzina la Ambuye athu Yesu Khristu.
maimouh ni lungpataw awh e Barnabas hoi Pawl tinaw hoi reirei patoun hanelah tami kahni touh rawi hane ka lungkuep awh.
27 Nʼchifukwa chake, tikutumiza Yudasi ndi Sila kuti adzachitire umboni ndi mawu a pakamwa pawo za zimene ife talemba.
Hatdawkvah Judas hoi Silas hah ka rawi awh teh nangmouh koe ka patoun awh. Ahnimouh ni lawk hoi hai a dei awh han doeh.
28 Pakuti zinakomera Mzimu Woyera ndiponso ife kuti tisakusenzetseni katundu wina, kupatula zoyenera zokhazi:
Hete phunglamnaw hloilah alouke hnokari titca hai nangmouh van toung sak hoeh nahanlah Kathoung Muitha hoi kaimouh ni ka hnâbo awh.
29 Mupewe kudya chakudya choperekedwa nsembe kwa mafano, musadye magazi, kapena nyama yopha mopotola ndiponso musachite dama. Mudzachita bwino mukapewa zimenezi. Tsalani bwino.
Hote phunglam teh nangmouh ni meikaphawk bawknae hno, thi, lahuen kara e moi, hoi kamsoumhoehe napui tongpa yonnae hah roun awh. Nangmouh teh hete hnonaw hoi kathoung lah na awm awh pawiteh ahawi. Na tak dam awh naseh telah a thut pouh awh.
30 Anthu aja anatumidwa ndipo anafika ku Antiokeya, kumene anasonkhanitsa mpingo pamodzi napereka kalatayo.
Gunceinaw a patoun navah Antiok kho lah a cei awh teh, haw a pha hoi kayuemnaw a pâkhueng awh hnukkhu ca hah ahnimae kut dawk a poe awh.
31 Anthuwo anawerenga kalatayo ndipo abalewo anakondwa chifukwa cha mawu ake achirimbikitso.
Ahnimouh ni hote ca a touk awh teh thapoenae lawk dawk a konawm awh.
32 Yudasi ndi Sila amene analinso aneneri, ananena zambiri zowalimbikitsa ndi kuwapatsa mphamvu abalewo.
Judah hoi Silas amamouh roi hai profet lah ao roi dawkvah ahnimouh koe thapoenae lawk a dei pouh roi.
33 Atakhala kumeneko kwa kanthawi, abale aja anatsanzikana nawo mwamtendere kuti abwerere kwa amene anawatuma.
Ahnimanaw teh hnin dongdeng ao awh teh, hmaunawnghanaw ni lungmawng lah a thak awh teh kapatounkungnaw koe let a ban sak awh.
34 Koma Sila anasankha kuti akhale komweko.
Hatei Silas teh hawvah tongtang ao.
35 Koma Paulo ndi Barnaba anatsalira ku Antiokeya kumene iwo pamodzi ndi ena ambiri anaphunzitsa ndi kulalikira Mawu a Ambuye.
Pawl hoi Barnabas teh Antiok kho ao navah alouke taminaw hoi cungtalah Bawipa e lawk hah a cangkhai awh.
36 Patapita masiku ena Paulo anati kwa Barnaba, “Tiyeni tibwerere kuti tikaone abale ku mizinda yonse imene tinalalika Mawu a Ambuye ndipo tikaone mmene akuchitira.”
A hnin moi ao hoi Pawl ni Barnabas koe, Bawipa e lawk pâpho tangcoungnae kho dawk kaawm e hmaunawnghanaw, bangtelane ao awh tie yo hloe hanelah ahnimouh koe bout cet awh sei atipouh.
37 Barnaba anafuna kutenga Yohane, wotchedwanso Marko, kuti apite nawo.
Barnabas ni Mark tie Jawhan hai hrawi hanelah a ngai.
38 Koma Paulo anaganiza kuti sichinali cha nzeru kumutenga Yohane chifukwa iye anawathawa ku Pamfiliya ndipo sanapitirire nawo pa ntchito.
Hateiteh, Pawl ni Pamfilia ram vah ahnimouh hoi a kamphei teh oun a cei dawkvah, a thaw tawknae koe ahnimouh hoi reirei ka cet ngai hoeh e teh kaw hanelah awmhoeh telah a pouk.
39 Iwo anatsutsana kwambiri kotero kuti anapatukana. Barnaba anatenga Marko ndipo anakwera sitima ya pamadzi kupita ku Kupro.
Hatnavah puenghoi kâounnae ao dawkvah buet touh hoi buet touh a kamphei roi toe. Barnabas ni Mark a hrawi teh Saipras tuilum lah a cei.
40 Paulo anasankha Sila. Abale atawapempherera kwa Ambuye kuti alandire chisomo, ananyamuka.
Pawl ni Silas a rawi teh hmaunawnghanaw lahoi Bawipa e lungmanae dawk hnawng lah ao hnukkhu a kamthaw.
41 Iye anadutsa ku Siriya ndi ku Kilikiya kupita akulimbikitsa mipingo.
Ahni teh Siria ram hoi Cilicia ram lah tawngtang a cei teh, kawhmounnaw hah a cak sak.

< Machitidwe a Atumwi 15 >