< Machitidwe a Atumwi 12 >

1 Inali nthawi yomweyi imene mfumu Herode anamanga ena a mu mpingo ndi cholinga chakuti awazunze.
Mu thangu yina, ntinu Elode wukangisa ndambu yi batu ba dibundu di Yelusalemi mu diambu di kuba yamisa.
2 Iye analamula kuti Yakobo mʼbale wa Yohane, aphedwe ndi lupanga.
Wuvondisa Zaki, khomba Yowani, mu sabala.
3 Ataona kuti zimenezi zinakondweretsa Ayuda, anawonjeza ndi kugwiranso Petro. Izi zinachitika pa nthawi ya Chikondwerero cha Buledi wopanda Yisiti.
Bu kamona ti Bayuda bamuena diambu beni khini wubuela kangisa Piela; yiba mu thangu nyengo mapha makambu tulu luvi.
4 Atamugwira Petro, namutsekera mʼndende, anamupereka kwa magulu anayi a asilikali kuti amuyangʼanire, gulu lililonse linali ndi asilikali anayi. Herode anafuna kumuzenga mlandu pamaso pa anthu onse chikondwerero cha Paska chitapita.
Bu kankangisa, wunkotisa mu nloko ayi wutula kumi masodi masambanu muingi mansunga. Mayindu maba yandi, Pasika yawu vioka, ma kunsambisa va ntuala batu.
5 Kotero Petro anasungidwa mʼndende, koma mpingo unamupempherera kolimba kwa Mulungu.
Piela wuba mu nloko; vayi dibundu disambila zitsambulu, mu kambu vonga kuidi Nzambi mu diambu diandi.
6 Usiku woti mmawa mwake Herode amuzenga mlandu, Petro amagona pakati pa asilikali awiri, atamangidwa maunyolo awiri, ndiponso alonda atayima pa khomo.
Vayi thangu Elode kaba mayindu ma kunsambisa, mu builu buna Piela wuba wuleka va khatitsika masodi muadi. Wuba wukangama mu zisieni zizole. Minsungi miba va muelo mu sunga nloko.
7 Mwadzidzidzi mngelo wa Ambuye anaonekera ndipo kuwala kunawunika mʼchipindamo. Mngeloyo anamugwedeza Petro mʼnthiti ndi kumudzutsa. Iye anati, “Fulumira, imirira!” Ndipo maunyolo anagwa kuchoka mʼmanja a Petro.
Tala mbasi yi Pfumu yitotuka ayi kiezila kingolo kikienzulanloko. Mbasi yisimba Piela mu luvati, yinkotula ayi yinkamba: —Temala nsualu. Zisieni ziba mu mioko miandi zidabuda.
8 Kenaka mngelo anati kwa iye, “Vala zovala ndi nsapato.” Ndipo Petro atachita izi mngeloyo anamuwuzanso kuti, “Funda chovala chako ndipo unditsate.”
Bosi mbasi yinkamba: —Vuata minledi miaku ayi zisapatu. Wuvanga buawu. Mbasi yinkamba diaka: —Buela tetika yunga kiaku bosi ndandakana.
9 Petro anatsatira natuluka mʼndende, koma sanazindikire kuti zimene mngeloyo amachita zimachitikadi; iye amaganiza kuti amaona masomphenya.
Piela wutotuka mu nloko, wunlandakana. Kasia zaba ko ti mambu momo mavanga mbasi maba makiedika vayi kabanzila ti tsongolo kalembo moni.
10 Iwo anadutsa gulu loyamba ndi lachiwiri la asilikali ndipo anafika pa chitseko chachitsulo cholowera mu mzinda. Chitsekocho chinatsekuka chokha ndipo anadutsa. Pamene anayenda kutalika kwa msewu umodzi, mwadzidzidzi mngelo uja anachoka.
Bu bavioka vaba minsungi mitheti ayi vaba minsungi mimmuadi, buna batula va muelo wusengo wuyenda ku ndambu yi divula, wuzibuka wawu veka! Bu batotuka ayi bayenda nate ku tsongi nzila. Tumbu zimbukila mbasi yizimbala va meso ma Piela.
11 Pamenepo Petro anazindikira nati, “Tsopano ndikudziwa mosakayika kuti Ambuye anatuma mngelo wake kudzandipulumutsa mʼmanja mwa Herode, ndi ku zoyipa zonse zimene Ayuda amafuna kundichitira.”
Diela di Piela bu divutukisa, Piela wukamba: “Buabu khikinini ti Pfumu fidisidi mbasiꞌandi, yikhudidi mu mioko mi Elode ayi mu mambu momo Bayuda bazodidi kuphangila.”
12 Atazindikira zimenezi anapita ku nyumba ya Mariya amayi ake a Yohane, wotchedwanso Marko, kumene kunasonkhana anthu ambiri ndipo amapemphera.
Bu kabakula buawu, wuyenda ku nzo Maliya, ngudi yi Yowani diodi baba ntedilanga Malako, kuawu kukutakana batu bawombo ayi basambila.
13 Petro anagogoda pa chitseko cha panja, ndipo mtsikana wantchito dzina lake Roda anabwera kuti adzatsekule chitseko.
Piela bu kakokuta va muelo, kisadi kimosi kinketo, dizina diandi Lode wuyiza mu vana mvutu.
14 Atazindikira mawu a Petro anakondwa kwambiri ndipo anabwerera osatsekula ndipo anafuwula kuti, “Petro ali pa khomopa!”
Bu kabakula mbembo Piela; mu diambu di khini kasia zibula ko muelo vayi wuvutuka mu nsualu ayi wuba kamba: —Piela widi va muelo.
15 Anthuwo anati kwa iye, “Wopenga iwe!” Atalimbikira kunena kuti zinali zoona, iwo anati, “Ameneyo ndi mngelo wake.”
—Bawu bankamba: —A ngeyo bati lawukidi e? Vayi wuba kamba ti diambu beni didi di kiedika. Vayi bawu batuba: —Buna mbasi andi.
16 Koma Petro anapitiriza kugogoda ndipo atatsekula chitseko ndi kumuona, anthuwo anadabwa kwambiri.
Piela wutatamana kokuta, buna bazibula; bammona ayi basimina.
17 Petro anakweza dzanja ndi kuwawuza kuti akhale chete ndipo anawafotokozera mmene Ambuye anamutulutsira mʼndende. Iye anati, “Uzani Yakobo ndi abale ena za zimenezi.” Kenaka anachoka napita kumalo ena.
Piela wuba labikisa mu koko muingi babika biyoko, wuba sudikisa buevi Pfumu kantotudila mu nloko. Wuba kamba: —Lukamba mambu mama kuidi Zaki ayi kuidi bakhomba. Bu katotuka, wuyenda ku buangu kinkaka.
18 Pamene kunacha kunali phokoso lalikulu pakati pa asilikali, iwo anafunsa kuti, “Kodi chamuchitikira Petro ndi chiyani?”
Buisi bu bukia, tsisi yingolo yibua mu masodi mu diambu masia zaba ko mambu mbi mabuila Piela.
19 Herode atamufunafuna ndipo wosamupeza, anawafunsa asilikali ndipo analamulira kuti asilikaliwo aphedwe. Kenaka Herode anachoka ku Yudeya ndi kupita ku Kaisareya ndipo anakhala kumeneko kwa kanthawi
Elode bu kantombisa ayi bu kasia kummona ko, buna wusambisa minsungi mi nloko, ayi wuvana lutumunu lu kuba vondisa. Elode wubotuka mu Yuda ayi wuyenda ku Sezali, wuvuanda kuna.
20 Herode anakwiyira anthu a ku Turo ndi Sidoni; anthuwo anagwirizana zoti akambirane naye. Atapeza thandizo kuchokera kwa Blasito, wantchito wokhulupirika wa mfumu, anapempha kuti pakhale mtendere, chifukwa dziko lawo limadalira dziko la mfumuyo pa chakudya chawo.
Elode wufuemina ngolo basi Tile ayi basi Sidoni. Vayi basi Tile ayi Sidoni bawizana, bayiza kuidi niandi. Mu lusadusu lu Balasitusi, mutu wowo wuba nsalanga mu vinga kiba nlekanga ntinu, batomba vutula ndembama bila tsi yi ntinu Elode yiba zingisanga zitsi ziawu.
21 Pa tsiku limene anasankha Herode, atavala zovala zake zaufumu, anakhala pa mpando wake ndipo anayankhula kwa anthuwo.
Mu lumbu kioki bawizana, Elode wuvuata minledi miandi mi kitinu; wuvuanda va kundu kiandi ki kitinu, wutona kuba yolukila mu luniemo.
22 Anthuwo anafuwula nati, “Amenewa ndi mawu a mulungu osati a munthu ayi.”
Batu bayamikina: “A keti mbembo yi Nzambi yoyi; yisi yi mutu ko!”
23 Nthawi yomweyo mngelo wa Mulungu anamukantha chifukwa sanapereke ulemu kwa Mulungu ndipo anadyedwa ndi mphutsi nafa.
Vana vawu, mbasi yi Nzambi yiyiza kumbeta mu diambu kasia vana nkembo kuidi Nzambi ko. Zimvidi zindia; bosi wufua.
24 Koma Mawu a Mulungu anapitirirabe kufalikirafalikira.
Muaki mambu ma Nzambi maluta tembakana ngolo.
25 Barnaba ndi Saulo atamaliza ntchito yawo anachoka ku Yerusalemu, atatenga Yohane wotchedwanso Marko.
Balinabasi ayi Sawuli bu bamanisa kisalu kiawu, babika Yelusalemi. Bayenda ayi Yowani, diodi baba ntedilanga Malako.

< Machitidwe a Atumwi 12 >