< 2 Timoteyo 1 >

1 Paulo mtumwi wa Khristu Yesu mwa chifuniro cha Mulungu. Anandituma kuti ndilalike za lonjezo la moyo umene uli mwa Khristu Yesu.
An Paulo jaote mar Kristo Yesu kuom dwaro mar Nyasaye, kaluwore gi singo mar ngima man kuom Kristo Yesu,
2 Kwa Timoteyo, mwana wanga wokondedwa: Chisomo, chifundo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate ndi Ambuye athu Yesu Khristu.
Andikoni in Timotheo nyathina mahero: Ngʼwono gi kech kod kwe moa kuom Nyasaye Wuoro kod Kristo Yesu Ruodhwa obed kodi.
3 Ndikuyamika Mulungu amene ndimamutumikira ndi chikumbumtima chosatsutsika, monga momwe ankachitira makolo anga. Usiku ndi usana ndimakukumbukira mosalekeza mʼmapemphero anga.
Adwokone Nyasaye erokamano ma atiyone gi paro maler maonge bura, mana kaka kwerena bende notiyone, ka apari odiechiengʼ gotieno e lemona mapile.
4 Ndikamakumbukira misozi yako, ndimalakalaka nditakuona kuti ndidzazidwe ndi chimwemwe.
To ka aparo kaka pi wangʼi ne chwer to chunya gombo neni ahinya mondo abed gi mor mogundho.
5 Ndakumbukira za chikhulupiriro chako choona chimene chinayamba mwa agogo ako a Loisi ndi mwa amayi ako Yunike ndipo ndikutsimikiza mtima kuti chilinso mwa iwe.
Nikech aparo kuom yie mar adier ma in-go. Yienino chalo gi yie mane Lois dani nigo mokwongo. Kendo mane Yunike minu nigo. An gi ratiro ni in bende in gi yie makamano
6 Nʼchifukwa chake ndikukukumbutsa kuti upemerere monga amachitira moto, mphatso imene Mulungu anakupatsa nditakusanjika manja.
Mano emomiyo ajiwi mondo ichier mich ma in-go mane Nyasaye omiyi chiengʼ mane aketo lweta kuomi.
7 Pakuti Mzimu amene Mulungu anatipatsa, si Mzimu wotipatsa manyazi, koma Mzimu wotipatsa mphamvu, chikondi ndi kudzisunga.
Nikech Nyasaye ne ok omiyowa chuny mar bedo ngoche, to nomiyowa chuny mar bedo gi teko, gihera kod ritruok.
8 Choncho usachite manyazi kuchitira umboni Ambuye athu, kapena kuchita manyazi chifukwa cha ine wamʼndende. Koma umve nane zowawa chifukwa cha Uthenga Wabwino, mothandizidwa ndi mphamvu za Mulungu.
Kuom mano kik wiyi kuodi kuom timo nend Ruodhwa kata nenda an Jatichne motwe. To kuom teko mar Nyasaye yie mondo osandi koda nikech Injili,
9 Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
ma nowarowa kendo noluongowa mondo wadag e ngima maler. Mano ok nikech wasetimone gimoro maber to nikech dwarone owuon kuom ngʼwonone. Ne omiyowa ngʼwononi kuom Kristo Yesu kane piny pok obetie, (aiōnios g166)
10 Koma tsopano Mulungu watiwululira kudzera mʼkuoneka kwa Mpulumutsi wathu, Khristu Yesu, amene anathetsa mphamvu za imfa ndipo mwa Uthenga Wabwino anaonetsa poyera moyo umene sungafe.
to sani koro osefwenynwago kuom biro mar Jawarwa, Kristo Yesu. En ema osetieko tho mi okelo ngima kod ngima mak rum e ler kuom Injili.
11 Ine ndinasankhidwa kukhala wamthenga, ndi mtumwi ndi mphunzitsi wa Uthenga Wabwinowu.
Ne oyiera mondo aland Injilini kaka jaote kendo kaka japuonj.
12 Nʼchifukwa chake ndikuvutika monga ndililimu. Komabe zimenezi sizikundichititsa manyazi, popeza ndikumudziwa amene ndamukhulupirira ndipo ndikutsimikiza mtima kuti akhoza kusamalira chimene ndinamusungitsa mpaka tsiku lijalo.
Mano emomiyo asandora kama. To wiya ok kuodi, nikech angʼeyo Jal ma aseyie kuome, kendo angʼeyo chutho ni onyalo rito ngimana gi chunya ma asechiwone nyaka ndalo nogono.
13 Zimene unamva kwa ine, uzisunge kuti zikhale chitsanzo cha chiphunzitso choona, mwa chikhulupiriro ndi chikondi mwa Khristu Yesu.
Weche mane iwinjo kuoma, ritgi kaka ranyisi mar puonj maber, kod yie gihera kuom Kristo Yesu.
14 Samalira bwino zokoma zimene anakusungitsa. Uzisamalire mothandizidwa ndi Mzimu Woyera amene amakhala mwa ife.
Rit mwandu maber mosemiyi, kirite gi teko mar Roho Maler modak kuomwa.
15 Iwe udziwa kuti onse a mʼchigawo cha Asiya anandithawa, kuphatikizapo Fugelo ndi Herimogene omwe.
Ingʼeyo ni ji duto ma noa e piny Asia oseweya, koda ka Fugelo gi Hermogene.
16 Mulungu achitire chifundo banja lonse la Onesiforo chifukwa ankandisangalatsa kawirikawiri ndipo sankachita nane manyazi ngakhale ndinali womangidwa ndi maunyolo.
Mad Ruoth Nyasaye okech jood Onesiforo nikech nosiko kokonyo chunya kendo wiye ne ok okuot koda kata kane an e od twech.
17 Mʼmalo mwake, atangofika ku Roma, anandifunafuna ndipo anandipeza.
To kane ochopo Rumi ne omanya matek nyaka nonwangʼa.
18 Ambuye amulole kuti adzalandire chifundo kwa Ambuye pa tsiku lijalo! Ukudziwa bwino momwe iye anandithandizira mʼnjira zosiyanasiyana ku Efeso.
Ingʼeyo maber kaka nokonya e yore mathoth e dala ma e Efeso. Akwayo mondo Ruoth okeche e odiechiengʼno mar Ruoth.

< 2 Timoteyo 1 >