< 2 Timoteyo 1 >

1 Paulo mtumwi wa Khristu Yesu mwa chifuniro cha Mulungu. Anandituma kuti ndilalike za lonjezo la moyo umene uli mwa Khristu Yesu.
अवं पौलुस ई चिट्ठी लिखने लोरोईं। परमेशरे अवं यीशु मसीहेरो प्रेरित भोनेरे लेइ च़ुनो, ताके अवं इस सन्देशेरो प्रचार केरि कि परमेशरे यीशु मसीह पुड़ विश्वास केरनेरे ज़िरिये वादो कियो कि हमेशारी ज़िन्दगी देलो।
2 Kwa Timoteyo, mwana wanga wokondedwa: Chisomo, chifundo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate ndi Ambuye athu Yesu Khristu.
अवं ई चिट्ठी तीमुथियुसे लिखने लोरोईं, ज़ैन मेरे मट्ठेरू ज़ेरूए, हे तीमुथियुस अवं प्रार्थना केरताईं बाजी परमेशर ते इश्शे प्रभु यीशु मसीह तीं अनुग्रह ते दया ते शान्ति देतो राए।
3 Ndikuyamika Mulungu amene ndimamutumikira ndi chikumbumtima chosatsutsika, monga momwe ankachitira makolo anga. Usiku ndi usana ndimakukumbukira mosalekeza mʼmapemphero anga.
ज़ैस परमेशरेरी सेवा अवं अपने दादे पड़दादां केरे रीति पुड़ शुद्ध ज़मीरे सेइं केरताईं, तैसेरू शुक्र भोए, कि अवं एपनी प्रार्थनान मां तीं रात दिहैड़ी याद रखताईं।
4 Ndikamakumbukira misozi yako, ndimalakalaka nditakuona kuti ndidzazidwe ndi chimwemwe.
मीं यादे ज़ैखन अस अलग भोने लोरे थिये तैखन तू केन्च़रे लेरां देने लोरो थियो, ते तीं सेइं मिलनेरी बड़ी इच्छा रखताई कि ज़ैखन मिली त अवं आनन्दे सेइं भरी गेइ।
5 Ndakumbukira za chikhulupiriro chako choona chimene chinayamba mwa agogo ako a Loisi ndi mwa amayi ako Yunike ndipo ndikutsimikiza mtima kuti chilinso mwa iwe.
ते अवं तेरे अम्मा यूनीके ते तेरी नानी लोइसेरो तै सच़्च़े विश्वास याद केरताईं। तेरो विश्वास भी तेरहो आए, ते मीं याकीने तीं मां भी आए।
6 Nʼchifukwa chake ndikukukumbutsa kuti upemerere monga amachitira moto, mphatso imene Mulungu anakupatsa nditakusanjika manja.
एल्हेरेलेइ अवं तीं याद कराताईं, कि तू परमेशरेरे तैस वरदाने ज़ैन मेरे हथ रखने सेइं तीं मैल्लोरू थियूं चमका।
7 Pakuti Mzimu amene Mulungu anatipatsa, si Mzimu wotipatsa manyazi, koma Mzimu wotipatsa mphamvu, chikondi ndi kudzisunga.
किजोकि परमेशर अस डरपोक नईं बनावरे बल्के तैसेरो आत्मा इश्शे दिलन मज़बूत केरते, ते मद्दत केरते कि अस होरि लोकन सेइं प्यार केरम ते ताके आपे कैबू मां रखम।
8 Choncho usachite manyazi kuchitira umboni Ambuye athu, kapena kuchita manyazi chifukwa cha ine wamʼndende. Koma umve nane zowawa chifukwa cha Uthenga Wabwino, mothandizidwa ndi mphamvu za Mulungu.
एल्हेरेलेइ होरि लोकन प्रभु यीशुएरे बारे मां ज़ोने करां शरमा ते एल्हेरेलेइ शरमा कि अवं प्रभुएरी सेवा केरनेरे लेइ कैदे मां आईं। बल्के तू परमेशरेरे तैस शेक्ति इस्तेमाल केर ते मीं सेइं साथी खुशखेबरारे लेइ दुःख झ़लने मां शामिल भो।
9 Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
परमेशरे असन मुक्ति दित्ती, ते अस पवित्र ज़िन्दगी ज़ींनेरे लेइ कुजाए, तैने अस एल्हेरेलेइ नईं कुजवरे कि असेईं रोड़ां कम्मां कियां, किजोकि दुनिया बनाने करां पेइलो परमेशरेरो ई मकसद थियो कि तै यीशु मसीह इश्शे लेइ इस दुनिया मां भेज़तां असन पुड़ अनुग्रह हिराए। (aiōnios g166)
10 Koma tsopano Mulungu watiwululira kudzera mʼkuoneka kwa Mpulumutsi wathu, Khristu Yesu, amene anathetsa mphamvu za imfa ndipo mwa Uthenga Wabwino anaonetsa poyera moyo umene sungafe.
पन हुनी इश्शे मुक्ति देनेबाले यीशु मसीह ओरोए ते तैनी अपनो अनुग्रह हिरावरोए। तैने मौतरी शक्ति नाश की, तैने असन खुशखेबरारे ज़िरिये हमेशारे ज़िन्दगरी बत हिराई।
11 Ine ndinasankhidwa kukhala wamthenga, ndi mtumwi ndi mphunzitsi wa Uthenga Wabwinowu.
इस खुशखेबरारे लेइ परमेशरे अवं प्रचारक ते प्रेरित ते शिक्षा देनेबालो च़ुनो।
12 Nʼchifukwa chake ndikuvutika monga ndililimu. Komabe zimenezi sizikundichititsa manyazi, popeza ndikumudziwa amene ndamukhulupirira ndipo ndikutsimikiza mtima kuti akhoza kusamalira chimene ndinamusungitsa mpaka tsiku lijalo.
एल्हेरेलेइ अवं कैदखाने मां दुःख भी झ़ैल्लने लोरोईं, पन शरमेई न, किजोकि अवं मसीहे ज़ानताईं ज़ैस पुड़ मीं विश्वास कियोरोए, ते मीं याकीने, कि ज़ैन मसीहे दितोरू ज़ांतगर तै वापस न एज्जे तांतगर तै तैसेरी रखवाली केरि बटते।
13 Zimene unamva kwa ine, uzisunge kuti zikhale chitsanzo cha chiphunzitso choona, mwa chikhulupiriro ndi chikondi mwa Khristu Yesu.
ज़ैना रोड़ी शिक्षां तीं मीं करां शुनोरिन तैन तू मिसालरे रूपे मां रख, इन तू विश्वासे ते प्यारे सेइं साथी केर, किजोकि तू मसीह यीशु सेइं साथी अक भोरोस।
14 Samalira bwino zokoma zimene anakusungitsa. Uzisamalire mothandizidwa ndi Mzimu Woyera amene amakhala mwa ife.
ते तैस सच़्च़ेरी रखवाली केर, ज़ैन पवित्र आत्मारे ज़िरिये सेइं तीं सोंफेरू, ज़ै असन मां रहते।
15 Iwe udziwa kuti onse a mʼchigawo cha Asiya anandithawa, kuphatikizapo Fugelo ndi Herimogene omwe.
तू ज़ानतस, कि आसिया इलाकेरे बड़े विश्वासी लोक ज़ैनेईं अवं शारोरोईं, ज़ैन मां फूगिलुस ते हिरमुगिनेसे भी अवं शारो।
16 Mulungu achitire chifundo banja lonse la Onesiforo chifukwa ankandisangalatsa kawirikawiri ndipo sankachita nane manyazi ngakhale ndinali womangidwa ndi maunyolo.
उनेसिफुरूसेरे घराने पुड़ प्रभु दया केरे, किजोकि तै बड़े बार मीं कां अव ते मीं होसलो दित्तो, ते मीं सेइं कैदखाने मां एजनेरे लेइ न शरमाव।
17 Mʼmalo mwake, atangofika ku Roma, anandifunafuna ndipo anandipeza.
पन ज़ैखन तै रोम नगरे मां अव, त बड़े कोशिश सेइं तोप्तां मीं सेइं मुलाकात केरि।
18 Ambuye amulole kuti adzalandire chifundo kwa Ambuye pa tsiku lijalo! Ukudziwa bwino momwe iye anandithandizira mʼnjira zosiyanasiyana ku Efeso.
प्रभु इन्साफेरे दिहाड़े अपनि महान दया उनेसिफुरूसे पुड़ हिराए। तू एप्पू रोड़े च़ारे ज़ानतस कि इफिसुस नगरे मां तैनी मेरी केत्री मद्दत की।

< 2 Timoteyo 1 >