< 2 Timoteyo 4 >
1 Pamaso pa Mulungu ndi pamaso pa Khristu Yesu, amene adzaweruza amoyo ndi akufa omwe pamene adzaonekera ndi ufumu wake, ndikukulamula kuti:
Ngunakunnajila pa meyo ga a Nnungu na a Yeshu Kilishitu, bhaapinga kwaukumulanga bhandunji bhabhakoto na bhawilenje, pene pushibhaishe mu upalume gwabho.
2 Lalikira Mawu; khala wokonzeka pa nthawi yake, ngakhale pamene si pa nthawi yake. Konza zolakwa zawo, dzudzula ndipo limbikitsa moleza mtima kwambiri ndi malangizo osamalitsa.
Nnunguye lyene lilobheli, na nnjime ukoto mobha gowe, gapwaa na ganngapwaa, na nkalipile, na nnimbiye, na mwaaleyanje bhandu nnikwaajiganyanga kwiitimalika.
3 Pakuti idzafika nthawi imene anthu adzakana chiphunzitso choona. Mʼmalo mwake, chifukwa chokhumba kumva zowakomera zokha, adzasonkhanitsa aphunzitsi ambiri omawawuza zimene iwo akufuna kumva.
Pabha shigaishe mobha gushibhakananje majiganyo ga kweli ga gumi, ikabheje shibhakagulilanje ng'aniyo yabhonji, nikwiigumbashiya bhaajiganya bhabhonji bhabhagwinji, nkupinga bhapilikananje indu ikwaanonyelanga.
4 Sadzafuna kumva choona koma adzafuna kumva nthano chabe.
Numbe shibhakananje kupilikanishiya malobhe ga kweli, nitendebhushila ndango ya unami.
5 Koma iwe, khala tcheru nthawi zonse, pirira mʼzovuta, gwira ntchito ya mlaliki, gwira ntchito zonse za utumiki wako.
Ikabheje mmwe ntame nkwiitimalika na indu yowe, mwiipililile mmboteko, nkamule liengo lya lunguya Ngani ja Mmbone, mmalishiye liengo lyenu.
6 Pakuti moyo wanga wayamba kale kuthiridwa ngati nsembe, ndipo nthawi yakwana yoti ndinyamuke ulendo wanga.
Pabha, nnaino nne ngunashoywa mbuti mbepei, malanga gangu gawa gaishile.
7 Ndamenya nkhondo yabwino, ndatsiriza bwino mpikisano wa liwiro ndipo ndasunga chikhulupiriro.
Njikomana ngondo ja mmbone ja ngulupai, mwanja nigumaliye, na njikamulila ukoto ngulupai.
8 Tsopano mphotho yanga ikundidikira imene ndi chipewa cha chilungamo, imene Ambuye, woweruza wolungama, adzandipatsa pa tsiku lijalo, osati ine ndekha komanso onse amene akufunitsitsa kubwera kwake.
Nnaino, njibhishilwa shilemba sha aki shishibhambe Bhakulungwa lyene lyubhalyo, numbe ngabha nne pe nne, ikabheje na bhandu bhowe nkwaapinga bhanalolelanga kuika kwabho.
9 Uyesetse kubwera kuno msanga.
Ntende shangu kwiya akuno.
10 Paja Dema anandisiya chifukwa chokonda dziko lapansi lino, ndipo anapita ku Tesalonika. Kresike anapita ku Galatiya ndipo Tito anapita ku Dalimatiya. (aiōn )
Pabha a Dema ga pinga indu ya pa shilambolyo, bhashineka gubhapite ku Teshalonike, na a Keleshike gubhapite ku Galatia, na a Tito bhapite ku Dalimatia. (aiōn )
11 Ndatsala ndi Luka yekha basi. Mutenge Marko ndipo ubwere naye kuno, chifukwa amandithandiza mu utumiki wanga.
Bhali na nne apano, ni a Luka jikape. Mwaaloleye a Maliko, nnjiye nabho, pabha bhananyanguta mmaengo.
12 Ndatumiza Tukiko ku Efeso.
A Tikiko naatumile ku Epesho.
13 Pobwera, unditengere chofunda pamwamba chimene ndinachisiya kwa Kupro ku Trowa. Unditengerenso mabuku anga, makamaka aja azikopawa.
Pushinnjiyepo nnyigalile likoti lyangu lineshile kwa a Kalipashi bha ku Toloa, nnyigalile na itabhu, na kaje ya mapende ila.
14 Alekisandro, mmisiri wa zitsulo anandichitira zoyipa kwambiri. Ambuye adzamubwezera pa zimene anachita.
A Alekishanda bha yana itale bhala, bhashindendela ya nyata yaigwinji, Bhakulungwa shibhaalipe kwa itendi yabho.
15 Iwenso ukhale naye tcheru chifukwa anatsutsa kwambiri uthenga wathu.
Na mmwe mwiiteije na bhenebho, pabha bhashinkutauka kwa puya malobhe getu.
16 Podziteteza koyamba pa mlandu wanga, panalibe ndi mmodzi yemwe amene anandithandiza, koma aliyense anandithawa. Mulungu awakhululukire.
Punaibheleketelaga malobhe ga kwiitapula gwa ntai, jwakwa mundu ajimi na nne kunyangutila, ikabhe bhowe bhashinkunekanga, nne ngunakwaajujilanga kwa a Nnungu bhaleshelelwanje, na bhanabhonekanje kulebha kwa genego!
17 Koma Ambuye anayima nane limodzi, ndipo anandipatsa mphamvu, kuti kudzera mwa ine, uthenga ulalikidwe kwambiri, ndikuti anthu a mitundu ina amve. Ndipo ndinalanditsidwa mʼkamwa mwa mkango.
Ikabheje Bhakulungwa gubhajimi na nne, nigubhambele mashili, nkupinga nunguye ntenga gula ukoto, nkali ku bhandu bha ilambo ina, na nne gundapwilwe nshiwo, mbuti ngutapulwa nkang'wa ja imba.
18 Ambuye adzandilanditsa ku chilichonse chofuna kundichita choyipa ndipo adzandisamalira bwino mpaka kundilowetsa chonse mu ufumu wake wakumwamba. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya. (aiōn )
Bhakulungwa shibhandapule na indu yowe ya nyata, shibhandole ng'ishe ku Upalume gwabho gwa ku nnungu. Ukonjelo ni gwabho pitipiti! Amina. (aiōn )
19 Pereka moni kwa Prisila ndi Akura pamodzi ndi banja lonse la Onesiforo.
Mwaalamushilanje a Pilishika na a Akula na bhandunji bha munngwabho a Oneshipolashi.
20 Erasto anatsalira ku Korinto. Trofimo ndinamusiya akudwala ku Mileto.
A Elashito kubhatama ku Kolinto, na a Tolopimo kunaaleshile ku Mileto, bhalwele.
21 Uyesetse kubwera kuno nthawi yozizira isanafike. Eubulo akupereka moni, ndiponso Pude, Lino, Klaudiya ndi abale onse nawonso akupereka moni.
Ntende shangu kwiya akuno, gakanabhe ishila mobha ga mmbepo. A Ebhulo bhanakunnamushilanga, na a Pudenishi na a Linushi, na a Kilaudia, na Bhakilishitu bhowe.
22 Ambuye akhale ndi mzimu wako. Chisomo chikhale ndi inu nonse.
Bhakulungwa bhatame muntima gwenu. Nema jitame na mmanganyanji mmowe.