< 2 Timoteyo 1 >

1 Paulo mtumwi wa Khristu Yesu mwa chifuniro cha Mulungu. Anandituma kuti ndilalike za lonjezo la moyo umene uli mwa Khristu Yesu.
Paulo muutung'wa nuang'wa Yesu Kilisto anga Itunda nuloilwe, uulukulu anga ilago nilaupanga nuukole mukati ang'wa Yesu Kilisto.
2 Kwa Timoteyo, mwana wanga wokondedwa: Chisomo, chifundo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate ndi Ambuye athu Yesu Khristu.
Kung'wa Timoteo ung'wana numuloilwe: Nekanda, nuukende nuupolo kupuma kung'wi Tunda Tata nu Yesu Kilisto Mkulu witu.
3 Ndikuyamika Mulungu amene ndimamutumikira ndi chikumbumtima chosatsutsika, monga momwe ankachitira makolo anga. Usiku ndi usana ndimakukumbukira mosalekeza mʼmapemphero anga.
Numusongeeye Itunda, uyu nikumitumela kisigo niza anga uu naeatendile iatata ane, ange nkimbuke ninkole mumalompi ane. Utiku nu
4 Ndikamakumbukira misozi yako, ndimalakalaka nditakuona kuti ndidzazidwe ndi chimwemwe.
mung'wi nkete nsula akuuona, inge gwa wizule uulowa. Nulukimbukile uliholi lako.
5 Ndakumbukira za chikhulupiriro chako choona chimene chinayamba mwa agogo ako a Loisi ndi mwa amayi ako Yunike ndipo ndikutsimikiza mtima kuti chilinso mwa iwe.
Aenekeze kimbushigwa uuhueli wako nueli, apo naeng'wandyo aikie kung'wa nyukulu nuako u Loisi nuia nuako u Yunisi. Hange ngila itai kina uhueli nuanso wikie mukati ako gwa.
6 Nʼchifukwa chake ndikukukumbutsa kuti upemerere monga amachitira moto, mphatso imene Mulungu anakupatsa nditakusanjika manja.
Iye inge nsoko nakukimbusha kukiusha ekipegwa kang'wi Tunda nikikole mukati ako kunzila akuekiiligwa imekono nane.
7 Pakuti Mzimu amene Mulungu anatipatsa, si Mzimu wotipatsa manyazi, koma Mzimu wotipatsa mphamvu, chikondi ndi kudzisunga.
Kunsoko Itunda singukupee inkolo nawoa, inge angulu nuulowa nikulyo.
8 Choncho usachite manyazi kuchitira umboni Ambuye athu, kapena kuchita manyazi chifukwa cha ine wamʼndende. Koma umve nane zowawa chifukwa cha Uthenga Wabwino, mothandizidwa ndi mphamvu za Mulungu.
Kuite ulekekuonela iminyala nua Mukulu witu, sunga ganuwu nuane unene Paulo mutungwa nuakwe. Inge utule palung'wi mulwago kunsoko autananti uu lukulu angauhumi wang'wi Tunda.
9 Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
Inge Itunda aukugunile nukuitanga uitangi nuutakatifu. Shanga aewitumile itensoko amelimo itu inge angaukende nuunonelya wakwe nuanso. Aukupee imakani aya mung'wa Kilisto Yesu aeakili imatungo kanza. (aiōnios g166)
10 Koma tsopano Mulungu watiwululira kudzera mʼkuoneka kwa Mpulumutsi wathu, Khristu Yesu, amene anathetsa mphamvu za imfa ndipo mwa Uthenga Wabwino anaonetsa poyera moyo umene sungafe.
Kuite itungo ele uguni nuang'wi Tunda wakunukulwe kiza kumuguni witu u Yesu Kilisto. Ukilisto wikamipelwe insha nukuleta uupanga nisiga ukupela kuwelu nuankani niza.
11 Ine ndinasankhidwa kukhala wamthenga, ndi mtumwi ndi mphunzitsi wa Uthenga Wabwinowu.
Kunsoko yiyi nikabagulwa kulula nimutananti, mutumi hange nemumanyisi.
12 Nʼchifukwa chake ndikuvutika monga ndililimu. Komabe zimenezi sizikundichititsa manyazi, popeza ndikumudziwa amene ndamukhulupirira ndipo ndikutsimikiza mtima kuti akhoza kusamalira chimene ndinamusungitsa mpaka tsiku lijalo.
Kunsoko yiyi kaga gwa, kuite singa minyala soko numulengile ninamukuela. Nkete itai kina nuanso ukumile kukigoza iki nenakiika kung'waakwe sunga uluhiku lulo.
13 Zimene unamva kwa ine, uzisunge kuti zikhale chitsanzo cha chiphunzitso choona, mwa chikhulupiriro ndi chikondi mwa Khristu Yesu.
Ukimbuke umufano nualukani nulauhueli naewigule kupuma kung'waane, palung'wi nuuhueli nuulowa nuukole mukati ang'wa Yesu Kilisto.
14 Samalira bwino zokoma zimene anakusungitsa. Uzisamalire mothandizidwa ndi Mzimu Woyera amene amakhala mwa ife.
Magoze imakani nimaza naeukupee Itunda kukiila ung'waung'welu nuikie mukali itu.
15 Iwe udziwa kuti onse a mʼchigawo cha Asiya anandithawa, kuphatikizapo Fugelo ndi Herimogene omwe.
Ulengile kina, neikie mu Asia aeanalekile’ Mumbi ele akole ia Figelo nia Hemogene.
16 Mulungu achitire chifundo banja lonse la Onesiforo chifukwa ankandisangalatsa kawirikawiri ndipo sankachita nane manyazi ngakhale ndinali womangidwa ndi maunyolo.
Umukulu walisamile ito lang'wa Onesiforo kunsoko nkua yedu aundoeye hangi shangaaunionee iminyala ekitungo kane.
17 Mʼmalo mwake, atangofika ku Roma, anandifunafuna ndipo anandipeza.
Kuleka gwa iti, naukole ku Roma aundumile kungulu hange wikandija.
18 Ambuye amulole kuti adzalandire chifundo kwa Ambuye pa tsiku lijalo! Ukudziwa bwino momwe iye anandithandizira mʼnjira zosiyanasiyana ku Efeso.
Itunda nuamujalie kumupa ukende kupuma kung'waakwe uluhiku nutanso. Anga naunzaiye naenkole ku Efeso uwe ulengile iza.

< 2 Timoteyo 1 >