< 2 Atesalonika 2 >
1 Pa za kubweranso kwa Ambuye athu Yesu Khristu ndiponso za kusonkhana kwathu kuti tikumane naye, abale, tikukupemphani
Mayelana lokuza kweNkosi yethu uJesu Khristu lokubuthana kwethu kuyo, siyalicela bazalwane
2 kuti musagwedezeke msanga mʼmaganizo kapena kuopsezedwa ndi uneneri, mbiri kapena kalata yokhala ngati yachokera kwa ife, yonena kuti tsiku lija la Ambuye linafika kale.
ukuthi lingaphangi likhathazeke kumbe lethuswe ngeyinye imfundiso loba isiphrofethi kumbe ilizwi eliphuma emlonyeni loba incwadi okungathiwa ivela kithi kuthiwa usuku lweNkosi selufikile.
3 Musalole kuti wina aliyense akunamizeni mwa njira ina iliyonse. Pakuti tsikulo lisanafike, kudzakhala mpatuko waukulu kwambiri, ndipo kudzaoneka munthu woyipitsitsa uja, munthu woyenera kuwonongedwayo.
Lingavumeli muntu elikhohlisa langayiphi indlela ngoba lolosuku kaluyikufika umvukela uze wenzakale, lomuntu ongelamthetho abonakaliswe yena omiselwe ukubhujiswa.
4 Iyeyo adzatsutsa ndi kudziyika pamwamba pa chilichonse chimene anthu amachitcha mulungu kapena amachipembedza. Iyeyo adzadzikhazika mʼNyumba ya Mulungu ndi kudzitcha Mulungu.
Uzaphikisa, azikhukhumeze ezintweni zonke ezibiza uNkulunkulu loba ezikhonzwayo, aze azihlalise ethempelini likaNkulunkulu, amemezele ukuthi yena unguNkulunkulu.
5 Kodi simukukumbukira kuti pamene ndinali nanu pamodzi ndinkakuwuzani zimenezi?
Kalisakhumbuli yini ukuthi ngisesekini ngangijayele ukulitshela izinto lezi?
6 Ndipo tsopano mukudziwa chimene chikumuletsa kuonekera, koma adzawululika pa nthawi yake yoyenera.
Khathesi selikwazi okumvimbelayo ukuze abonakaliswe ngesikhathi esifaneleyo.
7 Pakuti mphamvu yobisika yoyipitsitsa ikugwira ntchito ngakhale tsopano; koma amene akutchinga mphamvuyo adzapitiriza kutero mpaka pamene wotchingayo adzachotsedwe.
Ngoba amandla afihlakeleyo okungabi lamthetho asesebenza kodwa lowo owavimbelayo khathesi uzaqhubeka esenza njalo aze asuswe endleleni.
8 Ndipo kenaka woyipitsitsayo adzaonekera, amene Ambuye Yesu adzamugonjetsa ndi mpweya otuluka mʼkamwa mwake ndi kumuwononga ndi ulemerero wa kubwera kwake.
Lapho-ke, lowo ongelamthetho uzabonakaliswa, lowo iNkosi uJesu ezamchitha ngomoya womlomo wayo, imqede ngenkazimulo yokufika kwayo.
9 Woyipitsitsayo adzabwera ndi mphamvu za Satana. Adzaonetsa mphamvu zake pochita zizindikiro ndi zodabwitsa zachinyengo.
Ukufika kwalowo ongelamthetho kuzakuya ngendlela yemisebenzi kaSathane. Uzasebenzisa inhlobo zonke zokubonakalisa amandla ngezibonakaliso lezimanga zamanga
10 Iye adzagwiritsa ntchito mtundu uliwonse wachinyengo kupusitsa amene akuwonongeka. Iwo akuwonongeka chifukwa akukana kukonda choonadi ndi kuti apulumutsidwe.
kanye lezinhlobo zonke zobubi obukhohlisa ababhubhayo. Babhubha ngoba bala ukuthanda iqiniso ukuba basindiswe.
11 Chifukwa cha chimenechi, Mulungu akuwatumizira chinyengo chachikulu kuti akhulupirire bodza.
Ngenxa yalokhu, uNkulunkulu ubehlisela inkohliso elamandla ukuba bakholwe amanga
12 Choncho adzalangidwa onse amene sanakhulupirire choonadi, koma anakondwera mu zoyipa.
ukuze balahlwe bonke abangalikholwanga iqiniso kodwa bathokoziswa yibubi.
13 Koma tiyenera kuyamika Mulungu chifukwa cha inu abale okondedwa mwa Ambuye, pakuti Mulungu anakusankhani pachiyambi pomwe kuti mupulumuke chifukwa cha ntchito yoyeretsa ya Mzimu ndi chikhulupiriro chanu mʼchoonadi.
Kodwa kufanele sibonge uNkulunkulu kokuphela ngenxa yenu, bazalwane abathandwa yiNkosi, ngoba uNkulunkulu walikhetha kusukela ekuqaleni ukuba lisindiswe ngomsebenzi ongcwele kaMoya langokukholwa eqinisweni.
14 Iye anakuyitanirani zimenezi kudzera mwa uthenga wathu wabwino, kuti mulandire nawo ulemerero wa Ambuye athu Yesu Khristu.
Walibizela kulokhu ngevangeli lethu ukuze lihlanganyele enkazimulweni yeNkosi yethu uJesu Khristu.
15 Kotero tsono, abale, imani mwamphamvu ndi kugwiritsa ziphunzitso zimene tinakupatsani kudzera mʼmawu apakamwa kapena kudzera mʼkalata.
Ngakho-ke bazalwane, qinani libambelele ezifundweni esalinika zona, kungaba ngelizwi lomlomo loba ngencwadi.
16 Ambuye athu Yesu Khristu mwini ndi Mulungu Atate wathu, amene anatikonda ife ndipo mwachisomo chake anatipatsa kulimba mtima kwamuyaya ndi chiyembekezo chabwino, (aiōnios )
Sengathi iNkosi yethu uJesu Khristu uqobo kanye loNkulunkulu uBaba owasithandayo kwathi ngomusa wakhe wasinika induduzo engapheliyo lethemba elihle (aiōnios )
17 akulimbikitseni ndi kukupatsani mphamvu yogwirira ntchito ndi kuyankhula zabwino zilizonse.
angakhuthaza inhliziyo zenu njalo aliqinise kuzozonke izenzo ezinhle lasemazwini amahle.