< 2 Atesalonika 1 >

1 Paulo, Silivano ndi Timoteyo. Kulembera mpingo wa ku Tesalonika, umene uli mwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu.
Neni Paulu na Silwanu na Timotewu twankuwalembelera shipinga sha wantu yawamjimira Yesu aku Tesaloniki, wantu yawawera wa Mlungu yakawera Tati gwetu na Mtuwa gwetu Yesu Kristu.
2 Chisomo ndi mtendere kwa inu kuchokera kwa Mulungu Atate ndi Ambuye Yesu Khristu.
Manemu na ponga ya Mlungu Tati gwetu na ga Mtuwa Yesu Kristu, gaweri pamuhera na mwenga.
3 Ife tiyenera kuyamika Mulungu nthawi zonse chifukwa cha inu abale. Ndipo tiyenera kutero chifukwa chikhulupiriro chanu chikukulirakulirabe, ndiponso chikondi chimene aliyense wa inu ali nacho pa mnzake chikuchulukirachulukirabe.
Walongu wayetu, tufiruwa kulonga mayagashii Mlungu mashaka goseri toziya ya mwenga, toziya njimiru yenu yongereka nentu na kulifira maweni kwankwongereka.
4 Nʼchifukwa chake, timayankhula monyadira mʼmipingo yonse ya Mulungu za kupirira kwanu ndi chikhulupiriro chanu pakati pa masautso onse ndi mayesero amene mukudutsamo.
Ndo mana twenga tulitumbira mwenga muvipinga vya wantu wa Mlungu yawamjimira Kristu, ntambu yamwendereya kujimira muntabika zyenu zoseri na mumagaziwu gampata.
5 Zonsezi zikutsimikiza kuti Mulungu amaweruza molungama. Zotsatira zake ndi zakuti mudzatengedwa kukhala oyenera kulowa mu ufumu wa Mulungu umene mukuwuvutikira.
Goseri aga gankulanguziya utoza yaukamilika wa Mlungu, su mwenga hamuweri na unakaka Muufalumi wa Mlungu, ndoweni kwa toziya yakuwi mwankutabika.
6 Mulungu ndi wolungama ndipo adzalanga amene amakusautsaniwo
Mlungu hakatendi shitwatira shiheri kulongolu kwakuwi, hakawawuziliri ntabika walii yawawatabisiya mwenga.
7 ndikukupatsani mpumulo amene mukusautsidwa, pamodzi ndi ifenso. Izi zidzachitika Ambuye Yesu akadzaoneka mʼmalawi amoto kuchokera kumwamba pamodzi ndi angelo ake amphamvu.
Na hakatupanani kwoyera twenga pamuhera na mwenga wantu yatugazika, shipindi Mtuwa Yesu pakaliwonisiya kumpindi kwa Mlungu pamuhera na wantumintumi wa kumpindi yawawera na makakala,
8 Iye adzalanga amene sadziwa Mulungu ndi amene samvera Uthenga Wabwino wa Ambuye athu Yesu.
hakawatozi kwa kuwayasa mumbamba zya motu wantu woseri walii yawamlemiti Mlungu na walii yakashijimira ndiri Shisoweru Shiwagira sha Mtuwa Yesu.
9 Adzalangidwa ndi chiwonongeko chamuyaya ndipo sadzaonanso nkhope ya Ambuye ndi ulemerero wamphamvu zake (aiōnios g166)
Womberi hawatabiki muntabika ya mashaka goseri na kutulwa gweka kutali na ukwisa wakuwi mkulu, (aiōnios g166)
10 pa tsiku limene iye adzabwera kudzalemekezedwa mwa oyera mtima ndi kuyamikidwa ndi onse amene anakhulupirira. Inu mudzakhala nawo mʼgulumo chifukwa munakhulupirira umboni wathu.
yomberi pakiza mulishaka lilii kuwanka ukwisa kwa wantu wakuwi wananagala na ligoya kulawa kwa woseri yawajimira. Mwenga viraa hamuweri wamwawu, toziya mjimira ujumbi ulii yatuwajegiriti.
11 Nʼchifukwa chake timakupemphererani nthawi zonse, kuti Mulungu wathu akusandutseni oyenera mayitanidwe ake, ndi kuti mwa mphamvu zake akwaniritse cholinga chanu chilichonse chabwino ndi chilichonse chochitika mwachikhulupiriro.
Su twenga tuwaluwirani kwa Mlungu mashaka goseri, tumluwa Mlungu gwetu kawatendi makaliru gakawatenditi mlikali. Na kawamemiziyi makakala gakuwi gatendi nfiru ya mwenga ya kutenda maheri na kumalira lihengu lyenu lya njimiru.
12 Ife timapempherera zimenezi kuti dzina la Ambuye athu Yesu lilemekezedwe mwa inu, ndi inu mulemekezedwe mwa Iyeyo. Zonsezi zidzachitika chifukwa cha chisomo cha Mulungu wathu ndi Ambuye Yesu Khristu.
Twankuluwa hangu su litawu lya Mtuwa gwetu Yesu Kristu halikwiswi mngati mwenu, na mwenga mupati ukwisa kwa kuwera pamuhera nayomberi kulawirana na manemu ga Mlungu na Mtuwa gwetu Yesu Kristu.

< 2 Atesalonika 1 >