< 2 Samueli 1 >

1 Atamwalira Sauli, Davide anabwerako kumene anakagonjetsa Aamaleki ndipo anakakhala ku Zikilagi masiku awiri.
Solo da bogoloba, Da: ibidi da A: malege fi dunu ilima hasalasilalu, Sigela: ge moilai bai bagadega buhagili, eso aduna esalu.
2 Pa tsiku lachitatu munthu wina wochokera ku msasa wa Sauli anafika, zovala zake zitangʼambika ndiponso anali atathira dothi pamutu pake. Atafika kwa Davide, anadzigwetsa pansi, kupereka ulemu kwa Davideyo.
Amalalu, diahabe goi ayeligi afae da Solo ea fisisu awali diasu amoganini manebe ba: i. Ea da: i dioi dawa: digima: ne, e abula gadelale amola e da osobo ea dialuma da: iya duduli gala: i ba: i. E da Da: ibidima misini, ema nodone dawa: digima: ne osoboga beguduli diasa: i.
3 Davide anamufunsa iye kuti, “Kodi iwe wachokera kuti?” Iye anayankha kuti, “Ine ndathawa ku misasa ya Aisraeli.”
Da: ibidi da ema amane adole ba: i, “Di da habogainini misibala: ?” Ayeligi da bu adole i, “Na da Isala: ili ilia ha wa: i fisisu amoganini hobeale misi.”
4 Davide anafunsa, “Tandiwuza, chachitika ndi chiyani?” Iye anati, “Anthu athawa ku nkhondo ndipo ambiri aphedwa. Sauli ndi mwana wake Yonatani aphedwa.”
Da: ibidi da amane sia: i, “Di da gegei amo hou huluane nama adodole ima.” Ayeligi dunu da amane sia: i, “Ninia dadi gagui dunu da huluane gegesu amoba: le hobeale asi dagoi. Amaiba: le, ninia dunu da bagohame bogogia: i dagoi. Solo amola ea mano Yonada: ne da elegalu bogoi dagoi.”
5 Ndipo Davide anati kwa mnyamata amene anabweretsa nkhaniyi, “Ukudziwa bwanji kuti Sauli ndi mwana wake Yonatani afa?”
Da: ibidi da ema adole ba: i, “Di da Solo amola Yonada: ne ela bogoi da habodane dawa: bela: ?”
6 Mnyamatayo anati, “Zinangochitika kuti ndinali pa phiri la Gilibowa, ndipo Sauli anali komweko ataweramira pa mkondo wake, pamodzi ndi magaleta ndi okwera ake atamuyandikira.
Ayeligi da bu adole i, “Na da Giliboua agolo amo da: iya lela ba: i, Solo da ea gogega udidili lelebe ba: i, amola ha lai dunu ilia sa: liode, amola dunu ilia da hosi da: iya fila heda: i amola da gagadenena ahoanebe ba: i.
7 Pamene anatembenuka ndi kundiona ine, iye anandiyitana, ndipo ndinati, ‘Kodi ndichite chiyani?’”
Amalu Solo da beba: loba, na ba: beba: le, e da nama wele sia: i. Na da bu ema adole i `Wae! Ada!’
8 Iye anandifunsa, “Iwe ndiwe yani?” Ine ndinayankha kuti, “Ndine Mwamaleki.”
E da na nowayale naba ba: i. Na da bu adole i, `Na da A: malege dunu.’
9 “Kenaka iye anati kwa ine, ‘Bwera pafupi ndipo undiphe! Ndikumva ululu kwambiri, koma ndikanali ndi moyo!’
Amalu e da amane sia: i, `Di da guiguda: misini, na fane legema! Na da baligiliwane fane odahida: iba: le, na da bogomu gadenei esala.’
10 “Kotero ndinabwera pafupi ndi kumupha, chifukwa ndinadziwa kuti mmene anagweramo sakanakhalanso ndi moyo. Ndipo ndatenga chipewa chaufumu chimene chinali pamutu pake ndi khoza la pa dzanja lake ndipo ndazibweretsa kwa inu mbuye wanga.”
Amaiba: le, na da ema gadenena heda: le, e fane legei dagoi. Bai na dawa: loba ea bogomu asigi dawa: su amo gisigisia, bogomu agoane ba: i. Amanoba na da ea dialuma da: iya habuga amola ea lobofasele fei huluane lale, dima gaguli misi wea!”
11 Apo Davide ndi anthu onse amene anali nawo anangʼamba zovala zawo.
Da: ibidi da da: i dione fofagiba: le, ea abula huluane gagadelai. Amola ea fi dunu ilia da amo defele ilila: abula gagadelai.
12 Iwo analira maliro ndi kusala zakudya mpaka madzulo chifukwa cha Sauli ndi mwana wake Yonatani, komanso chifukwa cha gulu la ankhondo la Yehova ndi nyumba ya Israeli, chifukwa anaphedwa ndi lupanga.
Ilia da Hina Gode Ea fi Isala: ili dunu bagohame amola Solo amola Yonada: ne ilia da bogogia: i amo dawa: beba: le, ilia da ha: i mae nawane didigia: lala soge gasi.
13 Davide anati kwa mnyamata amene anabweretsa uthengawo, “Iwe umachokera kuti?” Iye anayankha kuti, “Ine ndine mwana wa mlendo Mwamaleki.”
Da: ibidi da amo sia: gaguli misi ayeligi ema adole ba: i, “Di da nowa fi dunula: ?” E da bu adole i, “Na da A: malege fi dunu, be amomane na da soge dia ouligi amo ganodini esala.”
14 Davide anamufunsanso kuti, “Nʼchifukwa chiyani sunaope kukweza dzanja lako ndi kupha wodzozedwa wa Yehova?”
Da: ibidi da ema amane adole ba: i, “Abuliba: le di da Hina Gode Ea ilegei Hina bagade amo fane legemu amo hame beda: bela: ?”
15 Kenaka Davide anayitana mmodzi mwa anyamata ake ndipo anati, “Pita ukamukanthe!” Kotero iye anapita kukamukantha, ndipo mnyamata uja anafa.
Amalu, Da: ibidi da ea dunu afae misa: ne sia: i, amalu ema amane sia: i, “Goe dunu fane legema!” Amabeba: le, e da amo ayeligi fane legei dagoi.
16 Pakuti Davide anali atanena kwa iye kuti, “Iwe wadzipha wekha. Pakamwa pako pakunena zokutsutsa wekha, pamene unanena kuti, ‘Ine ndapha wodzozedwa wa Yehova.’”
Amola Da: ibidi da A: malege dunu bogolala amo ba: lu, e da amane sia: i, “Di bogoma: ne di fawane olela misi dagoi. Di da Hina Gode Ea ilegei hina bagade amo dia fane legei sia: i dagoiba: le, di fawane da dima bogoma: ne fofada: i dagoi.”
17 Davide anayimba nyimbo iyi ya maliro, kulira Sauli ndi mwana wake Yonatani.
Da: ibidi da Solo amola egefe Yonada: ne elama asigili, goe fofagini disu gesami hea: i.
18 Ndipo analamula kuti anthu a ku Yuda aphunzitsidwe nyimbo ya maliroyi imene yalembedwa mʼbuku la Yasari:
Amola Da: ibidi da amo gesami ilia da Yuda dunu fi huluane ilima olelema: ne sia: i. (Amo gesami da Ya: isia Buga ganodini dialoma: ne dedene legei.)
19 “Ulemerero wako iwe Israeli, wagona utaphedwa ku zitunda. Taonani amphamvu agwa kumeneko!
“Isala: ili agolo amo da: iya ninia ouligisu dunu da bogogia: i dagoi. Ninia gasa bagadedafa dadi gagui dunu bagohame da amogai dafane bogoi dagoi.
20 “Musakanene zimenezi ku Gati, musazilengeze ku misewu ya ku Asikeloni, kuti ana aakazi a Afilisti angasangalale, ana aakazi a osachita mdulidwe angakondwere.
Ga: de moilai bai bagadega amola Asegelone logoga maedafa adole gama. Filisidini uda ilia hahawane nodosa: besa: le, mae adole gama. Wadela: i fi ilia idiwi ilia gadele osa: besa: le, mae sia: ma.
21 “Inu mapiri a ku Gilibowa, musakhalenso ndi mame kapena mvula, kapena minda yobereka zopereka za ufa. Pakuti kumeneko chishango cha munthu wamphamvu chinadetsedwa, chishango cha Sauli sanachipakenso mafuta.
Giliboua agolo amoga da gibu amola oubi mogele hamedafa sa: imu da defea. Giliboua bugili nasu soge amoga ha: i manu hamedafa heda: mu da defea. Ninia gasa bagade dadi gagui dunu ilia ibidigi da ilia gogosiasu olelema: ne amogai diafula. Be Solo ea ibidigi da doga: le susuligi amoga legesu, be wali da hame legesa.
22 “Pa magazi a ophedwa, pa mnofu wa amphamvu, uta wa Yonatani sunabwerere, lupanga la Sauli silinabwere chabe.
Yonada: ne ea dadi da giolasi galu. Be Solo ea gegesu gobihei sedadega mae dawa: le, buluduli fane legele, maga: me bususu dawa: i.
23 “Sauli ndi Yonatani, pa moyo wawo anali okondedwa ndi okoma mtima, ndipo pa imfa yawo sanasiyanitsidwe. Iwo anali ndi liwiro loposa ziwombankhanga, anali ndi mphamvu zoposa mkango.
Solo amola Yonada: ne ela da noga: idafa amola hahawanedafa galu. Ele galu esalu, amola ele galu bogoi. Ela da buhiba ea hagili ahoasu baligi, amola elea gasa da laione wa: me ea gasa baligi dagoi.
24 “Inu ana aakazi a Israeli, mulireni Sauli, amene anakuvekani zovala zofiira ndi zofewa, amene anakometsera zovala zanu ndi zokometsera zagolide.
Dilia Isala: ili uda! Dilia huluane Soloma asigiba: le dadawa: loma. E da dilima abula yoi noga: idafa dilima ga: ma: ne i. Amola e da dili nina: hamoma: ne, gouli amola igi ida: iwane dilima iasu.
25 “Taonani amphamvu agwa ku nkhondo! Yonatani wagona ataphedwa ku zitunda.
Ninia gesa: i dadi gagui dunu ilia da dafane bogogia: i. Ilia da gegenana bogogia: i. Yonada: ne da agolo amoga dafane bogoi diala.
26 Ine ndikuvutika mumtima chifukwa cha iwe mʼbale wanga Yonatani, unali wokondedwa kwambiri kwa ine. Chikondi chako pa ine chinali chopambana, chopambana kuposa chikondi cha akazi.
Naeya Yonada: ne! Na da diha fofagini disa. Di da na dogolegeidafa galu. Amola di da nama dogolegeidafa galu. Dia nama dogolegesu hou da udama magedasu hou amo da baligili ba: su.
27 “Taonani amphamvu agwa! Zida zankhondo zawonongeka!”
Gesa: i dadi gagui da dafane bogoi dagoi. Ilia gegesu liligi da udigili fisili, gugunufinisi dagoi ba: sa.”

< 2 Samueli 1 >