< 2 Samueli 4 >

1 Isiboseti mwana wa Sauli atamva kuti Abineri waphedwa ku Hebroni, anataya mtima ndipo Aisraeli onse anachita mantha kwambiri.
Şaulne duxayk'le İşboşetık'le, Avner Xevron eyhene şaharee gik'uva ats'axhxhamee, mang'us zeze ooxha. İzrailin milletıd man g'ayxhı qəyq'ən giyğal.
2 Koma Isiboseti anali ndi anthu akuluakulu awiri amene ankatsogolera magulu a ankhondo. Mmodzi mwa iwo dzina lake linali Baana ndipo mnzakeyo anali Rekabu. Iwo anali ana a Rimoni wa banja la Beeroti wa fuko la Benjamini Beeroti. Iwo ankatengedwa ngati mbali imodzi ya Benjamini,
Şaulne duxayqa İşboşetıqa q'öyre cune destebışda xərna ıxha. Manbı Benyaminaaşinbı vooxhene Beerotğançene Rimmonun dixbı vuxha. Manbışde sang'un do Baana, mansang'unud Rexav ıxha. Beerot vucub Benyaminaaşinacab vuxha.
3 chifukwa anthu a ku Beeroti anathawira ku Gitaimu ndipo akhala ali kumeneko ngati alendo mpaka lero lino.
Beerotbı Gittayimeeqa heepxı qabı vuxha, g'iyniyne yiğılqameeyib manbı maa'ab menne cigaynbı xhinne aaxva.
4 (Yonatani mwana wa Sauli anali ndi mwana wamwamuna amene anali wolumala mapazi ake onse awiri. Iye anali ndi zaka zisanu pamene nkhani ya Sauli ndi Yonatani inamveka kuchokera ku Yezireeli. Amene amamulera anamunyamula ndi kuthawa naye, koma pamene amachita zinthu mofulumira mwanayo anagwa ndipo analumala. Dzina lake linali Mefiboseti).
(Şaulne duxayqa Yonatanıqa q'öyudsana g'el k'aana Mefiboşet donana dix ıxha. İzre'elyğançe Şaulıy Yonatan gyapt'ıva xabar qabımee, mang'uqa xholle sen ıxha. Mane k'ıning'uqa ileekang'vee mana mançe alyart'u, zaara heexvava, gade xılençe g'a'araççe mang'un g'elybı hayq'var.)
5 Choncho Rekabu ndi Baana ana a Rimoni wa ku Beeroti ananyamuka kupita ku nyumba ya Isi-Boseti, ndipo anafika nthawi ya masana kukutentha pamene iye amapumula.
İşboşetee yı'q'ı'hna manzil haa'amee, Beerotğançene Rimmonun dixbı Rexaviy Baana yəqqı'l gyabak'va. Manbı pırane gahıl qabı mang'une xaasqa hiviyxhar.
6 Iwo analowa mʼchipinda chamʼkati ngati kuti amakatenga tirigu, ndipo anamulasa mʼmimba. Kenaka Rekabu ndi mʼbale wake Baana anathawa.
İşboşet cune gozee tyulee g'alirxhu eyxhe. Rexaviy cuna çoc Baana suk alyabat'anbı xhinnee xaaqa ikkeepç'ı, mang'une vuxneeqa xincal hi'yxə. Qiyğab vuk'ul g'ats'pk'ın, vucub alyapt'ı, mançe heebaxanbı. Xəmvolle manbı Arava eyhene qadaalyne yəqqı'le k'ena avayk'ananbı.
7 Iwo analowa mʼnyumbamo iye akugona pa bedi mʼchipinda chake. Atamulasa ndi kumupha, anadula mutu wake nʼkuwutenga, nayenda usiku wonse mʼnjira yopita ku Araba.
8 Iwo anabweretsa mutu wa Isi-Boseti kwa Davide ku Hebroni ndipo anati kwa mfumu, “Nawu mutu wa Isiboseti mwana wa Sauli, mdani wanu, amene anafuna kukuphani. Lero lino Yehova wabwezera mbuye wanga mfumu adani anu, Sauli ndi ana ake.”
İşboşetna vuk'ul manbışe Xevroneeqa Davudne k'anyaqa abı, paççahık'le eyhen: – İna Şaulne yiğne duşmanna duxayna İşboşetna vuk'ul vob. Mane Şaulısniy ğu gik'as ıkkan. G'iyna Rəbbee, yişde xərıng'ul – paççahıl-alla Şaulukeyiy cune nasılıke in hı'ı, qəl qığavhu.
9 Davide anayankha Rekabu ndi mʼbale wake Baana, ana a Rimoni wa ku Beeroti kuti, “Pali Yehova wamoyo, amene wandipulumutsa ku mavuto anga onse,
Davudee Beerotğançene Rimmonne dixbışis Rexavısiy cune çocus Baanays inəxdın alidghıniy qele: – Zı Tsiklageenang'a culygena ixheene zas yugna xabar ana insanniy arı: «Şaul qik'unava». Zı mançil-allar mana aqqı gik'as alikkı. Mang'vee zas abıyne xabarın mukaafat mang'us man ıxha. Həşde karaı'dəən insanar qopkune insanne xaaqa ikkeepç'ı, mana cune tyulee gik'uyng'a, şosqa nəxüdiy qöö, zı mang'una eb ç'iyel g'alepçı, manbı ç'iyene aq'val gidyapt'ı g'alyaa'aye? Zı gırgınçike g'attixhan ha'ane Vorne Rəbbilqan k'ın ixhen məxdın kar ixhes deş!
10 pamene munthu wina anandiwuza kuti, ‘Sauli wafa’ ndipo ankaganiza kuti wabweretsa nkhani yabwino, ine ndinamugwira ndi kumupha ku Zikilagi. Iyi inali mphotho imene ndinapereka kwa iyeyo chifukwa cha uthenga wake!
11 Nanji pamene anthu oyipa apha munthu wosalakwa ali mʼnyumba mwake ndiponso pa bedi lake! Kodi ine ndingaleke kukulangani ndi kukuchotsani pa dziko lapansi pano?”
12 Kotero Davide analamulira ankhondo ake, ndipo anawapha. Iwo anawadula manja ndi mapazi ndi kupachika matupi awo pa dziwe la ku Hebroni. Koma anatenga mutu wa Isi-Boseti nawuyika mʼmanda a Abineri ku Hebroni.
Davudee cune insanaaşilqa əmr haa'a, manbışeb manbı avqu gyabat'anbı. Qiyğad manbışin g'elybıyiy xıleppı gyatxı, Xevroneene xhyan səəne cigayne k'ane k'eyxə. İşboşetna vuk'ulyub alyapt'ı, Xevroneene Avnerne nyuq'vneeqa k'evxhu.

< 2 Samueli 4 >