< 2 Samueli 14 >
1 Yowabu mwana wa Zeruya anadziwa kuti maganizo a mfumu ali pa Abisalomu.
Manghai kah a lungbuei tah Absalom taengla a om te Zeruiah capa Joab loh a ming.
2 Kotero Yowabu anatuma munthu wina kupita ku Tekowa ndi kukatengako mkazi wanzeru. Yowabu anati kwa mkaziyo, “Ukhale ngati namfedwa. Uvale zovala zaumasiye ndipo usadzole mafuta ena aliwonse. Ukhale ngati mkazi amene wakhala akulira masiku ambiri.
Te dongah Joab loh Tekoa la ol a tah tih te lamkah huta aka cueih te a khuen. Te phoeiah anih te, “Nguekcoi mai lamtah nguekcoinah himbai bai mai laeh. Situi hluk boeh, aka duek ham khohnin yung ah aka nguekcoi huta bangla om laeh.
3 Kenaka upite kwa mfumu ndipo ukayankhule mawu awa.” Ndipo Yowabu anamuwuza mawu oti akanene.
Te phoeiah manghai taengla cet lamtah amah taengah hekah ol bangla thui pah,” a ti nah tih Joab loh anih ka dongah ol a khueh pah.
4 Mkazi wochokera ku Tekowa uja atapita kwa mfumu anadzigwetsa pansi, napereka ulemu kwa mfumu nati, “Thandizeni mfumu!”
Tekoa nu loh manghai te a voek vaengah a maelhmai diklai la a buluk thil tih a bawk pueng. Te phoeiah ni, “Manghai nang loh ng'khang,” a ti nah.
5 Mfumu inamufunsa kuti, “Kodi chikukusautsa iwe nʼchiyani?” Iye anayankha kuti, “Ine ndine mkazi wamasiye, mwamuna wanga anamwalira.
Te dongah amah te manghai loh, “Nang te ba dae lae,” a ti nah. Te vaengah, “Kai tah nuhmai nu tih ka va khaw duek coeng.
6 Ine wantchito wanu ndinali ndi ana aamuna awiri. Iwo anayamba kumenyana mʼmunda, ndipo panalibe woti awaleretse. Wina anakantha mnzakeyo mpaka kumupha.
Na salnu taengkah capa panit he amamih rhoi Te lohma ah hnuei uh rhoi. Amih rhoi laklo ah sim uh pawh. Te dongah pakhat loh pakhat te a ngawn tih duek.
7 Tsono banja lonse landiwukira ine, wantchito wanu. Iwo akuti, ‘Utipatse mwana amene anakantha mʼbale wakeyo kuti timuphe chifukwa cha moyo wa mʼbale wake amene anaphedwayo. Ife tidzaphanso mlowamʼmalo.’ Anthuwo adzapha mwana wanga amene wanditsalira, ndipo dzina la mwamuna wanga silidzakumbukika pakuti sipadzakhalanso mwana pa banja lathu.”
Te dongah a huiko boeih loh na salnu he m'pai thil tih, 'A manuca aka ngawn te han tloeng lamtah anih loh a ngawn a manuca kah hinglu ah anih te ka ngawn uh pawn eh. A pang tueng khaw ka phae uh ni,’ a ti uh. Te dongah ka hmai-alh aka sueng te thih koinih ka va ming neh a meet he diklai hman ah khueh rhoe khueh mahpawh he,” a ti nah.
8 Mfumu inati kwa mkaziyo, “Pitani ku nyumba kwanu ndipo ine ndidzalamula mʼmalo mwanu.”
Te dongah manghai loh huta te, “Na im la mael laeh, nang ham Te kamah loh ka uen bitni,” a ti nah.
9 Koma mkazi wochokera ku Tekowayo anati kwa mfumu, “Mbuye wanga mfumu, kulakwa kukhale pa ine ndi banja la abambo anga ndipo mfumu ndi mpando wanu waufumu mukhale osalakwa.”
Tedae Tekoa nu loh manghai taengah, “Ka boei manghai kathaesainah he kamah so neh a pa imkhui ah om saeh lamtah manghai neh a ngolkhoel ta ommongsitoe la om saeh,” a ti nah.
10 Mfumu inayankha kuti, “Ngati wina aliyense anene kanthu kwa iwe, umubweretse kwa ine, ndipo sadzakuvutitsanso.”
Te phoeiah manghai loh, “Nang taengah aka thui te kamah taengla hang khuen, nang koep m'ben ham Te khoep boel saeh,” a ti nah.
11 Mkaziyo anati, “Mfumu ipemphe kwa Yehova Mulungu wake kuti aletse wobwezera imfa asaphenso wina kuti mwana wanga asawonongedwe.” Mfumu inati, “Pali Yehova wamoyo ngakhale tsitsi limodzi la pamutu pa mwana wako silidzathotholedwa.”
Te phoeiah, “BOEIPA na Pathen loh manghai te n'thoelh pawn saeh. Thii phu aka suk te a rhaep, rhaep la thup nawn saeh. Te daengah ni ka capa te a diil sak uh pawt eh,” a ti nah. Te vaengah manghai loh, “BOEIPA kah hingnah rhangneh na capa kah a sam pakhat pataeng diklai la rhul mahpawh,” a ti nah.
12 Kenaka mkaziyo anati, “Lolani kuti wantchito wanu ayankhule mawu kwa inu mbuye wanga mfumu.” Iye anayankha kuti, “Yankhula.”
Te phoeiah huta loh, “Na salnu long he ka boeipa manghai taengah ol kan thui dae eh,” a ti nah hatah, “Thui saw,” a ti nah.
13 Mkaziyo anati, “Nʼchiyani tsono chimene mwaganiza kuchitira zimenezi anthu a Mulungu? Pamene mfumu yanena izi, kodi sikudzitsutsa yokha, pakuti mfumu sinayitanitse mwana amene anamupirikitsa?
Te dongah huta loh, “Balae tih tahae kah bangla, Pathen kah pilnam he na moeh thil. A heh uhTe manghai loh na khue pawt vaengah, a rhaem banghui la hekah ol he manghai loh a thui.
14 Koma poti madzi akatayika sawoleka, ndiye tonsefe tiyenera kufa ndithu. Koma Mulungu safuna kuti moyo wa munthu utayike kotero anakonza njira yakuti wopirikitsidwayo asakhale wotayikiratu.
Diklai dongah tui a luh tih a coi thai voel pawt bangla n'duek rhoe n'duek uh pawn ni. Pathen loh a hinglu bawt pah pawt cakhaw a kopoek te a moeh pah ta. Te dongah a heh tangtae khaw amah taeng lamloh loh a bung moenih.
15 “Tsopano ine ndabwera kudzanena izi kwa inu mbuye wanga mfumu chifukwa anthu andichititsa mantha. Mdzakazi wanu anaganiza kuti, ‘Ndikayankhula kwa mfumu, mwina adzachita zimene mdzakazi wake adzamupempha.
Te dongah he ol he ka boei manghai taengah thui ham ni ka pawk coeng. Pilnam loh kai ng'hih cakhaw a ti banglam ni na salnu loh manghai taengah ka thui eh. A salnu kah olka Te manghai loh a rhoirhi mai khaming.
16 Mwina mfumu idzavomereza kupulumutsa mdzakazi wake mʼdzanja la munthu amene akufuna kupha ine pamodzi ndi mwana wanga kutichotsa pa cholowa chimene Mulungu anatipatsa.’
Pathen kah rho dong lamloh kamah neh ka capa rhenten aka mitmoeng sak ham khaw, hlang kut lamloh a sal nu a huul ham khaw manghai loh ya pai saeh.
17 “Ndipo tsopano mtumiki wanu akuti, ‘Lolani mawu a mbuye wanga mfumu abweretse mpumulo kwa ine, pakuti mbuye wanga mfumu ali ngati mngelo wa Mulungu pozindikira chabwino ndi choyipa. Yehova Mulungu wanu akhale nanu.’”
Na salnu long tah ka boei manghai kah ol he Pathen puencawn bangla duemnah la om saeh a ti dae ta. Ka boei manghai loh a thae a then khaw a yaak dongah BOEIPA na Pathen tah namah taengah om nawn saeh,” a ti nah.
18 Kenaka mfumu inati kwa mkaziyo, “Usandibisire chilichonse pondiyankha chimene ndidzakufunsa.” Mkaziyo anati, “Mbuye wanga mfumu yankhulani.”
Te phoeiah manghai loh huta te a doo tih, “Namah kan dawt bangla kai taengah ol phah boel mai,” a ti nah. Te vaengah huta long khaw, “Ka boei manghai nang thui laeh,” a ti nah.
19 Mfumu inafunsa kuti, “Kodi zimenezi sukuchita motsogozedwa ndi Yowabu?” Mkaziyo anayankha kuti, “Pali inu wamoyo, mbuye wanga mfumu, palibe munthu angakhotere kumanja kapena kumanzere pa chilichonse chimene mbuye wanga mfumu mwanena. Inde, ndi mtumiki wanu Yowabu amene wandilangiza ine kuchita zimenezi ndipo ndi amene anandipatsa mawu onsewa woti ine mtumiki wanu ndiyankhule.
Te vaengah manghai loh, “Nang taengkah olka boeih dongah he Joab kah kutngo om nama?,” a ti nah. Te dongah huta loh a doo tih, “Ka boei manghai kah na hinglu kah hingnah vanbangla ka boei manghai loh a thui te pakhat khaw banvoei bantang la a hlihloeh moenih. Na sal Joab loh kai ng'uen tih he rhoek kah olka boeih he na salnu kah a ka dongah a khueh.
20 Mtumiki wanu Yowabu anachita zimenezi kuti asinthe mmene zinthu zilili lero. Mbuye wanga muli ndi nzeru ngati za mngelo wa Mulungu. Mumadziwa zonse zimene zikuchitika mʼdziko.”
Olka te a hmuethma hoilae ham ni hekah olka he na sal Joab loh a saii. Tedae ka boeipa tah Pathen puencawn kah cueihnah bangla a cueih dongah, diklai hman kah khaw boeih a ming,” a ti nah.
21 Mfumu inati kwa Yowabu, “Chabwino, ine ndichita zimenezi. Pita kamutenge Abisalomuyo.”
Te daengah manghai loh Joab te, “Ol he ka tloek bitni ne, cet lamtah Absalom camoe te lo laeh,” a ti nah.
22 Yowabu anawerama pansi kupereka ulemu kwa mfumu. Yowabuyo anati, “Lero mtumiki wanu wadziwa kuti wapeza chifundo pamaso panu, mbuye wanga mfumu, chifukwa mwavomera pempho lakeli.”
Te dongah Joab loh a maelhmai te diklai la a buluk tih a bawk phoeiah manghai te a uem. Te phoeiah Joab loh, “Tihnin ah tah ka boei manghai na mikhmuh ah mikdaithen ka dang te na sal loh ka ming. Na sal kah a sal patoeng ol he manghai loh a rhoi coeng,” a ti.
23 Choncho Yowabu anapita ku Gesuri ndipo anamubweretsa Abisalomu ku Yerusalemu.
Joab Te thoo tih Geshuri la cet tih Absalom te Jerusalem la a mael puei.
24 Koma mfumu inati, “Iye apite ku nyumba yake; asaone nkhope yanga.” Kotero Abisalomu anapita ku nyumba yake ndipo sanakumane ndi mfumu.
Tedae manghai loh, “Amah im la mael saeh lamtah ka maelhmai he hmu boel saeh,” a ti nah. Te dongah Absalom Te amah im la mael tih manghai kah maelhmai khaw hmu pawh.
25 Mʼdziko lonse la Israeli munalibe munthu amene anayamikidwa chifukwa cha maonekedwe ake wokongola ngati Abisalomu. Kuyambira kumutu mpaka ku mapazi ake, analibe chilema.
Absalom bangla sakthen hlang he Israel boeih khuiah a om moenih. A khopha lamloh a luki duela thangthen hamla om. A pum dongah a lolhmaih pakhat khaw om pawh.
26 Nthawi ina iliyonse akamameta tsitsi lake, ankameta pamene layamba kumulemera. Akatero amaliyeza, ndipo limalemera makilogalamu awiri pa sikelo yaufumu.
A kum, kum ah apat a pha atah a lu Te vok. Te khaw amah mat a nan vaengah ni a. vok pueng. A lu dongkah sam te a vok tih a thuek vaengah manghai coilung ah shekel yahnih a lo pah.
27 Abisalomu anali ndi ana aamuna atatu ndi wamkazi mmodzi. Mwana wamkazi dzina lake linali Tamara, ndipo anali mkazi wokongola kwambiri.
Absalom loh capa pathum neh canu pakhat a sak. A canu ming tah Tamar tih, a mueimae khaw sakthen nu la om.
28 Abisalomu anakhala zaka ziwiri mu Yerusalemu osaonekera kwa mfumu.
Absalom tah Jerusalem ah khohnin la kum nit kho a sak dae manghai maelhmai hmuh pawh.
29 Kenaka Abisalomu anatumiza mawu kwa Yowabu, kumutuma kuti apite kwa mfumu, koma Yowabu anakana kubwera. Kotero anatumizanso mawu kachiwiri, koma Yowabu anakananso.
Te dongah Absalom loh Joab te a tah tih manghai taengla a tueih. Tedae a taengla a pawk pah ham te a ngaih pah moenih. Te dongah a pabae la koep a tueih dae lo sak ham ngaih pah pawh.
30 Tsono Abisalomu anati kwa antchito ake, “Taonani, munda wa Yowabu uli pafupi ndi wanga ndipo muli barele mʼmenemo. Pitani mukawutenthe mundawo.” Ndipo antchito a Abisalomu anawutentha mundawo.
Te vaengah a sal rhoek taengah, “So uh lah, Joab kah lo he kamah kut ah om, te lamkah cangtun te paan uh lamtah hmai neh hlup la hlup pa uh,” a ti nah. Te dongah Absalom kah sal rhoek loh lo te hmai neh a hlup uh.
31 Ndipo Yowabu anapita ku nyumba ya Abisalomu ndipo anati kwa iye, “Nʼchifukwa chiyani antchito ako atentha munda wanga?”
Te daengah Joab Te too tih Absalom te a im la a paan. Te vaengah, “Balae tih na sal rhoek loh kai lo ke hmai neh a hlup uh,” a ti nah.
32 Abisalomu anati kwa Yowabu, “Taona, ine ndinatumiza mawu kwa iwe ndipo ndinati, ‘Bwera kuno kuti ndikutume kwa mfumu kukafunsa kuti, ‘Nʼchifukwa chiyani ine ndinabwera kuchokera ku Gesuri? Zikanakhala bwino ndikanakhala komweko!’ Tsono pano ndikufuna kuonana ndi mfumu, ndipo ngati ndili olakwa mfumuyo indiphe.’”
Absalom loh Joab te, “'Hela halo dae,’ ka ti tih la nang te kan tah. Te daengah man manghai te voek hamla nang te kan tueih ve. Geshuri lamkah ka pawk parhiTe kai hamla balae a then, ka om palueng vetih manghai kah maelhmai ka hmuh laeh mako, tedae kai pum dongah thaesainah a om atah kai he ng'ngawn saeh,” a ti nah.
33 Choncho Yowabu anapita kwa mfumu ndipo anayiwuza zimenezi. Ndipo mfumu inamuyitanitsa Abisalomu, ndipo analowa nawerama kugunditsa nkhope yake pansi pamaso pa mfumu. Tsono mfumu inapsompsona Abisalomu.
Joab Te manghai taengla cet tih a thui pah. Te daengah Absalom te a khue tih manghai taengla koep ha pawk. Te vaengah manghai kah mikhmuh ah a maelhmai diklai la a buluk tih a bawk. Manghai loh Absalom te a mok.