< 2 Samueli 11 >

1 Nthawi ya mphukira, nthawi imene mafumu amapita ku nkhondo, Davide anatumiza Yowabu ndi ankhondo a mfumu pamodzi ndi gulu lonse lankhondo la Aisraeli. Iwo anawononga Aamoni ndi kuzungulira mzinda wa Raba. Koma Davide anatsala ku Yerusalemu.
Yuxhxhan qadımee, paççahar dəv'əys qığeebaç'ene gahıl, Davudee Yoav cune insanaaşikayiy gırgıne İzrailyne g'oşunuka dəv'eeqa yəqqı'l ha'a. Manbışe Ammonbışikın hı'ı, manbışda paytaxt Rabba hıqiy-allançe avqaaqqa. Davud vucmee İyerusalimcar axva.
2 Tsiku lina cha kumadzulo Davide anadzuka pa bedi lake ndipo ankayenda pamwamba pa nyumba yake. Ali pa dengapo anaona mkazi akusamba. Mkaziyo anali wokongola kwambiri.
Sa yiğıl exheeqana, Davud tyuleençe suğotsu, cune paççahaaşine sarayne daxalqa ılqeç'u maa'ar iykar giyğal. Mana daxayle ilyakkımee, mang'uk'le sa zəiyfa əyeexər g'eece. Mana zəiyfa geer uftanna yixha.
3 Ndipo Davide anatuma munthu wina kuti akafufuze za iye. Munthuyo anati, “Kodi uyu si Batiseba, mwana wa Eliamu, mkazi wa Uriya Mhiti?”
Zəiyfayne hək'ee qiyghanasva Davudee insan g'ıxele. G'axuvuyne insanee eyhen: – Mana zəiyfa Q'etbışda eyxhene Uriyna xhunaşşe, Eliamnar yiş Bat-Şeva vor.
4 Ndipo Davide anatumiza amithenga kwa iye kukamuyitana. Batiseba anabwera kwa Davide ndipo anagona naye. (Nʼkuti mkaziyu atayeretsedwa ku masiku ake osamba). Kenaka anabwerera ku nyumba yake.
Davudee insanar g'axuvu mana cusqa ayree'e. Mana zəiyfa Davudusqa arımee, məng'ı'n yadaaşik eyxhenbı manke ç'əveetxha ıxha. Davud məng'ı'ka g'ılexhana. Mançile qiyğa zəiyfa cene xaaqa siyk'al.
5 Mkaziyo anakhala woyembekezera ndipo anatumiza mawu kwa Davide kunena kuti, “Ine ndine woyembekezera.”
Zəiyfa vuxhne eexva. Məng'ee Davudusqa insan g'ıxele «Zı vuxhne vorva» eyhes.
6 Ndipo Davide anatumiza mawu awa kwa Yowabu: “Nditumizire Uriya Mhiti.” Ndipo Yowabu anamutumiza kwa Davide.
Davudee Yoavne k'anyaqa insan g'axuvu eyhen: – Q'etbışda eyxhena Uriy yizde k'anyaqa g'axıle. Yoavee Uriy Davudne k'anyaqa g'ıxele.
7 Uriya atafika kwa Davide, Davide anamufunsa za momwe analili Yowabu, za asilikali ndi momwe nkhondo inkayendera.
Uriy Davudne k'anyaqa arımee, Davudee mang'uke Yoaviy g'oşun nəxübne, dəv'ə nəxübne əlyhəəva qiyghan.
8 Kenaka Davide anati kwa Uriya, “Pita ku nyumba yako ukapumule.” Choncho Uriya anachoka ku nyumba yaufumu, ndipo mfumuyo inatumiza mphatso kwa Uriya.
Qiyğa Davudee Uriyk'le eyhen: – Xaaqa hoora, sık'ırra g'alixhe. Uriy paççahne sarayeençe qığeç'umee, paççahee yı'q'əle mang'us pay g'uxoole.
9 Koma Uriya anagona pa chipata cha nyumba yaufumu pamodzi ndi antchito onse a mbuye wake ndipo sanapite ku nyumba yake.
Uriymee xaaqa ayk'an deş. Mana paççahne manesa nukaraaşika sacigee sarayne akkayne ghalee g'ılexha.
10 Davide atawuzidwa kuti, “Uriya sanapite ku nyumba yake.” Iye anafunsa kuti, “Kodi iwe sunachokera kutali? Nʼchifukwa chiyani sunapite ku nyumba yako?”
Davuduk'le «Uriy xaaqa ark'ın deşva» uvhumee, mang'vee Uriyke qiyghanan: – Nya'a, ğu yəqqı'le dişde qarı? Nya'a xaaqa idyark'ın?
11 Uriya anayankha Davide kuti, “Bokosi la Chipangano ndi Israeli ndiponso Yuda akukhala mʼmatenti, ndipo mbuye wanga Yowabu ndi ankhondo anu mbuye wanga amanga misasa pa mtetete. Ine ndingapite bwanji ku nyumba yanga kukadya ndi kumwa ndiponso kugona ndi mkazi wanga? Pali inu wamoyo, ine sindidzachita chinthu chimenechi.”
Uriyee Davuduk'le eyhen: – Allahıka mugavilenana q'utye, İzrailybı, Yahuder çadırbışee aaxvamee, yizda xərna eyxhena Yoaviy eskerar g'ab çolbışee aaxvamee, ho'ne zı xaaqa ark'ın otxhan-ulyoğa xhunaşşeyka g'alixhe? Valqaniy yiğne canılqan k'ın ixhen, zı məxdın kar mısacad ha'as deş.
12 Ndipo Davide anati kwa iye, “Ukhale konkuno tsiku lina limodzi, ndipo mawa ndikulola kuti upite.” Kotero Uriya anakhala mu Yerusalemu tsiku limenelo ndi tsiku linalo.
Davudee Uriyk'le eyhen: – Ğu g'iynar inyaa axve, zı ğu g'iyqa yəqqı'l ha'asda. Uriy mane yiğılir, qinne yiğılir İyerusalim axva.
13 Davide anayitana Uriya nadya ndi kumwa naye, ndipo Davide anamuledzeretsa. Koma madzulo Uriya anapita kukagona pa mphasa pamodzi ndi antchito a mbuye wake. Iye sanapite ku nyumba yake.
Davudee mana cusqa qort'ul yugda otxhun-ulyoğu'ı keçe xhinne qa'a. Uriy paççahısse exheeqana qığeç'e. Mana g'alixhasva meer cune ögilynecar cigeeqa, paççahne nukaraaşisqa ayk'an. Mana cune xaaqa meer ayk'an deş.
14 Mmawa Davide analemba kalata kwa Yowabu ndipo anayitumiza ndi Uriya.
Miç'eed qıxhamee, Davudee kağız otk'un, Yoavısqa hixhar he'ecenva Uriysqa qele.
15 Mʼkalatayo analembamo kuti, “Uriya mumuyike patsogolo penipeni, pamene pali nkhondo yoopsa. Ndipo mumusiye yekha kuti akanthidwe ndi kufa.”
Kağızee inva otk'un eyxhe: «Uriy it'umba dəv'ə əəne cigeeqa yəqqı'l he'e. Mana ögil ulyozar he'e, qiyğa zaraba şu yı'q'əlqa ts'ıts'eepxhe, hasre mana ı'xı' gik'ecen».
16 Kotero Yowabu atawuzinga mzindawo, anamuyika Uriya pamalo pamene amadziwa kuti pali asilikali amphamvu.
Yoavee şahar hiqiy-allançe avqumee, mang'uk'le şenbışin yugba aldaaxhvananbı nene surak vuxhay ats'anniy. Mançil-allar mang'vee Uriy mane suralqa salat' ha'a.
17 Ankhondo a mu mzindawo atabwera kudzamenyana ndi Yowabu, anthu ena a gulu la ankhondo la Davide anaphedwa ndipo Uriya Mhiti uja anaphedwanso.
Şaharın insanar Yoavıka səvxəsva, şaharıke g'aqa qığeebaç'e. Manke Davudne g'oşunun sabarabı habat'anbı, habat'anbışde yı'q'nee Q'etbışda eyxhena Uriyer ıxhana.
18 Yowabu anatumiza wamthenga kwa Davide kukafotokoza mwatsatanetsatane za nkhondoyo.
Yoavee Davudne k'anyaqa dəv'ə nəxübiy ılğevç'uva xabar ana insan g'ıxele.
19 Iye anamulangiza wa mthengayo kuti, “Pamene ukatsiriza kufotokozera mfumu za ku nkhondozi,
Mang'vee xabar ana g'ıxelene insanıs xət qa'an: – Ğu dəv'əyne hək'ee yuşan hı'ı ç'əvexhemee,
20 mfumu ikapsa mtima, ndipo akakakufunsa kuti, ‘Nʼchifukwa chiyani munapita pafupi ndi mzindawo kukamenya nkhondo? Inu simunadziwe kuti atha kukuponyerani mivi kuchokera pa khoma?
paççahıs sayıb mançike qəl vuxha vake qiyghınee: «Nya'a şu səvxəsva şaharısqa manimee k'ane qeepxha? Nya'a şok'le ats'a dişdiy, manbışe cabırbışile vukbı ahas ıxhay?
21 Kodi anapha Abimeleki mwana wa Yerubeseti ndani? Kodi mkazi sanamuponyere mphero kuchokera pa khoma? Kotero kuti anakafera ku Tebezi. Nʼchifukwa chiyani munafika pafupi ndi khoma?’ Ngati iye akafunsa zimenezi, iwe ukanene kwa iye kuti, ‘Mtumiki wanunso Uriya Mhiti wafa.’”
Şavaane Yerubbeşetna dix Avimelek gik'u? Nya'a, cabırıle dişdiy mang'ulqa sa zəiyfee yöxxəyna g'aye g'a'apçı, mana Tevetsee gik'u? Nya'a şu manimee cabırbışisqa k'ane qeepxha?» Manva paççahee vak'le uvheene, ğu mang'uk'le eyhe: «Yiğna nukar Q'etbışda eyxhena Uriyer qik'una».
22 Mthengayo ananyamuka, ndipo atafika anamuwuza Davide zonse zimene Yowabu anamutuma kuti akanene.
Xabar ana ı'qqəna insan yəqqı'lqa gexha. Mana qarı Davudusqa hirxhıl, Yoavee cuk'le uvhuyn gırgın mang'us yuşan ha'an.
23 Mthengayo anati kwa Davide, “Anthuwo anatiposa mphamvu ndipo anabwera kudzalimbana nafe poyera, koma ife tinawabwezera ku chipata cha mzindawo.
Xabar ana arıyne insanee Davuduk'le eyhen: – Şen insanar şalqa k'yoptul, şaka saç'uvkasva şaharıke g'aqa qığeepç'ı. Şinab manbı şaharne akkabışisqamee yı'q'əlqa g'ee'epşiynbı.
24 Ndipo anthu oponya mivi anatiponyera kuchokera pa khoma, anthu ena a mfumu afa. Kuwonjezera apo, mtumiki wanu Uriya Mhiti wafanso.”
Vukbı ayhenbışee cabırbışile paççahne eskeraaşilqa vukbı gyoğu'u, paççahne eskeraaşike habat'anbıb vuxhaynbı. Yiğna nukar Q'etbışda eyxhena Uriyer maa'ar qik'una.
25 Davide anamuwuza mthengayo kuti, “Ukanene izi kwa Yowabu: ‘Zimenezi zisakukhumudwitse; lupanga limapha wina nthawi zinanso wina. Limbikitsa nkhondo pa mzindawo ndipo uwuwononge!’ Ukanene zimenezi pomulimbikitsa Yowabu.”
Davudee xabar abıyng'uk'le eyhen: – Yoavık'le eyhe: «Mançil-alla aq'va havaxan hıma'acen. G'ılıncın ina-şena geer gik'u. Həşdiyle guc sacigeeqa sav'u, mane şaharılqa sayıb k'yoohre, mana hı'ğəəkar hee'e». Məxüd ğu Yoavıs yik'bı hele.
26 Mkazi wa Uriya atamva kuti mwamuna wake wafa, analira maliro.
Uriyne xhunaşşeyk'le Bat-Şevayk'le Uriy qik'uva g'ayxhımee, mang'us ak' avqaaqqa.
27 Nthawi yolira maliro itatha, Davide anamubweretsa ku nyumba yake, ndipo anakhala mkazi wake nabala mwana wamwamuna. Koma Yehova sanakondwe ndi zimene Davide anachitazo.
Ak' ç'əvuvxhayle qiyğa, Davudee insan g'axuvu, Bat-Şeva cune xaaqa qiyelee'e. Məng'ı'ke cus xhunaşşe hee'e. Qiyğa məng'ee Davudus dix uxooxa. Davudee hav'una mana iş Rəbbine yik'eençe vooxhe deş.

< 2 Samueli 11 >