< 2 Petro 1 >

1 Ndine Simoni Petro, mtumiki ndi mtumwi wa Yesu Khristu. Kwa anthu amene analandira chikhulupiriro cha mtengowapatali chomwe ifenso tinalandira chifukwa cha chilungamo cha Mulungu ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu.
Simon Peter renga, Jisua Khrista tîrlâm le tîrton, Han Jisua Khrista kin Pathien le Sanminringpu dikna sika kin chang anghan iemna luttak achang ngei:
2 Chisomo ndi mtendere zochuluka zikhale nanu pomudziwa Mulungu ndi Yesu Ambuye athu.
Pathien le ei Pumapa Jisua nin rietna han moroina le inngêina tamtak nin ta ni rese.
3 Mulungu mwa mphamvu zake anatipatsa zonse zofunika kukhala moyo opembedza, potidziwitsa za Iyeyo amene anatiyitana ku ulemerero wake ndi ubwino wake.
A roiinpuina le asatna chang ranga mi koipu ei rietna sika sakhuo diktak ringnuna ei om theina ranga neinuntin ei nâng murdi Pathien sinthotheina ânthieng mi pêk zoi.
4 Mwa ulemerero ndi ubwino wakewo, anatipatsa malonjezo opambana kwambiri ndi a mtengowapatali. Amenewa ndi malonjezo amene amakuthandizani kulandira nawo moyo wa Mulungu, titapulumuka ku chiwonongeko chimene chili mʼdziko lapansi chifukwa cha zilakolako zoyipa.
Ma anghan, neinunpêk roiinpui le luttak ânkhâm hah mi pêk zoi, ha neinunpêkngei sika han rammuola ôina saloi ngei renga rotpai, mi nina inthieng hah hong chang thei nin tih.
5 Choncho, chitani khama kuwonjezera moyo wabwino pa chikhulupiriro chanu, ndipo pa moyo wabwino muwonjezerepo nzeru.
Masika han nin theidôr songin nin taksônna han satna bôk ungla, nin satna han rietna bôk ungla,
6 Pa nzeru muwonjezerepo kudziretsa, pa kudziretsa muwonjezerepo chipiriro, ndipo pa chipiriro muwonjezerepo khalidwe lolemekeza Mulungu.
nin rietna han indîntheina bôk ungla, nin indîntheina han tuongdierna bôk ungla, nin tuongdierna han pathien angna bôk ungla,
7 Pa khalidwe lolemekeza Mulungu muwonjezerepo chifundo cha ubale, pa chifundo cha ubale muwonjezerepo chikondi.
nin pathien angna han lâibung inmoroina bôk ungla, nin lâibung inmoroina han inlungkhamna bôk roi.
8 Ngati zonsezi zikhala mwa inu nʼkumachuluka, zidzakuthandizani kuti musakhale aulesi ndi osapindula ndi chidziwitso chanu cha Ambuye athu Yesu Khristu.
Hi mi nina neinun ngei hih nin inâng ani, hi ngei hih nin dôn tam ok inchu, ei Pumapa Jisua Khrista nin rietna han nangni min râtin, malam nangni min pan a tih.
9 Koma ngati wina alibe zimenezi, ndi wakhungu sangathe kuona patali, ndipo wayiwala kuti anayeretsedwa machimo ake akale.
Aniatachu tukhom ha ngei dônloi chu a kôlrevêl vai amua, mitcho ania, a sietna muruo renga minsâi ani hah ai mingil ani.
10 Nʼchifukwa chake abale anga, funitsitsani kuti mayitanidwe ndi masankhidwe anu akhale otsimikizika. Pakuti ngati muchita zinthu izi, simudzagwa konse.
Masikin ka lâibungngei le sarnungei, Pathien'n a lungdoa nangni koina le thangna hah asôia omtit rangin ningsiet uol roi, ma anghan nin thôn chu nin taksônna hah mâk tet no tunui.
11 Mudzalandiridwa bwino kwambiri mu ufumu wosatha wa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. (aiōnios g166)
Ma anghan, ei Pumapa le Sanminringpu Jisua Khrista ringinlon Rêngrama lût theina akipin dikna pêk nîng nin tih. (aiōnios g166)
12 Tsono ine ndidzakukumbutsani nthawi zonse za zinthu zimenezi, ngakhale kuti mumazidziwa ndipo kuti munakhazikika mʼchoonadi chimene muli nacho tsopano.
Masikin, hi chong ngei hih zoratin rietmintharna nangni pêk bang ki tih, nin lei rietsai piel nikhomsenla, maleh chongtak nin changa han lei phun mindet ngit lei ni ta khom ungla.
13 Ndikuganiza kuti nʼkoyenera ndikanali mu msasa uno, kuti ndikutsitsimutseni ndi kukukumbutsani,
Ki ringkâr chu hima roi ngei hih nin riettitna hah mohôk minhar tit inlang sâng atih, tiin ki mindon ani.
14 chifukwa ndikudziwa kuti posachedwapa ndikuchoka mu msasa uno, monga Ambuye athu Yesu Khristu anandidziwitsiratu.
Ei Pumapa Jisua Khrista'n ânthârlaka mi lei ril anghan, hi thithei takpum hih chomolte suoleh chu khekpai ki tih, iti hih ki riet.
15 Ndipo ndidzayesetsa kuti nditachoka, mudzakumbukire nthawi zonse.
Ki thi suoleh khomin hi roi ngei hih zora tiin nin riettit theina rang lam nangni pêk rangin ke theidôr tho ki tih.
16 Ife sitinatsate nkhani zongopeka titakuwuzani za mphamvu zake ndi zakubweranso kwa Ambuye athu Yesu Khristu, koma tinaona ndi maso athu za ukulu wake.
Ei Pumapa Jisua Khrista juong nôkna roiinpui a roi nangni kin min riet hah kin rachama kin phuotot thurchi ngeia inding mak meh, kin mit lelên ânlalna kin mu ani.
17 Pakuti Iye analandira ulemu ndi ulemerero kuchokera kwa Mulungu Atate atamufikira mawu ochokera ku ulemerero wa ukulu akuti, “Uyu ndi mwana wanga amene Ine ndimukonda, amene ndimakondwera naye kwambiri.”
Ama hah Pa Pathien'n inlalna leh roiinpuina a pêka, a kôma Roiinpuina Ânchungtak renga rôl ajuon ringa “Ma hih ka Nâipasal moroitak, ka râisân tatak hah ani” a ti lâia han kin om ani.
18 Ifeyo tinamva mawuwa akuchokera kumwamba pamene tinali naye pamodzi pa phiri lopatulika lija.
Ha rôl hah a kôma muol inthienga kin om lâiin invân renga ajuonga, keini lelên kin iriet ani.
19 Tsono ifenso tili ndi mawu a uneneri amene ndi odalirika kwambiri ndipo inu mudzachita bwino mukawasamalira mawuwa, monga kuwunika kumene kukuwala mu mdima, mpaka tsiku lidzayambe kucha, pamene nthanda idzayambe kuwala mʼmitima mwanu.
Masikin dêipungei chongphuong hah adet uolin ei rietminthâr ani. Ama chong nin rangâia anin chu tho minsa nin ta, khuo avâra, sikhovâr hah nin mulungrîla avâr mâka chu, ajîngna châti vâr angha ani sikin.
20 Kuposa zonse, inu muyenera kuzindikira kuti palibe mawu a uneneri amene amatanthauzidwa pa okha.
Adadang nêkin Pathien lekhabua chongphuong ngei hih tutên atheiin rilminthâr thei ngâi ni mak iti riettit roi.
21 Pakuti mawu a uneneri sanadze mwa kufuna kwa anthu, koma anthu anayankhula zochokera kwa Mulungu, Mzimu Woyera atawayankhulitsa.
Dêipuchong chongbe hih miriem jôtna sika suok ngâi ni maka, aniatachu miriemngei hah Ratha Inthieng jêka omin Pathien renga juong suok chong hah an iril ngâi ani.

< 2 Petro 1 >