< 2 Petro 2 >

1 Koma panalinso aneneri onama pakati pa Aisraeli, monga padzakhalanso aphunzitsi onyenga pakati panu. Iwo adzalowetsa mwamseri ziphunzitso zonama ndi zowononga, nadzakana Ambuye amene anawawombola, ndipo motero adzadziyitanira okha chiwonongeko mwadzidzidzi.
Hatei, profetkaphawknaw teh Judahnaw thung hoi a tâco e patetlah nangmouh thung hoi hai saya kaphawknaw a tâco van han. Ahnimouh ni kamkonae koe kaphatkhai e tawm payonnae arulahoi thokhai awh vaiteh, na karatangkung Bawipa patenghai pahnawt awh vaiteh, amamae lathueng karang poung lah rawknae a pha sak han.
2 Ambiri adzatsata njira zawo zochititsa manyazi ndipo chifukwa cha iwowa, anthu adzanyoza njira ya choonadi.
Tami moikapap nihai, ahnimae hnopai lungradueknae hnukkâbang awh vaiteh, lawkkatang lamthung teh ahnimouh kecu dudam e lah kaawm han.
3 Pofuna kupeza chuma, aphunzitsiwa adzakudyerani chuma chanu pokuwuzani nkhani zopeka. Chiweruzo chawo chinakonzedwa kale, ndipo chikuwadikira.
Ahnimouh ni hounlounnae, pasawtpanepnae lawk hoi nangmouh na yo awh han. Ahnimouh lawkcengnae teh ayan hoi hnawng hoeh. Ahnimae kamkonae haiyah ngâm boihoeh.
4 Pakuti Mulungu sanalekerere angelo atachimwa paja, koma anawaponya mʼndende, nawayika mʼmaenje amdima, kuwasunga kuti adzaweruzidwe. (Tartaroō g5020)
Bangkongtetpawiteh, Cathut ni ka payon e kalvantami hah pasainae tawn hoeh. Hell hmai adungpoungnae koe hmonae sumbawtarui hoi a katek teh lawkceng hanelah a hruek toe. (Tartaroō g5020)
5 Iye sanalekerere dziko lapansi kalelo, koma anapulumutsa Nowa, mlaliki wa chilungamo, ndi anthu ena asanu ndi awiri atadzetsa chigumula pa dziko lapansi kwa anthu akhalidwe losapembedza Mulunguyo.
Ayan e talaivan hai pasai laipalah, lannae phung ka dei e Noah hoi tami sari touh e naw hah a hlout sak teh cathutlaipa e talai taminaw pueng teh tuikamuem hoi koung a raphoe.
6 Mulungu anaweruza mizinda ya Sodomu ndi Gomora nayiwononga ndi moto, kuti ikhale chitsanzo cha zimene zidzachitikira anthu osapembedza Mulungu.
Hothloilah Sawdom hoi Gomorrah khopui hah lawk a ceng teh hrabalah mueng a yawng sak teh, cathutlaipa e taminaw ni khetsin hanelah sut ao.
7 Koma Iye anapulumutsa Loti, munthu wolungama, amene ankavutika ndi khalidwe lonyansa la anthu oyipa.
Hatnavah, kâcakuepnae kaawm hoeh e taminaw e hounlounnae lahoi khosaknae ni rektap lah kaawm e tamikalan Lot hah a rungngang.
8 (Pakuti munthu wolungamayo, pokhala pakati pawo tsiku ndi tsiku ankavutika mu mtima ndi makhalidwe awo oyipa amene ankawaona ndi kuwamva).
Hote tamikalan teh, ahnimouh koe kho a sak navah, ahnimae kâlawklaipa hringnae hoi tawksaknae hnintangkuem a hmu teh a thainae ni a lannae lungthin hah puenghoi a rektap pouh.
9 Tsono mutha kuona kuti Ambuye amadziwa kuwapulumutsa kwake pa mayesero anthu opembedza. Amadziwanso kusunga osalungama kuti alangidwe mpaka tsiku la chiweruzo.
Hatdawkvah, cathutlae taminaw hah tacueknae dawk hoi rasa hanelah thoseh, tamikalan hoeh e naw lawkcengnae hnin dawk reknae khang sak hanelah hruek hane hai thoseh a panue e lah ao.
10 Makamaka amene amatsata zilakolako zonyansa zathupi nanyoza ulamuliro. Anthu amenewa ndi odzikuza, ndipo otsata chifuniro cha iwo eni, sasamala za munthu, saopa kuchitira chipongwe zolengedwa za mmwamba.
Alawkpui lah ka khin e hounlounnae lahoi takngainae hnukkâbang teh, kâtawnnae kadudamnaw hah hottelah a hruek han.
11 Komatu ngakhale angelo, amene ali akulu ndi amphamvu kuwaposa, sayankhula za chipongwe pobweretsa chiweruzo pa iwo kuchokera kwa Ambuye.
Ahnimouh hlak thao thasainae hoi bahu kaawm e kalvantami ni patenghai yah, Cathut hmalah lawkcengnae sak awh hoeh.
12 Koma anthu awa amachita chipongwe zinthu zimene sakuzidziwa. Ali ngati zirombo zopanda nzeru. Zirombo zolengedwa kuti zigwidwe ndi kuwonongedwa, ndipo ngati zirombozo adzawonongedwa.
Hatei, ahnimanaw hah man vaiteh, be thei hane moithangnaw patetlah ao awh teh amamouh ni a thai panuek hoeh e hah a dudam awh. Ahnimouh teh moithangnaw kahmakata e patetlah a kahmakata awh vaiteh, amamae lanhoehnae phu teh a khang awh han.
13 Iwo adzalangidwa chifukwa cha zoyipa zimene anachita. Koma chimene chimawakomera ndi kumangochita zokondweretsa thupi masanasana. Iwo ali ngati mawanga ndi zilema. Podya nanu pamodzi amakondwera kuchita za chinyengo.
Khodai patenghai yah canei hounloun e heh nawmnae lah a pouk awh teh, nangmouh hoi rei canei awh navah amamae dumyennae dawk a nawm awh teh nangmouh hanlah min mathoenae lah ao awh.
14 Ndi maso awo odzaza ndi chigololo, salekeza kuchimwa. Amanyengerera anthu osakhazikika. Iwo ndi akatswiri pa dyera ndi chuma, ndipo ndi ana otembereredwa!
Ahnimae mit teh uicuk ngainae hoi akawi dawkvah yon sak laipalah awm ngai awh hoeh. A lung kacakhoehe taminaw hah yonnae koe lah a tacuek awh teh, hounlounnae dawk a phunep awh toung dawkvah, thoebo e canu capa lah ao awh.
15 Iwo anasiya njira yolungama ndipo anapatuka kutsata njira ya Baalamu mwana wa Beori, amene anakonda malipiro a chosalungama.
Ahnimouh teh, lam kalan hah a pahnawt awh teh, lam a payon awh toung dawkvah, lanhoehnae kutphu lungpataw e Beor capa Balaam e lamthung a dawn awh.
16 Koma anadzudzulidwa chifukwa cha kulakwa kwakeko. Bulu, nyama imene siyankhula, inayankhula ngati munthu kuletsa misala ya mneneriyo.
Hatei, Balaam teh amae a payonnae dawk yue e lah ao. Lawk ka dei thai hoeh e la ni tami lawk lahoi a dei teh hote profet e pathunae hah a ngang.
17 Anthu amenewa ali ngati akasupe wopanda madzi, ndiponso ngati nkhungu yowuluzidwa ndi mphepo yamkuntho. Mulungu wawasungira mdima wandiweyani.
Ahnimanaw teh tui kahak e tuikhu, kahlî ni a palek e tâmai patetlah doeh ao awh. Ahnimouh hanelah yungyoe hmonae a hruek pouh toe. (questioned)
18 Pakuti anayankhula mawu opanda pake ndi onyada, ndipo ndi zilakolako zoyipa za thupi amanyenga anthu amene angopulumuka kumene pakati pa anzawo oyipa.
Bangkongtetpawiteh, ahnimouh ni lawk pacawt lahoi a kâoup awh teh, tami kahawihoehnaw thung hringnae koehoi nuengnueng kahlout e naw hah takngainae, hounlounnae hoi a dumyen awh.
19 Amawalonjeza ufulu, pomwe iwo eni ndi akapolo a zizolowezi zowononga. Pajatu munthu amakhala kapolo wa chilichonse chimene chikumulamulira.
Ahnimouh ni hote taminaw hah hloutnae na poe awh han atipouh awh nahlangva vah, amamouh rawknae san lah ao awh. Bangkongtetpawiteh, tami katâ e teh tami e bawi lah ao.
20 Ngati anapulumuka ku zodetsa za dziko lapansi podziwa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu, pambuyo pake nagwidwanso ndi kugonjetsedwa ndi zomwezo, potsiriza adzakhala oyipa kuposa mmene analili poyamba.
Maimae Bawipa hoi rungngangkung Jisuh Khrih panuenae lahoi talaivan khinnae dawk hoi hlout awh hnukkhu, hote hnonaw dawk bout kâman awh pawiteh, ahmaloe e hlak a hnukkhu e hoe a mathoe.
21 Kukanakhala bwino akanapanda kudziwa njira ya chilungamo, koposa ndi kuyileka atadziwa lamulo loyera limene Mulungu anawapatsa.
Bangkongtetpawiteh, lannae lamthung panue nahlangva, maimouh koe na poe e kathounge kâpoelawk hah hnamthun takhai hlak teh hote hah panuek laipalah awm pawiteh ahnimouh hanlah bet ahawihnawn.
22 Kwa iwo miyambi iyi ndi yoona, “Galu wabwerera ku masanzi ake,” ndipo, “Nkhumba imene inasamba, yakunkhunizikanso mʼmatope.”
Ui ni a palo bout a ca, tui pâhluk tangcoung e vok ni tangkan bout a kâkaawk tie cingthuilawk hah hot patet e taminaw koe akuep.

< 2 Petro 2 >