< 2 Yohane 1 >

1 Ndine mkulu wampingo, kulembera: Mayi wosankhidwa ndi Mulungu ndi kwa ana ake amene ndimawakonda mʼchoonadi. Ndipo sindine ndekha amene ndimawakonda, komanso onse odziwa choonadi.
Surat ini tulis oleh tetua kepada perempuan terpilih dan anak-anaknya, yang saya kasihi dalam kebenaran. Bukan hanya dari saya, tetapi dari setiap orang yang mengetahui kebenaran,
2 Timakukondani chifukwa cha choonadi chimene chimakhala mwa ife ndipo chidzakhala mwa ife mpaka muyaya. (aiōn g165)
karena kebenaran hidup di dalam kita dan akan bersama kita selamanya. (aiōn g165)
3 Chisomo, chifundo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate ndi kwa Yesu Khristu, Mwana wa Atate, zikhale ndi ife mʼchoonadi ndi mʼchikondi.
Semoga kasih karunia, belas kasihan, dan damai selalu menyertai kita selamanya, dari Allah Bapa dan dari Yesus Kristus, Putra Bapa, dalam kebenaran dan cinta-Nya.
4 Ndinakondwera kwambiri nditapeza ana anu ena akuyenda mʼchoonadi, monga Atate anatilamulira.
Saya bahagia menemukan bahwa beberapa anakmu mengikuti kebenaran, seperti yang diperintahkan Bapa kepada kita.
5 Ndipo tsopano, amayi wokondedwa, sindikukulemberani lamulo latsopano koma lomwe lija takhala nalo kuyambira pachiyambi. Ine ndikukupemphani kuti tidzikondana wina ndi mnzake.
Sekarang saya beri tahu kepadamu, hai perempuan, bukan sebagai instruksi baru, tetapi mengikuti apa yang sudah kita pahami sejak awal, bahwa kita harus saling mengasihi.
6 Ndipo chikondi ndiye kuyenda momvera malamulo ake. Lamulo lake ndi lakuti mukhale moyo wachikondi monga munamva kuyambira pachiyambi.
Inilah arti kasih itu: kita harus mengikuti perintah Allah. Perintahnya, seperti yang kita dengar sejak awal, adalah bahwa kita harus hidup dalam kasih.
7 Ndikunena zimenezi chifukwa anthu ambiri onyenga, amene savomereza kuti Yesu Khristu anabwera monga munthu, akuyenda mʼdziko lapansi. Munthu aliyense otere ndi wonyenga ndiponso wokana Khristu.
Saya memberi tahu kalian ini karena banyak penipu sudah pergi dan keluar mengikuti dunia ini. Mereka tidak menerima bahwa Yesus Kristus sudah datang sebagai manusia. Siapapun seperti ini adalah penipu dan antikristus.
8 Chenjerani kuti mungataye chimene mwagwirira ntchito, koma chitani khama kuti mukalandire mphotho yanu yonse.
Berhati-hatilah agar kalian tidak kehilangan apa yang sudah kita kerjakan dengan sangat keras, dan bahwa kalian menerima semua yang seharusnya.
9 Aliyense amene sasunga chiphunzitso cha Khristu, alibe Mulungu. Koma amene amasunga chiphunzitsochi, ameneyo alinso ndi Atate ndi Mwana.
Semua orang yang menjadi ekstremis dan tidak mengikuti ajaran Kristus, tidak memiliki Allah di dalam diri mereka. Mereka yang terus mengikuti ajaran Kristus memiliki baik Bapa maupun Putra di dalam diri mereka.
10 Ngati wina aliyense abwera kwa inu osaphunzitsa zimenezi, musamulandire mʼnyumba mwanu kapena kumupatsa moni.
Jika orang datang kepada kalian dan tidak menunjukkan bukti ajaran Kristus, jangan menerima dia, jangan menyambut dia —
11 Aliyense wolandira munthu wotere ndiye kuti akuvomerezana nazo ntchito zake zoyipa.
karena jika kalian menerima dia, kalian ikut serta dalam pekerjaan jahat yang dilakukannya.
12 Ndili nazo zambiri zoti ndikulembereni, koma sindikufuna kuzilemba mʼkalata. Mʼmalo mwake, ndikuyembekeza kufika kwanuko kuti tidzakambirane nanu pamaso ndi pamaso, potero chimwemwe chathu chidzakhala chathunthu.
Ada begitu banyak hal yang ingin kukatakan kepadamu sehingga saya tidak akan menulis lagi dengan kertas dan tinta, karena saya berharap dapat mengunjungi dan berbicara denganmu secara langsung. Hal itu akan membuat kita sangat bahagia!
13 Ana a mlongo wanu wosankhidwa ndi Mulungu akupereka moni.
Salam untukmu dari anak-anak dari saudari yang terpilih!

< 2 Yohane 1 >