< 2 Akorinto 9 >

1 Nʼkosafunika kuti ndikulembereni za utumiki othandiza anthu a Mulungu.
A szentek iránt való szolgálatról felesleges is néktek írnom.
2 Popeza ndikudziwa mtima wanu wofuna kuthandiza, ndipo ndakhala ndikuwawuza monyadira a ku Makedoniya za chimenechi. Ndimawawuza kuti inu a ku Akaya munakonzeka kale chaka chatha kuti mupereke. Ndipo changu chanu chapatsa chidwi ambiri mwa iwo kuti nawonso achitepo kanthu.
Hiszen ismerem a ti készségteket a melylyel dicsekszem felőletek a macedónoknak, hogy Akhája kész a mult esztendő óta; és a ti buzgóságtok, sokakat magával ragadt.
3 Koma ndikutumiza abalewo kuti kukunyadirani kwathu pa zimenezi kutsimikizike kuti si kwachabe ndi kuti mukhale okonzeka monga ndinanenera.
Mindamellett elküldöttem az atyafiakat, hogy a mi felőletek való dicsekedésünk ebben a részben hiábavaló ne legyen; hogy, a mint mondám, készen legyetek.
4 Pakuti nditabwera kumeneko ndi abale ena a ku Makedoniya, ndikukupezani kuti simunakonzeke, tingadzachite manyazi chifukwa chokudalirani. Koma amene angadzachite manyazi kwambiri ndi inuyo.
Hogy aztán, ha a macedónok velem együtt odajutnak és titeket készületlenül találnak, valamiképen szégyent ne valljunk mi, hogy ne mondjam ti, ebben a dologban.
5 Choncho ndinaganiza kuti nʼkofunika kupempha abale kuti adzakuchezereni ineyo ndisanafike, ndikuti adzatsirize kukonzekera mphatso zomwe munalonjeza kupereka mowolowamanja. Motero mphatsoyo idzakhala yokonzeratu, ndipo idzakhala mphatso yoperekedwa mowolowamanja, osati mokakamizidwa.
Szükségesnek véltem azért utasítani az atyafiakat, hogy előre menjenek el hozzátok, és készítsék el előre a ti előre megígért adományotokat, hogy az úgy legyen készen, mint adomány, és nem mint ragadomány.
6 Takumbukirani mawu awa: Amene adzala pangʼono, adzakololanso pangʼono, ndipo amene adzala zochuluka, adzakololanso zochuluka.
Azt mondom pedig: A ki szűken vet, szűken is arat; és a ki bőven vet, bőven is arat.
7 Munthu aliyense apereke chimene watsimikiza mu mtima mwake kuti apereka, osati monyinyirika kapena mokakamizidwa, pakuti Mulungu amakonda wopereka mokondwera.
Kiki a mint eltökélte szívében, nem szomorúságból, vagy kénytelenségből; mert a jókedvű adakozót szereti az Isten.
8 Ndipo Mulungu akhoza kukudalitsani kwambiri, kuti inuyo nthawi zonse mukhale ndi zinthu zokukwanirani, ndiponso ndi zina zochuluka kuti muthandize pa ntchito zonse zabwino.
Az Isten pedig hatalmas arra, hogy rátok áraszsza minden kegyelmét; hogy mindenben, mindenkor teljes elégségtek lévén, minden jótéteményre bőségben legyetek,
9 Paja analemba kuti, “Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya.” (aiōn g165)
A mint meg van írva: Szórt, adott a szegényeknek; az ő igazsága örökké megmarad. (aiōn g165)
10 Tsono Mulungu amene amapereka mbewu kwa wofesa, ndiponso chakudya kuti adye, adzaperekanso mbewu mʼnkhokwe zanu ndi kuzichulukitsa. Iye adzachulukitsanso zipatso za chilungamo chanu.
A ki pedig magot ád a magvetőnek és kenyeret eleségül, ád és megsokasítja a ti vetésteket és megnöveli a ti igazságtoknak gyümölcsét,
11 Adzakulemeretsani pa zonse kuti mukhale owolowamanja pa nthawi zonse. Ndipo kuwolowamanja kwanu kudzera mwa ife, kudzakhala kuthokoza kwa Mulungu.
Hogy mindenben meggazdagodjatok a teljes jószívűségre, a mely általunk hálaadást szerez az Istennek.
12 Ntchito imene mukugwirayi siyongothandiza kokha anthu a Mulungu kupeza zosowa, komanso ikuthandiza kuti anthu ambiri ayamike Mulungu.
Mert e tisztnek szolgálata nemcsak a szenteknek szükségét elégíti ki, hanem sok hálaadással bőséges az Isten előtt;
13 Chifukwa cha ntchito imene mwawatsimikizira nokha, anthu ena onse adzayamika Mulungu chifukwa cha kumvera kwanu kumene kumaonekera pamene mukuvomereza Uthenga Wabwino wa Khristu, ndiponso chifukwa chowagawira mowolowamanja iwowo pamodzi ndi wina aliyense.
A mennyiben e szolgálatnak próbája által dicsőítik az Istent a ti Krisztus evangyéliomát valló engedelmességtekért, és a ti hozzájuk és mindenekhez való adakozó jószívűségtekért.
14 Ndipo iwowo adzakupemphererani mwachikondi chifukwa cha chisomo choposa chimene Ambuye wakupatsani.
Mikor érettetek könyörögve ők is vágyakoznak utánatok az Istennek rajtatok való bőséges kegyelme miatt.
15 Tiyamike Mulungu chifukwa cha mphatso zake zosaneneka!
Az Istennek pedig legyen hála az ő kimondhatatlan ajándékáért.

< 2 Akorinto 9 >