< 2 Akorinto 8 >

1 Ndipo tsopano, abale, tikufuna kuti mudziwe za chisomo chimene Mulungu wapereka ku mipingo ya ku Makedoniya.
Kin lâibungngei le sarnungei, Macedonia rama koiindangngei lâia Pathien moroina sintho lenna hah nin riet rangin kin nuom ani.
2 Pakati pa mayesero owawitsa, chimwemwe chawo chosefukira ndi umphawi wawo otheratu, anapereka mowolowamanja kwambiri.
Intaknangei an tong han minsin tatakin an oma; aniatachu, an râisâna alien tatak sikin inriengtak nikhomsenla ngei, phaltakin pêkna an dôn ani.
3 Motero ndikuchitira umboni kuti anapereka mmene akanathera, ndipo mwinanso kuposera mmene akathera kupereka. Anapereka mosakakamizidwa,
An pharidôr chu an pêka, an phari nêka tam khom an nuom dodôrin an pêk ti nangni ki min riet minthâr ani.
4 ndipo anatipempha motiwumiriza kuti tiwapatse mwayi woti nawonso athandize anthu oyera mtima a ku Yudeya.
An theia mulungsuokin Judea rama Pathien mingei sanna thona tieng khom sintum dôn sa rangin min ngên ani.
5 Iwo anachita moposera mmene ife timayembekezera. Choyamba anadzipereka kwa Ambuye ndipo kenaka kwa ife monga mwa chifuniro cha Mulungu.
Maha kin sabeina pêna ani! Amotona Pumapa kôm an pêk baka; masuole chu, Pumapa lungdôn kin kôm anninanâkin an inpêk nôk ani.
6 Choncho tinamupempha Tito kuti atsirize poti nʼkuti atayamba kale ntchito yachisomoyi pakati panu.
Masikin hi sin phutpu, Titus hih kin ngên, hi lungkhamna chuonsin alieka sa uol hih sin minzom tita nangni zoipui rangin.
7 Popeza pa zinthu zonse munachita bwino, monga pachikhulupiriro, poyankhula, pachidziwitso, pakhama lambiri ndi pachikondi chanu pa ife, onetsetsani kuti muchitenso bwino pachisomo ichi chopereka.
Nin dôn murdi: taksônna ngei, thurchi misîr theina ngei, le rietna ngei, mi san ranga nin jôtna ngei le mi nin lungkhamna han nin nei oka. Masikin hi lungkhamna chuonsin khoma hin phaltaka nin inpêk sa rangin nangni kin nuom ani.
8 Sindikukulamulirani, koma ndikufuna kuona ngati chikondi chanu nʼchoona pofananitsa ndi changu cha anthu ena.
Ite balamngei nangni khang pe ma-ung. Nikhomsenla midangngeiin mi san rang an jôt tie ngei nangni min mûn, mi nin lungkham hih adik tatak mo ti riet rang ku pût ani.
9 Pakuti mukudziwa chisomo cha Ambuye athu Yesu Khristu, kuti ngakhale anali wolemera, koma chifukwa cha inuyo anasanduka wosauka, kuti umphawi wakewo, inuyo mulemere.
Ei Pumapa Jisua Khrista moroina hah nin rieta; nei bâk khomsenla, nangni a min nei theina rangin, nangni jârin amananâkin inrieng a chang ani.
10 Ndipo nawa malangizo anga pa zoyenera inu kuchita pa nkhaniyi. Chaka chatha munali oyamba, osati ongofuna kupereka kokha komanso okhala ndi mtima ofuna kupereka.
Ku nuomlam chu nikuma nin phut hah atûn hin zoi ungla chu nin ta rangin sa uol atih. Sin ranga aphut masa vai nimak choia, hannirese sin ranga a nuom masa khom nin ni sa.
11 Tsopano tsirizani ntchitoyi, ndipo changu chanu chofunitsitsa kugwira ntchitoyi ndi kuyitsiriza chichitike molingana ndi zimene muli nazo.
Hanchu ma chunga han minngam titin, nan chuonsin hah zoi ta roi! Nin lei mintuo anghan zoi rangin jôt ungla, male atûna nin dôn lam tak lehin tho roi.
12 Ndipo ngati mtima ofunitsitsa ulipo, mphatsoyo imalandiridwa molingana ndi zimene munthuyo ali nazo, osati zimene alibe.
Pêk rang nin jôtin chu, nin dônloi chunga niloiin, nin dôn chunga nin neinunpêk hah Pathien'n khôk atih.
13 Cholinga chathu sikuti tipeputse ena pamene inuyo mukuvutika, koma kuti pakhale kufanana.
Nin chunga puokrik nangni min pêlin midangngei mojôk rang pût mu-unga; aniatachu hi zora hin atam nin dôn sikin, ânsam ngei nin san ngei hah asa ani. Hanchu, nangni nin insama anni an dôn mintam khomin nangni san an tih. Ma anghan in-angna om atih.
14 Zambiri zimene muli nazo pakati panu muthandize nazo osowa, kuti nawonso akadzakhala nazo zambiri adzakuthandizeni pa zosowa zanu. Cholinga nʼkuchita mofanana,
15 monga kwalembedwa kuti, “Iye amene anatola zambiri sizinamutsalireko ndipo amene anatola pangʼono sizinamuchepere.”
Pathien lekhabu'n, “Arût mintam pu han dôn mintam uol maka, male arût mintôm pu han dôn mantôm uol mak,” ati anghan.
16 Tithokoze Mulungu amene anayika mu mtima wa Tito changu chomwecho chimene ine ndili nacho pa inu.
Nangni san ranga kin jôt anghan Titus mulung sûnga jôtna min dônpu Pathien chunga kin râiasân tatak!
17 Pakuti Tito sanangovomera kokha pempho lathu, koma yekha anafunitsitsa kwambiri kubwera kwa inu mwa iye yekha.
Kin ngênna a lei modôm vai niloiin; ama theia mulungsuokin nangni san rang jôtin nin kôm hong rangin a masat ani.
18 Ndipo tikumutumiza pamodzi ndi mʼbale amene mipingo yonse yamuyamikira chifukwa cha utumiki wake wa Uthenga Wabwino.
Ama leh lâibung inkhat thurchisa misîrna sin a thona sika koiindangngei murdi'n an jâ tatak ngâipu hah kin juongtîr sa.
19 Chowonjezera china nʼchakuti anasankhidwa ndi mipingo kuti atiperekeze pamene ife tikukapereka zopereka, zimene tikuchita pofuna kupereka ulemu kwa Ambuye mwini ndi kuonetsa kufunitsitsa kwathu pothandiza.
Male mapên han, ama hih lungkhamna sin Pathien roiinpuina rang le nangni san kin nuomna minlangna rang kin chuonsina le khuolchaina mi jûi ranga koiindangngeiin an thanga an phun ani.
20 Tikufuna kupewa kutikayikira kulikonse za mmene tikuyendetsera mphatso zochulukazi.
Phaltaka neinunpêk tam kin semna roia hin tute chiernangei akaithoi loina rangin kin indîn ani.
21 Pakuti tikuyesetsa kuchita zolondola, osati pamaso pa Ambuye pokha komanso pamaso pa anthu.
Kin neinunkhîn chu Pumapa mitmua vai niloiin, midangngei mitmua khom dikna sin hih ani.
22 Kuwonjezera apo, tikuwatumiza pamodzi ndi mʼbale wathu, amene nthawi zambiri watitsimikizira mʼnjira zosiyanasiyana kuti ndi wachangu ndiponso chifukwa ali ndi chikhulupiriro chachikulu mwa inu.
Masikin anni lehan kin lâibung inkhat kin juongtîra; vêl tamtak kin minsina male nangni san rang a jôt tatak tiin kin riet. Male atûn vâng chu nin chunga mulungngamna a dôn sabaka, nangni san rang a jôt uol ok zoi.
23 Kunena za Tito, ndiye mnzanga ndi wogwira naye ntchito pakati panu. Kunena za abale athu, ndiwo oyimirira mipingo ndi olemekezetsa Khristu.
Titus hi chu, ka champui le nangni sanna sin ni thopui ngâipu ani; lâibung dang a champuingei hi chu koiindangngei ruthûla Khrista kôm roiinpuina mintung ngei an ni.
24 Choncho anthu amenewa atsimikizireni za chikondi chanu ndipo adziwe chifukwa chimene ife timakunyadirani, kuti mipingo yonse iwone chimenechi.
Anni ngei kôm han nin lungkhamna minlang roi, masikin nangni kin songna chungroi hin kin dik ti hih koiindangngei murdi'n an riet theina rangin.

< 2 Akorinto 8 >