< 2 Akorinto 6 >

1 Pogwira naye ntchito pamodzi, tikukudandaulirani kuti musangolandira chisomo cha Mulungu pachabe.
Tun ki tidun yayi me bra yi na kpa hle ne dun Rji naRji.
2 Pakuti akunena kuti, “Pa nthawi yanga yabwino yokomera anthu mtima ndinakumvera, ndipo pa nthawi yopulumutsa ndinakuthandiza. Taonani, ndikukuwuzani kuti, ino ndiyo nthawi yabwino ya Ambuye, lero ndiye tsiku la chipulumutso.”
A tre ni ton wu dun Rji kiwo yin a i fin kpata chuwo. Ziza yin a ton wuadun Rji ye ziza a fin kpata chuwo.
3 Ife sitikuyika chokhumudwitsa pa njira ya wina aliyense, kuti utumiki wathu usanyozeke.
Ki na yo grun wu ku sho kubina ni shishi bru bina ki na so dun Hidima bu ni nha dun megina.
4 Mʼmalo mwake, mwanjira iliyonse timasonyeza kuti ndife atumiki a Mulungu popirira kwambiri mʼmasautso, mʼzowawa ndi mʼzodetsa nkhawa.
Sar he nayi kito tumbu naki ni bubu dunbu na ki gran Rji ki granma ni ta bubu vunson sar ije, tiwundi, iya.
5 Pomenyedwa, kuponyedwa mʼndende ndi mʼzipolowe. Pogwira ntchito mwamphamvu, posagona usiku onse, posowa chakudya;
Zin, kotron, inku, nime dun wuyah ne me kruna ni chun ne mrevanyi.
6 pokhala moyo woyera mtima, pomvetsa zinthu, wokoma mtima ndi wachifundo mwa Mzimu Woyera ndi mwachikondi choonadi
Ne me ba kiti kpe vusor, ti dindi ne min, Ruhu glansar isowu dindisur.
7 ndi poyankhula choonadi mwamphamvu ya Mulungu. Zida zimene zili mʼdzanja lamanja ndi lamanzere ndizo chilungamo.
Ki grama ni mehlan dindi ni wo kori ne wo komre.
8 Timatumikira Mulungu ngakhale ena amatinyoza ndi ena amatilemekeza, ena amatinenera chipongwe, enanso amatiyamikira. Ena amatitenga kukhala ngati onena zoona, ndipo enanso amatitenga kukhala ngati onena zabodza.
Ki tin dun ne daraja ni meme daraja ni gbrasa ba mreta di ki gurba ko na yi ki bin lah dindi ma.
9 Amatiyesa osadziwika komatu ndife odziwika kwambiri. Amatiyesa wooneka ngati tikufa, koma tikupitirirabe ndi moyo, okanthidwa, koma osaphedwa.
Ki tin dun ni ba na to ta na, Ba ton ta gregreme ki tin dun na kin kyu ki he ni vren bu kin tin dun na bin na no ba yah a na yah wu wun ndi na.
10 Amatiyesa achisoni, koma ndife achimwemwe nthawi zonse, aumphawi, koma olemeretsa ambiri; wopanda kanthu, koma tili ndi zonse.
Ke tin dun na bin ba no ba ki tinfun, ko ne ta ki ti dun ne gresan. ki tin dun na bin bana he ne kpena ki azurta ndin ba bra. ki tin dun na kina he ni kpena, naki ken vun ko ge ni ghrin
11 Tayankhula momasuka kwa inu, Akorinto, ndipo tanena zonse za kumtima kwathu.
Ki lah dindi ma ni jiwu conrontiyawa mesor bu heni bwu.
12 Ife sitikukubisirani chikondi chathu pa inu, koma inu mukubisa chikondi chanu pa ife.
Kina kange serbina bi yi biti kange ni kpa bi.
13 Pofuna kufanana zochita ndi kuyankhula monga kwa ana anga, nanunso muzinena za kukhosi kwanu.
Ziza sanading me tren ni yin na mhyre bi bwu na surbi.
14 Musamasenze goli pamodzi ndi osakhulupirira. Kodi pali mgwirizano wanji pakati pa kulungama ndi kusalungama? Kapena kodi pali mgwirizano wanji pakati pa kuwala ndi mdima?
Na chundun ni bin ba na tin bina. Aageh he ni tsutsu adalci ne Sharia? a ge he ni tsutsu kpa ni bwu?
15 Pali mgwirizano wanji pakati pa Khristu ndi Beliyali? Kapena munthu wokhulupirira angayanjane bwanji ndi munthu wosakhulupirira?
Wace yarjejeniya he ni tsutsu Almasihu ni ibrji? inge he ni tsustu bi tin ndindi ni bi tin dindina?
16 Pali mgwirizano wanji pakati pa Nyumba ya Mulungu ndi nyumba ya mafano? Popezatu ndife Nyumba ya Mulungu wamoyo. Monga Mulungu wanena kuti, “Ndidzakhala mwa iwo ndipo ndidzayendayenda pakati pawo, ndipo ndidzakhala Mulungu wawo, ndipo adzakhala anthu anga.”
A shutu ge he nitsutsu kho Rji di kho kachein? (Ibrji)? kin ta ki kho Rji wa ni vren in Rji tre wa wu ri me bin na tzre nitsu tsu bi ani sun ni Rji ba, ba he ndima
17 Nʼchifukwa chake “Tulukani pakati pawo ndi kudzipatula, akutero Ambuye. Musakhudze chodetsedwa chilichonse, ndipo ndidzakulandirani.”
18 Ndipo “Ndidzakhala Atate anu, ndipo inu mudzakhala ana anga aamuna ndi aakazi, akutero Ambuye, Wamphamvuzonse.”
A nahi bin rhun ni me ba, ni sun kebabbu inji Baci ni yowo kpen unmemema ne kpa yi. A he tinbi ni yin bin he mre lilun ni wha ni me. Titi Baci he iko.

< 2 Akorinto 6 >