< 2 Akorinto 5 >
1 Popeza tikudziwa kuti ngati msasa wa dziko lapansi umene tikukhalamo uwonongeka, tili ndi nyumba yochokera kwa Mulungu, nyumba yamuyaya yakumwamba, osati yomangidwa ndi manja a anthu. (aiōnios )
Fedege agoane, ninia da: i hodo da ninia osobo bagade diasu gala. Gode da amo mugulusia, e da Hebene soge amo ganodini eso huluane dialalalumu diasu, Hi fawane hamoi liligi ninima imunu, amo ninia dawa: (aiōnios )
2 Pakali pano tibuwula, ndi kulakalaka kuvala nyumba yathu ya kumwambayo,
Be wali, ninia Hebene diasu amo Gode da ninima abula agoane idiniginisima: ne, ninia da hanaiba: le, dadawa: la.
3 chifukwa tikavala, sitidzapezekanso amaliseche.
Ninia amo diasu lai dagosea, ninia da da: i nabado hame ba: mu.
4 Pamene tili mu msasa uno, timalemedwa ndipo timabuwula, chifukwa sitifuna kukhala amaliseche koma ovala nyumba yathu ya kumwamba, kuti chimene chili chakufa chimezedwe ndi moyo.
Ninia wali osobo bagade diasu amo ganodini esalebeba: le, da: i dioba: le, eganana. Bai ninia da osobo bagade da: i hodo fadegamu hame hanai. Be ninia bogomu liligi fadegale bu esalalalusu liligi lamu hanaiba: le, ninia gogonomosa.
5 Tsono ndi Mulungu amene anatikonzeratu ife kuti tilandire zimenezi. Iye anatipatsa Mzimu ngati chikole, kutsimikizira zimene zikubwera.
Gode da amo afadenesu hou ninima ima: ne hamoi dagoi. Amola ninia da Ea hobea imunu liligi huluane dafawaneyale dawa: ma: ne, E da Ea A: silibu ninima i dagoi.
6 Nʼchifukwa chake nthawi zonse timalimba mtima, ndipo timadziwa kuti pamene tikukhala mʼthupi, ndiye kuti tili kutali ndi Ambuye.
Amaiba: le, ninia da eso huluane mae beda: iwane esala. Ninia da ninia da: i hodo diasu agoane amo ganodini esalebeba: le, ninia Hina Gode Ea diasu amo ganodini hame esala, amo ninia dawa:
7 Ife timakhala mwachikhulupiriro, osati mwa zooneka ndi maso.
Ninia esalusu hou da siga ba: su liligi hame, be asigi dawa: su ganodini dafawaneyale dawa: su hou fawane.
8 Inde, ife tikulimba mtima, ndipo tikanakonda kulekana nalo thupi lathu ndi kukhala ndi Ambuye.
Ninia da beda: su hou hame dawa: Ninia da ninia da: i hodo diasu yolesili, heda: le, Gode Ea diasu ganodini esalumu baligiliwane hanai gala.
9 Choncho timayesetsa kukondweretsa Ambuye, ngakhale tikhale mʼthupi, kapena tichokemo.
Be ninia da: i hodo ganodini esalea o Gode Ea diasu ganodini esalea, ninia baligiliwane hanai liligi da Gode hahawane ba: ma: ne hou ida: iwane hamomu galebe.
10 Pakuti tonsefe tiyenera kukaonekera pa mpando woweruza wa Khristu, kuti aliyense wa ife akalandire zomuyenera molingana ndi zimene anachita ali mʼthupi; zabwino kapena zoyipa.
Bai ninia huluane da Yesu Gelesu Ea Fofada: su Fisu amoma doaga: mu. Amaiba: le, ninia Gode hahawane ba: ma: ne hawa: hamomu hanai. Yesu da nini huluanema, ninia osobo bagadega hawa: hamoi ida: iwane o wadela: iwane amo defele, bidi imunu.
11 Tsono popeza tikudziwa tanthauzo la kuopa Ambuye, ife timayesetsa kukopa anthu. Mulungu amatidziwa bwino lomwe, ndipo tikukhulupirira kuti inunso mumatidziwa bwino mʼmitima mwanu.
Ninia Godema beda: su hou dawa: Amaiba: le, ninia eno dunuma olelemusa: dawa: lala. Ninia asigi dawa: su huluane Gode da ba: lala. Dilia dogo ganodini, dilia na hou amola dawa: mu, amo na da hanai gala.
12 Sitikudzichitiranso tokha umboni kwa inu, koma tikukupatsani mwayi oti muzitinyadira. Tikufuna kuti muwayankhe amene amanyadira zinthu zooneka ndi maso osati zimene zili mu mtima.
Dilia da ninima asigima: ne, ninia da ninia hou bu hame olelesa. Be eno dunu da asigi dawa: sudafa mae dawa: le udigili dabua liligi ba: sa. Amaiba: le, dilia amo dunuma moloiwane olelema: ne, ninia houdafa da noga: i amo ninia dilima olelesa.
13 Ngati ndife amisala, monga amanenera ena, nʼchifukwa chofuna kuti Mulungu alemekezedwe. Ngati si ife amisala, nʼkuti inu muthandizike.
Ninia da dafawane dadousala: ? Ninia Gode Ea hou fidima: ne dadousu agoai hamosa. Nini da dadousa hame? Ninia dili fidima: ne, agoane hamosa.
14 Pakuti chikondi cha Khristu ndicho chimatikakamiza, chifukwa tikutsimikiza kuti mmodzi anafera anthu onse, kotero kuti anthu onse anafanso.
Ninia Yesu Gelesu Ea asigidafa hou lalegaguiba: le, amoga fawane hawa: hamosa. Dunu huluane gaga: ma: ne, Dunu afadafa da bogoiba: le, dunu huluane da Ea bogosu bidi agoane lai dagoi amo ninia dawa:
15 Ndipo Iye anafera anthu onse kuti amene ali ndi moyo, asakhale ndi moyo wofuna kudzikondweretsa okha, koma azikondweretsa amene anawafera naukitsidwa chifukwa cha iwowo.
E da dunu huluane gaga: ma: ne bogoi. E da hame bogoi dunu huluane ilia musa: hanai hou yolesili bu amo musa: bogoi Dunu (Gode da ili fidima: ne wa: legadolesi), Ea hanai hamoma: ne, Yesu da bogoi dagoi.
16 Choncho, kuyambira tsopano mpaka mʼtsogolo ife sitiganizirapo za munthu aliyense monga mwanzeru za umunthu, ngakhale kuti poyamba tinkaganiza za Khristu mʼnjira imeneyi, koma tsopano sititeronso.
Amaiba: le, musa: hou yolesili, ninia eno dunu ea hou amo osobo bagadedunu ea hou defele hame abodesa. Musa: ninia da Yesu Gelesu Ea hou osobo bagade dunu ea hou defei amo defele ba: i. Be wali agoane hame hamosa.
17 Nʼchifukwa chake, ngati munthu aliyense ali mwa Khristu, ndi wolengedwa kwatsopano; zinthu zakale zapita taonani, zakhala zatsopano.
Nowa dunu da Yesu Gelesuma madelagi galea, e da afadenene gaheabolo dunu hamoi dagoi. Hea liligi huluane da mugululi, fisi dagoi. Gaheabolo da doaga: i dagoi.
18 Zonsezi zichokera kwa Mulungu amene anatiyanjanitsa ndi Iye mwini kudzera mwa Khristu ndipo anatipatsa ife utumiki wa chiyanjanitso.
Gode Hifawane amo hawa: hamoi dagoi. Ninia musa: Ema ha lai esalu. Be Yesu Gelesu da hamobeba: le, Gode da ninia hou afadenene, nini bu Ema na: iyado hamoi. Amalalu E da eno dunu Ema na: iyado hamoma: ne, amo hawa: hamosu ninima i dagoi.
19 Mulungu ankayanjanitsa dziko lapansi kwa Iye mwini kudzera mwa Khristu, osawerengera anthu monga mwa zochimwa zawo. Ndipo watisungitsa ife uthenga uwu wa chiyanjanitso.
Ninia olelesu da agoane diala. Gode da Yesu Gelesu Ea hamobeba: le, osobo bagade fifi asi gala dunu huluane gousa: musa: dawa: lala. E da ilia musa: wadela: i hou mae dawa: le, ilima bu gousa: le na: iyado hamomusa: , amo olelesu ninia ilima sia: ma: ne, E da ninima sia: i.
20 Choncho ife ndi akazembe a Khristu, monga ngati Mulungu akudandaulira anthu kudzera mwa ife. Ife tikukupemphani inu mʼmalo mwa Khristu kuti, yanjanitsidwani ndi Mulungu.
Ninia da Yesu Gelesu Ea Sia: adole iasu dunu. Fedege agoane, Gode da ninia lafidili dilima sia: sa. Yesu Gelesu Ea dioba: le, ninia dilima ha: giwane adole ba: sa. Gode da dilia hou afadenene, dilia ha lai hou yolesili, bu Ea na: iyado hamoma: ne, dilia logo fodoma.
21 Chifukwa cha ife, Mulungu anasandutsa wopanda tchimoyo kukhala tchimo, kuti mwa Iye ife tikakhale chilungamo cha Mulungu.
Yesu Gelesu da ledo hou amola wadela: i hou hamedafa galu. Be Gode da nini fidima: ne, ninia da hobea Ema madelagiba: le Ea Hadigidafa hou gilisili gaguma: ne, E da ninia wadela: i hou lale, Yesu gisima: ne, Ea da: iga ligisi.