< 2 Akorinto 12 >
1 Ndiyenera kupitiriza kudzitamandira. Ngakhale palibe choti ndipindule, ndipitiriza kufotokoza za masomphenya ndi mavumbulutso ochokera kwa Ambuye.
Ni swanela ku litundumuna, kakwina chini wana mwateni. Muni yende che pono ni zini ba tondezwa kwa Simwine.
2 Ndikudziwa munthu mwa Khristu amene zaka khumi ndi zinayi zapitazo anatengedwa kupita kumwamba kwachitatu. Sindikudziwa ngati zinachitika ali mʼthupi kapena ayi, zimenezo akudziwa ndi Mulungu.
Nizi mukwame mwa Keresite ya ba hidiwa zilimo zina ikumi ni zone ukoo kapa mu mubili kapa hanze lyo mubili ime kanizi, Ireeza wizi- yava hidiwa mwi wulu lyo vutatu.
3 Ndipo ndikumudziwa munthu ameneyu. Sindikudziwa ngati zinachitika mʼthupi kapena ayi, zimenezo akudziwa ndi Mulungu.
Mi nizi kuti uzu mukwame - nji mukati ka mubili, kapa hanze ko mubili, kanizi, Ireeza njiwizi-
4 Munthuyu anatengedwa kupita ku paradizo. Ndipo anamva zinthu zosatheka kuneneka, zinthu zimene munthu saloledwa kunena.
Aba hindiwa mwi paradaisi ni ku zuwa zintu zi jolola mukuti zumwi ni zumwi a wambe
5 Ndidzatamanda za munthu ngati ameneyu, koma sindidzadzitamandira ine mwini kupatula za kufowoka kwanga.
Mu ku zimanina zuna muntu muni litundumune. Kono mukuli zimanina ni mwine kete ni li tundubule kwanda ka bufokoli bwangu.
6 Ngakhale nditafuna kudzitamandira, sindingakhale chitsiru, chifukwa ndikunena zoona. Koma ndimapewa kuti pasapezeke munthu wondiganizira moposera chimene ndili chifukwa cha zimene ndimachita kapena kuyankhula,
Ni bakusaka kulitundumuna, ni ni sana ni babi chihole, ni naba cha kuwamba bu niti. Kono mo ni lizwise ku ku litundubula, mi kakwina yeta ni hupule ahulu kuhita chibwenwe mwangu kapa kuzuwa zangu.
7 kapena chifukwa cha mavumbulutso aakulu kuposa awa. Choncho, kuti ndisadzitukumule, ndinayikidwa minga mʼthupi langa, wamthenga wa Satana, kuti adzindizunza.
Name bulyo kanizwe mu ku litundumuna bakeni chezo isinulo zi hitilize. Kuzwaho, ne ni sete ne ni balinyamuni ni mwiipo, ni bahewa mwiya mwinyama yangu, mutumiwa yo zwa kwa Satani ku ni kalihila, kuti kanji ni bi ni muipo ahulu.
8 Katatu konse ndinapempha Ambuye kuti andichotsere.
Totatwe ni ni kombelela Simwine ke ci, mu kuti iye achi hinde kwa ngu.
9 Koma anandiwuza kuti, “Chisomo changa ndi chokukwanira, pakuti mphamvu zanga zimaoneka kwathunthu mwa munthu wofowoka.” Choncho ndidzadzitamandira mokondwera chifukwa cha zofowoka zanga, kuti mʼkutero mphamvu ya Khristu ikhale pa ine.
Mi na wamba kwa ngu, “Muusa wangu mungi kwa ko, mi maata apangitwe mokulukela muvofokoli.” Chokuti ni ni balitundubuli ahulu mu bufokoli bwangu, njo kuti maata a Keresite nati na hala mwangu.
10 Tsono, chifukwa cha Khristu, ndimakondwera pamene ndili wofowoka, pamene akundinyoza, pamene ndikumva zowawa, ndi pamene akundizunza ndi kundisautsa. Pakuti pamene ndili wofowoka ndiye kuti ndili wamphamvu.
ku zwa aho ni li kolwisisa mu bu fokoli cha Kerisite, mu matapa, in masukuluka, ni mu manyando ni bwikalo bu zieze. Linu chi ni fokwele, nji ni kolete.
11 Ndadzisandutsa wopusa, koma inu mwandichititsa zimenezi. Ndinu amene munayenera kundichitira umboni. Ngakhale kuti sindine kanthu, koma sindine wochepetsetsa kwa “atumwi apamwamba” aja.
Chi ni babi chihole, mu bani hambilizi kuba bulyo, mu kuti ni bali ku swanela ku lumbekwa kwenu. Mukuti mi he kana ni babi mwi konde lyabo ba sumpwa ba apositola ba tota, ni hakuba bulyo kani cimwi.
12 Ndinapirira pokuonetserani zizindikiro za mtumwi weniweni, pochita pakati panu zizindikiro, zodabwitsa ndi ntchito zamphamvu.
Zi supo ze niti za ba apositola zi ba kuboneka mukati kenu che nkulo inde i zwile, zisupo ni mboniso ni misebezi ikolete.
13 Kodi inu munaoneka ochepa motani ku mipingo ina, kupatula kuti sindinali cholemetsa kwa inu? Mundikhululukire cholakwa chimenechi!
Mi he mubena bule basa sepahali kuhita zonse inkeleke, ni hebile kuti kena ni bali ni muziyo kwenu? mu ni wondele ko uu mulandu?
14 Ndakonzeka tsopano kudzakuyenderani kachitatu, ndipo sindidzakhala cholemetsa kwa inu chifukwa ndikungofuna inuyo osati zinthu zanu. Pakuti ana sasamalira makolo koma makolo ndiwo asamalira ana.
Mubone! ni li tukiseze kwiza kwenu lwa butatu. Kete ni be yo milemeze, ka kuti kani saki cheli chenu. Ni saka inwe. Mukuti ba hwile kete chiba wola ku biikila bazazi. Kono bazazi ba bikile ba hwile.
15 Motero ndidzakondwera kukupatsani zanga zonse zimene ndili nazo ndi kudziperekanso ine mwini chifukwa cha inu. Kodi ine ndikamakukondani kwambiri chotere, inuyo mudzandikonda pangʼono?
Cha kusanga muni sebeze ni ku belekiswa ba keñisa cha ihwuho zenu. heiba ni mi suna ahulu, ime ni sunwe ka buche?
16 Ena mwa inu amavomereza kuti sindinali cholemetsa. Komabe ena amaganiza kuti ndine wochenjera, ndipo ndinakuchenjererani.
Kono sina kamukwi kalile, kahena ni ba milemezi. Kono, mukuti ime ni chilokete mukupanga zintu ahulu, nje me ni ba mi kwati cha kucenga.
17 Kodi ndinakudyerani masuku pamutu kudzera mwa wina aliyense amene ndinamutumiza kwa inu?
Kana ni ba mihindili muhato wa kumi lyatilila ka cha bana ba ni ba tumite kwenu?
18 Ndinamupempha Tito kuti abwere kwanuko ndipo ndinamutumiza pamodzi ndi mʼbale wathu. Kodi kapena Tito anakudyerani masuku pamutu? Kodi iye ndi ine sitinachite zinthu mofanana ndi Mzimu mmodzi yemweyo?
Ni ba susuwezi Tite kuti ayende kwenu, mi niba mutumi ni zumwi mwaakwe. Kana Tite aba mi lyatilili? Kena tuba yendi mwi nzila iswana? Kena tuba yendi mu muhato u swana?
19 Kodi mukuyesa kuti nthawi yonseyi takhala tikudzitchinjiriza tokha? Takhala tikuyankhula pamaso pa Mulungu monga anthu amene ali mwa Khristu; ndipo abwenzi okondedwa, chilichonse chimene timachita ndi chofuna kukulimbikitsani.
Muzeza kuti i nako yonse ii tu bali kulihuna kwenu? Ha busu bwa Ireeza? Tubali kuwamba mwa Keresite zintu zonse za kumi koza.
20 Pakuti ndikuona kuti pamene ndibwera sindidzakupezani monga mmene ndikufunira kuti muzikhalira, ndipo simungadzandione monga mmene mukufunira kundionera. Ndikuopa kuti pangadzakhale mkangano, nsanje, kupserana mitima, kugawikana, ugogodi, miseche, kudzitukumula ndi chisokonezo.
Mi ni tite kuti chi neeza pona chini sa mi wana ka muni lakaleza. Ni tite kuti kete chi muni wana ka kuya ka muni lakaleza. Ni tite kuti pona cikuba ni nkaani, muuna, ku beenga ku kando, bu inuneki, kusooha, bu ikumusi ni kusa lukisa sinte. Ni tite kuti china boola, Ireeza wangu pona choni kokobeza habusu bwenu.
21 Ndikuopa kuti pamene ndidzabwerenso, Mulungu adzandichepetsa pamaso panu, ndipo ndidzamva chisoni ndi ambiri amene anachimwa kale ndipo sanalape zonyansa, zachigololo ndi zilakolako zoyipa zimene anachita.
Ni tite kuti pona chini chiswa kwi nkulo chabana bangi baba chiti chibi pili ku matangilo, mi nabana basana baba bakili ikwe ni busangu ni intakazo mubabenjili ni ba tenda.