< 2 Akorinto 11 >

1 Ndikukhulupirira kuti mupirira nako pangʼono kupusa kwanga. Chonde tandipirirani!
तुस होरन कबूल केरतथ ज़ैना अपनि बड़याई केरतन, ते एल्हेरेलेइ अवं उमीद केरतां, अगर अवं थोड़ी ज़ेरि बेवकूफी केरि त तुस झ़ैल्ले।
2 Nsanje imene ndimakuchitirani ndi yofanana ndi ya Mulungu. Ndinakulonjezani mwamuna mmodzi yekha, mwamunayo ndiye Khristu, kuti ndidzakuperekeni inuyo kwa Iyeyo monga namwali wangwiro.
किजोकि अवं तुसन सेइं प्यार केरताईं ते तुश्शो खियाल रखताईं ठीक तेन्च़रे, ज़ेन्च़रे परमेशर केरते, मीं वादो कियोरोए तुसन मसीह जो देनेरे लेइ, ज़ेन्च़रे लोक पूरे तरीके सेइं समर्पितन।
3 Koma ndikuopa kuti monga Hava ananyengedwa ndi kuchenjera kwa njoka, mitima yanunso ingasocheretsedwe kuleka nʼkudzipereka moona mtima ndi modzipereka kwenikweni kwa Khristu.
पन अवं डरताईं कि ज़ेन्च़रे शैताने सप्पेरे रूपे मां एइतां अपनि च़लैकी सेइं पेइली कुआन्श, हव्वा भटकवरी थी, तेन्च़रे तुश्शो मन तैसेरे सिधयैई ते पवित्रतैई सेइं ज़ै मसीहे कबूल केरते भोरी लोड़े भ्रष्ट न की गाए।
4 Pakuti ngati wina abwera kwa inu nalalikira Yesu wina wosiyana ndi Yesu amene tinamulalikira, kapena ngati mulandira mzimu wina wosiyana ndi Mzimu amene munalandira, kapena uthenga wabwino wina wosiyana ndi umene munawuvomereza, inuyo mumangolandira mosavuta.
ज़ैखन भी कोई तुसन कां एइते ते तुसन तैस यीशुएरी ज़ैस यीशुएरो असेईं नईं कियोरो एइतां, कोन्ची होरि यीशुएरो प्रचार केरते, ज़ेसेरो प्रचार असेईं नईं कियोरो: या ज़ै आत्मा तुसन मैल्लोरी तैस करां अलग किसमेरी आत्मा तुसन मैल्ले; या ज़ैस खुशखबरी पुड़ तुसेईं विश्वास कियूं तैस करां अलग किसमेरे खुशखबरी तुसन शुनाए, त तुस तैन शिक्षान कबूल केरने मां गलतथ।
5 Komatu sindikuganiza kuti ndine wotsika kwambiri kwa “atumwi apamwamba.”
अवं समझ़ताईं, कि अवं कोन्ची गल्ली मां, ज़ैना इस तरीके सेइं बर्ताव केरतन, कि तैना होरि सब प्रेरितन करां महान आन अवं भी तैन केरो ज़ेरो रोड़ो प्रेरित आई।
6 Mwina ndikhoza kukhala wosaphunzitsidwa kayankhulidwe, koma ndili ndi chidziwitso. Izi tinakufotokozerani momveka bwinobwino.
अगर अवं भाषण देने मां माहिर नईं, पन मसीह ते खुशखबरारे बारे मां मीं कां ज्ञाने; बल्के मीं हर गल शिखालने मां अपनू ज्ञान हिरावरूए।
7 Kodi linali tchimo kwa ine kudzichepetsa nʼcholinga chakuti ndikukwezeni pamene ndinkalalikira Uthenga Wabwino wa Mulungu kwa inu mwaulere?
कि मीं तुसन परमेशरेरी खुशखबरी मुखत शुनाई; ते अपनो आप निकड़ो कियो, कि तुस उच्चे भोथ, कुन इस मां मीं किछ पाप कियो?
8 Ndinkalanda mipingo ina pomalandira thandizo kwa iwo kuti ndikutumikireni.
मीं होरि कलीसियान करां दान कबूल कियूं, ताके तुश्शी सेवा मुफते मां केरि बेटि, तैस जो लूट न ज़ोथ।
9 Ndipo pamene ndinali pakati panu, nditasowa kanthu, sindinalemetse munthu aliyense, pakuti abale ena amene anachokera ku Makedoniya anandipatsa zonse zimene ndinkazisowa. Ndayesetsa kuti ndisakhale cholemetsa kwa inu mʼnjira ina iliyonse, ndipo ndidzapitiriza kutero.
ते ज़ैखन तुसन सेइं साथी थियो, ते मीं पेइंसेरो घाटो भोव, ते मीं केन्ची पुड़ भार न छ़ड्डो, किजोकि विश्वासी ढ्लाएईं, मकिदुनिया इलाकेरां एइतां मेरो घाटो पूरो कियो: ते मीं हर गल्ली मां अपनो आप तुसन पुड़ भार भोने करां रोको, ते अग्रोवं जो भी रोकेलो।
10 Kunena moona mtima molingana ndi chilungamo cha Khristu chimene chili mwa ine, palibe amene angandiletse kudzitamandira mʼzigawo za ku Akaya.
मसीहेरी सच़्च़ाई मीं मां आए, मीं अखाया इलाके मां कोन्ची करां दान नईं नेवरू, एल्हेरेलेइ अखाया इलाके मां इस घमण्डे केरने करां कोई मीं न रोकी बटे।
11 Nʼchifukwa chiyani ndikutero? Kodi nʼchifukwa choti sindikukondani? Mulungu akudziwa kuti ndimakukondani!
किजो मीं तुश्शो पेइंसो नईं नेवरो? कुन मीं एन कियूं, कि अवं तुसन सेइं प्यार न केरि? परमेशर ज़ानते कि अवं तुसन सेइं प्यार केरताईं।
12 Ndipo ndipitiriza kuchita zomwe ndikuchitazi nʼcholinga chakuti ndisapereke mpata kwa amene akufuna kupezera mwayi woti afanane nafe pa zinthu zimene iwowo amadzitamandira.
पन ज़ैन अवं केरताईं, तैने अग्रोवं भी केरतो रेइलो; अवं तुसन करां मद्दत न नेइलो ज़ैस सेइं अवं तैन ज़ैना घमण्ड केरनेरो मौको चातन, कि ज़ेरू कम अस परमेशरेरे लेइ केरतम तेरहु कम तैना भी केरतन।
13 Pakuti anthu oterewa ndi atumwi onama, antchito achinyengo, odzizimbayitsa ngati atumwi a Khristu.
किजोकि एरे लोक झूठे प्रेरित आन, ते दगो केरतां कम केरनेबालन, ते मसीहेरे प्रेरितां केरू ज़ेरू रूप बनाने बालेन।
14 Sizododometsa zimenezi, pakuti Satana mwini amadzizimbayitsa kuoneka ngati mngelo wowunikira anthu.
ते ई हैरान राने बाली गल नईं किजोकि शैतान एप्पू भी महिमा बाले स्वर्गदूतां केरू रूप बनाते।
15 Nʼzosadabwitsa tsono ngati atumiki ake akudzizimbayitsa ngati otumikira chilungamo. Matsiriziro awo adzalandira zoyenerana ndi ntchito zawo.
ते अगर तैसेरे सेवक भी धर्मी सेवकां केरू ज़ेरू रूप बनान, त कोई बड़ी गल नईं पन तैन केरो अन्त तैन केरे कम्मां केरे मुताबिक भोनोए।
16 Ndibwereze kunena kuti, wina aliyense asandiyese chitsiru. Koma ngati mutero, mundilandire monga mmene mukhoza kulandirira chitsiru, kuti ndinyadirepo pangʼono.
अवं फिरी ज़ोताईं, कोई मीं बेवकूफ न समझ़े; नईं बेवकूफ समझ़तां मीं कबूल केरे, ताके अवं थोड़ू ज़ेरू घमण्ड केरि।
17 Kudzinyadira kwangaku, sindikuyankhula monga mmene Ambuye akufunira koma ngati chitsiru.
ज़ैन किछ अवं ज़ोताईं ज़ेरू यीशु चाते तेरहु नईं बल्के बेवकूफी सेइं ज़ोताईं।
18 Popeza ambiri akudzitama monga dziko lapansi limachitira, inenso ndidzitamanso.
ज़ैखन कि बड़े लोक इस दुनियारे लोकां केरू ज़ेरू घमण्ड केरतन, त अवं भी घमण्ड केरेलो।
19 Inu mumalolera kukhala ndi zitsiru mokondwera chifukwa mumati ndinu anzeru!
तुस त समझ़दार भोइतां आनन्दे सेइं बेकूफां केरि झ़ैलतथ।
20 Kunena zoona mumangololera aliyense; amene amakusandutsani akapolo, kapena amene amakudyerani masuku pamutu, kapena amene amakupezererani, kapena amene amadzitukumula, kapena amene amakumenyani khofi.
किजोकि ज़ैखन तुसन कोई गुलाम बनातन, या ज़ैन किछ तुसन कां आए नेते, या तुसन सेइं धोखो केरते, या सोचतन कि तैना तुसन करां बड्डेन, या तुश्शे तुतरे पुड़ थप्पड़ बातन, त तुस झ़ल्लतथ।
21 Ndikuvomera mwamanyazi kuti ife sitinali olimba mtima kuti nʼkuchita zinthu zimenezi. Ndikuyankhula ngati chitsiru kuti chimene wina aliyense akhoza kudzitama nacho, Inenso ndikhoza kudzitama nachonso.
एल्हेरेलेइ कुन तुस सोचतथ कि मीं छिथोरू लोड़ते किजोकि मीं तैन नईं कियोरू; पन ज़ै कोई कोन्ची गल्ली मां घमण्ड केरते, अवं बेवकूफी सेइं ज़ोताईं, फिरी भी घमण्ड केरताईं।
22 Kodi iwo ndi Ahebri? Inenso ndine Mhebri. Kodi iwo ndi Aisraeli? Inenso ndine Mwisraeli. Kodi iwo ndi zidzukulu za Abrahamu? Inenso ndine mdzukulu wa Abrahamu.
कुन तैन्ना इब्रानी आन? अवं भी आईं। कुन तैन्ना इस्राएली आन? अवं भी आईं, कुन तैना अब्राहमेरे खानदाने मरां आन? अवं भी आईं?
23 Kodi iwo ndi atumiki a Khristu? Ndikuyankhula ngati wamisala. Ine ndine woposa iwowo. Ndagwira ntchito kwambiri kupambana iwo, ndakhala ndikuyikidwa mʼndende kawirikawiri, ndakwapulidwapo kwambiri, kawirikawiri ndinali pafupi kufa.
कुन तैना मसीहेरे सेवक आन? (अवं पागलेरो ज़ेरो ज़ोताईं) अवं तैन करां बेद्धतां आईं! मीं तैन करां जादे मेहनत कियोरीए, तैन करां जादे बार अवं कैद कियोरोईं, बड़े बार मीं मार बज़ोरीए, हमेशा मेरी जान मुश्किली मां पेवरीए।
24 Andikwapulapo kasanu zikoti zija za Ayuda, makumi anayi kuchotsapo chimodzi.
मीं यहूदन लीडरेईं करां पंच़ बार 39 कोड़े खाए।
25 Katatu anandimenya ndi ndodo. Kamodzi anandigendapo miyala. Katatu sitima yathu ya panyanja inasweka, ndipo ndinakhala usiku ndi usana ndi kuyandama pa nyanja.
ट्लेइ बार मीं बेंतेइं खेइ; एक्की बार मीं पुड़ घोड़ेव कियो जेव; ट्लेइ बार ज़िहाज़े मां ज़ैन पुड़ अवं चढ़ोरो थियो, ट्लुटी जेआं, अक रात ते दिहाड़ी मीं समुन्द्रे मां कट्टी।
26 Ndakhala ndikuyenda maulendo ataliatali. Moyo wanga wakhala ukukumana ndi zoopsa pa mitsinje, zoopsa za achifwamba, zoopsa zochokera kwa abale anga Ayuda, zoopsa zochokera kwa anthu akunja. Ndinakumana ndi zoopsa mʼmizinda, mʼmidzi, pa nyanja, ndi pakati pa abale onyenga.
अवं बार-बार सफरे मां; दरियारे खतरन मां; डैकू केरे खतरन मां; अपने ज़ातरे खतरन मां; गैर कौमां केरे खतरन मां; नगरां केरे खतरन मां; जंगल्लेरे खतरन मां; झूठे विश्वासी लोकां केरे खतरन मां;
27 Ndakhala ndikugwira ntchito molimbika ndipo kawirikawiri ndakhala ndikuchezera usiku wonse osagona. Ndakhala ndikumva njala ndi ludzu ndipo kawirikawiri ndakhala wopanda chakudya. Ndakhala ndi kuzizidwa ndi wosowa zovala.
बड़े मेहनती मां ते तकलीफी मां; बार-बार बींझ़े बिशने मां; बार-बार बरत रखने मां; ढ्लुख ट्लिशी मां; हिवतड़े मां; ते नग्गे रानेरी हालती मां राहोरोइं।
28 Kuwonjezera pa zonsezi, tsiku ndi tsiku ndimakhala pa chipsinjo cha nkhawa ya mipingo yonse.
ते होरि इना गल्लां केरे अलावा ज़ैन गल्लां केरे बारे मां अवं न ज़ोईं सेब्भी कलीसिया केरे फिक्र मीं रोज़ दुबातीए।
29 Ndani ali wofowoka, ine wosakhala naye mʼkufowoka kwakeko? Ndani amene mnzake amuchimwitsa, ine wosavutika mu mtima?
ज़ैखन कोई कमज़ोर भोते अवं भी कमज़ोर भोताईं। ज़ैखन कोई पापेरे पासे गाते त मेरो दिल बड़ो दुखी भोते?
30 Ngati nʼkoyenera kudzitamandira, ndidzadzitamandira pa zinthu zimene zimaonetsa kufowoka kwanga.
अगर घमण्ड केरनू ज़रूरीए, त अवं एपनी कमज़ोरारी गल्लन पुड़ केरेलो।
31 Mulungu, Atate a Ambuye Yesu, amene tiyenera kumutamanda nthawi zonse, akudziwa kuti sindikunama. (aiōn g165)
परमेशर इश्शे प्रभु यीशुएरो बाजी ज़ै सदा धने, तै ज़ानते, कि अवं झूठ नईं लोरो ज़ोने। (aiōn g165)
32 Ku Damasiko, bwanamkubwa woyimira Mfumu Areta, anayika alonda kuzungulira mzinda wonse kuti andigwire.
ज़ैखन अवं दमिश्क नगरे मां थियो त अरितास राज़ेरे हाकिमे अवं कैद केरनेरे मकसदे सेइं सारे नगरे मां पेरहो रखोरो थियो।
33 Koma abale anandiyika mʼdengu nanditsitsira pa chipupa kudzera pa zenera la mpandawo, motero ndinapulumuka mʼmanja mwake.
ते अवं टोकरे मां शहरपनाहेरे दैरारे बत्तां दुवारी उन्ढो औसालोरो थियो, ते अवं हाकिमेरे हथ्थे करां बच़ो।

< 2 Akorinto 11 >